M’busa anayankhula izi pa imfa ya Chilima ndipo wamangidwa zomweso a Kamlepo anamangidwila

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 73

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 4 วันที่ผ่านมา +8

    Azibusa ambiri adzuka tsono mumanga ambiri kmso kupalamura mkwiyo wa mulungu.

  • @augustMag
    @augustMag 4 วันที่ผ่านมา +1

    Man of God do not give up go ahead ngakhale mwamangidwa kuno kudziko musataye mtima ku umzimu ndinu omasulidwa 🙏

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 4 วันที่ผ่านมา +10

    Kaya Chakwera alamulira moyo wake onse koma chilungamo mchakuti wapha Chilima wapha munthu amene anamuthandiza kukhala president 💔💔💔💔

    • @Hong_sing
      @Hong_sing 3 วันที่ผ่านมา +1

      Exactly osamati adziwa ndi mulungu yenkha chilichonse ai ifeso anthu timadxiwa timaopa kumagwidwa kapena 2025 kukamvotela ku maula ndinthu 😅😅😅

    • @MosesNyalugwe-ll8hh
      @MosesNyalugwe-ll8hh 3 วันที่ผ่านมา

      Osayiwaranxo miya

    • @MosesNyalugwe-ll8hh
      @MosesNyalugwe-ll8hh 3 วันที่ผ่านมา

      Osayiwaranxo miya

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 4 วันที่ผ่านมา +1

    Choonadi chimamasula anthu sachifuna chilungamo God is with you pastor nanga akatolika aja .uja adati mwagawana zovala zake.zazii.apolice alibe zochita Haas mcp woyeer 2025

  • @henryibrahimsailes4638
    @henryibrahimsailes4638 4 วันที่ผ่านมา +6

    Aaa inu apolice ndi zitsiru kwambiri mumanga bwanji munthu osalakwa,kodi mukutenga ngati dziko ndi malamulo ali mmanja mwanu bwanji,kodi satana wanu chakwera akukupatsani zingati kuti muzikazunza anthu chonchi mukubwereza ulamuliro wachipani chimodzi wa kamuzu komatu ulendo zofuna zanu sizitheka chifukwa anthu tinatseguka mmaso ndipo izi mukupangazi malipiro ake nanu muwaona sikalenso ayi anthu opusa inu muphe ndi kumanga amalawi tonse if you can evils 😈

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 4 วันที่ผ่านมา

      A police ndi abale anthu,Koma akupangidwa force kut azigwira ntchito yausatanayi

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 4 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwera akungopitiliza kupeleka mkwiyo kwa a Malawi, anthu ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa MCP ndi chakwera. Asamange anthu chonchi.

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e 4 วันที่ผ่านมา +2

    Chowamangila anthuwocho,nde kuti zoona wapha ndiye.akanakhala kuti sanaphe ndiye akanangokhala chete ndikuuza ntundu wa a malawi zoona zeni zeni

  • @Imtiyazkalikodole
    @Imtiyazkalikodole 4 วันที่ผ่านมา +4

    Anakati aziyakhura Chichewa kapena English

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe8501 4 วันที่ผ่านมา +3

    Tsono watukwana ndani kuti mpaka amumange ????

  • @meeksonmkhala
    @meeksonmkhala 4 วันที่ผ่านมา +1

    This makes sense Sir, why MCP police???? Siku lina tizakuukiran muzathawa

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 4 วันที่ผ่านมา +1

    Apolice nanuso ndinu zitsiru ,,,,chakwera chilima unamupha ndiweyo

  • @user-jj3oo6jh1l
    @user-jj3oo6jh1l 4 วันที่ผ่านมา +1

    Chilungamo mchimenecho palibe nkhani yowamangira akunena zimene akudziwa km panja ukankhala olakwa umafuna umboni udzibisika anthu atopa nanu anthu 9 pakamodzi ai mudaonjenza tulanidi pansi udindo bwanji kd anthu amamwalira ochuluka pa ulamuliro onkhaonkha wa mcp ena ifanzo zimankhala kt?

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 2 วันที่ผ่านมา

    prophet liabunya wanena kuti chakwera ali crean sakukhusidwa ndi imfa ya chilima.
    n wanena kuti 2025 azawinaso . mnya alomwe mwauponda

  • @SaidiMilaji-dk8sr
    @SaidiMilaji-dk8sr 4 วันที่ผ่านมา +1

    Khaniyiyi or ayipinda kaya kuopseza anthu zoona zake ndizoti athu aja ana chita kuphedwa
    Ngati sizoona akumangilanji anthu

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r 4 วันที่ผ่านมา

      Akuwamanga kuti akapelekele umboni mesa iwo alinawo

  • @GraceBanda-t4r
    @GraceBanda-t4r 3 วันที่ผ่านมา

    😮sorry a Malawi ino indiyo nthawi yosiliza okamba choonandi sazapeza mtendere ndi dziko lapatsi bible ikutelo

  • @user-wd5tw1mz8h
    @user-wd5tw1mz8h 3 วันที่ผ่านมา

    Mumakwana big pamoza ndi DC tili pambuyo panu

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 4 วันที่ผ่านมา

    Kodi mukufuna muzinamiza anthu Mesa imeneyo ndi voice ya kamulepu ndiye inu mukuti ya M'busa

  • @fostersimbi8820
    @fostersimbi8820 4 วันที่ผ่านมา +1

    Nothing but the truth was spoken here

    • @GreshamKadzembe-tn8cq
      @GreshamKadzembe-tn8cq 4 วันที่ผ่านมา

      Chilungamo chomwe wanenacho nkana amutenga kuti akaperekere ku police umboniwo, ndi umboni okwanira

  • @SabitSamohgruva
    @SabitSamohgruva 4 วันที่ผ่านมา

    Kodi zikukhala bwanji voice imeneyi ndiyomweso anamangidwa nayoso Akamlepo Kalua ,? Ndiye koma atumbuka onse samangidwa

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 4 วันที่ผ่านมา

    Ndingomva ngat nditukwane mwina mtima undiphwa chakwera asandiyakhulise pa mbali

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 4 วันที่ผ่านมา

    Nanunso apolice mwasowa zochita, mumangatu ndye amalawi onse hiyaaa osangozitsiya bwanji? Akukulipirani ma million angati?

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe8501 4 วันที่ผ่านมา +1

    All of us are angry 😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s 4 วันที่ผ่านมา

    Achakwera mizimu yakwiya olo mutawamanga onse amene akulakhulawa koma akasiya anthu wa kulakhula Mlungu adzutsa myala kuti ilakhule za imfa ya Chilima

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 4 วันที่ผ่านมา

    Mr chakwera sinu amuyaya PA zomwe mukuchita

  • @user-it5zv2nz7f
    @user-it5zv2nz7f 4 วันที่ผ่านมา

    Remember Bingu atakangana ndi Synod ,mkumanga anthu akupeleka maganizo awo inuyo ngat muli ndi umbon tiwuzen,munthu mwamuchita tintin Chakwera wopusa kwambiri

  • @user-gg6uh2wo4x
    @user-gg6uh2wo4x 4 วันที่ผ่านมา

    Choti muziwe dziko lino ndi la demokilase mphamvu ZOMWE muli manasozo tsiku lina sizatha ndie NDI pamene musalimve dziko kununkha agalu anu

  • @LeendaDeborah2005
    @LeendaDeborah2005 4 วันที่ผ่านมา

    Komatu nde mumanga ndi azungu omwe. Cos enanso akuyankhula zokuti ndegeyi mudaipangila plan kuti igwe

  • @user-kl5fo1rb5z
    @user-kl5fo1rb5z 3 วันที่ผ่านมา

    Wayankhula chizungu chakumpoto amvana okhaokha

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 4 วันที่ผ่านมา

    Ndipo chakwela waputa m,kwiyo wa mulungu kumanga azibusa ndiwe otembeleledwa ndi nduna zako

  • @cynthiandekhakatundu6890
    @cynthiandekhakatundu6890 3 วันที่ผ่านมา

    Boma likupindukanji pomanga anthu amene AKULIRA MOBANGULA ?

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 4 วันที่ผ่านมา

    Tonse alliance osawopa logo

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss 4 วันที่ผ่านมา

    This is not a bad voice

  • @user-ig9qk6gi6g
    @user-ig9qk6gi6g 4 วันที่ผ่านมา

    This pastor was saying the truth.
    Why mu kumumanga?

  • @emmakamwana9724
    @emmakamwana9724 3 วันที่ผ่านมา

    This audio is for Kamlepo kalua can you share the audio of the pastor

  • @dysonmsamba5778
    @dysonmsamba5778 3 วันที่ผ่านมา

    KOMA NGATI MULI NDI INFORMATION INA YAKE MUKAWAUZE A POLICE KAPENA ANY EMBASSY THAN KU POSITA IZI CHOMWE MUNGADZIWE MUKHOZA KUYAMBA KUMENYANA OPANDA CHIFUKWA CHENICHENI NONSE MUUPEZE MNTIMA

  • @ceciliathole
    @ceciliathole 4 วันที่ผ่านมา

    Mulungu si analume for tipemphele kuti mutuluke abusa chilungamo chimamasula

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 4 วันที่ผ่านมา

    Chapha chilima chachakwerachi mfiti

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 4 วันที่ผ่านมา

    Ine pamene ndavera audio ya busa anga cholakwa sindikuchiona. Ngati aboma or kalaya mayi yolamu akuti ndege inafika ku mzuzu apereke umboni kuti tipeze ngati abusa ndiwolakwa ndege kusowa 10 o'clock kufufuza kuziwisa 4 o'clock mmm ndiye muzimanga anthu wu police munaphuzira kuti wopanda nawo zeru

  • @sinoiajamu9484
    @sinoiajamu9484 4 วันที่ผ่านมา

    Same thing is Wrong ndiboma, pamalilo people are free to say what ever they fell why arresting them government did you do anything on SKC if not stop this nonsense,MCP don't bring Kamuzu lifestyle to us

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9w 4 วันที่ผ่านมา

    Jipangeni respect mwekha kuyowoya nge wana yayi, wana wasambizgeni makola

    • @user-nt4fr2le3f
      @user-nt4fr2le3f 3 วันที่ผ่านมา

      Iwe ndiwe ukulemba nge ndiwe mwana,chifukwa icho walemba uchimanya yay

    • @user-ms8tm3yf7d
      @user-ms8tm3yf7d 3 วันที่ผ่านมา

      Imwe namwe ndiwe wachindere munthu waleke kuyowoya uwo mbunenesyo kupusa kwako iwe mumalenge mosi nthena na Boma ili mukuona yayi likukoma wanthu mwe mukopha

  • @BlessMnyenyembe
    @BlessMnyenyembe 4 วันที่ผ่านมา

    Mulimosemo kumeneko chilungamo chioneke

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 4 วันที่ผ่านมา

    Good voice

  • @kajawejawadu7844
    @kajawejawadu7844 3 วันที่ผ่านมา

    Kwachema akutapa.

  • @RhodneyBwa3
    @RhodneyBwa3 4 วันที่ผ่านมา

    Angomuttulusa mwaulemu

  • @HsjsmzmHsjsnsjaja
    @HsjsmzmHsjsnsjaja 4 วันที่ผ่านมา

    Ndiye mumanga angati

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss 4 วันที่ผ่านมา +1

    Police sono yanyanyisa esh there is no reason kut amumange uyuyu

  • @user-rm2xv8ys1i
    @user-rm2xv8ys1i 4 วันที่ผ่านมา

    Ineso ninamva same thing abusa anthu muwatuluse pls

  • @isaacchirwa9518
    @isaacchirwa9518 4 วันที่ผ่านมา +1

    Thanks you for arresting him, akanene bwino komanso akapereke dzina la police yemwe anamuuza kuti palivi zoti ndege ya vice president ikubwera ku mzuzu

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo 4 วันที่ผ่านมา

    Kodi ufulu omwe timaukondwelera uja uli kuti?why are we still moving backward?

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 4 วันที่ผ่านมา

    Kwacha Kwacha basi😂

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p 4 วันที่ผ่านมา

    Chakwera anapha chilima

  • @jomochirwa
    @jomochirwa 4 วันที่ผ่านมา

    Njee wamangidwa chonchi basi ?

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 4 วันที่ผ่านมา

    Police yakumalawi kupusa ndchifukwa mukumafa muli amphawi shit

  • @user-nw6ie3xx8b
    @user-nw6ie3xx8b 4 วันที่ผ่านมา

    Aaaaaa that's why kuzolozolo wanambembe muchalitchi

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r 4 วันที่ผ่านมา

      😅😅😅😅😅 imwe mwaneneska ka mubusa nayo vikamukhuza nivi va ndege

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d 4 วันที่ผ่านมา

    Sorry abusa chakwera azafa chagada

  • @ChimwemweJuwao
    @ChimwemweJuwao 4 วันที่ผ่านมา

    M c p chimpani cha magazi

  • @Kilocssreaction
    @Kilocssreaction 4 วันที่ผ่านมา

    Palije apo chifukwa chakumangira mnthu mmalo mwakuti mlimbane namasuzgo ayo yali mumalawi imwe bizy wa mcp kukoma wanthu mwezi uno pera mwakoma wanthu 10 nakuyamba kukaka wanthu pala wamuzuzulani mapoli mose mlije no zeru yyi vimavi vinu this is no one party system this is democracy" how many people u need to kill?

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r 4 วันที่ผ่านมา

      Imwe namwe zeru mulije mukuwa nga ndimwe wachewa kutinangila mutundu chaa ise wanthu wala wslikufwa kwithu ku mzuzu wakawa wa mcp

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r 4 วันที่ผ่านมา

      Iye muliska va ndege vikamukhuza niviii ndiwo wakuwa waliska waboza awa wanyawo wakuwa busy kupemphelela malawi kuti muwe mutende iyo walibusy namilandu nawanthu wachita makola kumumanga wakayowoye chilungamo

  • @user-hg2cw1om1p
    @user-hg2cw1om1p 4 วันที่ผ่านมา +1

    Mlw so bad