Choonadi chimamasula anthu sachifuna chilungamo God is with you pastor nanga akatolika aja .uja adati mwagawana zovala zake.zazii.apolice alibe zochita Haas mcp woyeer 2025
KOMA NGATI MULI NDI INFORMATION INA YAKE MUKAWAUZE A POLICE KAPENA ANY EMBASSY THAN KU POSITA IZI CHOMWE MUNGADZIWE MUKHOZA KUYAMBA KUMENYANA OPANDA CHIFUKWA CHENICHENI NONSE MUUPEZE MNTIMA
Same thing is Wrong ndiboma, pamalilo people are free to say what ever they fell why arresting them government did you do anything on SKC if not stop this nonsense,MCP don't bring Kamuzu lifestyle to us
Thanks you for arresting him, akanene bwino komanso akapereke dzina la police yemwe anamuuza kuti palivi zoti ndege ya vice president ikubwera ku mzuzu
Palije apo chifukwa chakumangira mnthu mmalo mwakuti mlimbane namasuzgo ayo yali mumalawi imwe bizy wa mcp kukoma wanthu mwezi uno pera mwakoma wanthu 10 nakuyamba kukaka wanthu pala wamuzuzulani mapoli mose mlije no zeru yyi vimavi vinu this is no one party system this is democracy" how many people u need to kill?
Azibusa ambiri adzuka tsono mumanga ambiri kmso kupalamura mkwiyo wa mulungu.
Man of God do not give up go ahead ngakhale mwamangidwa kuno kudziko musataye mtima ku umzimu ndinu omasulidwa 🙏
Kaya Chakwera alamulira moyo wake onse koma chilungamo mchakuti wapha Chilima wapha munthu amene anamuthandiza kukhala president 💔💔💔💔
Exactly osamati adziwa ndi mulungu yenkha chilichonse ai ifeso anthu timadxiwa timaopa kumagwidwa kapena 2025 kukamvotela ku maula ndinthu 😅😅😅
Osayiwaranxo miya
Osayiwaranxo miya
Choonadi chimamasula anthu sachifuna chilungamo God is with you pastor nanga akatolika aja .uja adati mwagawana zovala zake.zazii.apolice alibe zochita Haas mcp woyeer 2025
Aaa inu apolice ndi zitsiru kwambiri mumanga bwanji munthu osalakwa,kodi mukutenga ngati dziko ndi malamulo ali mmanja mwanu bwanji,kodi satana wanu chakwera akukupatsani zingati kuti muzikazunza anthu chonchi mukubwereza ulamuliro wachipani chimodzi wa kamuzu komatu ulendo zofuna zanu sizitheka chifukwa anthu tinatseguka mmaso ndipo izi mukupangazi malipiro ake nanu muwaona sikalenso ayi anthu opusa inu muphe ndi kumanga amalawi tonse if you can evils 😈
A police ndi abale anthu,Koma akupangidwa force kut azigwira ntchito yausatanayi
Chakwera akungopitiliza kupeleka mkwiyo kwa a Malawi, anthu ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa MCP ndi chakwera. Asamange anthu chonchi.
Chowamangila anthuwocho,nde kuti zoona wapha ndiye.akanakhala kuti sanaphe ndiye akanangokhala chete ndikuuza ntundu wa a malawi zoona zeni zeni
Anakati aziyakhura Chichewa kapena English
Tsono watukwana ndani kuti mpaka amumange ????
This makes sense Sir, why MCP police???? Siku lina tizakuukiran muzathawa
Apolice nanuso ndinu zitsiru ,,,,chakwera chilima unamupha ndiweyo
Chilungamo mchimenecho palibe nkhani yowamangira akunena zimene akudziwa km panja ukankhala olakwa umafuna umboni udzibisika anthu atopa nanu anthu 9 pakamodzi ai mudaonjenza tulanidi pansi udindo bwanji kd anthu amamwalira ochuluka pa ulamuliro onkhaonkha wa mcp ena ifanzo zimankhala kt?
prophet liabunya wanena kuti chakwera ali crean sakukhusidwa ndi imfa ya chilima.
n wanena kuti 2025 azawinaso . mnya alomwe mwauponda
Khaniyiyi or ayipinda kaya kuopseza anthu zoona zake ndizoti athu aja ana chita kuphedwa
Ngati sizoona akumangilanji anthu
Akuwamanga kuti akapelekele umboni mesa iwo alinawo
😮sorry a Malawi ino indiyo nthawi yosiliza okamba choonandi sazapeza mtendere ndi dziko lapatsi bible ikutelo
Mumakwana big pamoza ndi DC tili pambuyo panu
Kodi mukufuna muzinamiza anthu Mesa imeneyo ndi voice ya kamulepu ndiye inu mukuti ya M'busa
Nothing but the truth was spoken here
Chilungamo chomwe wanenacho nkana amutenga kuti akaperekere ku police umboniwo, ndi umboni okwanira
Kodi zikukhala bwanji voice imeneyi ndiyomweso anamangidwa nayoso Akamlepo Kalua ,? Ndiye koma atumbuka onse samangidwa
Ndingomva ngat nditukwane mwina mtima undiphwa chakwera asandiyakhulise pa mbali
Nanunso apolice mwasowa zochita, mumangatu ndye amalawi onse hiyaaa osangozitsiya bwanji? Akukulipirani ma million angati?
All of us are angry 😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡
Achakwera mizimu yakwiya olo mutawamanga onse amene akulakhulawa koma akasiya anthu wa kulakhula Mlungu adzutsa myala kuti ilakhule za imfa ya Chilima
Mr chakwera sinu amuyaya PA zomwe mukuchita
Remember Bingu atakangana ndi Synod ,mkumanga anthu akupeleka maganizo awo inuyo ngat muli ndi umbon tiwuzen,munthu mwamuchita tintin Chakwera wopusa kwambiri
Choti muziwe dziko lino ndi la demokilase mphamvu ZOMWE muli manasozo tsiku lina sizatha ndie NDI pamene musalimve dziko kununkha agalu anu
Komatu nde mumanga ndi azungu omwe. Cos enanso akuyankhula zokuti ndegeyi mudaipangila plan kuti igwe
Wayankhula chizungu chakumpoto amvana okhaokha
Ndipo chakwela waputa m,kwiyo wa mulungu kumanga azibusa ndiwe otembeleledwa ndi nduna zako
Boma likupindukanji pomanga anthu amene AKULIRA MOBANGULA ?
Tonse alliance osawopa logo
This is not a bad voice
This pastor was saying the truth.
Why mu kumumanga?
This audio is for Kamlepo kalua can you share the audio of the pastor
KOMA NGATI MULI NDI INFORMATION INA YAKE MUKAWAUZE A POLICE KAPENA ANY EMBASSY THAN KU POSITA IZI CHOMWE MUNGADZIWE MUKHOZA KUYAMBA KUMENYANA OPANDA CHIFUKWA CHENICHENI NONSE MUUPEZE MNTIMA
Mulungu si analume for tipemphele kuti mutuluke abusa chilungamo chimamasula
Chapha chilima chachakwerachi mfiti
Ine pamene ndavera audio ya busa anga cholakwa sindikuchiona. Ngati aboma or kalaya mayi yolamu akuti ndege inafika ku mzuzu apereke umboni kuti tipeze ngati abusa ndiwolakwa ndege kusowa 10 o'clock kufufuza kuziwisa 4 o'clock mmm ndiye muzimanga anthu wu police munaphuzira kuti wopanda nawo zeru
Same thing is Wrong ndiboma, pamalilo people are free to say what ever they fell why arresting them government did you do anything on SKC if not stop this nonsense,MCP don't bring Kamuzu lifestyle to us
Jipangeni respect mwekha kuyowoya nge wana yayi, wana wasambizgeni makola
Iwe ndiwe ukulemba nge ndiwe mwana,chifukwa icho walemba uchimanya yay
Imwe namwe ndiwe wachindere munthu waleke kuyowoya uwo mbunenesyo kupusa kwako iwe mumalenge mosi nthena na Boma ili mukuona yayi likukoma wanthu mwe mukopha
Mulimosemo kumeneko chilungamo chioneke
Good voice
Kwachema akutapa.
Angomuttulusa mwaulemu
Ndiye mumanga angati
Police sono yanyanyisa esh there is no reason kut amumange uyuyu
Ineso ninamva same thing abusa anthu muwatuluse pls
Thanks you for arresting him, akanene bwino komanso akapereke dzina la police yemwe anamuuza kuti palivi zoti ndege ya vice president ikubwera ku mzuzu
Kodi ufulu omwe timaukondwelera uja uli kuti?why are we still moving backward?
Kwacha Kwacha basi😂
Chakwera anapha chilima
Njee wamangidwa chonchi basi ?
Police yakumalawi kupusa ndchifukwa mukumafa muli amphawi shit
Aaaaaa that's why kuzolozolo wanambembe muchalitchi
😅😅😅😅😅 imwe mwaneneska ka mubusa nayo vikamukhuza nivi va ndege
Sorry abusa chakwera azafa chagada
M c p chimpani cha magazi
Palije apo chifukwa chakumangira mnthu mmalo mwakuti mlimbane namasuzgo ayo yali mumalawi imwe bizy wa mcp kukoma wanthu mwezi uno pera mwakoma wanthu 10 nakuyamba kukaka wanthu pala wamuzuzulani mapoli mose mlije no zeru yyi vimavi vinu this is no one party system this is democracy" how many people u need to kill?
Imwe namwe zeru mulije mukuwa nga ndimwe wachewa kutinangila mutundu chaa ise wanthu wala wslikufwa kwithu ku mzuzu wakawa wa mcp
Iye muliska va ndege vikamukhuza niviii ndiwo wakuwa waliska waboza awa wanyawo wakuwa busy kupemphelela malawi kuti muwe mutende iyo walibusy namilandu nawanthu wachita makola kumumanga wakayowoye chilungamo
Mlw so bad