Dr Bingu Wa Mutharika best advice to malawians; Malangizo a Bingu kupita kwa amalawi.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 31 พ.ค. 2022

ความคิดเห็น • 69

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj หลายเดือนก่อน +2

    Anthu abwino sakhalisa paxiko I remember you Bingu Mtharika I miss your voice and incouge

  • @selectorbillbox3505
    @selectorbillbox3505 2 ปีที่แล้ว +9

    ZIMANGOONA KUVUTA BUT THIS MAN USED TO INSPIRE ME A LOT
    MAY YOUR SOUL CONTINUE RESTING IN PEACE
    WISE TALKING

  • @seanmsutu6848
    @seanmsutu6848 ปีที่แล้ว +7

    This was a real man to govern Malawi

  • @chisomombeta6446
    @chisomombeta6446 6 หลายเดือนก่อน +2

    Ulemelero wa malawi unachoka basi ....Bingu was q blessing and special gift to us malawians koma tinali mu m'dima.May forgive our country and give us someone like him😮

  • @sakingomane5819
    @sakingomane5819 2 ปีที่แล้ว +15

    He was best President ever in our loved country Malawi

  • @brinobota6637
    @brinobota6637 11 วันที่ผ่านมา

    The best president ever in Malawi, continue resting in peace Pro Bingu Wa Munthali. It's my prayer that God should give us a wise n strong president

  • @Slyvester-zs6ww
    @Slyvester-zs6ww 25 วันที่ผ่านมา +2

    M'dima sumadziwa kut kuwala kuli pomwepo.
    This man, anali muongoli wa dziko lino la malawi.
    Koma dziko silinadziwe.

  • @brinokasekani7295
    @brinokasekani7295 2 ปีที่แล้ว +5

    We lost such a great and visionary leader in him. May you still continue resting well Pro Bingu Wa Muthalika

  • @tingo3155
    @tingo3155 ปีที่แล้ว +5

    I'm one of a Malawian who was inspired by Bingu,
    May his soul continue to rest in peace

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 ปีที่แล้ว +2

    I will mourn and celebrate Bingu Wa Mutharika for the rest of my life he was a good and wise president..RIP MY PRESIDENT.

  • @AlexisKantondo
    @AlexisKantondo 6 หลายเดือนก่อน +1

    We're still crying for you late Genius Bingu

  • @ririvilla1423
    @ririvilla1423 ปีที่แล้ว +3

    True leader we miss u

  • @aaronkachipeso3586
    @aaronkachipeso3586 2 ปีที่แล้ว +4

    Kuno chomwe amadziwa atolankhani ndikufalitsa zoipa zokhazokha osati zabwino kkkkkkk apapa am glad kuti Bingu anawatsukuluza hvy
    And ichi ndichidziwitso chimodzi kuti atolankhaniso nawo ali patsogolo pakubwezeretsa chitukuko cha dziko lino pa mmbuyo.
    mutha kudabwa inu kwaona atolankhani omwewo lero akumutamanda Bingu kuti anali mtsogoleri wabwino

  • @xanderotc
    @xanderotc 2 ปีที่แล้ว +5

    We had a true leader. Honest and caring character.

  • @bilali869
    @bilali869 ปีที่แล้ว +2

    great leader ever n ever

  • @goodwellchanunkha1971
    @goodwellchanunkha1971 2 ปีที่แล้ว +3

    A leader with fatherly heart and love. Keep resting easy ngwazi

  • @robertnyasulu1384
    @robertnyasulu1384 ปีที่แล้ว +1

    Ndinadziwa how great he was atamwalira. You the best president we ever had

  • @RICHARDA.Y.SAKALI
    @RICHARDA.Y.SAKALI หลายเดือนก่อน

    l proud of speeches of this formar president.Rest in peace boss.

  • @felixsaidi6715
    @felixsaidi6715 2 ปีที่แล้ว +5

    We miss our best president ever In Malawi 🇲🇼

  • @imranmposa2788
    @imranmposa2788 2 ปีที่แล้ว +2

    That was the best advice from bingu

  • @dominicmphepo-jk8lk
    @dominicmphepo-jk8lk 7 หลายเดือนก่อน +1

    We had genius
    But God love him most
    Keep on resting well our hero

  • @benjaminkampiyon1130
    @benjaminkampiyon1130 2 ปีที่แล้ว +2

    This dude was genius indeed

  • @williamdaisithom5913
    @williamdaisithom5913 2 ปีที่แล้ว +4

    Good speech that people with good confidence will follow it forever, he died for body only but spirit for him still alive. Your body rest in peace almighty name of Jesus Christ Amen
    🕊📖.............✍

  • @michealmussah261
    @michealmussah261 ปีที่แล้ว +2

    We really miss him now

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 ปีที่แล้ว +1

    Amalawi Amapangirana Nsanje Mpaka zaka Zino, Ndimaopa Kupanga Associate Ndi Amalawi Anzanga.
    Amalawi Ndinu anthu oipa kwambili

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 11 หลายเดือนก่อน

    I miss this president and we've never had a president like Bingu wa Mutharika and we'll never have a president like Dr Bingu wa Mutharika in Malawi

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 2 ปีที่แล้ว +3

    Awa ndiwo mawu amawi amalawi kaduka basi chomwe timadziwa😁😁👍

  • @louisbonongwe4864
    @louisbonongwe4864 2 ปีที่แล้ว +2

    We lost such a great Leader

  • @WiseJordan-ds6km
    @WiseJordan-ds6km หลายเดือนก่อน

    Marvelous

  • @kassimjummah3018
    @kassimjummah3018 2 ปีที่แล้ว +2

    Abingu muwuse muntendele 😭😭😭😭

  • @allanmakwiti5145
    @allanmakwiti5145 2 ปีที่แล้ว +3

    Inu aBakili News Channel mukuamva malangizowo?

  • @glorytchezan5157
    @glorytchezan5157 2 ปีที่แล้ว +2

    Rest well Mr bingu

  • @hopeskafumbiphiri6011
    @hopeskafumbiphiri6011 ปีที่แล้ว +1

    wow ine kumva kukoma

  • @owenmalongo4116
    @owenmalongo4116 ปีที่แล้ว

    Only the one and the best president in our country anaphuladi dziko pamoto may continue rest in peace 😭😭😭

  • @hendrixkaitano4242
    @hendrixkaitano4242 2 ปีที่แล้ว +1

    Wiseman

  • @user-ux6cw2gq2n
    @user-ux6cw2gq2n 3 หลายเดือนก่อน

    We will never to forget sir🙏🙏🙏🙏🙏💔

  • @sab311
    @sab311 ปีที่แล้ว

    On point

  • @FatimaMwanyali
    @FatimaMwanyali 25 วันที่ผ่านมา

    Kodi jelouse mupita nayo kit?
    ❤❤❤❤❤

  • @chrismakhela7133
    @chrismakhela7133 ปีที่แล้ว

    We loss ...RIP Father Muthalika

  • @levisonmthawanji4232
    @levisonmthawanji4232 2 ปีที่แล้ว +2

    RIP

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 2 ปีที่แล้ว +1

    Zinali Mbubzi za aKAZITAPE.

  • @ibrahimjim281
    @ibrahimjim281 2 ปีที่แล้ว +2

    Munthuyu amaona kut akumutaisa nthawi 😂😂

  • @longimtimabii1017
    @longimtimabii1017 5 หลายเดือนก่อน

    Sunga yelekeze ndi manyi ali lelowa.awa anali wakulu

  • @anifoiuene6301
    @anifoiuene6301 2 ปีที่แล้ว +3

    Takutoperani a MCP

    • @elufedavid3788
      @elufedavid3788 2 ปีที่แล้ว +1

      Tavelani malangidzo

    • @aaronkachipeso3586
      @aaronkachipeso3586 2 ปีที่แล้ว

      @@elufedavid3788 ndipo ugalu wakesotu nde winawina nanga zugwirizana bwanji ndi MCP apa? Uchimidzi

  • @aubreychuma5449
    @aubreychuma5449 2 ปีที่แล้ว +1

    Madala kuyionera patali game

  • @user-ne9qn5nm9d
    @user-ne9qn5nm9d 10 หลายเดือนก่อน

    Inuyo Munali Tate weniweni, Rest in peace

  • @user-ig7dv8rp7r
    @user-ig7dv8rp7r 5 หลายเดือนก่อน +1

    Anali tate wa nfuko

  • @anoldkapolo4493
    @anoldkapolo4493 ปีที่แล้ว

    Mzimu wake uziusa mumtendere osatha munthu oyipa uyu mafuta atavuta mkumati kagone pamsewu. Aaah kunapita mfiti

  • @peteruko
    @peteruko 2 ปีที่แล้ว

    Am dying 😂🤣

  • @leviticusbonfancio
    @leviticusbonfancio 7 หลายเดือนก่อน

    Awa adali am'dala bambo

  • @innocentmanyera1861
    @innocentmanyera1861 ปีที่แล้ว

    Wa dpp iwe hiyaaa

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 ปีที่แล้ว

    I like Donald Trump's stand on CNN, He calls them fake news kkkkk

  • @enockthomasloyidi4914
    @enockthomasloyidi4914 2 ปีที่แล้ว

    🤣🤣🤣🤣

  • @gastahlubi
    @gastahlubi 2 ปีที่แล้ว +5

    ndine wa mcp koma pa bingu hmmm zinali nkhani zina mpaka 2009 mutu wanga unapenga bingu ngati anatumidwa ndi ambuye kudzatilamulira moti pazoipa zake zimene anthu amanena ine ndimaziika m'manja mwa mulungu coz satana anakwanitsa gawo lake kutitseka maso ndikumadana ndi utsogoleri wangilo

    • @gastahlubi
      @gastahlubi 2 ปีที่แล้ว

      koma osati zinazi kungoonjezela kuipitsa mbili yake koma sindikukhulupira kudzaonaso tsogoleri ngati ameneyu ngakhale kamuzu sangafike pamzelu zake rest in piece baba

    • @cadohjabu5565
      @cadohjabu5565 ปีที่แล้ว +1

      Tulukani Mcp man mutaya nthawi

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 9 หลายเดือนก่อน

      Zooonadi zokhazokha satana ndiwochenjera koma pomaliza💔💔

  • @imaanasibu7267
    @imaanasibu7267 2 ปีที่แล้ว +3

    Wiseman

    • @amoschilimba4377
      @amoschilimba4377 ปีที่แล้ว

      Nthito za manja ake ndio nkhani lero Anasiya zonse phazi ndi mulomo Mzimu wake ukuusa ndi mtendere