MICHAEL USI FIRST INTERVIEW AS A VICE PRESIDENT - UBALE WAKE NDI MALEMU SAULOS CHILIMA UNALI OTANI?

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 19 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 322

  • @MargaretLindaChikapa-Phiri
    @MargaretLindaChikapa-Phiri หลายเดือนก่อน +4

    Indeed the Vice President, you are a brilliant, humble and wise person. As you help our President in governing Malawi, may the Almighty God help you and give you all the desires of your heart.

  • @tiflo2012
    @tiflo2012 2 หลายเดือนก่อน +1

    One wise statement that caught my attention " ine ndinalowa mmalo mwa a Chilima...when he died, was he out or inside Alliance? " Wakumva wamva...yankho la straight 🔥 👌 💯

  • @KhaliluGiftMasala
    @KhaliluGiftMasala 2 หลายเดือนก่อน +7

    I have learned something from Michael usi akuti ukakhala tsogoleri don't rush kuyankhula because as being a leader you need kukonza ma speech olakwakika kwa okutsatira

  • @WistedFole
    @WistedFole 2 หลายเดือนก่อน

    Very familiar with people, may god bless you Dr usi

  • @SaulosiPhiri-e9f
    @SaulosiPhiri-e9f 2 หลายเดือนก่อน +3

    Bravo wander msisha olive you big

  • @elizabethbalalasdp721
    @elizabethbalalasdp721 2 หลายเดือนก่อน +2

    Of course I don't underate Wonder Msiska in this interview! He is also very challenging and well composed!! Bravo Mr Msiska!

  • @FatimaSande-lb1hd
    @FatimaSande-lb1hd 2 หลายเดือนก่อน +3

    Am getting your points mr vp and you are a wise person big up mr usi❤❤❤❤❤

  • @elizabethbalalasdp721
    @elizabethbalalasdp721 2 หลายเดือนก่อน +1

    I loved so much Usi when he was abambo a Sikono in ADRA Koma pano mmmmmmm ayi, I can't take him on board as the VP of Malawi! Zinthuzi aliyense amakhala ndi malo ake choondeee!

  • @Prianka567
    @Prianka567 2 หลายเดือนก่อน +2

    Woow Manga you are blessed ,wishing to learn more from you.very good answers with examples without any complications

  • @WahiedaWadie
    @WahiedaWadie 2 หลายเดือนก่อน +1

    Young talent vp i salute you kuyankha mopanda mantha komanso chimene mukudziwa odya zake alibe mulandu

  • @PrinceMittochi
    @PrinceMittochi 2 หลายเดือนก่อน +3

    Watching from Vietnam ..Ooh my beloved Malawi

    • @EdwardZuze-r7w
      @EdwardZuze-r7w 26 วันที่ผ่านมา

      how are you there bra

  • @yotamumkandawire-k8j
    @yotamumkandawire-k8j หลายเดือนก่อน

    Wise and humble leader. God bless you.

  • @StewartMustafa
    @StewartMustafa 2 หลายเดือนก่อน +4

    Wonder sangamukwanitse Dr Usi.
    Olo Brian Banda amanama koma Britain banda amayesesa

    • @dennissawamba2939
      @dennissawamba2939 2 หลายเดือนก่อน

      Uyuyu simbuli chomwe amapanga amachidziwa 🙌

  • @SakaPrince-s8m
    @SakaPrince-s8m 2 หลายเดือนก่อน +7

    Michael Usi. you are number 1,ndiwe ochenjera kwambiri

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 2 หลายเดือนก่อน +9

    Chilima anakukondani a Usi ndi mtima wake onse, koma inuyo chikondi chanu chinali cha mitala, that's why nzanu uja atafa mumapanga ma celebration ndi Chakwera wanuyo ku state house, olakwa ndi Chilima mwina pokukondani 😢 still in our heart SKC 😭😭😭😭😭

    • @DanielKaombe-im3pr
      @DanielKaombe-im3pr 2 หลายเดือนก่อน +3

      Two mistakes made by chilima
      1. Making alliance with MCP
      2. Trusting Michael Usi

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya 2 หลายเดือนก่อน +1

      @@DanielKaombe-im3pr ndipo that's a big mistake

    • @KarongaDiocese
      @KarongaDiocese 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ur seeing this in a small minded point of view

    • @JuvenileDebwe-bv8ow
      @JuvenileDebwe-bv8ow 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ndipo udindowu ankausakasaka ndipo zikuoneka kuti njira ayisaka kuti afikepo basi ndipo panopo is happy

    • @happychavula4469
      @happychavula4469 2 หลายเดือนก่อน

      Mwanena chilungamo

  • @SHABILUKAZEMBE
    @SHABILUKAZEMBE 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ngat yudasi adapheleka yesu kulibwanji Dr usi

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 หลายเดือนก่อน +9

    Uyu amafunika Brain banda sanyengerela mafunso.usi adamupeleka skc.wamagazi mmanja iwe

  • @ManeyBen
    @ManeyBen 2 หลายเดือนก่อน

    Thanks Mr VP for your clarification

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 2 หลายเดือนก่อน +10

    Exclusive iyi imafunika Bryan Banda uyu akanaithawa interview imeneyi ndithu

    • @dennissawamba2939
      @dennissawamba2939 2 หลายเดือนก่อน

      Anakanika kale adamawa nda nzeru osat masewela

    • @KUCHEKATULI
      @KUCHEKATULI 2 หลายเดือนก่อน

      Brian Banda ake aja adalephela kwa fusa ma a m'sonda........
      Amwene kwa onse panopa amene akumafusa ma funso omvekandiwa nkazi uja amene amampanga interview
      Winiko uja

  • @CliveWhitman-rr9ew
    @CliveWhitman-rr9ew 2 หลายเดือนก่อน +1

    Politician is not a person that will give u a direct response in most cases...

  • @peterchiutsi
    @peterchiutsi 2 หลายเดือนก่อน +6

    Vuto la a Malawi ndiloti when it comes to Presidency, we always miss the right person to be the President guys Micheal Usi hes has the characters of a right president and he can deliver the gest kungoti a Malawi timangomuona pa angle yolakwika munthuyi sinthila kuwili guys ndimunthu oyenela uyuyu Lets believe him and give him a chance

  • @UchizieFMtemela
    @UchizieFMtemela 2 หลายเดือนก่อน +1

    Brilliant Usi
    🔥🔥🔥🔥🔥

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow 2 หลายเดือนก่อน +7

    Don't forget that UTM wants to be independent

  • @carlossadimba595
    @carlossadimba595 2 หลายเดือนก่อน +4

    ❤❤ our new virce president Dr micheal Usi......😊😊

    • @jamiel-gr9ny
      @jamiel-gr9ny 2 หลายเดือนก่อน

      Kma ndfe anthu anu bwana mukanamatiyankha kut tidxiwe

  • @SiphamandlaNcaphayi
    @SiphamandlaNcaphayi หลายเดือนก่อน

    Good interview and we learnt a lot

  • @assankamwendo852
    @assankamwendo852 2 หลายเดือนก่อน +12

    DR Michael Usi is a man with wisdom and a philosopher.proud of you VP

  • @RemaniNkhoma
    @RemaniNkhoma 2 หลายเดือนก่อน +25

    yankha bwino fuso iwe wunapereka chilima ndiweyo

  • @MustaphaChimangeni
    @MustaphaChimangeni 2 หลายเดือนก่อน +4

    Wonder you should have given this interview Brian banda

  • @hopesato
    @hopesato 2 หลายเดือนก่อน

    Leading between the lines, and ofcoarse without forgetting about the plane crush... Usi is with MCP

  • @MustaphaChimangeni
    @MustaphaChimangeni 2 หลายเดือนก่อน +2

    Wander wachepa nayotchitiyi Brian banda is very capable

  • @MirajLaja
    @MirajLaja 2 หลายเดือนก่อน +1

    Wonder kuyang'ana kwake ngati ungomewamenya khofii

  • @fabianochimenya7231
    @fabianochimenya7231 2 หลายเดือนก่อน +6

    Brilliant Dr Usi, am encouraged with your sentments

  • @sandersonmayuni7557
    @sandersonmayuni7557 2 หลายเดือนก่อน +3

    Dr Usi is unifying leader who don't want to injure the divided party. His agenda is to bring unity In the party. UTM should nurture the wisdom in their Leader.

  • @OdalaaSifa-wj3vw
    @OdalaaSifa-wj3vw 2 หลายเดือนก่อน

    This guy is in Very Serious Situation. If he won't reveal his Intentions avutika Mumtima hvy

  • @GloriaWalawala
    @GloriaWalawala 2 หลายเดือนก่อน +2

    Ndinu 1 , munthu wa mzeru our VP🎉

  • @georgezaya1071
    @georgezaya1071 2 หลายเดือนก่อน +1

    Usi just do your job but don't forget where you come from

  • @simeonwilliamsbanda3132
    @simeonwilliamsbanda3132 หลายเดือนก่อน

    This man has very clear points and feelings before towards his country.
    He has points step by step well analysised

  • @surveyscqcdirect2618
    @surveyscqcdirect2618 2 หลายเดือนก่อน

    Awa ndebolaso kalindo straight to the point osati kulambalalaso apa.

  • @PhilomenaChikabadwa-dt6vy
    @PhilomenaChikabadwa-dt6vy 2 หลายเดือนก่อน

    Keep it up sir.Mulungu amadziwa zonse,

  • @PatriciaVictor-o5s
    @PatriciaVictor-o5s 2 หลายเดือนก่อน +8

    Olo mutapeleka ngongole yopanda chikole koma palibe chomwe tingachite ife anthu osauka chifukwa nima ndiodula sitikudya ndalamayo izingothela madeya ndiposo deyayo kupezeka nd mwayi ingotsisani zinthu ife osauka tizikalima ganyu bas palibe chanzelu chomwe mukupangapo apa ngongole ndiye chan mukuganiza kut munthu wagona ndinjala masiku atatu mumpase ndalama imeneyo bizinesi itheka inutu mutokhuta

  • @RobertChimenya
    @RobertChimenya 2 หลายเดือนก่อน +8

    Usi Ali ngati Judahs skaliyoti adamupereka SKC koma anva ululu owopsa

    • @innocentmagaleta492
      @innocentmagaleta492 2 หลายเดือนก่อน

      I think it is you bra uli judahs

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza 2 หลายเดือนก่อน +1

      Komatu mmayankhula ngati muli ndi umboni.Just guessing but kuyankhula as of you have concrete evidence

    • @Rometcma
      @Rometcma 2 หลายเดือนก่อน

      Concrete evidence iposele SKC adamwalila😂😂😂😂

  • @shekinahgloriah
    @shekinahgloriah 2 หลายเดือนก่อน

    Dr. I sulute you 💯

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama 2 หลายเดือนก่อน +7

    Now I love this guy he is doing anything for malawians achakwela aziyamiza ma vp awoo ndi a nzelu koma achakwela musamavele mafana anu akuchipani kwanu plz ma members aku mcp ndi nsanje kwambili komanso amadalila kwambili zaufiti but good job Mr usi under the president chakwela

    • @frankiechasokoneza5802
      @frankiechasokoneza5802 2 หลายเดือนก่อน

      @@StevenMjMbama bwana opoila ndi Chakwerayo he don't have leadership

  • @elijahausi2274
    @elijahausi2274 2 หลายเดือนก่อน +3

    Usi ndi machine

  • @BeynoMike
    @BeynoMike 2 หลายเดือนก่อน +1

    Michael your number one, mupitilize because anthu ena akumakudelerani dada

  • @MisheckKamwendo-w9n
    @MisheckKamwendo-w9n 2 หลายเดือนก่อน +5

    Musiye manganya asakukulakwise ameneo ndiwa mcp ameneyo akugulisa utm ndimwana pandale kutha kwamanyanya

  • @MargaretLindaChikapa-Phiri
    @MargaretLindaChikapa-Phiri หลายเดือนก่อน

    I repeat, Dr Usi ndakunyadirani, ufulu tilinawo koma tsopano what remains now - is the battle against disease, poverty and discipline.

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 2 หลายเดือนก่อน

    Genius Michael usi bravo

  • @goldenbanda6757
    @goldenbanda6757 2 หลายเดือนก่อน

    God bless Mr Vp

  • @LouisMisha
    @LouisMisha หลายเดือนก่อน

    Bwana vice president pempho langa lakuti pitirizani kupanga zabwino ndi maganizo okonda anthu osati wina akusokonezeni kaamba ka udindo wanu please try to do good things koma moopa Mulungu poti iye ndiye mwini zonse. ❤ Love your country ❤❤❤❤ monga tonse ndife anthu amodzi posayang'ana mbali kapena mtundu wa anthu kuti uyu ndiwakumpoto kapena chigawo chapakati kapenaso uyu ndiwakumwera ai, inu ndinu kholo la a Malawi wonse ndipo mukhale ngati m'mayi amene adabala ana amapasa amagona pakati chagada kuti mwana wina akafuna kuyamwa ayamwe osagonera mbali imodzimodzi ai kumbukirani kuti odyetsa anthu wonse ndinu ndipo tikunena panopa Thiko ulindiinu.

  • @jnrsibonelo9444
    @jnrsibonelo9444 2 หลายเดือนก่อน +11

    But this guy is trying to cover himself in terms of answering questions.😢 My point of view this Usi is an Mcp member not Utm🤞powers can make people completely change. Let's meet next year bwana Usi mulungu akuona chilichose atimenyera nkhondo🙏 muzaululika.....

  • @stelladolizyi
    @stelladolizyi 2 หลายเดือนก่อน

    Izi akadakhala Brian ❤

  • @DonsondouglasKim
    @DonsondouglasKim 2 หลายเดือนก่อน

    Munapereka bwana wanu Dr utsi, nkulakwa kodi kutero, akanakhala Brian Banda tu akanafutsa limenelo

  • @JohnWyson-z3x
    @JohnWyson-z3x 2 หลายเดือนก่อน

    High time to hear that

  • @OsmanMailosi
    @OsmanMailosi 2 หลายเดือนก่อน +4

    He should not confuse utm people he is mcp member for long time. People will meet him at utm convetion leave him adzatha ngati curtain

  • @aggiemlotha1208
    @aggiemlotha1208 2 หลายเดือนก่อน +1

    Onaa nzeruu 🎉!!

  • @chimwemwenyirenda7911
    @chimwemwenyirenda7911 2 หลายเดือนก่อน +1

    God is the best judge all the best bwana vp we have to move on as a country

  • @MarthaTwisaSelemani
    @MarthaTwisaSelemani หลายเดือนก่อน

    Or ka minute of silence in honour of Chief odya naye mtedza, taaaa!

  • @obrienalfkarmaysir9372
    @obrienalfkarmaysir9372 2 หลายเดือนก่อน

    Watching from Rosenberg Germany

  • @elizabethbalalasdp721
    @elizabethbalalasdp721 2 หลายเดือนก่อน

    Brian Banda would have been the best host in this Times Exclusive interview!

  • @BaxterKachelenga-mb7wx
    @BaxterKachelenga-mb7wx 2 หลายเดือนก่อน +2

    Bwana you is brave enough,bweresani UTM pamodzi

  • @SiphamandlaNcaphayi
    @SiphamandlaNcaphayi หลายเดือนก่อน

    Bravo hon usi

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 2 หลายเดือนก่อน +1

    Watching from south Africa

  • @CosmasChikwindi
    @CosmasChikwindi 2 หลายเดือนก่อน +4

    Tathokoza kuti mwanva pempholathu kuti muzichosa sound yomwe imanveka pansi.

  • @Chipilirosafalaoh-hl4vz
    @Chipilirosafalaoh-hl4vz 2 หลายเดือนก่อน +6

    Usi ur brilliant but don't be deceived with this so called position..... build ur own party aise

  • @CosmasMaluwah-mh4ji
    @CosmasMaluwah-mh4ji 2 หลายเดือนก่อน +2

    Dr Usi mukumubalalisa Wonder

    • @quincyswart1884
      @quincyswart1884 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo nde wabalalikiratu😂

    • @ThoccoPearson
      @ThoccoPearson 2 หลายเดือนก่อน

      @@quincyswart1884wabalarika kale koyambilirako ine zandimvekera mokolana kolana 🙌🏻🙌🏻🙌🏻😳

    • @quincyswart1884
      @quincyswart1884 2 หลายเดือนก่อน

      Aliyese mayankho aziwapeza yekha apo sanamvetse 🤣🤣

  • @AngungaThatcherNgoma
    @AngungaThatcherNgoma 2 หลายเดือนก่อน +5

    Micheal Usi ndi dolo. Atukula dziko.

  • @unfortunatelyfoikencharles6092
    @unfortunatelyfoikencharles6092 2 หลายเดือนก่อน

    Ndalamazo zikupelekedwa lelo nthawi yonseyi mmene Malawi wakhala aku kulukutika ndi umphawi zidali kuti
    Don't play with our mind,we need serious leaders and leadership
    So Michael wayamba bwino do not change,please we recognize you

    • @CeciliaNthenda
      @CeciliaNthenda 2 หลายเดือนก่อน

      Ife talandira kale

  • @AzaliahEvessDakahDakahChangach
    @AzaliahEvessDakahDakahChangach หลายเดือนก่อน

    Eeeeh km tinva zithu kumalawi tilipano tidziwe which is truth about this issue

  • @realsu7816
    @realsu7816 2 หลายเดือนก่อน +6

    You may have full support if you just play ur cards well Mr VP....

  • @edsonphangula5817
    @edsonphangula5817 2 หลายเดือนก่อน

    Well-done Mr VP wonderful speach keep it up

  • @iangondwe6857
    @iangondwe6857 2 หลายเดือนก่อน

    mr vice president and mr president himself all the best God help you

  • @unfortunatelyfoikencharles6092
    @unfortunatelyfoikencharles6092 2 หลายเดือนก่อน +11

    You deserve Michael,let's hold hands malawians let's support Michael

    • @VictoriaSibande
      @VictoriaSibande 2 หลายเดือนก่อน

      Kupusa kwako nyau iwe

  • @MicyThobve
    @MicyThobve 8 วันที่ผ่านมา

    U r true veep in mw

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2he 2 หลายเดือนก่อน +1

    Usi you're moving computer, l salute 👏 👌

  • @LawrencePhiri-tt9zq
    @LawrencePhiri-tt9zq 2 หลายเดือนก่อน +3

    Watching form Lusaka Zambia 🇿🇲 big up vp of Malawi 🇲🇼

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2he 2 หลายเดือนก่อน +4

    Wonder wachepa nazo Usi si size yako

    • @AbelBlack-f9q
      @AbelBlack-f9q 2 หลายเดือนก่อน

      I thought you will help the Nation bwana

  • @nicholasshema9016
    @nicholasshema9016 2 หลายเดือนก่อน

    I would feel gud if Wander ask him about v investigation about v crash of Airplane VT MW we ready to hear

  • @LysonKumwenda-v1m
    @LysonKumwenda-v1m 2 หลายเดือนก่อน +2

    Usi your number One

  • @MargaretLindaChikapa-Phiri
    @MargaretLindaChikapa-Phiri หลายเดือนก่อน

    Ndakunyadirani a Vice President. Mwanena zowona.. Mudziko muno anthu ndawona kuti zowonadi wanthu akuvutika ndiposo so ma schools Mudziko muno achepa ndiposo atalikirana kwambili. Tinthandizenipo.

  • @tamalangoma2765
    @tamalangoma2765 2 หลายเดือนก่อน +2

    My VP

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 2 หลายเดือนก่อน

    Udasi miss Usi Munthu Oipa zedi 😢😢😢

  • @StewartMustafa
    @StewartMustafa 2 หลายเดือนก่อน

    Usi u r the best if u don't interact with MCP Party. Coz MCP no matter what MCP can do.
    Prease be wise

  • @kondwanimwafulirwa-jh4hj
    @kondwanimwafulirwa-jh4hj 2 หลายเดือนก่อน

    Genius Usi

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 2 หลายเดือนก่อน

    The best person who answers interview without any force is only born kalindo not awa iyayi

  • @brightbwanali2509
    @brightbwanali2509 2 หลายเดือนก่อน

    Bwana Usi mukuyankha bwino. And apapa musamukakamize kuti ayankhe zopanda umboni.
    Usi sakugwira ntchito ngati wa MCP. Michael Usi ndi m'malawi, akuyenela kugwira ntchito paliponse. Let's not mixup things guys. MCP ndi chipani, UTM ndi chipansinso. Amalawi tiyeni tikule mu zochitika zathu. MCP si malawi. Let' him work for malawian's sakugwirila ntchito MCP

  • @moosaalliekanyumba8886
    @moosaalliekanyumba8886 2 หลายเดือนก่อน +1

    I can hear beautiful Adhan maashaa allah

  • @mccarthykonyani9866
    @mccarthykonyani9866 2 หลายเดือนก่อน

    He is wise

  • @EthelKubalasa
    @EthelKubalasa 2 หลายเดือนก่อน +3

    This man is indecisive, wadziika pa mpani sakudziwa kuti aliku UTM or MCP .

  • @StanleyMayenda
    @StanleyMayenda 2 หลายเดือนก่อน +1

    Inuyo Amalawi ndinu mbuzi ..Kodi ndale NDI uzimu zikugwizana bwanji .mfiti Za wathu inu

  • @JosephMwanza-o5c
    @JosephMwanza-o5c 2 หลายเดือนก่อน

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 หลายเดือนก่อน

    Kopenga anga nanga ngati chilima amakukonda bwanji osamulira anzako...chitsiro iwe chilima wagona kuchikangawa iwe busy kusangalala ndi mr chifunga...wait you wl follow chilima osachenjerapo apa😮😮

  • @MakuLuni-si1wd
    @MakuLuni-si1wd 2 หลายเดือนก่อน

    VIVA USSI

  • @JamesMalinga-x4j
    @JamesMalinga-x4j 2 หลายเดือนก่อน +2

    Well done Mr usi

  • @FrancisDominic-w1s
    @FrancisDominic-w1s 2 หลายเดือนก่อน

    Chief emweyo sizikumveka akurankhurazo

  • @AzaliahEvessDakahDakahChangach
    @AzaliahEvessDakahDakahChangach หลายเดือนก่อน

    🎉

  • @BehindThecamera-xo1qg
    @BehindThecamera-xo1qg 2 หลายเดือนก่อน +4

    Akulephera kuyakha mafunso uyu

  • @PatrickMbewe-pf5fp
    @PatrickMbewe-pf5fp 2 หลายเดือนก่อน

    Never judge a book by its cover

  • @NumbDee
    @NumbDee 2 หลายเดือนก่อน

    Koma nzeru zilimo
    APM my vote

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂manganya chilungamo alibe according the way he is swaying the straight simple question