Atsogoleri Satopa Atsogoleri Sagona - Samuel Lwara
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 9 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara commends President Dr. Lazarus Chakwera for demonstrating strong leadership during the first round of voting at the MCP convention in Lilongwe. He noted that good leaders do not get tired or complacent. Lwara emphasized that his remarks were not only to commend Chakwera but also to caution the opposition. He urged them to stop being complacent and to intensify their efforts, as once the convention is over, MCP will be fully mobilized and strategizing for the 2025 elections.
Ku Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara ayamikira mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera chifukwa chowonetsa utsogoleri wamphamvu pa nthawi yoyamba yovotera pa msonkhano wa MCP ku Lilongwe. Iye ananena kuti atsogoleri abwino satopa kapena kunyozeka. A Lwara ananenetsa kuti zomwe ananena sizinali zongoyamikira a Chakwera komanso kuchenjeza otsutsa. Iwo adawapempha kuti asiye kunyong’onyeka komanso alimbikire chifukwa msonkhanowu ukatha, MCP ikhala yokonzeka ndikukonzekera zisankho za 2025.
#malawi
Chikangawa achoke bazii akwana
At national level he is very indecisiveness - so slow to act
🔥🔥🔥🔥💪💪💪
Ichitu chichoka chochita bwino chichokapo bola atipase chilima wathu sadic mia ndi enawo
Utsogoleri wake opanda chitetezo ngt uwu sindinamuwonepo mix kuphana, ndalama ikungokwera, palibe chabwino chikuchitika
Iweyo ndiweso munthu otani bola azikakhala ku opposition a mcp
Anakamba fundo yo mveka chakwela koma report laku chikangawa. Kumupha chilima kokhako aaaa achoke basi
Yes tili limodzi ndipo akachoka kumeneko za atiuze zosatira za chilima
Awawa akungoyenela kupeleka report ndithu
Ndipo live report la chilima
Koma apa sanagone kumalilo achilima anagona kuchikangawa pomufuna
Palibe kuwina MCP tikufuna report la chilima mwamva still panopa tikumulilila skc
Mmmmmmm uziti iweyo ine ndikavota ndekha isati uzikamba zine anthu uziti ine example ine ndidzavotera chakwera not tidza no
Lwara nkhani ukuyifotokoza momvweka bwuno kwambiri.
Put things higher,is not isus but the is problem is killer,,if he go to win,, Will no having people in Malawi
Ife timanena nthawizonse MCP sikuchoka boma ndipo ndikubwelezaso MCP idzawinaso ndi mavoti oposa amene inapeza 2020
Palije chakuti chingasintha ,vilinangika pala pa juzi or imwe mukulu Luwala mungakwaniska yayi, ukavu ngunandi so tiyeni tilindizge
Kodi nkhope Za newone Zo, ziri ndinphamvu yoosintha system yakupha? Crocodile party ndiyomweyo basi