ZOOPSA IZI CHAKWERA ZAMUTONG’OLETSA MASO POTI ZIKUMUDIKILA PA ZOMWE WACHITA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 16 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 50

  • @user-co6sc8om5n
    @user-co6sc8om5n 10 วันที่ผ่านมา +8

    M'MALAWI WENIWENI SANGAVOTERE MCP MALAWI CHIKANGAWA PARTY YASATANIC

  • @ChristinaMdeza
    @ChristinaMdeza 10 วันที่ผ่านมา +2

    Abusa muuzeni uyu chikangawa yi Ambuye Yesu akumusiya poyera inu anapanga zoyipa kwambiri. anayiwala kuti maso Ambuye amamuona pamene amapha chilima munthu wosalakwa kom inuyo Ambuye azikutetezani inuyo Abusa❤❤

  • @GeorgeBanda-x6l
    @GeorgeBanda-x6l 10 วันที่ผ่านมา +5

    kumawauza kumene anthu sakuwafuna cz munthu amene anawalowetsa m'boma ndi amene anamupha uja

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 10 วันที่ผ่านมา +7

    Akuti akuyesela zobela ma ballot paper apitisidwa ku south africa kuti azabere 😂

  • @lacksonkim9622
    @lacksonkim9622 10 วันที่ผ่านมา +6

    Kuyankhula Koma uku ❤❤❤❤❤

  • @user-gx8or3yz9u
    @user-gx8or3yz9u 10 วันที่ผ่านมา +5

    Malawi chikangawa party ng'ona partys

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 10 วันที่ผ่านมา +3

    MCP means malawi chikangawa party 😂😂😂

    • @user-ol1hf7ru1v
      @user-ol1hf7ru1v 9 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @blessingsnyalo-rp9ko
    @blessingsnyalo-rp9ko 10 วันที่ผ่านมา +1

    Kuswakuswa koma mwachilungamo😂😂😂😂

  • @user-qf7ko2dd5g
    @user-qf7ko2dd5g 10 วันที่ผ่านมา +2

    Good meditation pastor

  • @AbudulJohn
    @AbudulJohn 10 วันที่ผ่านมา +2

    Ine Sidik Mia ineso anandithandizapo ndili kwa Ngabu mpaka ananditenga ku mpaka ku Walisa farm kukawona anali munthu wa bwino kwambili

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje 10 วันที่ผ่านมา +2

    Ndipo apa nde anapanga mistek yaikulu anyatu

  • @user-ws9sy7pp3w
    @user-ws9sy7pp3w 10 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi Chikangawa Party nick name yake (ng'ona party)

  • @BenjaminGasten
    @BenjaminGasten 9 วันที่ผ่านมา +1

    DPP vote yanga

  • @AngolanChinga
    @AngolanChinga 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mr shumba musalile even ifey tikulila paka pano za chipani chakupha ngat chimenechi mulungu ndiwamkulu akuona zimene zikuchitik chakwela 2025 akuchok Mu Mphavu ya mulungu inshaallah

  • @Thewarrior7093
    @Thewarrior7093 10 วันที่ผ่านมา +1

    The next government should just deregister MCP for all the crimes they have committed against the people of Malawi and for mismanaging the economy of our country and made Malawi poorer and useless in all of the world

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 9 วันที่ผ่านมา

    Tchera kumwezi nkhanga zaona ,kupezeka kugidwa mwayankhula mwamphanvu Malawi Chikangawa party 😂

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 10 วันที่ผ่านมา +2

    I thank you for such a speech Reverend.I suggest if all religious leaders in Malawi could call H E and discuss how to redress the current problems Malawians are facing.

  • @JohnAssan-dn1he
    @JohnAssan-dn1he 7 วันที่ผ่านมา

    Osaopa pastor mulungu alinanu

  • @ThomsonChipwele
    @ThomsonChipwele 10 วันที่ผ่านมา +2

    Zoona mawu amenewo ineso ndikuti chandelier amalawi osavotela mcp

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 10 วันที่ผ่านมา +3

    Mau amphanvu 🙏

  • @berlz12k
    @berlz12k 7 วันที่ผ่านมา +1

    Anapanga mistake kupha chilima and ambiri ozindikira anamutuluka uyu sangawine olo,anthu Ngati afika kudya chitedze ingawine?akhalamo okhaokha agalu amenewa..mcp 2025 ou”😡💩🦧

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm 7 วันที่ผ่านมา

    Mulungu akudalitseni pa uthenga wanu wachikondi kwa Amalawi

  • @Thewarrior7093
    @Thewarrior7093 10 วันที่ผ่านมา

    Chakwera ali Maso tudzuuuu diso ngati nkhwezule galu wachabechabe oononga dziko lathu la Malawi 🇲🇼.

  • @WillieKalipinde
    @WillieKalipinde 10 วันที่ผ่านมา +1

    😂😂😂 Malawi Chikangawa Party (M.C.P)

  • @juliochiwalo
    @juliochiwalo 6 วันที่ผ่านมา

    Chakwera Mulungu anamusiya kalekale ndi chifukwa chake Malawi ali mmavuto opsa werengani 2 mbiri, 15: vs 1 mpaka 5

  • @KaliyapaSeeter
    @KaliyapaSeeter 10 วันที่ผ่านมา +1

    Nde mwati mcp ikuyimira chani😂😂

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 9 วันที่ผ่านมา

    Palibe angavotere mcp palibe

  • @rhodamaunge-uq5dz
    @rhodamaunge-uq5dz 10 วันที่ผ่านมา

    Amen pastor

  • @Donald378
    @Donald378 9 วันที่ผ่านมา

    Ine wamangochi kom sindingavotele mcp

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali 10 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤❤ kung'alila kwabwino ndithu ❤❤❤ Mr chikangawa azipita kukasiya

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mdipo asatana awq

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 9 วันที่ผ่านมา

    Masamu ake akugwiritsa ntchito am'ma 60s

  • @user-gm9xj1wc2m
    @user-gm9xj1wc2m 10 วันที่ผ่านมา +1

    Ok bwana

  • @MalizeniOliviaBridan
    @MalizeniOliviaBridan 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mawu mfiti zimenezi

  • @user-ol4cf2oh5u
    @user-ol4cf2oh5u 10 วันที่ผ่านมา

    Anangowona kuzichita 💔 akanadzapikisana ndi chilima or akanadzathesa gwilizano myb akanawina

  • @ernestphiri5507
    @ernestphiri5507 10 วันที่ผ่านมา +1

    Abusa mukunena zoonadi

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k 10 วันที่ผ่านมา

    APM my vote

  • @MussaChilembwe
    @MussaChilembwe 10 วันที่ผ่านมา

    Mcp thawi yawo yatha panakakhala kuti ali ndi umuthu anakasiya pansi kuti ena apitilize kuti zithu zibwerele ngati kale koma Allah akuona zikuchitikazi ndiye thawi yake ya Allah ikakwana palibeso kususa ma comrade tikuvuka kwambili ndi dziko rathu

  • @jamessheki4293
    @jamessheki4293 10 วันที่ผ่านมา

    Ukakhala oipa anthu amakuthawa

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 6 วันที่ผ่านมา

    Komaso no one can join mcp ngati allowance awa ulendo basi

  • @philipoga2401
    @philipoga2401 10 วันที่ผ่านมา

    mboli ya make chakwera or sidik miya anachita kumuphaso sinali corona

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti 10 วันที่ผ่านมา

    This is 2024 Century.

  • @rhodamaunge-uq5dz
    @rhodamaunge-uq5dz 10 วันที่ผ่านมา +1

    Ku mpoto
    0%

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 10 วันที่ผ่านมา

    Ndipo malawi weniweni sangachongele mcp aataaaa kupha 2 much

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 10 วันที่ผ่านมา

    Mulungu walankhura kudzera mwa mtumiki wake 😅😢

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 10 วันที่ผ่านมา

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤸🤸🤸🤸🤸kumeneko M C P

  • @EnockMunthali
    @EnockMunthali 10 วันที่ผ่านมา

    Ali ndi manganya yekha

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 10 วันที่ผ่านมา

    Ulemu wanu mung'aluleni basi

  • @KenMalasa
    @KenMalasa 10 วันที่ผ่านมา

    Km mcp abalee