CHIHANA NDI NANKHUMWA AVUTA UKU |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 126

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt หลายเดือนก่อน +7

    Nduona ngati akuopaa kkk ufulu weni weni tilibe kweni kweni

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 29 วันที่ผ่านมา +4

    Big up Mr Chihana though sinamveere zomwe mwayankhula ndangowona anthu akuyamikira

  • @Edson-sj8vn
    @Edson-sj8vn หลายเดือนก่อน +11

    Mawa lisathe kalindo amasulidwe chakwera &usi tionana 2025

  • @JIMMYWATHONJE
    @JIMMYWATHONJE หลายเดือนก่อน +3

    Straight to the point Mr Chihana

  • @ChristinaLigomeka
    @ChristinaLigomeka หลายเดือนก่อน +5

    Amene adzapite ku mapephero amenewo mutu wake suyenda bwino mwalo mopangitsa mapephero olapa mudzikapephera chani Mulungu akamva zimenezo magazi akuyenda Malawi mo simukuwawona, mwazi wa anthu osalakwa ukufuulawo simukuoona mapephero achani mudziwerenga bible before kuchita zithu za ziiii mudzikapha Ana azanu ngati khuku mtendere simudzaupeza mpaka mutabwera poyera kulula

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h หลายเดือนก่อน +4

    Dzaka 60 really 😢😢😢 Malawi udzakula liti 60 years still kuvala pampaz shame on you kunkuyu

  • @JohnsonRannel18
    @JohnsonRannel18 หลายเดือนก่อน +10

    Ufulu wake ndiye wutiwo mungomanga adzanu ndi kuphaso azanu

  • @user-jd9yz5hp7y
    @user-jd9yz5hp7y หลายเดือนก่อน +3

    Anthu amenewo ofufuzawo pls Mr Chihana muwonetsetse kuti asachokele ku Butchery kumene amatinamiza kuja kuti akagura Feteleza anthu akuba awa ndi kupha oyipa a MCP

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 28 วันที่ผ่านมา

    Nkukuyu ungotaya nthawi kulankhula zopusazo asakuziwa kuti Chakwera ndi nsogoleri ndani sangalalani ndi gulu lanulo LA uchigawenga mcp 😭😭😭😭😭🐊🐊🐊🐊

  • @user-zi8pj5ey4t
    @user-zi8pj5ey4t หลายเดือนก่อน +3

    A kunkuyu mzimu wa witika muli nao pamutupo

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +3

    Good Mr Chihana

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 29 วันที่ผ่านมา +1

    Iwowa mituyao sigwira kunkuyu ndi chakwera wakoyo ndinu mbuzi mukati ufulu odziramulira what do you mean? Momwe mukuyendetsera boma lero mukuona ngati dziko liri pa ufulu popeza muli busy kupha anthu komaso kumanga anthu omwe akukudzudzulani ndiye nkumati dziko liri pa ufulu inu agalu kwabasi zigawenga

  • @PaulMwachande
    @PaulMwachande หลายเดือนก่อน +3

    Nankhumwa wayamba kulankhula chifukwa sanamusankhe kukhala vp

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf หลายเดือนก่อน +2

    Memories will remain fresh even after 100 years. Let's remember them in a special way and continuously pray for their Souls to rest in eternal peace.

  • @HeedsonJere
    @HeedsonJere 29 วันที่ผ่านมา +1

    Chihana anamumana udindo ku tonse allias

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 29 วันที่ผ่านมา

    Aaa atenga anthu osadziwika cholinga choti adzattwudze mabodza ANTHU AKADZAMANENA KUTI CHILUNGAMO ACHIBUTSA ADZIMANGIDWA NDE MCP IMENEYO NDEGE YOTI DZIPANGIDZO DZINA ANACHOTSA MO MA PHONE KUTENGA KUMAFUFUDZA POKAPELEKA MA FON AFUTAMU CHILICHOTSE AAAAA amalawi mufunilanji omboni wina apa zawoka dzokha kuti chiwembu chokodza MR CHIHANA THANKS U SO MUCH KOMA A MCP AKATULUTSA BODZA LAWOLO ngati inu mudzayankhule potsusana a MCP mudzayembekedzele kumangidwa CHIFUKWA PANO DZIKO LA MALAWI LAFIKA ULAMULILO WACHIPANI CHIMODZI CHAKAKA NYALENDA NDADZANU ENA MUNATILAKWILA AMALAWI MUDZIWE DZIMENEDZO

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 29 วันที่ผ่านมา +1

    Akuziwa kuti anthu sazapitako awatuluka anthu awa

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 29 วันที่ผ่านมา

    Nanga anthu amene mukuwamangao mukutathauza kuti mukulira bodza bwanji Mr president

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN หลายเดือนก่อน +6

    Boon kalindo ndikumufuna osat inuo,chokan apaaaa

  • @user-kr4wb2th9i
    @user-kr4wb2th9i 29 วันที่ผ่านมา +1

    Anawo akhala osabereka

  • @LamieTiger-ff7cj
    @LamieTiger-ff7cj 29 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera mukanangot kukhala Za satanic metsa inu ndi satana

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe8501 29 วันที่ผ่านมา

    Bring back Bon Kalindo

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 29 วันที่ผ่านมา +1

    Agalu mumuziwaso Mulungu

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 29 วันที่ผ่านมา +1

    Agalu kumkuyu mapwala ako

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py หลายเดือนก่อน +1

    Ofufuza akhare a independent osati oziwana ndi mcp ai sipamveka black box ili kutiko choyamba?

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 29 วันที่ผ่านมา +1

    Muchoseko zaka 4 zomwe mwalamulilaz kulibe ufulu ndiye kt tili ndi zaka 56 xaufulu

  • @JamesOsman-cz9cw
    @JamesOsman-cz9cw หลายเดือนก่อน +2

    Mcp people machende anu nonse

  • @OmarManjawira-up3ns
    @OmarManjawira-up3ns หลายเดือนก่อน +1

    Chihana well spoken,

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 29 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi ufulu ulikuti, ku malawi kulibe ufulu chifukwa achina kamulepo ndi kalindo mudawamanga chifukwa chomenyera ufuluo, komatu Boma ili litipweteka ndithu

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet หลายเดือนก่อน +2

    Iwe mukuyu matako yako wapulika chakwel nayo pathako pake

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh หลายเดือนก่อน +1

    Amaio akunama mwana sangabadwe kutha miyedzi 6 asanamupitenao ku chipatala ku scale

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 29 วันที่ผ่านมา +1

    Ukuona ngati anthu akukukhululukini mwanya akupha

  • @JacksonChayibu
    @JacksonChayibu หลายเดือนก่อน +2

    Ife tikufuna bon kalindo mawa atulusidwe

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 29 วันที่ผ่านมา

    Hmm iwe Kunkuyu, ndi Chakwera musatiputsitse apa.

  • @user-hp4rl8cv3h
    @user-hp4rl8cv3h 29 วันที่ผ่านมา +1

    Chihana very good

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p 29 วันที่ผ่านมา +1

    Bodza limenero manyazi achakwera

  • @viennasamuel2976
    @viennasamuel2976 29 วันที่ผ่านมา +1

    Mwamasukatu mpaka zikhulupiliro zosakhala bwino? Globe vaccine akukupatsani thandizowo ndi ayesu? OK.

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 29 วันที่ผ่านมา

    Dzaka 60 za democracy minus 4 ya chakwela tikusangala dzaka 56 coz dzaka 4 za chakwela kulibe ufulu

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn หลายเดือนก่อน +1

    Mukut mulira maliro nanga chowangira anthu mukulira maliro ndi chan?

  • @chimwemwekamwana787
    @chimwemwekamwana787 หลายเดือนก่อน +1

    Mukuopa kut anthu akutukwanani.. nanga mmene mukuoneramu amalawi tili pa ufulu ifeeee.. ai muli ndi manyazi ndithu

  • @josephchirwa-jt7jx
    @josephchirwa-jt7jx หลายเดือนก่อน +2

    Kodi ku malawi kuliso ufulu?

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 28 วันที่ผ่านมา

    Musatinyasepo apa ufulu womwe mukunena ndiye wuti Malawi wake wuti womwe Muli wufulu za ziiiii

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 29 วันที่ผ่านมา +4

    Akuna adzakondwerere kuti zomwe.amafuna zatheka pokupha chilima

  • @ElizabethKhosa-gx3wt
    @ElizabethKhosa-gx3wt 29 วันที่ผ่านมา

    Chingawenga choopya cha chakwela panopa chikufuna kuphe bon kalindo

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo หลายเดือนก่อน +1

    Good

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 29 วันที่ผ่านมา

    Ziko la Malawi lakwanisa zaka 60 pokweza pasogolo umphawi wathu

  • @ShaliyaMusa
    @ShaliyaMusa 29 วันที่ผ่านมา

    Ndiwomwewo mfiti. Chikwelayo paribe kikna

  • @yusufbakali
    @yusufbakali หลายเดือนก่อน +1

    Kukhuyu zikhare chimwendo chakwela osewa adyeretu chaka chamawa chawoo palibe anthu tinavota kare kufa kwa chilima

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll หลายเดือนก่อน +1

    Opemphera ake ndani zigawenga inu?

  • @DennisDonework
    @DennisDonework หลายเดือนก่อน +1

    Afiti inu palibe ufulu nanga born kalindo akutani ku selo

  • @user-rd2ft5uk3q
    @user-rd2ft5uk3q หลายเดือนก่อน +2

    Ufulu wake utiwo

  • @AndrewMukhwapa-qj4vo
    @AndrewMukhwapa-qj4vo หลายเดือนก่อน +2

    Very good a Chihana

  • @user-nn7sv5yb8h
    @user-nn7sv5yb8h หลายเดือนก่อน +1

    Kunkuyu udzinena kuti presdent wakoyo wanena kuti osati walamula ai

  • @user-tn2qg1vs9j
    @user-tn2qg1vs9j หลายเดือนก่อน +1

    Inu nosenu ndinu agalu kwabasi ifetu tikungo funa kuti bon Kalindo wathuyo tipaseni achainiyakefe

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 หลายเดือนก่อน +1

    Ngakhale atapanga zokoma bwanji a mcp kuphiphilitsa za imfa ya chilima even atati apereka nseu wot chilima road sadzawinabe awa.ndinu okupha okupha basi munapha nzanu mbili sizafufutika.

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt หลายเดือนก่อน +1

    Koma kachere anachulukitsa kulibe dzina lina

  • @richardManemba
    @richardManemba 29 วันที่ผ่านมา

    Ayii akupangila kt ufulu wa amalawi uchoke km osalola kungolola bas zabwelela zakale

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 29 วันที่ผ่านมา

    Akuopa kuti akakuwidwa ku 6 July 😂😂😂😂 mwabalalika makape

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet หลายเดือนก่อน +1

    Inu ti onana 2025 mukutuluka inu

  • @VanPaul-sv9yx
    @VanPaul-sv9yx 29 วันที่ผ่านมา

    Nanu tazingodurani nkhani zofunikirazo ndikumaponya apa osati ndi nkhani zopoira zomwe

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 29 วันที่ผ่านมา

    Muvesen akunena ufulu obela a malawi galuyu okukuda kukeqma

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 หลายเดือนก่อน +1

    Iweyo Kumkuyu ndi Chakwera wakoyo God must punish you, Mukukamba za kukhudza Maliro a Dr Chilima chonsecho mukungotiphimba kumaso.

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 27 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu uzipemphela kwambili kuti boma lisasinthe ...boma kungosintha iwe uzafela kumdende ....unapha allan witika chifukwa cha mkazi .....munthu wopusa iwe kwambili mbuzi

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo ofufudza sakuyenera kuitanidwa kuchoka ku boma cos ndiwomwe analephela kupulumutsa anthu, in other way, boma ndilimwe lapha anthu

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d หลายเดือนก่อน +1

    Wanena zoona chihana

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera ndi lwe nkukuyu agalu nose mapemphera achani fiti lnu nose ndi manganya tikulira chilima wanthu lnu mumumasure bon kalindo ndi kamulepu boma lakhaza lri mwayiwara kt mupeze ma udindo ndi chilima nose 😢

  • @yusufbakali
    @yusufbakali หลายเดือนก่อน +1

    Mbudzi iwe

  • @user-nr4mi7pt8g
    @user-nr4mi7pt8g 29 วันที่ผ่านมา

    Ma billion chikondwererowo nde tigawanepotu sizausiru apa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน +1

    Chokani ana amahule inu kungokhalira umoyo wauchigawenga

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 27 วันที่ผ่านมา

    Mulila bwanji poti mwachita kumupha chilima koma ndizokhumudwisa kwambili

  • @ThomasMunyolowa
    @ThomasMunyolowa หลายเดือนก่อน +1

    Osati kuopa ku kuwizidwa

  • @user-mk3fy9nl2u
    @user-mk3fy9nl2u 29 วันที่ผ่านมา

    Inunso mukuziziwa zimenezo

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q หลายเดือนก่อน +4

    KOMA BOMA LA MCP 😢😢😢
    AWA SI ANTHU KOMA AFITI ASATANIKI

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 29 วันที่ผ่านมา

    Akuti muli wufulu m'malawi zoona

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน +1

    Dzaka 60 yoh bwanji dziko lili paumphawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 shame

  • @TwayibuChimbama
    @TwayibuChimbama หลายเดือนก่อน +1

    Kusilamulila kwake kopa anthu

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 29 วันที่ผ่านมา

    Masiran born kalindo kaye mukubisa chan pomumanga iyeyo

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d หลายเดือนก่อน +1

    Following

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 หลายเดือนก่อน +1

    Zaziiii

  • @MatiasChimsakasa
    @MatiasChimsakasa 29 วันที่ผ่านมา

    Komano bwanji anthu anasangalala polumbilitsa olemekezeka a vp koma 6jly ayi Kodi undiuthenga wanji mukupeleka kwa ife achinyamata

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi หลายเดือนก่อน +2

    Stupid you guys in chakwera team
    Mwapha chilima anthu inu mukukayankhula zautsiru

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 29 วันที่ผ่านมา

    Mufika kumeneko nonsenu kumeneko za chamba 6 July muzakhalamulibe moyo inu agalu eti mboloyako

  • @mussakathumba128
    @mussakathumba128 27 วันที่ผ่านมา

    Komanotu kunena chilunga amalawife tikufatsa kwambiri plus ulemu too much.chakwera wationjeza akungopha anthu ngati khuku tinayenera kumuchotsa before mavoti

  • @JosephKuyeli-rc9on
    @JosephKuyeli-rc9on 28 วันที่ผ่านมา

    Or mpunga wa nyama tisadyenso?? 😢😢😢

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f 29 วันที่ผ่านมา

    Mapemphero ake ati komanso abusa achokera mpingo uti
    Please leave God alone please

  • @user-xf6dn7pv9b
    @user-xf6dn7pv9b 29 วันที่ผ่านมา

    Chakwera ndiwe mbuzi wamva , galu , nyani chittsru cha munthu

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 หลายเดือนก่อน +1

    Well done Enoch chihana utsogoleri ndiumeneo. Tikufuna tiwaziwe anthu amene achoka ku Germany ofufuza za ngozi ya vice president ndi azathu 9. Awapeza bwanji anthu aku Germany owo aboma anene.

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 29 วันที่ผ่านมา

    Iwe kumkuyu ndiiwe mbuz et ufulu wake ulikut popeza mungomanga aliyese brushit zako

  • @louisgolden
    @louisgolden 28 วันที่ผ่านมา

    Kodi July yili Liti Koti muyambe kunena Za 6 July

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 29 วันที่ผ่านมา

    Anthu tili ndi mafunso kumene

  • @ClementMinyanga
    @ClementMinyanga 28 วันที่ผ่านมา

    Ufulu wake ulikut???

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂

  • @charlesvenacio9773
    @charlesvenacio9773 29 วันที่ผ่านมา

    Malawi muno mulibe umfulu

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 28 วันที่ผ่านมา

    Ufulu wake utiwo?????

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 29 วันที่ผ่านมา

    Akunkuyu machende

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 29 วันที่ผ่านมา

    Kulibe ufulu ku malawi mcp is fokolo

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 27 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu panyapako galu iwe

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py หลายเดือนก่อน +1

    Inet imfa yachilima ndalota utsiku tapephera mosweka mtima akundilakhula kuti pangoz damulumuka koma anthu adandipha pondikhapa mendo zanga ndiy achakwera musamalet enafe ndi daniel tikapephera mulungu amayakha kumaloto athu mudapha inu pomukha chilima ndi zikwanje munyaaaaa nane daniel omasulira maloto kuuulurani

    • @ChristinaLigomeka
      @ChristinaLigomeka หลายเดือนก่อน +1

      😭😭😭 Km kulakwatu uku ayaluka awa akusewera ndi Mulungu km😭😭😭😭

    • @ManifoldPhiri
      @ManifoldPhiri หลายเดือนก่อน

      Usatchure dzina la mulungu wako pachabe mingochimwa nazo izi

    • @ChristinaLigomeka
      @ChristinaLigomeka หลายเดือนก่อน +2

      @@ManifoldPhiri atchula pacha be pempherani nanu mosweka mtima Mulungu sapepusa PEMPHELO losweka mtima Koditu amakani nu choona muchidziwa posachedwapa mwazi ukufula ohoooo wanthu 9 mmmmmm anthu mimba zamangidwa kufuna kudziwa choona chochoka kumwamba anthu kukugonedwa mapili kufuna kudziwa nchoonadi chochoka kumwamba inu ngati mafoloko alimanja daily musaganize ngati dziko lonse anthu avula dzuwa liliphweeee mukucheza ndi Mulungu

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr 29 วันที่ผ่านมา +1

      ​@@ChristinaLigomekakunena zoona imfa iyiyi sikundigonetsa tulo ndizowawa ndipo ngati bodza Chilima kulibe zoona. Mulungu munaloleranji? 😢 ndikufuna tidziwe zoona

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w หลายเดือนก่อน +1

    Mbolo zanu

  • @Sugerman-tw4do
    @Sugerman-tw4do 29 วันที่ผ่านมา

    Zopusainu