Umboni wa a Twaibu pa 8 July 2023 ku Blantyre - "Zinthu zomwe satana samafuna anthu adziwe"

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024
  • Mverani zinthu zodabwitsa ndi zobisika zomwe satana samafuna anthu atadziwa. Nthawi yatsala pang'ono. Tiyeni tikonzekere kubwera kwa Ambuye wathu Yesu Khristu mu mkwatulo womwe watsala pang'ono kuchitika.

ความคิดเห็น • 68

  • @tintophiri2312
    @tintophiri2312 9 หลายเดือนก่อน +2

    God of Mercy save my life.😭😭 Thank you for sending salvation for my life tthrough this great man of God. 🇿🇲

  • @BeautyMtambo
    @BeautyMtambo 13 วันที่ผ่านมา +2

    Mulungu adzikudalitseni baba Twainu apitilize kikuwulilani zaku mbwamba

  • @user-vl5go3nr2v
    @user-vl5go3nr2v ปีที่แล้ว +3

    Yehova awadalise mr twaibu nthawi zonse...koma otumizanu chonde musaiwale kutitumizilaso zinthu tenizo tiziwekoso nafe

  • @RyleChole
    @RyleChole หลายเดือนก่อน

    Satana amalamulira dziko lonse lapansi koma Mulungu amalamulira oyera mtima onse Masalimo 23 amati odala omwe Yehova akhala m'busa wao, amatero malemba

  • @ShieldHenryHills-nm2wt
    @ShieldHenryHills-nm2wt 9 วันที่ผ่านมา +1

    Ndine APOSTLE SHIELD HENRY PHIRI ku Zambia PETAUKE district. Ndine ofunitsitsa ku kumana ndi inu mtumiki wamulungu....ndilaka laka kwambiri mudzina la yesu khristu..mundi thandiza bwanji?

  • @ArnoldKamanga-wm7gc
    @ArnoldKamanga-wm7gc 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu akudalitseni brother Twaibu

  • @user-wb5vp7km4z
    @user-wb5vp7km4z 10 หลายเดือนก่อน

    Amen amen abuye akupatseni mavumbulutso ochuluka mwandichotsa Pena mwandika Pena kumwaba kulemekezeke kwambili 🙏🙏🙏👏

  • @EmilyManase-fz6cv
    @EmilyManase-fz6cv ปีที่แล้ว

    Amen, Mulungu ndi okoma mtima ndi anthu ake Ndipo amawawululira zi nsisi zake kudzera mwa atumiki ake. Mulungu akudalitseni mtumiki.

  • @DanielMbuzu-sf4ey
    @DanielMbuzu-sf4ey ปีที่แล้ว +2

    Atsogoleri uthenga wanu umandizindikilitsa za ntchito ya ikulu kwambili yomwe okhulupilira ambuye Ali nayo pa dziko lapansi lino

  • @user-nx8gy8lq4q
    @user-nx8gy8lq4q ปีที่แล้ว +2

    Palibe chobisika pamaso pa mulungu ambuye adzikutsogolelan thawi zonse atsogoleri kuti tiphunzile zambili

  • @user-mo3rz4zp8e
    @user-mo3rz4zp8e 8 หลายเดือนก่อน

    Thank you for exposing the devil, may God protect you

  • @user-cv1ob9uo1t
    @user-cv1ob9uo1t ปีที่แล้ว

    Ndife amwayi tingompempha mulungu apitilize kukutetezani mtumiki wa mulungu Mr twibu

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh ปีที่แล้ว +1

    Amen mtumiki
    Tikudikira zithu ten
    Mutidziwitse please

  • @mikebernabechimundi3472
    @mikebernabechimundi3472 ปีที่แล้ว +4

    Amen Christ,,following all the way from Mozambique,Atamandike mu nthawi zonse

  • @papelariareis.e.
    @papelariareis.e. ปีที่แล้ว +1

    This guy he knows more about devils future plans

  • @LontiaZimba-z4d
    @LontiaZimba-z4d 12 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @husseinmoffatt
    @husseinmoffatt ปีที่แล้ว +3

    Zoona Mr twaibu

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 ปีที่แล้ว

    Ulaliki wanu Mr Twaibu siulaliki okha ai komanso ndi chiphunzitso, chenjezo, chidziwitso, ulangizo ndi chitsitsimutso

  • @fapsonbanda3453
    @fapsonbanda3453 ปีที่แล้ว +1

    Amen God help us in Jesus name 🙏🙏🙏

  • @MaryRasmussen-mr4zo
    @MaryRasmussen-mr4zo 10 หลายเดือนก่อน

    Amen
    May God help us all Sir
    God nless you for what your doing thank you for the truth
    Amen

  • @LeonardKantondo-fu9tf
    @LeonardKantondo-fu9tf ปีที่แล้ว

    Amen
    May God help us and protect Mr Twaibu in Jesus Christ

  • @jamesphiri9930
    @jamesphiri9930 8 หลายเดือนก่อน

    Go deeper man of God

  • @jeffmalizan9878
    @jeffmalizan9878 ปีที่แล้ว +1

    Kodi bwanji nthawi zambiri mmakonda kuduliza nkhani mukatero simudzanenaso zathera pomwepa ,tilindi ma lonjezo ambiri ochokera kutinihani Tanu tomwe tumangothera panjira mkudzati mufzapitilizabe nthawi ina yake koma mpaka lero kuliziii

  • @richardchirwa7030
    @richardchirwa7030 10 หลายเดือนก่อน

    Please continue assisting and teaching us of Gods groly

  • @tonyinocent1770
    @tonyinocent1770 11 หลายเดือนก่อน +1

    Blessings

  • @ChiccoChintendere
    @ChiccoChintendere 9 หลายเดือนก่อน

    Hossana ! Hossana! To God Almighty. I would like to beg the WhatsApps link for God teaching through Mr Twaibu Ali, if any.

  • @alexchipanda1669
    @alexchipanda1669 9 หลายเดือนก่อน

    We love u Mr twaibu mulungu akudaliseni

  • @KeffasSimion
    @KeffasSimion 10 หลายเดือนก่อน

    Pepani ndava mokwana ndithu kom 10 zija mwina ngati ndikotheka ndiziveko kuti ndiyendere limodzi nanu pepani thandizani atsogoleri ndine mmodzi wotayika

  • @KeffasSimion
    @KeffasSimion 10 หลายเดือนก่อน

    Amen ndikuvetsera mwachidwii

  • @RyleChole
    @RyleChole หลายเดือนก่อน

    Palibe chipembezo chili mmanja mwa Mulungu

  • @user-cv1ob9uo1t
    @user-cv1ob9uo1t ปีที่แล้ว

    Mwayi umenewu maiko ena alibe woti Ave zisisi za satana koma ife lero ndi Feb

  • @yolandamasaiti-mf8gu
    @yolandamasaiti-mf8gu ปีที่แล้ว +1

    Pitilizani kuti dziwitsa ambuye azikudalitsani..

  • @alicephiri3706
    @alicephiri3706 ปีที่แล้ว

    Amen amen following Mr Twaibu

  • @user-xg9lq3pj8h
    @user-xg9lq3pj8h 10 หลายเดือนก่อน

    Ambuye akudalitseni

  • @samuelnyirongo8965
    @samuelnyirongo8965 ปีที่แล้ว +1

    KEPT UP MR TWAAIB

  • @mauricetayali8041
    @mauricetayali8041 ปีที่แล้ว

    Ambuye mulungu akusungeni a twaibu

  • @user-nz7lj3qk4g
    @user-nz7lj3qk4g ปีที่แล้ว

    Amen ndasunthika nfimawu anu

  • @frankkaipa8925
    @frankkaipa8925 ปีที่แล้ว +1

    Ameeen

  • @user-cb8sp9ip3r
    @user-cb8sp9ip3r ปีที่แล้ว

    Amen powerful uthenga

  • @jeffmalizan9878
    @jeffmalizan9878 ปีที่แล้ว +1

    Mudzaipituliza liti nanga

  • @KeffasSimion
    @KeffasSimion 10 หลายเดือนก่อน

    Koma zasitha moyo wanga ngati pari njila ina chonde tapangani motero

  • @ChikondiKaliza
    @ChikondiKaliza ปีที่แล้ว +1

    Kufutukula zobisika munthu wamulungu

  • @user-ko8qd9wh6f
    @user-ko8qd9wh6f 10 หลายเดือนก่อน

    Amen and Amen

  • @user-ro1yw7op1c
    @user-ro1yw7op1c 8 หลายเดือนก่อน

    Ndisaname mtumiku off ndikhala ndikusatira maumboni anu kuyambira kale ndimakusatani bwino bwino mukufotokoza kwanu in brief munafotokokoza kut before you was a Muslim mpaka munafika pa udindo wa mufut munafotokozanso za makorona angapo oophsya ku chipembezo chomwe munali mzaka zapitazi mukufotokoza kwanu munaphatikizapo za korona wa asilamu mkati kati mommu ndikumamva mukumavomerezanso kut machitidwe ena asilam alibwino kusiyana ndi akhirisitu eg kupempera akachoka kapena akachita chimbudzi malingana ndi ziwanda Zina zonse zimakonda fungo lakuchimbudzi pepani mungafotokozenso paichi kuopa kut ndingataike

  • @husseinmoffatt
    @husseinmoffatt ปีที่แล้ว +1

    Zoonadi Mr

  • @user-mc6tz2yb8s
    @user-mc6tz2yb8s ปีที่แล้ว

    Kp going Mr Twaibu but with the truth

  • @user-xx7xj8br3x
    @user-xx7xj8br3x ปีที่แล้ว

    Thanks mr

  • @ClementDkamwendo
    @ClementDkamwendo ปีที่แล้ว

    Amen🙏🙏🙏

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 ปีที่แล้ว

    Monga mwa funso lanu Mr Twaibu kuti : kodi mungasiye chuma chanu ndikutumikira Mulungu ?? Yankho ndikukhulupilira kuti palibe munthu angatero

  • @preciousmkute4041
    @preciousmkute4041 ปีที่แล้ว

    Following

  • @user-bf1px4nv8d
    @user-bf1px4nv8d 11 หลายเดือนก่อน

    The devil is always liar

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 ปีที่แล้ว +1

    Nkhan zopand tsogl
    Komanso zabodz zokh zokha

  • @AfunikaTembo-ty1qy
    @AfunikaTembo-ty1qy ปีที่แล้ว

    TH-cam

  • @agnes7675
    @agnes7675 7 หลายเดือนก่อน

    AMEN

  • @user-if1kd3kh4d
    @user-if1kd3kh4d 7 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @user-cv1ob9uo1t
    @user-cv1ob9uo1t ปีที่แล้ว

    Mwayi umenewu maiko ena alibe woti Ave zisisi za satana koma ife lero ndi Feb

  • @user-it1kn8ux9g
    @user-it1kn8ux9g 10 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @user-lf5ou9lc4e
    @user-lf5ou9lc4e 11 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @Samyohane
    @Samyohane ปีที่แล้ว +2

    Amen

  • @user-cc4dz5rw3i
    @user-cc4dz5rw3i 10 หลายเดือนก่อน

    amen amen

  • @thirdgenerationmovies710
    @thirdgenerationmovies710 ปีที่แล้ว +1

    Amen

  • @nyanguoipa6996
    @nyanguoipa6996 ปีที่แล้ว +1

    Amen 🙏

  • @muyabasamson
    @muyabasamson ปีที่แล้ว

    Amen

  • @user-pm2bo8vb2z
    @user-pm2bo8vb2z ปีที่แล้ว

    Amen

  • @leonwisikesmwkbyowner
    @leonwisikesmwkbyowner ปีที่แล้ว

    Amen

  • @user-ds9sx4rt4j
    @user-ds9sx4rt4j ปีที่แล้ว

    Amen