ANA NDI ACHIBALE A ZIMAYI WADZUKA KUMANDA KULONGOSOLA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 24 ก.พ. 2024
  • ANA NDI ACHIBALE A ZIMAYI WADZUKA KUMANDA KULONGOSOLA

ความคิดเห็น • 86

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ku mpoto nde kuli ufiti wa serious akapha akapha anthu aphabasi tsamauka ku manda pamene kumwela amauka kumpoto kuli ufiti oyipa!anthu ambiri kumwera akumauka ku mpoto zero🙄

  • @siskanyirenda
    @siskanyirenda 4 หลายเดือนก่อน +5

    Mukamapanga zinthu please khalani serious munthuyo muzimuonetsa tizimuona munthuyo

  • @user-dk8ey5pu5w
    @user-dk8ey5pu5w 4 หลายเดือนก่อน

    Mzimayi ameneyo mugwireni,mumumenye makofi auluru omwe anamutuma. Wamutuma ndi prophet

  • @SleepyAnteater-bh5zo
    @SleepyAnteater-bh5zo 4 หลายเดือนก่อน +8

    Hanifa chonde uzitionetsako muthuyo ngati momwe amapangila azanu

  • @ziyamikanmakowa5981
    @ziyamikanmakowa5981 4 หลายเดือนก่อน +2

    Munthu wabwelayo sakufana ndi yemwe anamwalila ndiye akhalawao bwanji

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi ku lilongweko sanabwereko aaa

  • @user-ih3qe8ho3v
    @user-ih3qe8ho3v 4 หลายเดือนก่อน

    Zonama idzi akuchita kulakatula ngat thano hiyaa 😊

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 4 วันที่ผ่านมา

    Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo

  • @gracemphande550
    @gracemphande550 4 หลายเดือนก่อน +1

    Ulendo waku Lilongwe ayendako bwanji?

  • @user-rd4ft9nd8t
    @user-rd4ft9nd8t 4 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi ku Lilongwe kwake mbali iti koma ngati zili zoona Ambuye alemekezeke

  • @BarnabeMacuane
    @BarnabeMacuane 9 วันที่ผ่านมา

    Ndikupemba mamba ya profit ine Kuno ku mozambiaue

  • @user-co4ej4cw8r
    @user-co4ej4cw8r 3 หลายเดือนก่อน

    God have mercy

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 4 หลายเดือนก่อน +2

    Za satanic izii munthu anamwalila ndi mzimai abwera bwanji zibambo aaa komatu anthu amulungu samalani tili mmasiku osiliza 😮😮

    • @WysonMpatama-cv1mc
      @WysonMpatama-cv1mc 2 หลายเดือนก่อน

      Inu ndalama izi kodi anawapatsa zingati

  • @user-hx4mz9nk9g
    @user-hx4mz9nk9g 3 หลายเดือนก่อน +3

    Aaa munthu wamayi kumwalira mpaka kuzabwela ngati nyamata bwino nazotu tizalandila nazo ziwanda zakomweko

    • @ChrissyChakhala
      @ChrissyChakhala 3 หลายเดือนก่อน

      H😊😊😊😊😊😊😮😊😢😢😅😅😅😮

  • @selinaalufasi3150
    @selinaalufasi3150 4 หลายเดือนก่อน +2

    ine sindikumva ataa

  • @user-dh4xl3jb9d
    @user-dh4xl3jb9d 4 หลายเดือนก่อน +1

    Zakumidima izi aaaa

  • @JosèFelixsailessFelixsailess
    @JosèFelixsailessFelixsailess 9 วันที่ผ่านมา

    Zoipatu zimenesi

  • @JamLifa-xz8nc
    @JamLifa-xz8nc 3 หลายเดือนก่อน

    Mudzina Lamulungu wachifundo komaso wachisoni khulupilani mwa mulungu mmodzi ekha ndipo wanu sameneyoyo wanu adapita ndithu

  • @janetchinga695
    @janetchinga695 4 หลายเดือนก่อน

    Kuli profet ku Tanzania ku dasalama auka anthu ambiri pitani komweko kubuza dasalama

  • @sarahkamphanga
    @sarahkamphanga 4 หลายเดือนก่อน

    Tipasileni ndithu

  • @arseniomoraisfabiao6342
    @arseniomoraisfabiao6342 3 หลายเดือนก่อน

    Tatiwuzaniko dzina lá a prophet

  • @LufanMenard
    @LufanMenard หลายเดือนก่อน

    Mmm zavta kwambili😂😂

  • @WysonMpatama-cv1mc
    @WysonMpatama-cv1mc 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi a prophet amenewa anakupatsani zingati

  • @danielmaganiza
    @danielmaganiza 4 หลายเดือนก่อน

    Munthu anamwalira Ali wankazi abwela bwela bwanji Ali wammuna mmm😢

  • @kondwanimalikita5604
    @kondwanimalikita5604 4 หลายเดือนก่อน

    Iya za boza izizi zakumidima basi anangotumiza nkhalambyo

  • @JasiGoche
    @JasiGoche หลายเดือนก่อน

    Nafe timazisowa ndipo zachitikanso ifa yotelo

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 หลายเดือนก่อน +1

    Komatu mulandira nazo mzukwa aaaaaosowa munthu wa mmkazi abwera wa mmuna bwanji aaaaakomatu

  • @user-io8ig8xm6z
    @user-io8ig8xm6z 3 หลายเดือนก่อน

    Mau zitolelen muziyankhura bwno bwno man aaha

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 4 หลายเดือนก่อน

    Tangotibweleselani ulendo wakulilongwe Kuti anayendako bwanji

  • @charityamos2183
    @charityamos2183 3 หลายเดือนก่อน

    Komadi akufanana ndi m'bale wanudi kapena zauneneri zomwezi

  • @user-nr8ww2oo4w
    @user-nr8ww2oo4w 4 หลายเดือนก่อน

    Aaaaah komatu anthu mudzikhala serious Pena inu bwanj sanabwele munthu wanu wen wen anafayo mutakhale ndi dziwanda dzaku satanic pa khomo mukumutenga munthu oti simukudziwa zoona zot dziko linayipa inu zimenezo simukudziwa ikanakhala nkhope ya munthu wanu yo bola Koma mukunamizanazo ndizosatheka

  • @livemonkaposka3714
    @livemonkaposka3714 4 หลายเดือนก่อน

    Number ya prophet please

  • @Khadjajemes
    @Khadjajemes 4 หลายเดือนก่อน

    Mwana Wako ungasowe komatu muthetsa nazo chakudya

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 4 หลายเดือนก่อน

    Zamasiku akumapeto

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 4 หลายเดือนก่อน

    Kodi video imeneyi mumajambulila foni ya tilili kapena ayi

  • @mwale1154
    @mwale1154 4 หลายเดือนก่อน

    Last day

  • @WatsonMayor-lf3ey
    @WatsonMayor-lf3ey หลายเดือนก่อน

    Eeee ngat boza koma ndozona

  • @Jermah51kennias
    @Jermah51kennias 3 หลายเดือนก่อน

    Sanabwelebe

  • @KennethKachokola-er3us
    @KennethKachokola-er3us 3 หลายเดือนก่อน

    Zoopsatu eesh

  • @slatielchipeni-zy3wb
    @slatielchipeni-zy3wb 4 หลายเดือนก่อน

    Ziwanda iziiii

  • @paulchilola5462
    @paulchilola5462 4 หลายเดือนก่อน

    Aaaa

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 4 หลายเดือนก่อน

    Zabodza izi munthuyo ndi wina

  • @mercyphiri6867
    @mercyphiri6867 4 หลายเดือนก่อน

    Timve zosatira plz

  • @BeatriceSaulo
    @BeatriceSaulo 2 หลายเดือนก่อน

    Ili ndy bodza la nyooo munthu kumwalira mximai kuzazuka ali mwamuna ndy kut chani

  • @HardyGutu
    @HardyGutu 22 วันที่ผ่านมา

    Chipo

  • @LoveNatala
    @LoveNatala 4 หลายเดือนก่อน

    Zamatsiku osiliza owerenga khala maso

  • @user-hs8vn6wc4b
    @user-hs8vn6wc4b 3 หลายเดือนก่อน

    😢

  • @AmaduJuma
    @AmaduJuma 4 หลายเดือนก่อน +2

    Zakumidima izii,akhristu musocherela ,inu munthu oti ndi wanu mungalemphele kumuzindikila?

  • @lasmoboko5989
    @lasmoboko5989 4 หลายเดือนก่อน

    Zabodza zeni zeni kulibe zimenezo

  • @user-ws2xi7ch7z
    @user-ws2xi7ch7z 4 หลายเดือนก่อน

    Inu nkhope take mwaiwala ya munthu?

  • @ShiraSaidi-oz5mx
    @ShiraSaidi-oz5mx 4 หลายเดือนก่อน

    Tionetseni munthuyo

  • @user-tj2vx2xf7e
    @user-tj2vx2xf7e 4 หลายเดือนก่อน

    Koma muzionetsako akulankhulayo ndinso munthu omwalirayo

  • @user-iq3iv8tp8t
    @user-iq3iv8tp8t 4 หลายเดือนก่อน

    Don't stress your self please,munthu àmene mukunenayo ndi scammer amango panga pretend ngati wa asma nditambwali ameneyo he used Kuma panga zakeko ku Lilongwe around kanengo komanso area 43 titamuzindikira maplan ake adathawa

  • @SurprisedDriftwood-ef3lc
    @SurprisedDriftwood-ef3lc 4 หลายเดือนก่อน

    Bodza mukufuna ma comment 5:25

  • @user-hp8du2lx3z
    @user-hp8du2lx3z 4 หลายเดือนก่อน

    Zaziii

  • @user-dk8ey5pu5w
    @user-dk8ey5pu5w 4 หลายเดือนก่อน +1

    Munthu amene anabwera kunamizira ku wa esthma uja ndi mmene ndi amene anadzafufuza maina anu

  • @EvansKatambo-hi3sr
    @EvansKatambo-hi3sr 4 หลายเดือนก่อน

    M'bale wako oti wamwalira angabwere akuoneka ngati munthu wina mkumati ndameneyo zoona?guys come on come on,these so called prophets asokoneza anthu Kwambiri,

  • @user-ju3kj9vy9e
    @user-ju3kj9vy9e 4 หลายเดือนก่อน

    Za ziii

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 2 หลายเดือนก่อน

    Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili

  • @osbornleman2500
    @osbornleman2500 4 หลายเดือนก่อน

    mmmmm profit wanama apa

  • @andrewmwachande7612
    @andrewmwachande7612 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂

  • @DolineDalison-br1et
    @DolineDalison-br1et 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂

  • @BenfordChuzu
    @BenfordChuzu หลายเดือนก่อน

    Zoopsatu

  • @user-ky4nh4wg7y
    @user-ky4nh4wg7y 3 หลายเดือนก่อน

    Koma zikoli

  • @user-kn3ym1zf3m
    @user-kn3ym1zf3m 4 หลายเดือนก่อน

    Zabodza

  • @user-ln7wg9jn4x
    @user-ln7wg9jn4x 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk

  • @augustMag
    @augustMag 4 หลายเดือนก่อน

    Funso langa ndi Ili kunena kuti koyamba kunabwera mnyamata amene amaonesa kuti Ali ndithenda yomwe amadwala m bale wanu asma eti? Ndipo abusa anakuyimbirani phone munthu mukamufuna uja anabwera simunamusama pamene wanu yemwe anamwalira ndi mkazi sichoncho tinene kuti athufe tikamwalira timakasitha matupi anthu? Muthu oti anali mzibambo kudziko lapansi pano ndiye bambo uja mwalira pozauka Kwa akufa azauka ndinthupi la mzimai? Koma anthu amene munakhala busy ndi azibusa musamale inutu ameneyo simunthu amene mumamuyembekezera ai ndichiwanda chimenecho chochokera Kwa busa pofuna kuti atchuke ku dziko kuno

  • @AnjelinaKasowanjete-fo8it
    @AnjelinaKasowanjete-fo8it 3 หลายเดือนก่อน

    🤣🤣🤣🤣🤣koma athu muri ndichibwana muthu waikidwa manda kumati wabweraso tangomvomeredzani muthu akamwarira

    • @mphatsomonjeza4371
      @mphatsomonjeza4371 3 หลายเดือนก่อน

      Zina ukamva 😅😅😅kambanga mwala munthu okhala wawo kulephera kumudziwa😂😂

  • @ThomsonNyirenda-df9io
    @ThomsonNyirenda-df9io 4 หลายเดือนก่อน

    Wasting time for nothing I can't believe that

  • @Allieshaibu8612
    @Allieshaibu8612 4 หลายเดือนก่อน

    Malawi ❤❤❤❤❤

  • @ZefaniyaWelios-e5y
    @ZefaniyaWelios-e5y 2 วันที่ผ่านมา

    poop?

  • @fredlemani
    @fredlemani 12 วันที่ผ่านมา

    Anali yemweyo kapena ayi? Nkhope imasiyana bwanji? Mprothet ameneyo anamutumiza Mulungu kapena ndani?
    You and your prothets are fools and you don't know God.

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 4 วันที่ผ่านมา

    Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo

  • @JosèFelixsailessFelixsailess
    @JosèFelixsailessFelixsailess 9 วันที่ผ่านมา

    Zoipatu zimenesi

  • @EmmaRichard-hr7jj
    @EmmaRichard-hr7jj 3 หลายเดือนก่อน

    😭😭

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 2 หลายเดือนก่อน

    Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili