Imvani zoona zeni zeni zama demo apa 10 osati zomwe akukamba anthu zija ayi

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 96

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu วันที่ผ่านมา +3

    Anyamata tili kuno ku South africa 🇿🇦 tiyeni titumize rand tatopa ndichakwela makolo athu akuvutika pamodzi ndiife tomwe .malawi sangasithe popanda ife kulimba mtima .chakwela asatenge malawi ngati mudziwake ndi dziko lathu malawi boys moo 🔥 fire 🔥 👌

  • @user-cx7ep1dt8z
    @user-cx7ep1dt8z 2 วันที่ผ่านมา +4

    Come to nkhatabay ndipo zikhhale Ku nkhata asabwele kuno ngati akufuna kubwela kuno nkhatabay abwele ndi chilima

  • @user-cx7ep1dt8z
    @user-cx7ep1dt8z 2 วันที่ผ่านมา +4

    Ngati akufuna achakwela mademo asakhelepo abwelese chilima wathu

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z 2 วันที่ผ่านมา +5

    TIZAKALA KONKO OSAOPA NO PAIN NO GAIN WANING TWO CHAKWEL KUNKUY CHEMWENDO BANDA AD TIKUBWEL PA STREET

  • @robinfeb5684
    @robinfeb5684 2 วันที่ผ่านมา +3

    Ifeso ngakhale tilikutali from south africa komaso ifeso tikumva kuwotchamtima zikutiwawa kom cz mwaiwala bwanji ma boma ochulula akumva kuwawa enafe tikulephela kubwelera kumalawi kamba ka iyeeee chakweraa😢😢😢😢😢😠😠😠😠😠

  • @user-cx7ep1dt8z
    @user-cx7ep1dt8z 2 วันที่ผ่านมา +4

    Chakwela you mast go president oipa kwambili iwe

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 วันที่ผ่านมา +2

    Tikumva kuwawa mademo ankharepo amphamvu 💪💪

  • @user-cx7ep1dt8z
    @user-cx7ep1dt8z 2 วันที่ผ่านมา +2

    Pelekani ma number account abwana tithandizapo

  • @user-pk6vq1cr1b
    @user-pk6vq1cr1b วันที่ผ่านมา

    Power voice comrade, more 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 am with you always

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 2 วันที่ผ่านมา +3

    Chakwera you mast go

  • @BhekiMavundla-po2bq
    @BhekiMavundla-po2bq 2 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwelayi achoke ndithu tatopa naye ndizochita zake,nzeru zautsogoleri alibenso.Munthu wosaziwa zilizonse akhala bwanji president wa dziko lino? Langa ndi funso apa amalawi😢😢

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 2 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwela achoke basi tatopa naye ameneyu mbuli palibe chimene akudziwa dzokhudzana ndi u president amati ndikaphudzilakomweko ndiye sikunotu ayi kumalawi ayi machendako iwe chakwela

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 2 วันที่ผ่านมา +2

    Azibusa ndi ena omwe akupita kwa chakwera akungofuna ndalama sakuziwa kuti amalawi ndi omwe ndi owawidwa mutima kuposa chakwelayo

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn วันที่ผ่านมา

    💪💪 osafooka ndikale anthu akhala akuyakhula,mwina pa 10 pa akamvese

  • @GiftSimbi-cv6kl
    @GiftSimbi-cv6kl วันที่ผ่านมา +1

    Tililimodzi ngat kupha akatiphe tonse zopusa tatopa nazo

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs 2 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwela pa kholopako uchoke watikwana R1000 singakhale 100pn Malawi kwacha

  • @Robertmkango
    @Robertmkango วันที่ผ่านมา +1

    Asalemphere ndipo achitike palibeso boma mpamenepo police 🚔 inkhare gulu yomenyedwa akalowerera boma

  • @user-rm2xv8ys1i
    @user-rm2xv8ys1i 2 วันที่ผ่านมา +2

    Lilongwe kuno tiona kuchedwa

  • @user-sy3fz5nz3v
    @user-sy3fz5nz3v 2 วันที่ผ่านมา +1

    More fire 🔥🔥🔥🔥 Flames osaopa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chilungamo ma comrades, a Malawi akuzunzika kwambiri ndipo anthu ndi okwiya kwiya , osati chifukwa cha maliro a Chilima ayi, koma Chifukwa cha mavuto ali mu dziko, boma silikuyenda bwino. Chakwera achoke basi

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela you mast go

  • @hassanrasheed1379
    @hassanrasheed1379 2 วันที่ผ่านมา

    ✌Moto buuuuuu🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z วันที่ผ่านมา +1

    Ndalama ikungwa dairy tatopa ife pa nseu ine kuno ku USA

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x วันที่ผ่านมา

    Mademo awawa avuta koopsa zedi

  • @watsonmhango8794
    @watsonmhango8794 วันที่ผ่านมา

    More fire

  • @user-ve4zn2ne1k
    @user-ve4zn2ne1k 2 วันที่ผ่านมา

    Tayikani nambala tinyikeko ka ndalama yisanafike 10yoooooo

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

    Amenyedweso apolice ngati akuletsesa mademo ngati ili nkhundo basi timenyane nawo mwazikumwazi amalawi tatopa nazo

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x วันที่ผ่านมา

    Guys tikavute koopsa kumademoku tikaphwasule state house ndi Parliament pokhapokha Chakwera achokeeeee

  • @user-rm2xv8ys1i
    @user-rm2xv8ys1i 2 วันที่ผ่านมา +1

    Wait u will see uzakuumudwa iwe ukuona ngati chakwera wakoyo anga wine

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 2 วันที่ผ่านมา

    Nkhani ndi imeneyi osaopa nkhondo ikufunika ku Malawi anthu achenjele chifukwa ndife opusa kwambiri

  • @user-dh1oi8mb4v
    @user-dh1oi8mb4v 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndipo mademo akhalepo ndithuu tikajende ku state atijaila

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z วันที่ผ่านมา +1

    Mademo amenewo mmmhhh dzikolatha likupita kut mkhazazi bwanji boma la nkhazali lichoke basi

  • @CeciliaMphili
    @CeciliaMphili 2 วันที่ผ่านมา +3

    Nkagova zama demo moyo wangawu umachita kuva bwino bwaji😂😅😊TITHAMANGE NOW

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา +2

      🤣🤣🤣🤣🤣 tiyeni limodzi pa tsewu

    • @CeciliaMphili
      @CeciliaMphili 2 วันที่ผ่านมา +2

      @@Pangolinimw Ndipo ndili konko 🤣🤣🤣

    • @TamalaSoko-vg5wq
      @TamalaSoko-vg5wq 2 วันที่ผ่านมา +2

      Kayatsen moto tiyen tiyen tiyen

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x วันที่ผ่านมา

      Tiyeni tiyeni kukavute koopsa zedi tikaphwasule state house ndi parliament pokhapokha Chakwera achoke

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 วันที่ผ่านมา

      Zaziiii ukaluze moyo chifukwa chazithu zopanda nzeru ngat izi

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q 2 วันที่ผ่านมา +1

    😢😢😢😢Tikulira misozi yathu sidzatha ndithu

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu วันที่ผ่านมา

    Madhemo apangike .chakwela achoke paphando.tatopa ndinyasi za chakwela.

  • @patriciap.bandah3385
    @patriciap.bandah3385 วันที่ผ่านมา

    Achakwera komwe muliko tangoyimikiranitu manja musanawone zokuda, haaa cooking oil 2 ltrs kukoma 10,000 malawulo sindinaziwone chibadwire zimene zikuchitika panodzi

  • @user-hx6ly3cl8m
    @user-hx6ly3cl8m 2 วันที่ผ่านมา

    Dzoona zimenezo mademo achitike bass kufuna osafuna chifukwa Malawi tingovutika

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 2 วันที่ผ่านมา +1

    Zaphavu kumeneko 💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼

  • @user-ve4zn2ne1k
    @user-ve4zn2ne1k 2 วันที่ผ่านมา

    Yoooooooomweyo tilnanu pamozi ngakheare tirìmusasafirika

  • @SpancerChikopa
    @SpancerChikopa 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera must go imidiatly

  • @StevenTembo-mb7rm
    @StevenTembo-mb7rm วันที่ผ่านมา

    Tili konkho ku msewu agalu amenewo atikwana

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala วันที่ผ่านมา

    Kuswa kuswa bas💪💪💪💪💪💪💪💪✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊

  • @FortunePhiri-kl7oe
    @FortunePhiri-kl7oe 2 วันที่ผ่านมา

    Kenya kenya pa 10

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

    Tilipanseu basi pa 10nipa

  • @hopesuzMgawadere
    @hopesuzMgawadere 2 วันที่ผ่านมา +1

    Powerful....

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z 2 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂 awuzen adzinvere achakwerawo apakire kumeneko

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy วันที่ผ่านมา

    Tiyen tiyen komweko

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 2 วันที่ผ่านมา

    Go koko Mcp yationesa mbwaza

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 2 วันที่ผ่านมา

    Mafumuwotu samapita kukapeoetsa koma kukapepha njala mmamidzimu yavuta kutero mmakomo mwawo munalibe kanthu ndiye amanamidzira kuti akukapepesa maliro koma njala njaja mafumuwo

  • @user-uw3sp6rq8m
    @user-uw3sp6rq8m 2 วันที่ผ่านมา

    Ineso moto wanga ndamva bwino ndamva za mademo

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h 14 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    President wama devaluation galu kwa basi kwacha kungogwa opanda mwadongosola galu kwa basi kungopha anthu

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

    Madestrations samakhalaso opempha president ai amangodzuka from no where like here in south africa they dont even ask for any 1 who called him self boss no

  • @MaggieChiomba
    @MaggieChiomba วันที่ผ่านมา

    Tili komko

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 2 วันที่ผ่านมา +1

    Zamphanvu 🙏

  • @user-cx7ep1dt8z
    @user-cx7ep1dt8z 2 วันที่ผ่านมา

    Ziko lathu likupita koipa tabwelela kumbuyo kwabasi athu timalimba ntima chifukwa cha olemekezeka Dr chima ndie afa ife tipange bwanji? Ziko lathu ife tikulifuna

  • @StanleyMakombe-hy3fu
    @StanleyMakombe-hy3fu วันที่ผ่านมา

    Blantyre we are ready

  • @TryceMagombo-sh7kb
    @TryceMagombo-sh7kb วันที่ผ่านมา

    Tipange zapa Kenya basi !!!¡

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m 2 วันที่ผ่านมา

    Osaywala popta Ku nseu osaywala kutenga Petulo komaso mateyala Moto ukayake

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga 2 วันที่ผ่านมา

    Za ziiii

  • @MiracleMalichi
    @MiracleMalichi 2 วันที่ผ่านมา +1

    Abale tiluzenso miyoyo ina aaa achakwera ganizani bwino

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา

      palibe vuto tikaona komweko

  • @EstherChinyama-s6c
    @EstherChinyama-s6c 2 วันที่ผ่านมา

    Km nanga ana amayesowa inu?

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 วันที่ผ่านมา

    COMLAD TAKUMVANI BWINO KOMATU MADEMO AWAWA OSATINSO ZOTI A MALAWI AKAPEREKE MADANDAULO KWA TSOGOLERI AYI NKGANI NDI YOTI ACHAKWERA NDI OMUZUNGULIRA ACHOKE AZIPITA NDIPO MADEMO AWAWA APOSE A KU KENYA CHAKWERA MUST GO

  • @IgienacioPhiri
    @IgienacioPhiri 2 วันที่ผ่านมา

    Tipatse madetail anu titumeko kenakake pa mukuru

  • @IbrahimJasiten
    @IbrahimJasiten 2 วันที่ผ่านมา

    Koma ya ipase Moto kit buuuuu

  • @WittnessNamagunda
    @WittnessNamagunda 2 วันที่ผ่านมา

    Zowona tili chile ife kudikila mademo amenewa

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา

      🫡🫡🫡

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 2 วันที่ผ่านมา

    Kuno kulilongwe takozeka

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 2 วันที่ผ่านมา

    Kukapereka madandaulo kapena kuti kukamuudza cakwera kuti acoke sakufunika

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 2 วันที่ผ่านมา

    Go konko osaopa😅😢

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 2 วันที่ผ่านมา +2

    Bze ndizinthu zoti sizingatheke kuzolowela umphawi kapena kaumbuli chakwelatu sakuchoka ndipo 2025 mudzakhudwa bvuto simayenda basi kwanuko muli chakwela timuchotse maloto achumba

    • @EllahChikwatu
      @EllahChikwatu 2 วันที่ผ่านมา +1

      Machende ako kwa chaka chose

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา +1

      chakwela achoka muona nyani iwe

    • @MosesWitness
      @MosesWitness 2 วันที่ผ่านมา +2

      Machende ako chewa iwe

    • @MaggieChiomba
      @MaggieChiomba วันที่ผ่านมา

      😂😂azilamulira kunyumba kwako aise

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw วันที่ผ่านมา

      @@MaggieChiomba 🤣🤣🤣🤣 ndipo aona apolice awo aphedwa pa 10

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 2 วันที่ผ่านมา

    Zazii zenizeni

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา +2

      Inunso mapwala ako

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d 2 วันที่ผ่านมา

      Athu enanu ndulakwitsa m,mayakhulidwe

    • @RobertChimenya
      @RobertChimenya 2 วันที่ผ่านมา +4

      Kachisiru ako kasiyeni ife tili komweko akatiphera komweko

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา +1

      @@RobertChimenya indee bwana 🤝🤝🤝

    • @EllahChikwatu
      @EllahChikwatu 2 วันที่ผ่านมา +2

      Iweyo uli ndvuto kom nthawi zonse kususa zithu zacilungamo bwanji akumakutuma eti akuku tumayo waonjexa