ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

Zomwe wayankhula Michael Usi Lero atangofika mu Mzinda wa Blantyre

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 25 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 125

  • @benardisaac1986
    @benardisaac1986 หลายเดือนก่อน +1

    Nyengo ndizosintha manvuto sankha moyo wose wamunthu koma Dr usi all the best

  • @user-zs6qc9dx8s
    @user-zs6qc9dx8s หลายเดือนก่อน +5

    We all know kut anthu omwe avala makaka a UTM nd a MCP. Eni eni a UTM sitikupanga nawo zopusazo.

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya หลายเดือนก่อน

      Zoona akufuna kupusitsa

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya หลายเดือนก่อน

      Chilima nzake amane amakambilana naye ndi ndani nanga nthawi imene amakusekani pakamwa ndindani

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 หลายเดือนก่อน +3

    Manganya ndi wa MCP kuchokera kalekale

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 หลายเดือนก่อน +1

    Michael usi is a matured intellectual who doesn't entertain nosense.

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 หลายเดือนก่อน +4

    Wachepa nao u vice president.waiwala imfa ya skc.

    • @LukeKalima
      @LukeKalima หลายเดือนก่อน

      @@paulnyondo7572 aaaaaaaaaaa imfa ya skc ndiyotani anthu samamwalira kodi kapena munamuphera dala kuti muzipangira ndale imfa yake, kodi maliro akwanzanutu amaphweka chomchi akadzakhala akwanu zidzakuwawa kuti anthu azidzaseweretsa dzina la malemuwo

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 หลายเดือนก่อน +3

    Ndimaona ngati adziyankhula zogwira mtima

  • @moyowrobert3331
    @moyowrobert3331 หลายเดือนก่อน

    zoti akumanga thumba ngati Mphaka sukuziwa

  • @hastingskalambo8502
    @hastingskalambo8502 หลายเดือนก่อน +2

    Ndekuti zoti UTM yatuluka ku alliance iyeyo sakudziwa

  • @JacobKasalika
    @JacobKasalika หลายเดือนก่อน

    UTM ndimaikonda komano tikudzibalalitsa yokhatu.Uyu ndinthu ndinyamata wa SCK

  • @LukeKalima
    @LukeKalima หลายเดือนก่อน +1

    Wandisangalatsa usi sakupanga nawo za mtopola ena achita manyanzi kumeneko ndiye kulankhulatu ambuye akudalitseni dr usi

  • @sanddaniweck2703
    @sanddaniweck2703 หลายเดือนก่อน +2

    Zangongole ife tilibenazo ntchito nkhani musise zinthu zakwela kwambili coz za Neef zo anthu ena akumamizi kwina salandila koma mukasisa zinthu anthu onse athandizika

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o หลายเดือนก่อน

    Mbuz yamunthu iyi yudasi ife a Utm zopusazo ayi sitikupanga nawo

  • @LeviBlackson
    @LeviBlackson หลายเดือนก่อน

    Anthu sakumudziwa Kodi ku Blantyre kapana amapanga sewero

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j หลายเดือนก่อน +3

    Ngongole imeneyi udzabweza ndiwe .
    Fataleza udula konseko

  • @Jane-qb5qf
    @Jane-qb5qf หลายเดือนก่อน +1

    Amalawi look sharp amalawi tilindivuto akati uku komweko uku komweko lekani timapemphera kukhala ndi chiganizo chokhazikika zimandimvesa chisoni kwambiri tisinthe mindset plz plz tizagwa chagada ndikati ndione amazayesa zida kuti kuli bwanji uku aaaa kaya Malawi

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses หลายเดือนก่อน +3

    Muli mbali iti kodi Fada

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b หลายเดือนก่อน +3

    Palibe azalande m'dalitso wamunthu, Dr usi ndiodalitsika muzonse komanso olimbika.

  • @joeldaniel-pc3ij
    @joeldaniel-pc3ij หลายเดือนก่อน

    Mwapatsa anthu a MCP ma uniform a UTM kuti aziti chani?

  • @LeniaJosophat
    @LeniaJosophat หลายเดือนก่อน

    Mukutipatsirazi ndizabwino zeedi koma you need to fix the sound kuti zizikomabe( this is the VP)

  • @user-vb1iq5un5p
    @user-vb1iq5un5p หลายเดือนก่อน

    Kodi Usi ulimbali iti?. Koma umphawi luMalawi ukupepeletsa azibambo...

  • @VeronicaYohane
    @VeronicaYohane หลายเดือนก่อน

    Mudyelen bambo wasikono akabwela osadziwa kuyankhula odvala madiresiyo

  • @JuniorKalipinde-gy7dx
    @JuniorKalipinde-gy7dx หลายเดือนก่อน

    Usaone ngati ndi bugwe LA adla limenelo akupweteka

  • @johnbakali27
    @johnbakali27 หลายเดือนก่อน

    Kodi iwe ukumenyera kampeni ya mco kapena UTM?

  • @user-hh4xg4hf2k
    @user-hh4xg4hf2k หลายเดือนก่อน +2

    Enafe tisayankhire

  • @JonesSiliya
    @JonesSiliya หลายเดือนก่อน

    Mwachedwa ndi chilima simunapange chifukwa chiyani

  • @FrankidEugenio
    @FrankidEugenio หลายเดือนก่อน

    Ndale zayambika,Malawi ayiwale zambuyo.😂

  • @user-dv6rt6vb6e
    @user-dv6rt6vb6e หลายเดือนก่อน

    Umbuli suzatha anthu munayambila kunamizidwa muja zilero changamukani

  • @constancemkandawire7378
    @constancemkandawire7378 หลายเดือนก่อน

    You can't say that you love God if you don't love your nearby that's a total lie.You have failed to come together with your fellow utm members mukuti phala lomwe likudumpha mu mpoto lidumphe meaning you don't care ,ayi zikomo

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f หลายเดือนก่อน

    Mwschedwa nayo ngongoleyo bwana kkkkkkk nyimbo ikhale ya mpaka malilo vinyo watha

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f หลายเดือนก่อน +1

    Dziko la Malawi lafika pa uchitsiru weni weni

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA หลายเดือนก่อน

    Tasisani fertilizer zinthu zisike agalu inu muona muwina mosavuta

  • @RossanaMitha-tl9in
    @RossanaMitha-tl9in หลายเดือนก่อน

    Kodi akuti kwabwela ndani ?😂😂😂😂

  • @lumbaninyirenda8223
    @lumbaninyirenda8223 หลายเดือนก่อน

    tamangopitani muzikapanga ma drama,mfundo palibe apa

  • @ChrisjuZiyaya
    @ChrisjuZiyaya หลายเดือนก่อน

    Chizindikiro choti Usi siwa utm onani zomwe zavalidwazo , zomwe Malemu Sks sadapangepo. Tikufuna m'tsogoleri wa serious not this gys.

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g หลายเดือนก่อน

    Lelo akunamizila chilima lelo ndi mbuzi yamunthu

  • @genesismbewe
    @genesismbewe หลายเดือนก่อน

    genius

  • @jedoforsure2842
    @jedoforsure2842 หลายเดือนก่อน

    Umakwana us

  • @joekamphulusa4767
    @joekamphulusa4767 หลายเดือนก่อน

    Chitsilu chenicheni ichi watenga athu a mcp kumati a utm 🚮🚮🚮

  • @footballhighlightsofficial7248
    @footballhighlightsofficial7248 หลายเดือนก่อน

    Missing Chilima Already😢

  • @MlecheFatch
    @MlecheFatch หลายเดือนก่อน

    A manganya mmmh

  • @enockharry8039
    @enockharry8039 หลายเดือนก่อน

    koma izi wina aziona

  • @joma5327
    @joma5327 หลายเดือนก่อน

    champhamvu kopasa kale kuthanthauza chani

  • @KondwaniNdobvie-f4v
    @KondwaniNdobvie-f4v หลายเดือนก่อน

    Komatu adzake afanazo

  • @user-qu9ww1cd1y
    @user-qu9ww1cd1y หลายเดือนก่อน

    Anamizana zokuti akope Southern Region

  • @ellahmvula
    @ellahmvula หลายเดือนก่อน

    Hahaha awa a mcp achina Eliza avala za utm

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 หลายเดือนก่อน

    Wakupha iwe manganya

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba หลายเดือนก่อน

    Satan ndiyemwe ali kutsogolo kwakoyo

  • @RobertChisenga-ci2mq
    @RobertChisenga-ci2mq หลายเดือนก่อน

    BT chitsilu2 paja

  • @MerySaid-uw3cm
    @MerySaid-uw3cm หลายเดือนก่อน

    Tikufelanji

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 หลายเดือนก่อน

    Iweyo ukuti ukufuna ulongo sole, ndimaesa UTM yatuluka mungwirizano ukufuna kupusisanso Wanthu

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k หลายเดือนก่อน

    Basi tizingokhalira ma handouts mpaka liti abale?

  • @NkosDysonNkosDyson
    @NkosDysonNkosDyson หลายเดือนก่อน

    Tangotsitsani fertilizer muonanso mudzawina mosavuta ife amalawi sititichedwa kuiwala

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 หลายเดือนก่อน

    Wosokoneza uyu

  • @macdonaldchaonekera834
    @macdonaldchaonekera834 หลายเดือนก่อน

    Kodi akupanga sewero la tikuferanji et?

  • @frankwilliam9844
    @frankwilliam9844 หลายเดือนก่อน

    There's contradictory in his mind,chomwe amalawi akufuna singongole,tsitsani zinthu,chepetsani kudalira ngongole za IMF...koma ndithu 60yrs independent Malawi yukanikabe kudalira payokha pa nkhani ya zachuma? so sad...Kodi maiko amzathuwa amatani Kodi ..adatukuka bwanji atalandila ufulu???

  • @NELSONMULIMAH-fv6ub
    @NELSONMULIMAH-fv6ub หลายเดือนก่อน

    Zauchisilu zaziii

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p หลายเดือนก่อน

    Aaaaaaaaaaaaaaaaaaa chitsiru mbuzi garu nyani mfiti iwe

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 หลายเดือนก่อน +2

    Zaziiiiii

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g หลายเดือนก่อน

    Anthu 4 okha bs

  • @florenceharawa519
    @florenceharawa519 หลายเดือนก่อน

    Uku wapita uku wapita punsi anagwa chada😂😂😂😂

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k หลายเดือนก่อน

    Koma zimenezi zitithandiza izi????

  • @user-ep7gu2td6y
    @user-ep7gu2td6y หลายเดือนก่อน

    Sakudziwa zomwe a makawi akukumana nazo ....,

  • @MuhammadNyambalo
    @MuhammadNyambalo หลายเดือนก่อน

    😅😮😢😅😅😅😅😂 patumbo pako iwe nyo

  • @NathanMaunda-dz8gc
    @NathanMaunda-dz8gc หลายเดือนก่อน

    Awa sakuyankhula zotigwira mtima kodi nd wa chipani chanji ameneyi

  • @LottiAffati
    @LottiAffati หลายเดือนก่อน

    kod akuyankhula kut chan apa guys aaaaaa, komanso amalawi ngoputsadi ndithu

  • @MarthaChintolo
    @MarthaChintolo หลายเดือนก่อน

    Aaaaaa chifukwa chani Chilima unalakwitsa ee

  • @AbdullCassim
    @AbdullCassim หลายเดือนก่อน

    Iweso ndiye kayatu

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน

    Ayakhura ali pat?

  • @chikondiyovita7210
    @chikondiyovita7210 หลายเดือนก่อน

    My data hu!

  • @Vascomw
    @Vascomw หลายเดือนก่อน

    Ïn̈ë n̈d̈ïm̈än̈g̈än̈ïz̈ä k̈üẗ äÿäk̈ḧür̈ä z̈äz̈ël̈üüü k̈m̈ ääää b̈ün̈d̈l̈ë ÿän̈g̈ä amayo

  • @momuumro
    @momuumro หลายเดือนก่อน

    Situfuna kunva zimenezo Ife tufuna nkhani yotuluka mu tonse alliance

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 หลายเดือนก่อน

    Akufuna kugulitsa UTM KU MCP

  • @user-lu6nq9bs6w
    @user-lu6nq9bs6w หลายเดือนก่อน

    Nde ku MCP' ko akuti chani kkkk 😂😂😂

  • @elizabethnkhata3438
    @elizabethnkhata3438 หลายเดือนก่อน

    It's lik people are not happy

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh หลายเดือนก่อน

    Ndimwana uyu alibe fundo

  • @QuotienieMw
    @QuotienieMw หลายเดือนก่อน

    Tikufilanji episode 10

  • @user-ou4md5ud1u
    @user-ou4md5ud1u หลายเดือนก่อน

    Sizikuveka ai komas sizikugwilizana ayi

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh หลายเดือนก่อน

    Kupusa

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses หลายเดือนก่อน

    Palibe kunyengelerana ndi ngongore nbuzi za anthu.

  • @ElizabethMwakamogho-x7j
    @ElizabethMwakamogho-x7j หลายเดือนก่อน

    Sukuziwa make awo find alimbe

  • @user-zl1xz9kt5s
    @user-zl1xz9kt5s หลายเดือนก่อน

    Amalawi mitu sigwiradi sure

  • @Vascomw
    @Vascomw หลายเดือนก่อน

    Hhhhhhh

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p หลายเดือนก่อน

    Palibe chanzeru waywnkhula

  • @FysonKaliba
    @FysonKaliba หลายเดือนก่อน

    Kod ati Ali Mbali iti??????????

  • @SmithLikoswe
    @SmithLikoswe หลายเดือนก่อน

    Zamasewelo bac

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk ngabule moyo,thetsa,uthetsa suthetsa kkk yathayi kkk

  • @WindowSomanje
    @WindowSomanje หลายเดือนก่อน

    Za ziii

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm หลายเดือนก่อน

    Km malawi ndfe anthu opusa kwambiri tinakali kuvutika

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 หลายเดือนก่อน +1

    Za ziii tu

  • @MECChiona
    @MECChiona หลายเดือนก่อน

    wamisara uyu 😂😂

  • @NATASHAChimtolo
    @NATASHAChimtolo หลายเดือนก่อน

    Opepela uyu malemu amavala makaka achipani chake

  • @RighteousMhone
    @RighteousMhone หลายเดือนก่อน

    Shimeyi atukwane😂😂😂

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j หลายเดือนก่อน

    Emeneyi si dyera koma

  • @ChrisNkhoma-i8m
    @ChrisNkhoma-i8m หลายเดือนก่อน

    Mcp BOMA labwino kwamunthu woganiza mwazelu tiwone komwe tachoka .

  • @user-uq4hn4rp2j
    @user-uq4hn4rp2j หลายเดือนก่อน +2

    Nice

  • @thokofodya1583
    @thokofodya1583 หลายเดือนก่อน

    😢

  • @user-hl3vl9nt1b
    @user-hl3vl9nt1b หลายเดือนก่อน

    Aaaa zazi bas

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko หลายเดือนก่อน

    Sanje bac amalawi eeee

  • @sonkieleymanni6312
    @sonkieleymanni6312 หลายเดือนก่อน

    ndiopusatu awawa,,,,,,,,,,,,,,,palibepo chanzeru anena apa

    • @LukeKalima
      @LukeKalima หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

    • @LukeKalima
      @LukeKalima หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

  • @SiphiweTonnyChidumayo
    @SiphiweTonnyChidumayo หลายเดือนก่อน

    Anthu sakusangalaratu😂😂

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 หลายเดือนก่อน

      Ndizawo zimenezo komanso musawapangire Zochita anthuwo . ngati inuyo simukusangalala basi

    • @SiphiweTonnyChidumayo
      @SiphiweTonnyChidumayo หลายเดือนก่อน

      @@ancientnkhata1137 eh eh iwe im commenting according ndimmene zuonekera nsiye ine