APM Sanaluze Zisankho Mu 2019 Ndi Mu 2020 - Innocent Mutholo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 พ.ค. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, says that in his opinion, when he analyses the number of votes cast for APM in 2019 and 2020, APM won the election free and fair.
    Pa Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, wati malinga ndi maganizo ake, pamene amasanthula mavoti a APM mu 2019 ndi 2020, APM adapambana pachisankhocho mwaufulu.
    #malawi

ความคิดเห็น • 103

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +15

    Apapa chofunika tilape mulungu akhululukile Malawi chifukwa chakwela akadapanda kulamulila dziko la Malawi dziko la Malawi kukanakhala khondo yoopya chifukwa athu amafuna chakwela kwambili ndipo mulungu adalola kuti ateteze Malawi kusakhale khondo koma chakwela alamulile kuti athu adziwe kuti sakwela si muthu oyenela kutumikila dziko ndipo amaene amafuna chakwela aona okha kuti chakwela si muthu

    • @chrisneySwanepoel-yu5vd
      @chrisneySwanepoel-yu5vd หลายเดือนก่อน

      Ndiye anthu akalore kut munthu mmodz yekha galunso ndiwuyo akabwerese nkhondo

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน

      @@chrisneySwanepoel-yu5vd ambuye atithandize

    • @TopoTopo-bm4vw
      @TopoTopo-bm4vw หลายเดือนก่อน

      Zowonadi

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน +5

    Uku ndiye kuyankhula kwenikweni kwas chilungamo .....
    Mr game changer ayi ndithu mumaziwa kuyankhula kwambili

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t หลายเดือนก่อน +2

    Very true,amalawi avutika mokwaila,chifukwa cha adindo anjiru,mwaona zimene amapanga Mulungu, disorganized of Ministers chifukwa mulungu anakwiya,zonsezo Mulungu akuona,tionana 2025 sitilola zopusa zilizonse kudzikolanthu la Malawi

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 หลายเดือนก่อน +2

    I by myself personally I agree with this man, game changer he is 100%right, anaba boma a tonse alliance,

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g หลายเดือนก่อน +2

    Zoonad kwambiri Mr. Gama changer💪💪

  • @MorrisMapiri
    @MorrisMapiri หลายเดือนก่อน +1

    50+1 must be abolished

  • @FelixMatebule
    @FelixMatebule หลายเดือนก่อน

    Uku ndiye kukamba Mr game changer continue fighting for Malawi, Malawi open your eyes

  • @PhilipMatolino
    @PhilipMatolino หลายเดือนก่อน +2

    Im agree with you game changer

  • @yohanedaudi1740
    @yohanedaudi1740 หลายเดือนก่อน +2

    Very true

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 หลายเดือนก่อน +3

    Koma chakwera mulungu akuwone Malawi panopa wukuvesa chisoni Kuti wudye mavuto okhaokha

  • @user-mm3es3ph7h
    @user-mm3es3ph7h 12 วันที่ผ่านมา

    Come on Brother man game changer.

  • @user-jj7oz4lo9t
    @user-jj7oz4lo9t 27 วันที่ผ่านมา

    I agree with you Game changer🎉

  • @JMB804
    @JMB804 หลายเดือนก่อน +1

    God remember us🙌🏾

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka7486 หลายเดือนก่อน +1

    Manyaka aboma...mbuli zenizeni zankhanza

  • @user-pt5wn7nu1d
    @user-pt5wn7nu1d หลายเดือนก่อน +2

    Tikufuna anthu ngati inu

  • @user-xh1ve5ym3l
    @user-xh1ve5ym3l หลายเดือนก่อน

    Zowona big brother 🙏💕♥️

  • @WitnessMaulidi
    @WitnessMaulidi 25 วันที่ผ่านมา

    Osawopa Bwana tili nanu

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 23 วันที่ผ่านมา

    Gooooio !!!!!

  • @user-pj3qi7gb3s
    @user-pj3qi7gb3s หลายเดือนก่อน

    Keep it up brother

  • @chrischiwere7279
    @chrischiwere7279 หลายเดือนก่อน +2

    Zoonadi zolanda

  • @spargomw
    @spargomw หลายเดือนก่อน +2

    Ma Judge aku Malawi ndi adyera, amagwira ntchito akuyang'ana Umphawi wawo😂😂😂😂😂. Alipo oweluza wa Chilungamo ndiye Mulungu basi.Ma judge nawoso akayankha Milandu pamaso pa Mulungu.Kazilandiran ndithu ma Envelope'wo nd zomwe zikakhale Mboni zanu kumwamba

    • @timothymhone2340
      @timothymhone2340 29 วันที่ผ่านมา

      Ngwira tnchito akupasa ndalama msatiputsitsepo apa

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 23 วันที่ผ่านมา

    And God remains big judge even if earthly judges rule otherwise

  • @LovemoreSalima
    @LovemoreSalima หลายเดือนก่อน

    Ndizoona. Anaberadi

  • @MikeTheu-ic2dt
    @MikeTheu-ic2dt 24 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤ zowona DPP Vot kujoni Kuno kwatopesa mwina tingabwere kwa2

  • @user-gn4mx2es3k
    @user-gn4mx2es3k 11 วันที่ผ่านมา

    Totally true

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 หลายเดือนก่อน

    God bless you malawi wafika pa Zimbabwe lelo 2025 kumvota no ID ngati akufuna dzimenedzo polembetsa mamvoti popo pakakhale elembetsa ma ID chilinga aleyetse atsalephele kumvota chifukwa cha alibe ID dzikalepheka apo bolani vote ilepheleke adzilamula popanda kumvota kutsiyana kuti atibele tikuwona Maso anthu alephela chimene akufuna adzilamulilbe chiyani kuwopa mulandu bwanji

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 หลายเดือนก่อน

    That judgement was not fair indeed

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y หลายเดือนก่อน

    Fire 🔥🔥 plus 💪💪

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp หลายเดือนก่อน

    Kunena soona malawi wata boma lamalawi rochimtisa manyasi chivukwachani kumalawi kukukanika 🇱🇾😭

  • @user-gn4mx2es3k
    @user-gn4mx2es3k 11 วันที่ผ่านมา

    Alekeni athana okhaokha a tonse alliance wo. Ayamba kale.

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 27 วันที่ผ่านมา

    💪💪💪🔥🔥🔥

  • @JosephMwambe-rz2oy
    @JosephMwambe-rz2oy 25 วันที่ผ่านมา

    Zoona zimezo

  • @juliochiwalo
    @juliochiwalo หลายเดือนก่อน

    Ngakhale mayi Jane Ansah anenanso kuti APM ndi amene anawina ndipo chisankho chinayenda bwino

  • @MonicaChunga-wg6xz
    @MonicaChunga-wg6xz 22 วันที่ผ่านมา

    Mutichitire chifundo mulungu pautsogoleri uwu

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c หลายเดือนก่อน

    TIZALOWA AMBIRI PAMSEU

  • @user-oq7hi3hd4p
    @user-oq7hi3hd4p หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q หลายเดือนก่อน

    Chulungamo ukuyenda ngati madzi okumva wamva osamva asamve ndipo tikumvutika kwambiri kuno ku malawi chifukwa cha MCP Chakwera Chakwera ndi Chilima UTM 😢😢😢 Abuye chitanawoni anthu amenewa

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no หลายเดือนก่อน

    💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t หลายเดือนก่อน

    True,

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr หลายเดือนก่อน

    Mulungu awalange ma Judge amenewa.

  • @BistonNjobvu
    @BistonNjobvu หลายเดือนก่อน +1

    Koma antnhu amaziwa kutsata nkhani

  • @MasiyeDayton
    @MasiyeDayton หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkk game change ❤

  • @FranklinNdovi
    @FranklinNdovi 17 วันที่ผ่านมา

    Two blind persons can not lead each other properly for both of them are unable see what is ahead of them.

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 23 วันที่ผ่านมา

    Eeeeeeee Apm anaberedwa

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c หลายเดือนก่อน

    Achule awa achoka basi tizikavota ngati amalawi zoona ndithu

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 23 วันที่ผ่านมา

    Speak Game changer!!!!!?

  • @IssaKapalamula
    @IssaKapalamula 21 วันที่ผ่านมา

    Munthuyo ndi sapota wa dpp, ndiye mukuona ngati anganene za nzelu?

  • @BensonMalaulo
    @BensonMalaulo หลายเดือนก่อน

    Mumakwana Mr game changer

  • @user-qm1ri6cr6w
    @user-qm1ri6cr6w หลายเดือนก่อน

    Zen zen

  • @LivielMabvuto
    @LivielMabvuto 6 วันที่ผ่านมา

    Kwambiri kwake aliyenxe amadziwa kut APM anawina

  • @NicholasJames-cb7du
    @NicholasJames-cb7du หลายเดือนก่อน

    Big man bwanji simutumiza ma audio a dj munyanane pepani ngat ndalakwisa kufusa

    • @nyasavoicebox
      @nyasavoicebox  หลายเดือนก่อน

      Simukulakwitsa tiyesela tiziponya mungoti tipatsa ka mpata pang’ono

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 6 วันที่ผ่านมา

    Pitani ku court .mbuzi
    Iwe .
    Kulira kwa mbuzi

  • @TracyZiyaya-nz4pd
    @TracyZiyaya-nz4pd หลายเดือนก่อน

    Maka maka chilima mulungu athane nawe ndipo unapanga zonyasa kwambiri ku dziko lino lamalawi

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 28 วันที่ผ่านมา

    Chakwela woyeeee mcp m'paka 2063

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba หลายเดือนก่อน

    Ndiye ngati ukulimbana ndi majaji mbale wanga ndi dpp yakowo mulipamabvuto ndithu amene akutumawo akupweteketsa mbale wanga

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 27 วันที่ผ่านมา

    Kodi ku mcp kuribe wina wazeru

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 หลายเดือนก่อน

    Dzuka Malawi dzuka

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 17 วันที่ผ่านมา

    Galu iwe

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity หลายเดือนก่อน

    Chilungamo chimawawa,Koma mnthu wayankhula chilungamo uyu.

  • @user-xy9vz6jj4u
    @user-xy9vz6jj4u หลายเดือนก่อน

    MA judge pawo pawo ndthu

  • @user-mm3es3ph7h
    @user-mm3es3ph7h 12 วันที่ผ่านมา

    MCP, yawonga zambiri.

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 หลายเดือนก่อน

    Panopa MCP yayamba kuchotsela masiku, DPP yayamba kuwengela masiku

  • @SALIMASSAN-vr8ld
    @SALIMASSAN-vr8ld หลายเดือนก่อน

    Ndip iwey ulem wak srs chilungam chikuveka bwin kwambir

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 หลายเดือนก่อน

    Chi christu nthawi zina sichiri bwino, a chakwera ndi a khristu, zikuchitikazi ndi panichimeti kwa amalawi onse, chakwera ndi tonse alliance ndiakuba anaba boma kuli ndalama kukhala bwanji

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e หลายเดือนก่อน

    Kodi monse munayambila muja kuti mupita pa mseu muzapitapo liti pomwe zinthu zikupitilila kuwonongeka???

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj หลายเดือนก่อน

    Chakwela Ali ngat Hule wa pa saloon yemwe amazazionesa ngt munthu wabwino koma Ali ooopsa kuposa hule yemwe Ali ku Bar

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 หลายเดือนก่อน

    Majaji ndi amene ayika amalawi pamoto

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน

    Mulungu akuwona zonsezi tsiku la 40 lidzawakwanila anthu amenewa

  • @MonicaChunga-wg6xz
    @MonicaChunga-wg6xz 22 วันที่ผ่านมา

    Chitsime chakudya chimaoneka chikaphwa

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน

    Kodi APM , mukunena galu wakupha ma albinos ndi kuba ndi chisale

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 23 วันที่ผ่านมา

      Mukuganiza ngati mwanatu mesa achakwera amamufufuza sanamupedze ndi mulandu uliwose

  • @IssakeMateyo
    @IssakeMateyo หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkk

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm หลายเดือนก่อน

    Mau amphanvu 👊 👊

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p หลายเดือนก่อน

    Zoonadi munthu wamkulu

  • @Chiso2019
    @Chiso2019 หลายเดือนก่อน +1

    A munthalika amagona kwambili that's why analandidwa dziko....nanuso mukuyankhula kwambili koma action zilo

    • @ShabaniKuswere
      @ShabaniKuswere หลายเดือนก่อน

      Kupewa sikupusa anapewa nkhondo

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน

      Ndipo ndizoonadi mulungu samalakwitsa amafuna athu amuone chakwela kuti si muthu oyenela kutumikila Malawi

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 หลายเดือนก่อน

      Umafuna Peter apange nkhondo mbuziwe

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 หลายเดือนก่อน

      A judge amenewo tidzawamanga

    • @SolomonNjolomole
      @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน

      Kuyankhula kwabwanj uku mumafuna ayambitse nkhondo?

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 หลายเดือนก่อน +1

    Malawi panopa akuvesa chisoni machine opanga mapassport sakugwira ntchito panopa machine wopangira ma ID akuvutaso Koma chakwera wuziwe komwe wuliko Kuti wulamuliro wako ndi mulungu yemwe ndiwokwiya ndi iwe

    • @SolokingChimzy-yt7dj
      @SolokingChimzy-yt7dj หลายเดือนก่อน

      kkkkkkkk......Nebukadinezera uyu

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 23 วันที่ผ่านมา

      Ku Lilongwe kuli machine 8 opangila ma id pomwe ma district ena ndi zero

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba หลายเดือนก่อน

    Galu wa dpp kulila mobangula ndiye sunati ukanalila mcp 2025 boma kale

    • @mafukenimasangwi5487
      @mafukenimasangwi5487 หลายเดือนก่อน

      Dzinazi osamatengela kut bambo anu anali a mcp kapena a dpp koma kumaona kut nziko mwathu zinthu zikuyenda? kapena ayi ngati mumamwa tea sikuti ndi azibale anu nso onse akumwa tea ayi akuvutika mukatengala ku muziti simunaati muziwe kut azibale anunso ali mugulu lomwelo lomva zowawa

    • @FelleCasim
      @FelleCasim หลายเดือนก่อน

      Zitsilu za nyau inu wamzelu angavotele mcp panomso?

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 23 วันที่ผ่านมา

      Kumalikonda dziko lako osati umoyo wako ayi anthu akumva kuwawa

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 หลายเดือนก่อน

    Mutholo ndi anzako achina Ben Longwe mupeze zochita, what you're doing is not activism, this is stupidity of its highest order, mwasanduka oyankhukira zipani, zopusazi tasiyani, ngati mukufuna u activist pitani ku school mukaphunzire osati kumasokosa ndi zopusa zanuzi.

    • @EvanceEdson-fz1vn
      @EvanceEdson-fz1vn 28 วันที่ผ่านมา +1

      Akunena chilungamo, chilungamo chimawawa. Why 50+1, why alliance yet anakana a mec fresh vote registration? Don't you see kut the same rules of 2019, could apply for the fresh 2020 election

  • @user-mf7hf7we2u
    @user-mf7hf7we2u หลายเดือนก่อน

    Simungavumeleze

  • @ClementMisozo
    @ClementMisozo 6 วันที่ผ่านมา

    Very true

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf หลายเดือนก่อน

    Mau Amphamvu ngati amenewa tamva ndithu