Passport Scandal; Bendulo-Gate; Bango-Gate. Kuba kwaphweka ndi Chakwera.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 256

  • @user-pz7tf4js2t
    @user-pz7tf4js2t 6 หลายเดือนก่อน +15

    Waying'alula God bless you brother

  • @user-dj5hd4ys3n
    @user-dj5hd4ys3n 6 หลายเดือนก่อน +15

    Timkanena ife kuti awa si anthu awaaaa ziko lasokonekela Ili ndi anthu ochepa

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 6 หลายเดือนก่อน +20

    Honestly chakwela must leave a government

    • @allamalbertbeza2679
      @allamalbertbeza2679 6 หลายเดือนก่อน +1

      Honestly,Chakwera is not a president,

    • @allamalbertbeza2679
      @allamalbertbeza2679 6 หลายเดือนก่อน

      Must just go ok

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 6 หลายเดือนก่อน

      Yes he must step down it's too much guys mmmmmm Chakweraa mfiti ndithu

    • @christophermalinga2839
      @christophermalinga2839 5 หลายเดือนก่อน

      ​@😊😊😊😊😊😊😊allamalbertbeza2679

    • @christophermalinga2839
      @christophermalinga2839 5 หลายเดือนก่อน

      ​@@allamalbertbeza2679😊😊

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8d 6 หลายเดือนก่อน +4

    Why chakwela????why Malawi???? Mulungu tifikileni amalawi anthu ena omwe munaealenga ndinu akutizunza

  • @johnman4619
    @johnman4619 6 หลายเดือนก่อน +9

    Salute bwana mumaulula zinsinsi

  • @user-mw8dq4is6k
    @user-mw8dq4is6k 6 หลายเดือนก่อน +2

    mmmm koma anthu amenewa ndiomwe akupangitsaso kut mvula isabwere kumalawi...Let them go💪anthu oipa ongofuna ndalama zikhale mmatumba mwao bas a malawi azivutika.Thanks big taziwa nawo you are the best TV channel ever.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 6 หลายเดือนก่อน +7

    Ma advisor a president ndi zitsiru, zimenezi angaliuze dziko? Osangonena zoona kuti chifukwa cha umbuli zikutivuta kupanga run system ya immigration. Zimenezi sizoyima nazo pa podium kuliuza dziko.

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i 6 หลายเดือนก่อน +1

    Tinanena kuti mwasankha nkhumba siizi😢😢😢😢

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 6 หลายเดือนก่อน +1

    My Malawi mmmmmm wathatu zedi mudzaka 4 zokha mmmmm😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @KondieOne
    @KondieOne 6 หลายเดือนก่อน +8

    Powerful message

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h 6 หลายเดือนก่อน +3

    Ine ndimadikila inu man pakhani ya ma passport apa ndye ndaziwa chilungamo koma musasiye kutiziwisa tilinanu man

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 6 หลายเดือนก่อน +1

    Kuyankhula mwanvemve bg mn respect 🙏 'ifeyo ndilid pachiopsezo kwambiri look like this government

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 6 หลายเดือนก่อน +6

    Ife zimene tikudziwa ndizimenezi osati achakwela zimene akutinamiza chakwelayo apa

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6n 6 หลายเดือนก่อน +1

    Mulungu amene mumamva madandaulo awanthu,, chonde tichotselen chiphinjo cha azitsogoleri woipawa😭😭😭

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 6 หลายเดือนก่อน +9

    Chakwela ndi mbuzi ya munthu

  • @Emmy-y9f
    @Emmy-y9f 6 หลายเดือนก่อน +1

    Iweyo ndi zikhale ng'oma eeeh 🙌🙌🙌😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @ebrahimjannaphiri4715
    @ebrahimjannaphiri4715 6 หลายเดือนก่อน +6

    My best journalist. Bakili T.V my best channel

  • @justinjj25893
    @justinjj25893 6 หลายเดือนก่อน +3

    Shame on this leadership. They made a hasty decision to end the contract with former producers of passports.

  • @user-ne7rn4ki3c
    @user-ne7rn4ki3c 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ndi chifukwa chani sanafuse eni ake Malawi kuti tikufuna kugulitsa salima sugar kodi dzikoli ndila mcp no

  • @davenchimadzi6529
    @davenchimadzi6529 6 หลายเดือนก่อน +2

    Udindo olilila ndiwumenewo mavuto pamwamba pa mavuto amzake 😢 angotula pasi udindo bas zawakanika awa👋

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 6 หลายเดือนก่อน +3

    Panopo pamene lafika dzikoli..... olo kuliika pansika munthu saangagule laoleratu😅😅😅😅😅😅😅

  • @George-zd5le
    @George-zd5le 6 หลายเดือนก่อน +2

    Koma Abale Malawi 🇲🇼 ndidziko lamanyazi paziko lonse lapansi

  • @BonfaceMulera-px1jc
    @BonfaceMulera-px1jc 6 หลายเดือนก่อน +1

    😢 Chakwera tisiye ife tinakulakwira CHANI😭

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 6 หลายเดือนก่อน +4

    It's really unbelievable what's happening in my country

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 6 หลายเดือนก่อน +5

    Mau ndilibe naye president uyu akuti busa

  • @MwenyeCheNsoma-gb2yz
    @MwenyeCheNsoma-gb2yz 6 หลายเดือนก่อน +1

    And i quoted "chiyambileni Malawi" kkkk🤣🤣🤣

  • @user-to4lf5cr5v
    @user-to4lf5cr5v 6 หลายเดือนก่อน +3

    I just say things bakili muluzi tv Allah bless you and give long life

  • @ishakatimbe7341
    @ishakatimbe7341 6 หลายเดือนก่อน +6

    Koma katangale wafika poopsa kwambiri kumalwi

  • @georgechikafutwa1334
    @georgechikafutwa1334 6 หลายเดือนก่อน +6

    Yapheduka

  • @kennethmoyo8672
    @kennethmoyo8672 6 หลายเดือนก่อน +1

    Athufe tikuvutika koopsa chifukwa cha athu andale🤨

  • @Nulunulu634
    @Nulunulu634 6 หลายเดือนก่อน +5

    Dziko la Malawi kuchititsa manyazi

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 6 หลายเดือนก่อน +2

    Tinadziwa kale ife kuti so.mething fishy anthu awa alibe umunthu 🙆‍♀️🙆‍♀️🙆‍♀️

  • @zeckbmalawi8017
    @zeckbmalawi8017 6 หลายเดือนก่อน +2

    Best tv

  • @christophermkhize1991
    @christophermkhize1991 6 หลายเดือนก่อน +1

    Ndagalu amenewa

  • @ChiccoJelly-wp5wj
    @ChiccoJelly-wp5wj 29 วันที่ผ่านมา

    Man of history we love you

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 6 หลายเดือนก่อน +4

    Ambuye atithandize 😢

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 6 หลายเดือนก่อน +3

    Thanks for this video, but becareful cool junta channels get these videos a repost

  • @user-et5nz4vz2v
    @user-et5nz4vz2v 6 หลายเดือนก่อน +3

    Best TV

  • @matembamadadada8291
    @matembamadadada8291 6 หลายเดือนก่อน +2

    Boma iri rationesa zachilendo😊

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 6 หลายเดือนก่อน +5

    Agalu awa satithandiza or pang'ono

  • @Razarusmbavachakwera
    @Razarusmbavachakwera 6 หลายเดือนก่อน +4

    iiii nkhani yachisitsiyija yawululikakuno

  • @HusseinMachemba
    @HusseinMachemba 6 หลายเดือนก่อน +3

    Ine nde ndimaidikilatu Malawi kumuwolesa 😢😢😢

  • @HopefulCoralReef-tx4vx
    @HopefulCoralReef-tx4vx 6 หลายเดือนก่อน +4

    Ulemu wanu big ndizomwe timadikila

  • @wennabralecs4141
    @wennabralecs4141 6 หลายเดือนก่อน +3

    Koma boma limeneli sinaliwone ay mmmm Malawi akumowonong'a

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 6 หลายเดือนก่อน +2

    U r a great man ..kulankhula momveka bwno

  • @user-kf5xy1vp1z
    @user-kf5xy1vp1z 6 หลายเดือนก่อน +5

    HE made an error to decrale that the system has been hacked. Its so unfortunate

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 6 หลายเดือนก่อน +1

      Is this English or Chinglish?🥵🥵

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t 6 หลายเดือนก่อน

      Inu mwawelenga kuti ndi chani?

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 6 หลายเดือนก่อน +3

    Kodi chifukwa cha chakwera akupanga izi kodi amalawi alikuti???

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 6 หลายเดือนก่อน +1

    Independent channel ❤❤❤

  • @PeterGabriel-uh2lh
    @PeterGabriel-uh2lh 6 หลายเดือนก่อน +5

    Malawi wavuta eee

  • @evancenasoro922
    @evancenasoro922 6 หลายเดือนก่อน +2

    We love you boss

  • @gracetjomane-jj3ib
    @gracetjomane-jj3ib 6 หลายเดือนก่อน +2

    Koma man awawa eeeeh ndi dolo kwambili ❤❤❤❤

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ulemu wanu big❤❤❤

  • @Chiso2019
    @Chiso2019 6 หลายเดือนก่อน +2

    Mbambande information 🔥🔥🔥🔥

  • @falukujilani7545
    @falukujilani7545 6 หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu akudaliseni potiziwisa malawi wawonongeka ngati boza

  • @user-dx4zu1wv4q
    @user-dx4zu1wv4q 6 หลายเดือนก่อน +5

    Timakunyadila man kwambiri

  • @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot
    @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot 6 หลายเดือนก่อน

    What a shame leadership of Mr so called Chakwera. When you stilling little things from poor citizens this is what happens.

  • @truthtellerlastonk.m.p4985
    @truthtellerlastonk.m.p4985 6 หลายเดือนก่อน +1

    Best TV ever

  • @georgeabigailmaseko-ts3fq
    @georgeabigailmaseko-ts3fq 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ndinu dolo brother ulem wanu❤

  • @StarSterling-vl6to
    @StarSterling-vl6to 6 หลายเดือนก่อน +1

    Best Tv ever❤

  • @milajimussa4120
    @milajimussa4120 6 หลายเดือนก่อน +1

    Best tv in Malawi ❤

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 6 หลายเดือนก่อน +2

    Koma MCP ayi zikomo

  • @user-fg6ff9ex1i
    @user-fg6ff9ex1i 6 หลายเดือนก่อน +1

    Iyeyo sangayankhule zakuba kwake ayi

  • @Wizzeboycom
    @Wizzeboycom 6 หลายเดือนก่อน +3

    Respect ❤❤

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 6 หลายเดือนก่อน +2

    Kung'amba ku ng'amba basi...😅😅😅😅😅😅

  • @wydonmsongole8697
    @wydonmsongole8697 6 หลายเดือนก่อน +1

    Haha thanks for incredible info.. angogulisa Malawi

  • @thomasmwitiya1447
    @thomasmwitiya1447 6 หลายเดือนก่อน +5

    Koma adha iweyo ndidolo

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 6 หลายเดือนก่อน +1

    Ntchito koma Kuwabela ma Burundians ndima innocent aku Rwanda 😂😂😂

  • @user-mz4tk1pw3f
    @user-mz4tk1pw3f 6 หลายเดือนก่อน +3

    Ulemu wanu big zoona anthu amenewa achoke

  • @MonicaThocco
    @MonicaThocco 6 หลายเดือนก่อน

    Koma chipani ichi 😢 Mulungu achisasula ndithu ndithu Mulungu sagona pa ana ake ,anthu tikuzuzika ndi uchimo wa muthu m'modzi zowona ,ai Mulungu sawodzera tiyeni tigwirane manja ,kuti Mulungu akhale Mulungu

  • @user-fo5yn3ru6f
    @user-fo5yn3ru6f 6 หลายเดือนก่อน +1

    Bigy vuto Ku Malawi kuno police imakhara mmanja mwa boma

  • @giftmulima6615
    @giftmulima6615 6 หลายเดือนก่อน +2

    Malawi palibe chikuyenda 😢

  • @mercychirwa2147
    @mercychirwa2147 6 หลายเดือนก่อน +2

    Eeeeeeee kma boma ilili mmmmm 🙌💔... Mulungu awakanthe onse

  • @user-pe7lo1fe9b
    @user-pe7lo1fe9b 6 หลายเดือนก่อน +1

    Koma abusa achakwera,!
    Koma a busa achakwera!!,
    machende wawo

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 6 หลายเดือนก่อน +3

    Ndipo akunama anthu omwe akupita ku Gaza akuyenda bwanji

  • @CheloyaaChikwatuu-ob2mt
    @CheloyaaChikwatuu-ob2mt 6 หลายเดือนก่อน +1

    Amalawife ndiyomwe tili opusa kumuchosa mosemuja anayambiramuja tingomuyang'a bas aziba akubanjaraworo

  • @user-ml9fm2wm1o
    @user-ml9fm2wm1o 6 หลายเดือนก่อน +1

    god bless you ,

  • @DungaNya
    @DungaNya 5 หลายเดือนก่อน

    Ine kwathu ndiku South Africa Capetown kumeneko nditasamuka bye

  • @sanlakedickson6780
    @sanlakedickson6780 6 หลายเดือนก่อน +2

    respect always

  • @omarstambuli2105
    @omarstambuli2105 6 หลายเดือนก่อน +2

    We always with you

  • @cassimomar6027
    @cassimomar6027 6 หลายเดือนก่อน +3

    big boss

  • @albertojekemu3119
    @albertojekemu3119 6 หลายเดือนก่อน

    Aaaaa bodza apaangeso passport ndindani oti system idaloka. Technobrain is reputable , sinazi osanamiza amalawi

  • @Penguins_antartica
    @Penguins_antartica 6 หลายเดือนก่อน

    Lazarus Ango tuluka , he is just appointing people in his family to do jobs when the people are not experienced

  • @user-cj2bo4lf7c
    @user-cj2bo4lf7c 6 หลายเดือนก่อน

    Dziko laMalawi lafika povetsa chisoni..yet anthu osazindikira akusaporta MCP

  • @ManuelMoses-vv8mo
    @ManuelMoses-vv8mo 6 หลายเดือนก่อน +3

    uremu wanu boss man mumakwana

  • @lusolawo73
    @lusolawo73 6 หลายเดือนก่อน +1

    Continue Mr man

  • @imaanisuba9050
    @imaanisuba9050 6 หลายเดือนก่อน

    Nkhaniyi ikundionekera ya bodza,
    1. Ngati Daudi Sulaiman amayesa kupanga login and was blocked 🚫 nde kuti system siinapangidwe hack therefore information nde kuti ili safe, coz nde kut there are no hackers anywhere
    2. Kukakamiza system kuti munthu apange login sikungapatse kuti server ipse, server ngati ingapangidwe overwhelm ndi ma request imapanga shutdown osati kupsa.
    3. There is no way wina angapeze information pamene system siinalowedwe.
    It's either system yapangidwa hack or they were trying to login nde yapanga block koma sizingakhale zonsezo

    • @alinafe2
      @alinafe2 6 หลายเดือนก่อน

      sadziwa awa kuti zama computer zimayenda bwanji kkkk

  • @AustinChiyembekezo-cx4mz
    @AustinChiyembekezo-cx4mz 6 หลายเดือนก่อน +2

    Good talking king man

  • @user-xw6xf1gt7p
    @user-xw6xf1gt7p 6 หลายเดือนก่อน +1

    My man nice massages

  • @vytwistthelion98
    @vytwistthelion98 6 หลายเดือนก่อน

    Boma loyendesedwa ndie abulutu ndichoncho tisadabwe paja amati mistake imodzi kulira ndi zaka zaka

  • @AuffiPillo-cf9rn
    @AuffiPillo-cf9rn 6 หลายเดือนก่อน +1

    Angogulitsanso dziko lino aliyense atengepo gawo lake Aaaaaaah 😂😂😂😂😂

    • @StevoZimba
      @StevoZimba 6 หลายเดือนก่อน

      😅😅😅😅😅

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwera is here to stay up to 2030 woooooo

  • @user-bj6ig9zt9e
    @user-bj6ig9zt9e 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ine boma la mcp zaukira wait

  • @user-ud6qc9mw7b
    @user-ud6qc9mw7b 6 หลายเดือนก่อน +1

    Inuyo mulungu azikudalisani

  • @user-pn7ek7wb7n
    @user-pn7ek7wb7n 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ndipo alomwe zomwe mukupangazi m

  • @user-nu8oo6oc4j
    @user-nu8oo6oc4j 6 หลายเดือนก่อน +2

    Takulandilan bwana

  • @user-tx7cq2hr7k
    @user-tx7cq2hr7k 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwera must step down

  • @QueenVunga-fb9sj
    @QueenVunga-fb9sj 5 หลายเดือนก่อน

    Koma chakwera aonjeza kwambili mulungu alowelelepo ndinthu

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 6 หลายเดือนก่อน +1

    wobodza akufuna kuba mavote

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwera ndi zikhale ng'oma ndinu zisiru kwabasi anthu akuvutika inu muri busy kuba

  • @user-yn2xf7rs5o
    @user-yn2xf7rs5o 6 หลายเดือนก่อน

    Amalawi ife tanyanya kukhala nkhumba mcp inayamba lite kuzuza amalawi