ZIMENE PATRICIA KALIATI KOMANSO DALITSO KABAMBE AYANKHULA LERO......TAMVANI

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 7 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 92

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s หลายเดือนก่อน +4

    Kaliat anakonza mai wochenjera kwambiri Mmalawi muno atapezeka azimai awa awiri kungabvuti zedi umatha Pati i love you❤❤❤❤❤❤❤

    • @FrancisNyayi
      @FrancisNyayi หลายเดือนก่อน

      Tili nao koma amaopa apasaneni ma boord gurdz 😅😅

  • @DoYouKnow3838
    @DoYouKnow3838 หลายเดือนก่อน +9

    Koma Kaliati ndi machine opangila machine anzake 🤗😂

  • @BoysonNgwenya
    @BoysonNgwenya หลายเดือนก่อน +9

    Kaliati wadya ndalama from 2006 thawi ya bingu koma ndalama sikhutika respect madam kaliati proud of you 😂😂😂

  • @user-vi5qn7fj7z
    @user-vi5qn7fj7z หลายเดือนก่อน +3

    Iweyo Patricia kaliat unabwera kuzakhala pa ndale keep it up

  • @DoYouKnow3838
    @DoYouKnow3838 หลายเดือนก่อน +7

    Chakwera ndi Kaliati apikitsane pa debate eeeeeeee Chakwera akhoza kudwalatu😂

  • @AlexMatemba-r4w
    @AlexMatemba-r4w หลายเดือนก่อน +2

    PK you deserve to be the president of utm and Malawi nation

  • @wisemanjere6572
    @wisemanjere6572 หลายเดือนก่อน +3

    As it is, I vouch for mai Kaliti for UTM president. Go for it mama. Obwerawa asatinamize

  • @dzikomwahara4811
    @dzikomwahara4811 หลายเดือนก่อน

    What a strong woman ever seen . Proud of you keep it up

  • @kadijachilwan967
    @kadijachilwan967 หลายเดือนก่อน +4

    Never trust politicians onse ndiamozi amangofuna kutiyuza

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r หลายเดือนก่อน

      Exactly. Anthu opusa andalewa ndithu

  • @falesiwillas-k8r
    @falesiwillas-k8r หลายเดือนก่อน +3

    A utm ndikhalidwelawo lonyoza komwe akuchokera. Pitani kwinako nukayese ngat mtendere uliko. Zisankho simuwinaso agalu.

  • @EmmanuelChiwaka
    @EmmanuelChiwaka หลายเดือนก่อน +1

    My brother Salambula mumatiyimilira

  • @PatriciaNabanda
    @PatriciaNabanda หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤❤❤my name

  • @user-vh1pf9kv8v
    @user-vh1pf9kv8v หลายเดือนก่อน

    Akuti CHIKANGAWA😂 siinetuuuu osandisakasaka ai

  • @ophlexmkondowe8107
    @ophlexmkondowe8107 หลายเดือนก่อน +4

    Manifesto ya UTM akanaikwanitsa ndi Chilima yekha basi no one else

    • @BoysonNgwenya
      @BoysonNgwenya หลายเดือนก่อน +1

      Exactly and I don't trust these people

  • @hi-profileltd
    @hi-profileltd หลายเดือนก่อน +2

    Mcp boma 2050 woooo

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z หลายเดือนก่อน

    ❤ Unity with love all of Malawian people and activities with faith thanks for every one

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd หลายเดือนก่อน +2

    Usi better kaliyati....wangowona kunkhala zimayi....

  • @SaviourTepu
    @SaviourTepu หลายเดือนก่อน +1

    Usi is indeed not amember to UTM. Even ma speech onse amasonyeza ndithu kuti ndi wa mcp. Koma akungofuna chabe kubalalitsa anthu mitu

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h หลายเดือนก่อน

    You are the best mama at UTM

  • @RuthBinali-b8c
    @RuthBinali-b8c หลายเดือนก่อน +2

    Mama ndinu one

  • @GladesMhango
    @GladesMhango 12 วันที่ผ่านมา

    Monga wachinyamata ti vote pati UTM oyeeh

  • @user-vh1pf9kv8v
    @user-vh1pf9kv8v หลายเดือนก่อน

    Mama awawa ndikatunduuu

  • @virginiakanjala6310
    @virginiakanjala6310 หลายเดือนก่อน +2

    Nsaluzo zituluke kuno ku South. Tikukufunani pa Njamba

  • @StoneckJali
    @StoneckJali หลายเดือนก่อน +2

    Very unforyunate speech

  • @user-mm4sr9gy5j
    @user-mm4sr9gy5j หลายเดือนก่อน

    More fire kaliyati

  • @Dalitsozingani
    @Dalitsozingani หลายเดือนก่อน +4

    Kabambe wabwera kudzaba UTM. Ma factory ikuyika MCP. osatinamizapo apa. Mwadziwa liti a Kabambe kuti UTM ndichipani chabwino.

  • @ChikondiSmart-rz2vf
    @ChikondiSmart-rz2vf หลายเดือนก่อน

    Kaliat wa bodza ufuna utinamizepo apa a mtsogoleri wanu nd amene anangoculutsa kulonjeza km osakwanilitsa chakwera my vote

  • @VictorThemba
    @VictorThemba หลายเดือนก่อน

    Ur super mama

  • @EmmanuelChirwa-z3n
    @EmmanuelChirwa-z3n หลายเดือนก่อน +2

    Akaliyati azinamiza ana ama 2000, mpoto wake uti munamudzutsayo🤣🤣

    • @jestinanamkonda1495
      @jestinanamkonda1495 29 วันที่ผ่านมา

      you just talk too much without principles. Chikagfawa issues will not give you votes rather the truth.

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga หลายเดือนก่อน +2

    Inuyo simunawauze bwanji amzanuwo kuti asakwele ndege coz kuli chivungacho hahahahaha nde tsopano mwayamba kutsutsana ndi Michael Usi? Mmesa Chilima amati ayamba kuyimba bell tsopano

  • @ganizanitembo1492
    @ganizanitembo1492 หลายเดือนก่อน +1

    Tell people what you will do to improve the economy madam provide alternative leadership

  • @sarahchimwaza5647
    @sarahchimwaza5647 หลายเดือนก่อน +1

    Kaliatii umatha iweyo.

  • @BlessingsMaheya
    @BlessingsMaheya หลายเดือนก่อน +1

    Skc anasankha Mai olingalila

  • @TiyamikeJobe
    @TiyamikeJobe หลายเดือนก่อน +1

    Kaliyati anatha anthu anasiya ukukhulupilila

  • @user-om7yf5tq6g
    @user-om7yf5tq6g หลายเดือนก่อน +3

    Crook ya munthu iyi ngati pali ma minister anaba ndrama za boma she is one of them. She could even use a Government truck to buy goods from Tanzania uyu.

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 หลายเดือนก่อน +1

      Nanga osamumanga bwa? Kupusa

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r หลายเดือนก่อน

      @@tingamasi106amangidwa bwanji when oyenera kuchita ntchitoyo are corrupt like any other politician?? Palibe wandale yemwe azatukule dziko la Malawi

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @LukaThawe
    @LukaThawe หลายเดือนก่อน

    Zakumpoto ndiye musanene Mai ndiboza limenelo amene Azusa mpoto ndi chakwera. Ndiye akuziwa Kuti ku mpoto ndikumalawi not mbuzi inu ndizanu Peter machende anu

  • @yamikanimalunga8451
    @yamikanimalunga8451 หลายเดือนก่อน +1

    SKC RIP

  • @LuciusByson-z7u
    @LuciusByson-z7u หลายเดือนก่อน

    Aaaaaa athila kuwiri inu mesa mumkat tambala nde dzichan idzi hiyaaa dpp boma

  • @MarionMwenifumbo
    @MarionMwenifumbo หลายเดือนก่อน +1

    Aaaaa Patricia pena umasongoneza zinthu

  • @ShalifRoma
    @ShalifRoma หลายเดือนก่อน +1

    Akabambewa mulibe mfundo muli ziiii awa ndiye achita kutumidwa

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga หลายเดือนก่อน +1

    Kabambe chavuta chizungu proboka pro eish limbikilani Chichewa chomwecho basi

  • @stephennyirenda8809
    @stephennyirenda8809 หลายเดือนก่อน

    Ubwino wake a Malawi anatsekuka maso.
    It's up to them to decide in 2025.Talk is cheap.

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi หลายเดือนก่อน

    Ku gender kumakunkharani mama

  • @ReubenGama
    @ReubenGama หลายเดือนก่อน

    Mayiwa adayenera kutsogolera chipani utm

  • @joycemagalasi2207
    @joycemagalasi2207 หลายเดือนก่อน +2

    Same lies

  • @frankmzomera2798
    @frankmzomera2798 หลายเดือนก่อน

    Koma a kaliati😂😂😂😂😂

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga หลายเดือนก่อน +1

    Kodi mmesa utm inalindi ma mp 4 okha

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana หลายเดือนก่อน +1

    Koma kumeneko mwamuminitsa usi wanyaaa manyii

  • @ChristinaSimwaka
    @ChristinaSimwaka หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkkkkklkkkk😅😅😅

  • @danieleneya808
    @danieleneya808 หลายเดือนก่อน

    Koma mukuziwa kuti ena ali ku Israel 🇮🇱 Chipani chanuchii timachikonda apa nde mwanyereratu takutulukani ndinu anyapapi apapa 😢

  • @FranceQongwane-ro5yr
    @FranceQongwane-ro5yr หลายเดือนก่อน

    😂tizasiya katangale according to kabambe,and utm believes him

  • @ChidaPhiri
    @ChidaPhiri หลายเดือนก่อน

    Michael Usi akulakwa zedi ayenela kuchotsedwa

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o หลายเดือนก่อน

    Abiti makandulo yauzimu mukutokota heavy

    • @AmoTiamo
      @AmoTiamo หลายเดือนก่อน

      Iwe ndoomvesa chisoni chikanakhala Kuti mu ndege munali mbale wake am sure sukanalankhula matuzi akoo

  • @robsontyg3928
    @robsontyg3928 หลายเดือนก่อน +1

    Akwen kachaso bibida too much

    • @Dalitsozingani
      @Dalitsozingani หลายเดือนก่อน

      Fodya wake eeeeiiiishshsh

  • @BoysonNgwenya
    @BoysonNgwenya หลายเดือนก่อน

    A before jesus christ 😂😂😂😂

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx หลายเดือนก่อน

    Chonde osavotera Dr chikangawa chonde munthu oipa

  • @user-pc3jg6pd1h
    @user-pc3jg6pd1h หลายเดือนก่อน

    Uku nde kung'alulatu

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON หลายเดือนก่อน

    Tamuwuzani usi asiye kunyoza chilima please

  • @josemoises7742
    @josemoises7742 หลายเดือนก่อน

    A LUTA CONTINUWA koma amalemba A LUTA CONTINUA....
    ZIKUNDISANGALASA ZA NFUNDO YA UTM NDITI KU MOÇAMBIQUE NDIE KUATO MAPUTO

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb หลายเดือนก่อน

    Zomwezi zoweta agaluzi mpaka kukondela

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx หลายเดือนก่อน

    UTM moto usi apanika ndi chitseko Yudasi

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 หลายเดือนก่อน

    NDIKUFUNA KUKUWUZANI IZI PLESASE OSAMULOLA MAGANYA KU UTM CHIFUKWA CHOTI MANGANYA SIKUTI NDI WA UTM AI MOWOPA MULUNGU IZI NDIKUNENA MOWOPA MULUNGU AKUFUNA KUKUPUsiTSANI KUTI CHAKWERA apeze mpata wakupha anthu amene ndinu wodalilika ku chipani chanucho komaso mukuwoneratu kuti ndamene anapanga ma pulani wamupha Achilima pamodzi ndi gulu lachakwera nsimukutha kuwona pamenepa nokha manganya ndichitdilu kwambili

  • @muyabasamson
    @muyabasamson หลายเดือนก่อน

    Phavu osatakgwanika nigalu usi

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw หลายเดือนก่อน

    Makaliati zukani pano ndifundo zanu zili bwino

  • @solobertkamunga2826
    @solobertkamunga2826 หลายเดือนก่อน

    Kabambe ndi zero EQ

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere หลายเดือนก่อน +2

    Kodi akabambewa adziwa liti kuti UTM ndichipani chokoma?

    • @FrancisNyayi
      @FrancisNyayi หลายเดือนก่อน

      Namga chilima anaziwa bwanji kut mcp inali ya bho ndale us dirty game

  • @mathewschifya764
    @mathewschifya764 หลายเดือนก่อน

    Yongo wayongo anali chipani chanji?

  • @EnockMuyaya
    @EnockMuyaya หลายเดือนก่อน

    Musarore kubwerara kuthiko

  • @hopesonmumba1056
    @hopesonmumba1056 หลายเดือนก่อน

    zaziii😂😂😂

  • @FavourAmos-rx5fl
    @FavourAmos-rx5fl หลายเดือนก่อน

    Ndinyambo akufuna kukola msomba tikamadzazinfikila madzi afika nkhosi

  • @dawsonwaya4722
    @dawsonwaya4722 หลายเดือนก่อน +1

    Zaziiiii numadziwa kuti mukhala pa kaliyala ,ndikumayankhula zoti kudya katatu,komanso fertilizer otchipa,lero mukuti samaimba belo, hahaha malawi wake siwalero,muname zina,izo ayi,anzanu ayendetsa boma movutikira chifukwa cha manifesto anu abodzawo ,shut up ,patricia

    • @PearsonYonah
      @PearsonYonah หลายเดือนก่อน +2

      Choka iwe ukunyoza Mai Kaliyati Kaliyati akunena zoona otsutsana naye ndi nfiti mwazolowera kupha anthu inu

    • @florachizungu
      @florachizungu หลายเดือนก่อน

      Ndipo zoona anthu akupha inu...Mukumunyoza kaliati kuti watani zopusa basi mukhara choncho afiti inu