A Chakwera Ndi A Chilima Ntchito Yanu Yatha - Billy Banda

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 19 พ.ค. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Billy Banda says that time is up for His Excellency Dr Lazarus Chakwera and his Vice President Dr Saulos Chilima becuase they have failed to govern the country.
    Pa Nyasa VoiceBox, Billy Banda wati nthawi yatha kwa Olemekezeka Dr Lazarus Chakwera ndi wachiwiri wawo Dr Saulos Chilima chifukwa alephera kulamulira dziko.
    #malawi

ความคิดเห็น • 83

  • @stanleymollen7273
    @stanleymollen7273 24 วันที่ผ่านมา +6

    Dzikoli likufunika ma Demo....ngini zinakwera mitengo monyasa.anthu akuvutika heavy..
    Palibe chomwe tingaloze kuchiyenda.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 24 วันที่ผ่านมา +3

    Achoke amenewa awononga Malawi wokoma uja Lero mavuto okhaokha zawavuta basi

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 24 วันที่ผ่านมา +2

    Kumanga bakili mluzi tv Malawi azayaka moto

  • @TarPoor-ye9jx
    @TarPoor-ye9jx 24 วันที่ผ่านมา +3

    We need people like you not those people on times,zbs,mbc onse alikumbuto kwa boma lakuba ilili

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 23 วันที่ผ่านมา +1

    Big up boss,atikwana

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala 24 วันที่ผ่านมา +4

    From today, Commander atenge ulamuliro mpaka tsiku lachisankho. Chakwera out

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z 24 วันที่ผ่านมา +1

    NO PAIN NO GAIN INSHA ALLAH WAKUVA WAVA AKUT SIYAN NCHITO MWALEPHEL PLEASE GOOOOO

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 24 วันที่ผ่านมา +2

    Let's put everything to our God almighty. God is watching

  • @user-un6mw5wm3x
    @user-un6mw5wm3x 24 วันที่ผ่านมา +1

    good message Mr banda

  • @muhammadcassim4056
    @muhammadcassim4056 24 วันที่ผ่านมา +1

    big up brother that kind of citizen needed in our country than those people the get bribe and appreciate nonsense from chakwera and chilima mulungu akupaseni mphavu ndi kuima pa chilungamo

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q 23 วันที่ผ่านมา +1

    Tikulira ife a Malawi apa tithawira kuti dziko lathu lamvunda kwacha yagwaso zithu zakweraso 😢😢😢 MCP Chakwera ndi UTM Chilima vote yanga ikundimvutisaso malawi ineeeee 😢😢😢

  • @user-td6dy8mh3b
    @user-td6dy8mh3b 17 วันที่ผ่านมา

    We need more of you zithu zikhare bwino bwino

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 24 วันที่ผ่านมา +2

    Rev Chakwera kms Chilima kunena zoona zinthu zawakanika ndipo achikhala athu amzeru anakasiya pansi Udindo koma pakuti ndi agalu akakamirabe ubwino wake 2025 ndipompano..

  • @HafizahHarack-bn3bf
    @HafizahHarack-bn3bf 24 วันที่ผ่านมา +2

    Yes we are very disappointed ndi wulamuliro wathu amenewo

  • @moseskathekeni8848
    @moseskathekeni8848 24 วันที่ผ่านมา

    Very strong message.

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x 23 วันที่ผ่านมา

    Mumatiimilila Mr Banda mulungu akupatsen zabwino

  • @user-rd6zo8ry2d
    @user-rd6zo8ry2d 24 วันที่ผ่านมา

    God message

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 24 วันที่ผ่านมา +2

    AChakwera usogoleri mwa inu mulibe kwanu ndikuononga ziko amalawi ndiwokwiya

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 24 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera achoke basi enough is enough

  • @petrosmunthali5562
    @petrosmunthali5562 24 วันที่ผ่านมา +1

    2025 saiphuranso chifukwa zinthu sizilibwino, life now we struggles.

  • @user-oe1lg4xo7w
    @user-oe1lg4xo7w 24 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera ndi chirima Maso ngati Kazizi nchito yanu yathaaaaa. Tulukanimoni nyumbazathu zaboma . Palibenso chifukwa chokusungirani mmaudindo choncho ngati mukufuna ntendere muzipatse ulemu Nokha popular pansi maudindo and koma ngati mukufuna kuyaluka pokakamira maudindo amalawi azakutulutsamoni ndi Manama, mateche ndi zikoti kapena chakwera ndi chirima tayesani Zidane mumuwone mmalawi akakwiya.

  • @user-xx3hs6pw5y
    @user-xx3hs6pw5y 24 วันที่ผ่านมา +1

    Munthu oipa ameneyo chakwera azipita watipha amalawi

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c 24 วันที่ผ่านมา +1

    Zoona zache azipita basi ndithu

  • @DeekeyKamanga
    @DeekeyKamanga 24 วันที่ผ่านมา +1

    Ine kumangolankhula kt tsiyan udindo sizimandpasa sense iliyonse coz olankhula ndi ambili Koma zaka zikupitabe

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 19 วันที่ผ่านมา

    Exactly these is true All it's about Allah and let's ask our Almighty Allah to guide us and to help as to take out these mbava zimene zikuonga boma lathuli kumaba ndalama zathu zamisokho

  • @MateyoMalindi
    @MateyoMalindi 23 วันที่ผ่านมา

    Ndizona achoke akuba awa

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 24 วันที่ผ่านมา +1

    Achoke galu ameneyu

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op 24 วันที่ผ่านมา +1

    Kuyakhula kwabwino

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 24 วันที่ผ่านมา

    👏👏👏🙏

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 23 วันที่ผ่านมา +1

    Mbuzi zalephela zimenezo zichoke we don't want them useless president in Malawian history zitsiru zeni zeni za anthu

  • @user-eb7px2ex2q
    @user-eb7px2ex2q 23 วันที่ผ่านมา

    Tipita liti tikamupakilitse h failed us ,cement nt evn a year kukakwera kawiri eeee ai zikomo, we are nt tired

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 24 วันที่ผ่านมา +1

    Ambuye lithandizeni ziko lathu la malawi tikhululukireni zochimwa zathu ngati mwatikwiira bwezani nkhwiyo wanu

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 19 วันที่ผ่านมา

    My vote belongs to the dc booon kalindo

  • @user-dv5dv8je9t
    @user-dv5dv8je9t 23 วันที่ผ่านมา

    One more kachasu from me, kkkk

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 24 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela akufuna ataimanso koma mulungu akukana

  • @francischikaya3146
    @francischikaya3146 22 วันที่ผ่านมา

    Anthu opanda nzeru amayankhula zopusa ngati zimenezi. Ngati akuganiza kuti DPP ilowanso m'boma ndiye bodza. Chilima sanayendetse nawo dziko. Amene akukutumani a Banda tazingodyani ndalamazo. Iwe ndiwe wapangapo chiyani?.

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 23 วันที่ผ่านมา

    Zoonadi ,dziko ili achoke a chakwela ndi a chilima

  • @aloysiusdidymus7869
    @aloysiusdidymus7869 24 วันที่ผ่านมา

    Ndenge zikugwaso nza ku Iran zakuno ai

  • @LamiziIgshaan
    @LamiziIgshaan 22 วันที่ผ่านมา

    agalu amenewa atizuza ndithu

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 24 วันที่ผ่านมา

    Apandiku ona mosi akusapota mbusi chakwera achokekumen sisilu sawandu andichilima panopa akuspota chakwera mbusiya kape

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 24 วันที่ผ่านมา

    Ndakaika ngati zingatheke kaya mwina. Ndiye zikalepheleka kuti gologolo wakakamila zitani in that scenario 9

  • @HopesonBuledi
    @HopesonBuledi 24 วันที่ผ่านมา

    😢 😂 andiliza awa

  • @RenardYono
    @RenardYono 23 วันที่ผ่านมา

    Akufuna Kuti abwereyo adza pezengongore adzi dzatiso ramuka Nika apume bas

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m 24 วันที่ผ่านมา

    Dziko lamalawi likufunikila mademo akathithi ziko lapansi lidziwe

  • @user-xx3hs6pw5y
    @user-xx3hs6pw5y 24 วันที่ผ่านมา

    Munthu oipa chakwera watipha azipita

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 24 วันที่ผ่านมา +1

    Good message ❤

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka7486 24 วันที่ผ่านมา

    Akumangani

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 24 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk auzeeeee!

  • @tariroJinya
    @tariroJinya 19 วันที่ผ่านมา

    Brother my respect to u.inever been in any Malawi since multiparty system came in Malawi.but Chakwera is worsest and rubish president in the world

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 23 วันที่ผ่านมา

    Chakwera waononga dziko kuposa ma president onse

  • @user-rd6zo8ry2d
    @user-rd6zo8ry2d 24 วันที่ผ่านมา

    Zawakanika

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z 24 วันที่ผ่านมา

    Komatu a Malawi ufulu kuchuluka aliyense kungodzuka anyozepo chakwera koma izi tipita nazo kuti kodi ana athuwa adzakhala potani ufulu umenewu boma likugona olo Bingu samkaselera zopusazi

  • @OwenMajoni-qv3eg
    @OwenMajoni-qv3eg 24 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkk Zina ndi ziwanda. Mudzionongera nazo izi ndi uchitsiru wanuwo. Nsanje ikuphani baba

    • @udkconsultancy5567
      @udkconsultancy5567 24 วันที่ผ่านมา

      True some of these ndi mademoni awa a billy bwanji ? speak peace and unity ..

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e 24 วันที่ผ่านมา

      Ndiwe opusa kwambiri mmene anthu tikuvutikira ungamaikire cakwera kumbuyo zoona

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 24 วันที่ผ่านมา

    Mcp yakupa ndipo yangasa chakwera andi chilima alepela ose mbusi sawandu mbava sa kuba

  • @McNeverNjanji
    @McNeverNjanji 24 วันที่ผ่านมา

    Chakwela acoke sakufunika

  • @OumaOuma-ge4sd
    @OumaOuma-ge4sd 24 วันที่ผ่านมา

    Kodi anthu amenewa mfundo zawo kampeni wachakachino angamveledwe boza zisiluzo kunama bs

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 24 วันที่ผ่านมา +1

    Kagwere iwe ndiwe ndani chitsiru usatibowe ukuti ifeyo wina kuphatikiza ndani poti ukuyankhula wekha pomwe ulipo ndi milomo ya yothethekayo galu

    • @user-jd9yz5hp7y
      @user-jd9yz5hp7y 24 วันที่ผ่านมา

      Iwenso ndi wanyawu eti?
      Kapena ukudyanawo a MCP kwanu ndikutiko iwe?

    • @user-st6bt5vv9c
      @user-st6bt5vv9c 24 วันที่ผ่านมา

      Chitsiru iweyo galu uyu ukunena zoona ufunse uladi pa kk kuti panali bwanji

    • @user-st6bt5vv9c
      @user-st6bt5vv9c 24 วันที่ผ่านมา

      Zulo aziona uladi musa amanyozedwa akuva pa chigumula

    • @AllanChabwela
      @AllanChabwela 23 วันที่ผ่านมา

      Ngati mwadya nawo a mcp khalani chete,anthu akuvutika

  • @user-kr1tf2tu7s
    @user-kr1tf2tu7s 24 วันที่ผ่านมา

    Ndiye iweyo ukati chakwera ndi chilima maso ngati kadzidzi nanga peter uja afanana ndichiyani kuphatikiza iweyo ufuse athu akuuza mene ukuonekera.kodi iwe billy banda umadziwa malamulo ?uchoke ndiwe kaya mbuzi yotheratu cadet.

    • @AllanChabwela
      @AllanChabwela 23 วันที่ผ่านมา

      Peter munthalika sungayelekezele mbuzi ziwili zikutchilidwa apazi,

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 24 วันที่ผ่านมา

    Uchisilu abillywo ali nkuchikamwa ngati adya zowawa tiyeni wauko ndinu achisilu galu amalawi ake ati chimbwe

    • @EyobeAyala
      @EyobeAyala 24 วันที่ผ่านมา

      Mbolo yako iwe

  • @user-et3il7pi7t
    @user-et3il7pi7t 24 วันที่ผ่านมา

    Mademo ayambaliti

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 24 วันที่ผ่านมา

    Galu wachabechabe president yuti adakwanisapo zokhumba za anthu onse

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 24 วันที่ผ่านมา

    Chilima amayendetsa boma lake lambuyako? Zoti anamuimitsa ntchito for the past 2 years iwe sukudziwa? Kapena amagwira nyumba mwako? Leave chilima alone pliz wadutsa kale muzambiri

  • @franciscomkwanda2525
    @franciscomkwanda2525 19 วันที่ผ่านมา

    How can a fully grown up man Billy speak lik this ...u may have something to say but the way u present it its very poor . Go back to the drawing board

  • @user-ko1lk3br4r
    @user-ko1lk3br4r 24 วันที่ผ่านมา

    Judge wakumalawi akulankhula atakhuta ndalama za DPP mukuva km kkkkkkk akt sakuona magetsi kusaxima, at mukumukaniza kukateng

    • @user-ko1lk3br4r
      @user-ko1lk3br4r 24 วันที่ผ่านมา

      Mafut ku mela at sakuona HSA akulembedwa iyeyo a police akulembedwa ntchito akuvek ndithu

    • @AllanChabwela
      @AllanChabwela 23 วันที่ผ่านมา

      Magetsi anthu akumidzi samadya aise,ndipo kumaganiza poyankhula osayankha phala apa ngati munthu amadya msewu,munthu amadya magets,shame

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba 24 วันที่ผ่านมา

    Zazii zenzeni chitsilu chamunthu zolskhula zako zosabveka mbuzi yamunthu shupit

  • @SynodAudit
    @SynodAudit 24 วันที่ผ่านมา

    Good is good: no black out but prices of 3Fs, foods, fertilizer and Fuel eshiiiiiiiiiiiiiiiiii