God bless you Dr Michael Usi, for remembering the people who you worked with, when God changes your story, it's always Good to remember where you are coming from.
Kodi mukuti awa ndi apurezident a UTM nanga bwanji sakupita kukaona Malo womwe anapangika Ngozi kuwuzana ndi kwantere nzakeyo ? Amalawi khalani ndi nzeru awawa ndi afiti
kodi anthu enanu mukuti usi ntchito akuigwila kodi ntchito yake iti poti sitikuiona Amalawi muzikhala ndi nzeru because usi akungoyendayenda kumupangila Kampen chakwera this is nonsense
Apule mwandisangalatsa ndinu osadzikonda mwakumbukila amai amene mumagwira nao ntchito kt khalan apa wina kukhala pa bwino sangapange zimenezo kutengela udindo umene muli God bless you ndi zimene Mulungu amafuna
God bless you Dr Michael Usi, for remembering the people who you worked with, when God changes your story, it's always Good to remember where you are coming from.
All hospitals have the same problems. The approach should be targeting the general problem not individuals.
Mwa ma drama momwemo zikutheka bas😂 Nice
Well done Mr Kingsley Phariyao
Kodi mukuti awa ndi apurezident a UTM nanga bwanji sakupita kukaona Malo womwe anapangika Ngozi kuwuzana ndi kwantere nzakeyo ? Amalawi khalani ndi nzeru awawa ndi afiti
Mr kingsly phaliyao kuyakhula kwabwino with confidence that's wat we want to the youths
Well done a VP
Am happy mr president sumaona mutundu God bless you
VP visit Mitundu hospital, the situation is pathetic
a VP mukuyesetsa being humble
Mai wathuyo wawerengeratu pamenepo..ndiye osangobwerera mma jokes
Bwana usi akanena zinthu zimasintha ndipo zichitika
Mwachedwa zedi nthawi mulibe mwaiseweletsa nokha,busy kusula ma plan ophera anzanu basi.
Bwana mukamaliza u vp mupite ku ubusa bac missionary
Kkkk ichi ndicha drama ndithu eeee mai mulipo KKK
VP visit agriculture offices especially the EPA'S
Mr kingsly ndakuonani
Thank Mr VP focus on
Bwana ndani yr mad akupha ameneyo kafuse chilima 😢😢
Kukhala vice president ndikwabwino, mpaka usi wayamba kunenepa
Kuyendera zipatala ndi kumeneko koma mankhwala mulibe so zosowekera ndi zambiri mbiri
Zopempha zachuluka 😂😂😂
munthu angoyenda inu kungoona kt ndi vice president zopempha mbwee koma palibe chimene chikuchitika zopusa bc
Kumayamika usi tchito akuyigwira big up bwana VP
Kwambiri
Angonena zinthu zosathandiza anthu tikufuna pa galaundi
Mwachedwa mutalawila mudakapanga zimenezi dzana,,koma ma plan anu akupha tiyeni uko
Ndipo wachedweratu,,, olo apange motani chomwe ndikuziwa ine choti akuziwapo kanthu pa imfa ya CHILIMA😢
My vote vice president
Mmmmmm anapha nawo chilima ameneyo ukoooo
Ukuchedwa ndikumunena manganya musiyeni muthu agwile tchito yake
Aaaaaaaaaa kuononga ndalamako malo mogula mankhwala kuika muzipatalamo alibizy kujoya zazii
Kodi mukamati bwana president akhala liti?
And ma president alipo angati ku mbomako?
Usi ndi wachibwana achedwa ndipo anthu akuziwa zonse
Zoona Pena kumayamika usi akuyesa ku mbali yake
Zandale zimenezo anthu akumiduma amenewo
Mukupempha manganya uyu akusangala ndingongole angoyenda yenda opanda manyazi mankhwala kuzipatala mlibe basi kungofusa mumayamba liti ntchito abwana ali kuti pambuyo mumva ngongole zafika aliyese alandila pano ali ku nkhota kota akubwera kunu.
Bwanji ndalama zimene akuyenda yenda ndi muchimwene wake kuti agule mankhwala
kodi anthu enanu mukuti usi ntchito akuigwila kodi ntchito yake iti poti sitikuiona Amalawi muzikhala ndi nzeru because usi akungoyendayenda kumupangila Kampen chakwera this is nonsense
Yowoyani akulu wane, kwithu ku mpoto
Nanga ife ameneo?
Mukukwanira
Usi ntchito akugwira
Akugwira kuti kapena akuyenda yenda ndikuvesera mavoto wabwelesa chikangawa?
@@joyahmedjoma4615iweyo ndiwe gulukunyinda umafuna azivera PA phone zimenezo mutuwo uzigwira tchito si za sale izi ndizopititsa mtsongolomoyo WA athu osati zachibwanazo zogwetsa ulesi athuzo uzipanga pakhomo Palo wava
God bless
MA kuipatsa moto
Usi munthu wachitemwa chiuta wakhale namwe
Usi ndimunthu ofunikadi kukhala president ndimunthu ozichepesa komaso oziwa nchito yake