MZIMAYI UYU WAUKA KWA AKUFA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 ก.พ. 2024
  • Mzimayi wauka kwa akufa

ความคิดเห็น • 120

  • @user-cy9tu3ry3z
    @user-cy9tu3ry3z 4 หลายเดือนก่อน +7

    Osati wauka koma wapezeka nthawi yodzuka anthu akufa sinakwane ameneyo anangozembetsedwa mumasenga

  • @renardgift4023
    @renardgift4023 3 หลายเดือนก่อน +6

    Ine ndimaona ngati omwalirawo ndi awawa ...
    Heading mumayika akufuna ma viewers et?

  • @user-zo4yr9rx4u
    @user-zo4yr9rx4u 4 หลายเดือนก่อน +3

    Thankyou hainifa pondifikisa mmuzi mwathu

  • @TheLeezo
    @TheLeezo 3 หลายเดือนก่อน +1

    This lady councillor isa good story teller,I like her her narration.

    • @fuzimoyo
      @fuzimoyo 3 หลายเดือนก่อน

      Zaziii basi

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 2 วันที่ผ่านมา

    Km athu tikumuseweletsa mulungu

  • @hudsonkawinga685
    @hudsonkawinga685 3 หลายเดือนก่อน

    Watching from Mfuwe Zambia

  • @IshmaelSaidi-f8l
    @IshmaelSaidi-f8l 10 วันที่ผ่านมา

    Chiwanda chimenecho

  • @ranswellngwira2102
    @ranswellngwira2102 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mamuna openera ameneyo, munthu akafa sadzukanso. Amapemperowo angomunamiza pomupasa mkazi wina.

  • @VictoriaTanthole
    @VictoriaTanthole 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mwina anangosowesedwa m'masenga nkumakagwirisidwa ntchito eeh mulungu atipase chidziwiso

  • @user-lq4kx3lk4o
    @user-lq4kx3lk4o 4 หลายเดือนก่อน

    Watching from ntchisi

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 4 หลายเดือนก่อน +1

    Chamba munthu adzafa ndi kuuka mmanda tsiku la chiweluso/kiyama ndiye izi zikuchitikazi zopanda umboni chifukwa ndiza ufiti owoneka ndi maso zomvera anthu opanda chipembezo chenicheni 😢

  • @ZakeyoCjere-bd1gj
    @ZakeyoCjere-bd1gj 4 หลายเดือนก่อน

    Khani yopatsa chidwi zikomo man of god

  • @user-eg5io6mt4t
    @user-eg5io6mt4t 4 หลายเดือนก่อน

    Aaaa sanali akufa kom anangotekedwa mpweya

  • @BerthaChitsulo-ti2mz
    @BerthaChitsulo-ti2mz 3 หลายเดือนก่อน

    Iiii izi nde ndizoopsa asaaa sizoona ayi😢😢nde ndingathawe mmmm

  • @user-ds8yo7dn3q
    @user-ds8yo7dn3q 4 หลายเดือนก่อน +1

    Sidziwanda koma asakhaletu opephelawo atumiza chiwanda chofananako ndimuthuyo

  • @whitegadama4238
    @whitegadama4238 4 หลายเดือนก่อน

    wonderful

  • @IsaacAraujoMarcelino
    @IsaacAraujoMarcelino หลายเดือนก่อน

    Amati khulupirira ngakhare usanaone brod

  • @LindaChithumba
    @LindaChithumba หลายเดือนก่อน

    Amene sanaziwone amayankhul kwambil kt sizoona. Km apropheti alipo kunj kuno akupanga zodabwitsa zimenez taziwona ife

  • @ZephaniaPhiri-ro3lw
    @ZephaniaPhiri-ro3lw 3 หลายเดือนก่อน

    Zephania from Zambia show the person ti s boza

  • @jamesmakonyola4096
    @jamesmakonyola4096 4 หลายเดือนก่อน +1

    nkhani iyi ndiyabodza ...munthu yemwe akunenedwayo amapanga ngaiti mmmutu simmayenda bwino anangosochererako coz munthuyo ndiwakwa Chinakanaka ..

  • @DicksonLongwe
    @DicksonLongwe 2 หลายเดือนก่อน

    Aaaaa tkufun wakufayo ife

  • @ConfusedBabyTurtles-gi4hb
    @ConfusedBabyTurtles-gi4hb 23 วันที่ผ่านมา

    Izizi zimakhala Zabodza , Zimangokhala zauchiwanda basi pena amakhala kt Wabwelayo wangokhala openga Chabe. It also happened ku Migowi zabodzazi but it ended up kt sanali m'bale wawo

  • @mercyphiri6867
    @mercyphiri6867 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mundkodole akabwera kulilongweko

  • @wellingtonmilanzie
    @wellingtonmilanzie 3 หลายเดือนก่อน

    Eeeh komanso mafunso ake ambwelera bwanji😅

  • @JudithLaitani
    @JudithLaitani หลายเดือนก่อน

    Izi ndizo opsa asaa 😥😥😥

  • @janetchinga695
    @janetchinga695 4 หลายเดือนก่อน

    Ndintawi ya mulungu, ndaionanso ku Tanzania munthu wabwela

  • @PaulKumwendadaire
    @PaulKumwendadaire 26 วันที่ผ่านมา

    It can not happen that's so amazing.

  • @user-id7dj6uk7t
    @user-id7dj6uk7t 4 หลายเดือนก่อน

    Shaaa

  • @KimamboPk
    @KimamboPk 16 วันที่ผ่านมา

    Zam'Zam'masiku omaliza no wonder

  • @user-zc9ku5fw4n
    @user-zc9ku5fw4n 4 หลายเดือนก่อน

    Next waiting

  • @prettytambala5687
    @prettytambala5687 2 หลายเดือนก่อน

    Amalawi tili busy

  • @fulggiechilinda809
    @fulggiechilinda809 3 หลายเดือนก่อน

    Muziika bwino ma head line anuwa mwatipu tsitsaka a khansala kukhala so ngati ndiwo muukawoka kkkk

  • @xtinabrown
    @xtinabrown 4 หลายเดือนก่อน

    Mibawa ikafike uku

  • @bashirumalikiki358
    @bashirumalikiki358 4 หลายเดือนก่อน

    Musamatiwone ngati zitsilu ife ayi khani zikungofanana bwanji ndinu agalu kabasi

  • @MatthewsNyirongo
    @MatthewsNyirongo 2 หลายเดือนก่อน

    Kumalawi nako

  • @StevenKampira
    @StevenKampira 4 หลายเดือนก่อน

    Waoo 😢😢

  • @PaulNkhoma-iu1ny
    @PaulNkhoma-iu1ny 4 หลายเดือนก่อน

    Ndinzukwa ameneyu

  • @mercyphiri6867
    @mercyphiri6867 4 หลายเดือนก่อน +1

    Amakhala kut sanafe,anangosungidwa kumagwilisidwa ntcito nde amathawako kosungidwako

    • @joyedward45
      @joyedward45 3 หลายเดือนก่อน

      Pena kumakhala kuti mwini wake amene amawasunga matsengayo wamwalira ndi palibenso owasamalira basi awatsegulira kuti adzipita zoopsatu eee

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 4 หลายเดือนก่อน +1

    Part 2 please

  • @jacquelinemagwera155
    @jacquelinemagwera155 7 วันที่ผ่านมา

    Eti osawaonetsa?

  • @gabrielmaluwa1038
    @gabrielmaluwa1038 4 หลายเดือนก่อน

    Nzukwa umenewo

  • @lindakondowole8021
    @lindakondowole8021 4 หลายเดือนก่อน

    Nde mpaka zovala zamunthu wakufa Sept amasungabe

  • @user-zf6mf4ig6w
    @user-zf6mf4ig6w 4 หลายเดือนก่อน

    Ku Lilongwe ayendako bwanji

  • @BlessingsWakhutamoyo
    @BlessingsWakhutamoyo หลายเดือนก่อน

    Vdormc

  • @user-vq1ec9qc2s
    @user-vq1ec9qc2s 4 หลายเดือนก่อน

    Mutitumizilekonso akabwela kumapemphelo uthenga umenewu

  • @user-dk8ey5pu5w
    @user-dk8ey5pu5w 4 หลายเดือนก่อน

    Angofanana

  • @mackgozambia
    @mackgozambia 4 หลายเดือนก่อน +1

    Watching from KATETE Zambia

  • @user-mk3fq2sz1x
    @user-mk3fq2sz1x 4 หลายเดือนก่อน

    Mwina ndizoona kuli apulofet kulilongwe nsewu wa kasia

  • @IdrissahSadick
    @IdrissahSadick 20 วันที่ผ่านมา

    That's just jiin

  • @user-lq4kx3lk4o
    @user-lq4kx3lk4o 4 หลายเดือนก่อน

    Malawi

  • @sibokawana2358
    @sibokawana2358 4 หลายเดือนก่อน

    Aaaaa osamuona

  • @LisaMwemba
    @LisaMwemba 22 วันที่ผ่านมา

    We need to see her face why don't you show her face?

  • @bettiemgamphula6275
    @bettiemgamphula6275 4 หลายเดือนก่อน

    Tiyamike kumwamba kuti Ambuye akuchita z

  • @kondwanimwalani
    @kondwanimwalani 4 หลายเดือนก่อน

    Chikulupililo chani ndi chachabe

  • @user-cp5ci5sb2x
    @user-cp5ci5sb2x 4 หลายเดือนก่อน

    Zozizwitsa sizizatha

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 4 หลายเดือนก่อน

    Muzatiuzenso kuti kulilongweko mwaendako bwanji

  • @user-vq9xh7qm6j
    @user-vq9xh7qm6j 4 หลายเดือนก่อน

    Zoopsa

  • @SimonKokhwave-yr2mh
    @SimonKokhwave-yr2mh 4 หลายเดือนก่อน

    Za mstsenga munthu samwalira

  • @Omwale
    @Omwale 3 หลายเดือนก่อน

    mbwerera za channel
    mzimayi uyu?

  • @IqrahSikweya-wm5mn
    @IqrahSikweya-wm5mn 21 วันที่ผ่านมา

    Bodza.... Mzosatheka munthu kufa mkuukanso...... Anali asanafe ameneo

  • @RhodrickMathewe
    @RhodrickMathewe 3 หลายเดือนก่อน

    Zaziiii

  • @MarkoNyondo
    @MarkoNyondo 4 หลายเดือนก่อน

    Nkhaniyi isanthere pompho mudzatipasilitso

  • @user-kx4og4mv5y
    @user-kx4og4mv5y 4 หลายเดือนก่อน

    Zodabwisa

  • @innocentnkhwazi2331
    @innocentnkhwazi2331 4 หลายเดือนก่อน

    Headline yamtundu wanji iyii Kodi mumangoziyamba osadziwa malembedwe ankhani etiii mxiii

  • @AgnessMasilika-ti5mn
    @AgnessMasilika-ti5mn 4 หลายเดือนก่อน

    Koma masiku otsiriza timva mkuona zinthu 😮

  • @user-wm7db8zx6g
    @user-wm7db8zx6g 4 หลายเดือนก่อน

    timakukondani komanopenapake mukamasakaniza zinthu mumatipatsa peee kuti kodi akutibwanji amenewa

  • @thokoJames-gp8mk
    @thokoJames-gp8mk 4 หลายเดือนก่อน

    Zongofuna kuwagunguza mitu anthu basi

  • @GabrielMbaweMbonongo
    @GabrielMbaweMbonongo 3 หลายเดือนก่อน

    Alady didn't die, a devil is a liar

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 4 หลายเดือนก่อน

    Yooo 😢

  • @kondwanimwalani
    @kondwanimwalani 4 หลายเดือนก่อน

    Nde simunayitane A police bwanji!?

  • @whitekabird
    @whitekabird 2 หลายเดือนก่อน

    Why don't you show the picture of a person

  • @user-jo6wr4oq2q
    @user-jo6wr4oq2q 4 หลายเดือนก่อน

    Show the face of the risen .

  • @MAFAITI
    @MAFAITI 4 หลายเดือนก่อน

    👿 Demons power😈

  • @morganchimbaka5843
    @morganchimbaka5843 4 หลายเดือนก่อน

    Chezani ndi waukayo osati akhansala ngat zandele,mafumu kulibe?? Osamatinamizatu

  • @user-lj7lm6ly7z
    @user-lj7lm6ly7z 4 หลายเดือนก่อน

    Muli mzimayi uyu wauka kwakufa ,mzimai wake uti?

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 4 หลายเดือนก่อน

    Umboni akafukule pomwe adamuika

  • @GeraldJairos
    @GeraldJairos 19 วันที่ผ่านมา

    Zochitika m'masiku otsiriza machenjera amdyerekezi
    Osakhulupira kwa tonse owerenga tiyeni tikhale mmaso,wakufa sadziwa kanthu bii

    • @GeraldJairos
      @GeraldJairos 19 วันที่ผ่านมา

      Kodi inu bambo osapeza mkazi wina,ndikupemphera ,ngati mutachita bwino nkudzakumana ku ulemerero wa mulungu

  • @LindaPita-ki2fr
    @LindaPita-ki2fr 4 หลายเดือนก่อน

    L no UN

  • @fredsemu7136
    @fredsemu7136 4 หลายเดือนก่อน

    Last days

  • @JosephKumwenda-zq8ih
    @JosephKumwenda-zq8ih หลายเดือนก่อน

    Is this true

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 4 หลายเดือนก่อน

    Munthuyo ndiyemweyo, ngati anafika ndikuyitana ana ake komanso kukumbukira munthu woti anamusambitsa panthawi yaima yake. Ndiye choti, anthu mukayikirenso ndi chiyani?

  • @felixharry3117
    @felixharry3117 4 หลายเดือนก่อน

    Koma ndi omwewo

  • @user-bo2qy6su6c
    @user-bo2qy6su6c 4 หลายเดือนก่อน +14

    Why don't you show the face of the particular person?

    • @user-vq9xh7qm6j
      @user-vq9xh7qm6j 4 หลายเดือนก่อน +1

      Exactly

    • @ramiemkwezalamba1905
      @ramiemkwezalamba1905 3 หลายเดือนก่อน

      You don't just post someone's face without his/her consent. You can be sued. I guess thats the reason. Komanso a councilor kufikila Popeleka umboni ndiye kuti ndi zoona..

  • @user-nm9gj4eu5r
    @user-nm9gj4eu5r 4 หลายเดือนก่อน

    Show us the person pliz

  • @AgnessMasilika-ti5mn
    @AgnessMasilika-ti5mn 4 หลายเดือนก่อน

    Nanga osationesa mumthuyo bwanji???

  • @NavyShachele
    @NavyShachele หลายเดือนก่อน

    Tam Navy from Zambia that's total lie

  • @JoshuaAamon
    @JoshuaAamon 3 หลายเดือนก่อน

    That is not true😂😂😂😂😂 wait for God's judgement. The problem is that these people live for a while and then die forever.

  • @BerthaChitsulo-ti2mz
    @BerthaChitsulo-ti2mz 3 หลายเดือนก่อน

    Iiiiiiii Inu munawagwilaso? Mmmmmmm zolilisa

  • @user-km1js4ne8s
    @user-km1js4ne8s 4 หลายเดือนก่อน

    Kodi anthuwo samamuzindikira meaning kuti anasintha nkhope?

  • @kondwanimwalani
    @kondwanimwalani 4 หลายเดือนก่อน

    Ali kuti!?

  • @josejoaolamissone4195
    @josejoaolamissone4195 3 หลายเดือนก่อน

    The demons and Satanic devils

  • @MatthewsNyirongo
    @MatthewsNyirongo 2 หลายเดือนก่อน

    Do you realise your age to be cheating people like this.

  • @ranswellngwira2102
    @ranswellngwira2102 4 หลายเดือนก่อน

    Amapempere ena akufunika asiyisidwe msanga kumalawiko, akupengetsa anthu kwambiri

    • @user-pl2os7yl6z
      @user-pl2os7yl6z 4 หลายเดือนก่อน +1

      Kkkkkk mulungu akuulula zisisi zake

  • @user-bo2qy6su6c
    @user-bo2qy6su6c 4 หลายเดือนก่อน

    Why don't you she person's face?

  • @user-sh6ow1mv7n
    @user-sh6ow1mv7n 4 หลายเดือนก่อน

    Familiar spirits operations and impersonation

  • @user-wq9fq1yn6l
    @user-wq9fq1yn6l 4 หลายเดือนก่อน

    Wonder shall never end

  • @user-nm9gj4eu5r
    @user-nm9gj4eu5r 4 หลายเดือนก่อน

    She was not dead

  • @kondwanimwalani
    @kondwanimwalani 4 หลายเดือนก่อน

    Bible ndi Colani sanena choncho??????

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 4 หลายเดือนก่อน +2

    Ayi sanali wakufa, Koma nzamasenga zija amakonza abathwa aja kapena ndondocha zotenga ndalama zija ndima ziwa bwino za kumeneko nkwamasenga panopa Wanthu ambiri mbiri panopa akuma bwerera nzosadabwisa kumene ndiri kuno Wanthu ambiri akufa akuma bwera ati ku Blantyre mkumene amaka gwira Ntchito mwa A mwenye

  • @nestolmafosha394
    @nestolmafosha394 4 หลายเดือนก่อน

    It will end in tears. Akamazazindikira kuti Prophet akuwabera it will be too late.
    A similar episode of 2010. Ask me

    • @thokokawaza
      @thokokawaza 4 หลายเดือนก่อน

      Tiuzeni, what happened in 2010?