Ndichikhala Chilima Sindikanalola Kuti Mulandu Ungotha - Bon Kalindo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 4 พ.ค. 2024
  • As News is circulating that corruption charges against Vice President Saulos Chilima are to be dropped, Bon Kalindo says it would be wise for the Vice Presidenrt to not allow this happen becuase it might do more harm than good to his public image.
    Pomwe nkhani ikumveka yoti milandu ya katangale yomwe wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Saulos Chilima idanenedweratu ichotsedwa, Bon Kalindo wati chingakhale chanzeru kwa wachiwiri kwa pulezidenti kuti asalole kuti izi zichitike chifukwa zitha kuvulaza kwambiri mbiri yake.
    #malawi

ความคิดเห็น • 53

  • @WilsonLimited-fh1mz
    @WilsonLimited-fh1mz 27 วันที่ผ่านมา +4

    Chakwerayu akufunika bomba basi apo ai ndiye tichita kupha ndi miyala ngati stefano

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g 27 วันที่ผ่านมา +3

    Kalindo is a great and intelligent man Malawians let's support this man he is very wise

    • @GospelSoldiers-sr7np
      @GospelSoldiers-sr7np 27 วันที่ผ่านมา

      Aliyense yemwe akumadana ndi kalindo sakonda dziko,kalindo akusegura amalawi maso🎉🎉🎉

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 27 วันที่ผ่านมา +3

    Ulemu wanu Malume. Chilima anayenera kukana kuti mulandu wake uthetsedwa kufikira chilungamo chioneke

  • @user-pw2dq1yw4b
    @user-pw2dq1yw4b 27 วันที่ผ่านมา +2

    Mr chakwela akuziwa chimene akufuna kuthetsela mulandu ndichani chakwela nduwokubatso

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 27 วันที่ผ่านมา +3

    Anthuwa onse ndi akuba, apa akuberekana kumbuyo chakwera is also involved.. 💔💔

    • @robertrichman9376
      @robertrichman9376 27 วันที่ผ่านมา

      That's why wathesa mulandu, mbava zokha zokha izi

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillie 27 วันที่ผ่านมา +2

    Athuwa ndyakuba ndithu chilima mulungu amuyendele padeladela chifukwa naye ndiwakuba wazuza a Malawi kwabasi

  • @mosesmaxwell2737
    @mosesmaxwell2737 23 วันที่ผ่านมา +1

    Tikufuna akulamulireso paja ndi wachigawo chapakatitu Chili mayo, ndipo udakalira iweyo sunati

  • @PrinceJamali-ch2sj
    @PrinceJamali-ch2sj 27 วันที่ผ่านมา +2

    Bon kalindo umakwana ndipo malibeso

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 27 วันที่ผ่านมา +2

    Umatha born ndpo umamusengula mutu muthu ngti ali akumva achilima amve inu lero ndiinu advance wako ndpo amve ngti samva azamva ataphikira muphika

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillie 27 วันที่ผ่านมา +1

    Abon musayambepo kt mukhale mbali yachilima ayi mukaymba izi mutitayisa hope painu. Khalani wachilungamo ndipo chilungamo chanu chizakhuthandiza kt mukhale pule coming years

  • @graciousstanford5228
    @graciousstanford5228 27 วันที่ผ่านมา +1

    More fire 🔥🔥🔥

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 27 วันที่ผ่านมา

    Zabodza zimenezo, kuti komwe Munthu woniziridwa anayamba wanena kuti ayi ndikufuna mukandiyimbe Milandu?

  • @ToothyWebb
    @ToothyWebb 27 วันที่ผ่านมา

    Ndikuona ngati Chilima is tired of everything. At this point he just wants to live peacefully. If it’s money nde he has enough moves going on. Long live SKC!

  • @BandaEllias
    @BandaEllias 26 วันที่ผ่านมา

    More fire more fire

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v 27 วันที่ผ่านมา

    Munthu woti akuziwa kuti anachitadi angakane kuthesa mlandu? Kuteloko Chilima wasangalala kwambili.

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e 27 วันที่ผ่านมา

    Milandu siola tionesana September next year mr chilima

  • @user-oe6hy4fy5v
    @user-oe6hy4fy5v 27 วันที่ผ่านมา

    Zakhala bwino coz chilimayo akakana kuthatsa mlandu zitenga nthawi ife tikufuna akhale pule mmalawi muno

  • @Joydee1999
    @Joydee1999 27 วันที่ผ่านมา +1

    vuto bushiri safuna kuzaima ngati president

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 27 วันที่ผ่านมา

    Chilima next president 2025

  • @user-dj1zs3eo4f
    @user-dj1zs3eo4f 27 วันที่ผ่านมา

    Yes ask Mr cassim chilupha this malawi ,

  • @Moses51
    @Moses51 27 วันที่ผ่านมา

    The DC bon kalindo

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 27 วันที่ผ่านมา

    Tamenyelani ufulu anthu osauka basi nanga mwayambaso kumenyela ufulu chilima

  • @user-cz5xq8ct7m
    @user-cz5xq8ct7m 27 วันที่ผ่านมา

    Advisor was Chilima ndiwe Bon Kalindo ndipo iwe Chilima ukatsata zimenezi,BOMA iri udzalamula tsikulina.

  • @JohnRasheed
    @JohnRasheed 27 วันที่ผ่านมา

    Boni kalindo the D c

  • @user-pf5hu2pd2b
    @user-pf5hu2pd2b 27 วันที่ผ่านมา +1

    The DC

  • @andrewmtendere3167
    @andrewmtendere3167 27 วันที่ผ่านมา

    Machine

  • @user-vl8uw8mc3u
    @user-vl8uw8mc3u 27 วันที่ผ่านมา

    Onsewa ndi mbava zokhazokha so zikuopana kuti angaululanepo apa😂😂😂😂😂

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 27 วันที่ผ่านมา

    Mmene ndimamuonela chilima ndi mfana ofoila kwambili, izi kwa iye zatha bsi why ati ndi mfana oganiza bho za ziiiii . Asayankhuleso za nonsense zokhuza mlandu wake. Amakanika kuyankhula za mavuto womwe amalawi akukumana nawo , ndie akatiuza za mlandu wake za chani, anthuwa ndi amozi palibepo wabwino apa

  • @tasmania527
    @tasmania527 27 วันที่ผ่านมา +2

    That's why ndiwe mbuli iwe Bon kalindo because you don't understand the incompetence of Martha Chizuma based on how she presented and compiled the evidence in order to strengthen the state's case way back from the beginning. The problem with you Kalindo is that you think the top leadership has a hand in this decision without understanding that the office of Director Of Public Prosecution(DPP) has the prerogative to discontinue a case that lacks validity and stems from insufficient evidence, and that any evidence collected illegally can't be submissive in a court of law. Chizuma rushed to do what wasn't supposed to be done, hence the need to discontinue the case. So kalindo, please do not pause as a benevolent advisor to Saulos Chilima because you lack the understanding of the whole case. You are just a Copycat of what was debated on a Hot Current program of Times Television, and you want to exhibit some wisdom out of that program. Presenters of that Hot Current program of May 5th also lacked understanding the reasons behind the discontinuance of Chilima's case, but showed emotion and a biased approach to the same. Kalindo please shut up because you know nothing but ranting.

    • @awardjafar2928
      @awardjafar2928 27 วันที่ผ่านมา

      Acb singamange vice president chakwera asakuziwa

    • @tasmania527
      @tasmania527 27 วันที่ผ่านมา

      @@awardjafar2928 You don't know what you're talking about. ACB gets consent from DPP( Director Of Public Prosecution) who is independent of the executive. The president only follows proceedings thereafter , but has powers to offer clemency after conviction.

    • @BladesBullets-pu5uw
      @BladesBullets-pu5uw 27 วันที่ผ่านมา

      Mukamva izi muzimwa madzi ambiri zimathandiza, achipatala adatero, mqtupi odzadza mafutawa sachedwa kulefuka. Maka ukafuna kukonza zinthu ngat izi.

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g 27 วันที่ผ่านมา

    Mukulakwitsa chifukwa mulanduo siwanu musaoneke ozindikila ndinuo musireni mwiniwake aganizepo mofatsa osalankhula ngati mwamuona kuti chilima ndichitsilu

  • @anniedennis7127
    @anniedennis7127 27 วันที่ผ่านมา

    Non Kalindo , was Chilima found huilty of theft by the court of law ?

    • @hastingskaira324
      @hastingskaira324 27 วันที่ผ่านมา

      And even I Chilima declines the discharge, the DPP still has the authority to discontinue the case....without chilima's consent

  • @KondwaniKeniyasi
    @KondwaniKeniyasi 27 วันที่ผ่านมา

    Timakunyadira DC

  • @user-jb5hr4rz2s
    @user-jb5hr4rz2s 27 วันที่ผ่านมา

    Chilungamo chanu timakondwera nacho ife osauka

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 26 วันที่ผ่านมา

    tha DC😂😂😂😂😂😂...NTHAWI YA GYM😂😂

  • @user-pi8gu3zw4f
    @user-pi8gu3zw4f 27 วันที่ผ่านมา

    Chakwela akuopa kt wapatsindwi angaulule wapadzala

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillie 27 วันที่ผ่านมา

    Abon nayo asamale asakhale kumbuyo kwachilima ayi

  • @PSTPerivoli-xd1ot
    @PSTPerivoli-xd1ot 27 วันที่ผ่านมา

    iweyo kalindo ndiiiwe waphuma lopusa kwambiri that's why umasusa zinthu lero mawa nkumavomeleza nkhani yomweyo! suuziwa zimene uli ...sungakhale chilima ndipo sungamake pachilimaa that's why after all insults none answers you because they use 'kumenyana ndi wamisala nonse mumaoneka amisala'. onse omwe umaanyoza samakuyankha to avoid foolishness!! amene amakusapota iwet mmmmm kkkkkkk😂😂😂😂 ife tinakutuluka kalekale!! olo Mandela anamangidwapo but still he was voted into power!!! uzipaanga zakozo tizingokuyang'ana

  • @JailosiMussa
    @JailosiMussa 27 วันที่ผ่านมา

    Panyapako

  • @LacksonZungulila
    @LacksonZungulila 23 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk ok

  • @JailosiMussa
    @JailosiMussa 27 วันที่ผ่านมา

    Mwayamba ndale za a chilima Mr bon kalindo

  • @TrysonChimenya4-fm8nt
    @TrysonChimenya4-fm8nt 27 วันที่ผ่านมา

    Our Lovely Malawian Redeemer and wise man Kalindo, keep the fire burning

  • @OliverChimsewu
    @OliverChimsewu 27 วันที่ผ่านมา

    Mr bon kalindo ,if the case has no mature evidence there's no need to continue with the case.and also bringing false information to the case is also illegal.mr chilima is innocent man.

  • @henryhenry6632
    @henryhenry6632 27 วันที่ผ่านมา

    Dzimachende dzako bon mathanyula

    • @WilsonLimited-fh1mz
      @WilsonLimited-fh1mz 27 วันที่ผ่านมา

      Tchende lamako phwala lako

    • @henryhenry6632
      @henryhenry6632 27 วันที่ผ่านมา +1

      @@WilsonLimited-fh1mz pamtumbo pamako nachende iwe , dzi ma refugees dzothawa nkhondo ku Mozambique

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 27 วันที่ผ่านมา

    I don't trust any politician in Malawi

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 27 วันที่ผ่านมา

    Another problem ndiyokuti us people we don’t differentiate between stealing and bribery.
    Those are two different things.