Don't stress your self please,munthu àmene mukunenayo ndi scammer amango panga pretend ngati wa asma nditambwali ameneyo he used Kuma panga zakeko ku Lilongwe around kanengo komanso area 43 titamuzindikira maplan ake adathawa
M'bale wako oti wamwalira angabwere akuoneka ngati munthu wina mkumati ndameneyo zoona?guys come on come on,these so called prophets asokoneza anthu Kwambiri,
Anali yemweyo kapena ayi? Nkhope imasiyana bwanji? Mprothet ameneyo anamutumiza Mulungu kapena ndani? You and your prothets are fools and you don't know God.
Ku mpoto nde kuli ufiti wa serious akapha akapha anthu aphabasi tsamauka ku manda pamene kumwela amauka kumpoto kuli ufiti oyipa!anthu ambiri kumwera akumauka ku mpoto zero🙄
Mukamapanga zinthu please khalani serious munthuyo muzimuonetsa tizimuona munthuyo
Mzimayi ameneyo mugwireni,mumumenye makofi auluru omwe anamutuma. Wamutuma ndi prophet
Hanifa chonde uzitionetsako muthuyo ngati momwe amapangila azanu
Zooona tiziona
Zoonad
Munthu wabwelayo sakufana ndi yemwe anamwalila ndiye akhalawao bwanji
Kodi ku lilongweko sanabwereko aaa
Zonama idzi akuchita kulakatula ngat thano hiyaa 😊
Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo
Ulendo waku Lilongwe ayendako bwanji?
Kodi ku Lilongwe kwake mbali iti koma ngati zili zoona Ambuye alemekezeke
Ndikupemba mamba ya profit ine Kuno ku mozambiaue
God have mercy
Za satanic izii munthu anamwalila ndi mzimai abwera bwanji zibambo aaa komatu anthu amulungu samalani tili mmasiku osiliza 😮😮
Inu ndalama izi kodi anawapatsa zingati
Aaa munthu wamayi kumwalira mpaka kuzabwela ngati nyamata bwino nazotu tizalandila nazo ziwanda zakomweko
H😊😊😊😊😊😊😮😊😢😢😅😅😅😮
ine sindikumva ataa
Zakumidima izi aaaa
Zoipatu zimenesi
Mudzina Lamulungu wachifundo komaso wachisoni khulupilani mwa mulungu mmodzi ekha ndipo wanu sameneyoyo wanu adapita ndithu
Kuli profet ku Tanzania ku dasalama auka anthu ambiri pitani komweko kubuza dasalama
Tipasileni ndithu
Tatiwuzaniko dzina lá a prophet
Mmm zavta kwambili😂😂
Kodi a prophet amenewa anakupatsani zingati
Munthu anamwalira Ali wankazi abwela bwela bwanji Ali wammuna mmm😢
Iya za boza izizi zakumidima basi anangotumiza nkhalambyo
Nafe timazisowa ndipo zachitikanso ifa yotelo
Komatu mulandira nazo mzukwa aaaaaosowa munthu wa mmkazi abwera wa mmuna bwanji aaaaakomatu
Zabodza izi
Mau zitolelen muziyankhura bwno bwno man aaha
Tangotibweleselani ulendo wakulilongwe Kuti anayendako bwanji
Komadi akufanana ndi m'bale wanudi kapena zauneneri zomwezi
Aaaaah komatu anthu mudzikhala serious Pena inu bwanj sanabwele munthu wanu wen wen anafayo mutakhale ndi dziwanda dzaku satanic pa khomo mukumutenga munthu oti simukudziwa zoona zot dziko linayipa inu zimenezo simukudziwa ikanakhala nkhope ya munthu wanu yo bola Koma mukunamizanazo ndizosatheka
Number ya prophet please
Mwana Wako ungasowe komatu muthetsa nazo chakudya
Zamasiku akumapeto
Kodi video imeneyi mumajambulila foni ya tilili kapena ayi
Last day
Eeee ngat boza koma ndozona
Sanabwelebe
Zoopsatu eesh
Ziwanda iziiii
Aaaa
Zabodza izi munthuyo ndi wina
Timve zosatira plz
Ili ndy bodza la nyooo munthu kumwalira mximai kuzazuka ali mwamuna ndy kut chani
Chipo
Zamatsiku osiliza owerenga khala maso
😢
Zakumidima izii,akhristu musocherela ,inu munthu oti ndi wanu mungalemphele kumuzindikila?
Zabodza zeni zeni kulibe zimenezo
Inu nkhope take mwaiwala ya munthu?
Tionetseni munthuyo
Koma muzionetsako akulankhulayo ndinso munthu omwalirayo
Don't stress your self please,munthu àmene mukunenayo ndi scammer amango panga pretend ngati wa asma nditambwali ameneyo he used Kuma panga zakeko ku Lilongwe around kanengo komanso area 43 titamuzindikira maplan ake adathawa
Bodza mukufuna ma comment 5:25
Zaziii
Munthu amene anabwera kunamizira ku wa esthma uja ndi mmene ndi amene anadzafufuza maina anu
Wachamba ameneyo protect ndiwaboza
M'bale wako oti wamwalira angabwere akuoneka ngati munthu wina mkumati ndameneyo zoona?guys come on come on,these so called prophets asokoneza anthu Kwambiri,
Za ziii
Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili
mmmmm profit wanama apa
😂😂😂
😂😂😂😂
Zoopsatu
Koma zikoli
Zabodza
Kkkkk
Funso langa ndi Ili kunena kuti koyamba kunabwera mnyamata amene amaonesa kuti Ali ndithenda yomwe amadwala m bale wanu asma eti? Ndipo abusa anakuyimbirani phone munthu mukamufuna uja anabwera simunamusama pamene wanu yemwe anamwalira ndi mkazi sichoncho tinene kuti athufe tikamwalira timakasitha matupi anthu? Muthu oti anali mzibambo kudziko lapansi pano ndiye bambo uja mwalira pozauka Kwa akufa azauka ndinthupi la mzimai? Koma anthu amene munakhala busy ndi azibusa musamale inutu ameneyo simunthu amene mumamuyembekezera ai ndichiwanda chimenecho chochokera Kwa busa pofuna kuti atchuke ku dziko kuno
🤣🤣🤣🤣🤣koma athu muri ndichibwana muthu waikidwa manda kumati wabweraso tangomvomeredzani muthu akamwarira
Zina ukamva 😅😅😅kambanga mwala munthu okhala wawo kulephera kumudziwa😂😂
Wasting time for nothing I can't believe that
Malawi ❤❤❤❤❤
poop?
Anali yemweyo kapena ayi? Nkhope imasiyana bwanji? Mprothet ameneyo anamutumiza Mulungu kapena ndani?
You and your prothets are fools and you don't know God.
Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo
Zoipatu zimenesi
😭😭
Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili