MAYI MAWINDO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.พ. 2025
  • MAYI MAWINDO

ความคิดเห็น • 20

  • @IsaacJere-w1m
    @IsaacJere-w1m ปีที่แล้ว

    Mulungu akudaliseni chifukwa cha cha umboni wamphavu. Mu u bomboni wanu ndarimbikiskika mu zambiri. Zimozi mwa izo pa zimene mulungu anakuwoneskani. Naneso zina ananiwoneskapo. Nthawi za mbiri nimakayika kuti. Zoona izi ambuye mundikhululukire pokayika. Amen ambuye akhare nanu mai mawindo pa zonse 🙏

  • @MaxwellKalulu
    @MaxwellKalulu 2 หลายเดือนก่อน

    Very powerful testimony

  • @Sheepfoldfood
    @Sheepfoldfood ปีที่แล้ว +1

    I heard this from my mother. When I was young I use to attend Glory to God ministry, lords willing one of the faithful days wants to return their once again. Hearing from UAE Dubai❤

    • @dorothykalanda1742
      @dorothykalanda1742 ปีที่แล้ว

      Tipstseniko manambala a Mai maeindo chinde

    • @MaxwellKalulu
      @MaxwellKalulu 2 หลายเดือนก่อน

      Mulungu akudalitsen mai cfukwa cha umboni wamphamvuwu ndipo ndkuona anthu ochuluka akupulumusidwa cfukwa cha umboni uwu. Zikomo A mbuye YESU

  • @astridachirwa7743
    @astridachirwa7743 5 ปีที่แล้ว +3

    Tilape ndithu kuti ambuye atikhululukire

  • @nditumenichagunda4192
    @nditumenichagunda4192 ปีที่แล้ว

    Zonama mukunenazo mai simungandiopsezeso

  • @MaurineFunsani
    @MaurineFunsani 6 หลายเดือนก่อน

    Ku mwamba kulemekezeke

  • @BeatriceKhunje
    @BeatriceKhunje 10 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @AlvinJnr-rm6pe
    @AlvinJnr-rm6pe ปีที่แล้ว

    Umboni umenewu wasitha moyo wanga

  • @vitumbikokaundah2968
    @vitumbikokaundah2968 3 ปีที่แล้ว +2

    Umbon umeneyo wapangisa kut ndidziwa zambiri Ambuye aremekedzeke

  • @sibongiresambojere3280
    @sibongiresambojere3280 7 ปีที่แล้ว +3

    Ndiomboni umenewu mtima wanga ufunafuna nkhope ya Ambuye Yesu nthawi zose.

    • @sibongiresambojere3280
      @sibongiresambojere3280 7 ปีที่แล้ว

      Nanga mkukupezani bwanji kuti tifuse zambiri zonkhudza umboni umenewu

    • @jemussijeremias1857
      @jemussijeremias1857 3 ปีที่แล้ว

      Chonde anthu tiyeni tilapedi kuti tisakapezeke ku gehena Malo amazuzo.

  • @jesimoyomoyo3206
    @jesimoyomoyo3206 4 ปีที่แล้ว +1

    Umboni uwu wasuntha moyo wanga Ambuye alemekezeke

  • @jemussijeremias1857
    @jemussijeremias1857 3 ปีที่แล้ว

    Amen!! God help me

  • @caiphusgondwe6961
    @caiphusgondwe6961 5 ปีที่แล้ว +1

    Ambuye aleme kezeke

  • @chifundomopiwa5944
    @chifundomopiwa5944 2 ปีที่แล้ว

    Zikomo kwambiri abusa chifukwa cha uthenga wanu.

  • @knowledgekamanga1011
    @knowledgekamanga1011 5 ปีที่แล้ว +1

    Amayi mumandidalitsa kwambili

  • @danaziokanjadza6147
    @danaziokanjadza6147 5 ปีที่แล้ว +1

    Ambuye andichitile chifundo