Izizi zimakhala Zabodza , Zimangokhala zauchiwanda basi pena amakhala kt Wabwelayo wangokhala openga Chabe. It also happened ku Migowi zabodzazi but it ended up kt sanali m'bale wawo
You don't just post someone's face without his/her consent. You can be sued. I guess thats the reason. Komanso a councilor kufikila Popeleka umboni ndiye kuti ndi zoona..
Osati wauka koma wapezeka nthawi yodzuka anthu akufa sinakwane ameneyo anangozembetsedwa mumasenga
Ine ndimaona ngati omwalirawo ndi awawa ...
Heading mumayika akufuna ma viewers et?
Thankyou hainifa pondifikisa mmuzi mwathu
This lady councillor isa good story teller,I like her her narration.
Zaziii basi
Km athu tikumuseweletsa mulungu
Watching from Mfuwe Zambia
Chiwanda chimenecho
Mamuna openera ameneyo, munthu akafa sadzukanso. Amapemperowo angomunamiza pomupasa mkazi wina.
Mwina anangosowesedwa m'masenga nkumakagwirisidwa ntchito eeh mulungu atipase chidziwiso
Watching from ntchisi
Chamba munthu adzafa ndi kuuka mmanda tsiku la chiweluso/kiyama ndiye izi zikuchitikazi zopanda umboni chifukwa ndiza ufiti owoneka ndi maso zomvera anthu opanda chipembezo chenicheni 😢
Khani yopatsa chidwi zikomo man of god
Aaaa sanali akufa kom anangotekedwa mpweya
Iiii izi nde ndizoopsa asaaa sizoona ayi😢😢nde ndingathawe mmmm
Sidziwanda koma asakhaletu opephelawo atumiza chiwanda chofananako ndimuthuyo
wonderful
Amati khulupirira ngakhare usanaone brod
Amene sanaziwone amayankhul kwambil kt sizoona. Km apropheti alipo kunj kuno akupanga zodabwitsa zimenez taziwona ife
Zephania from Zambia show the person ti s boza
nkhani iyi ndiyabodza ...munthu yemwe akunenedwayo amapanga ngaiti mmmutu simmayenda bwino anangosochererako coz munthuyo ndiwakwa Chinakanaka ..
Aaaaa tkufun wakufayo ife
Izizi zimakhala Zabodza , Zimangokhala zauchiwanda basi pena amakhala kt Wabwelayo wangokhala openga Chabe. It also happened ku Migowi zabodzazi but it ended up kt sanali m'bale wawo
Mundkodole akabwera kulilongweko
Eeeh komanso mafunso ake ambwelera bwanji😅
Izi ndizo opsa asaa 😥😥😥
Ndintawi ya mulungu, ndaionanso ku Tanzania munthu wabwela
It can not happen that's so amazing.
Shaaa
Zam'Zam'masiku omaliza no wonder
Next waiting
Amalawi tili busy
Muziika bwino ma head line anuwa mwatipu tsitsaka a khansala kukhala so ngati ndiwo muukawoka kkkk
Mibawa ikafike uku
Musamatiwone ngati zitsilu ife ayi khani zikungofanana bwanji ndinu agalu kabasi
Kumalawi nako
Waoo 😢😢
Ndinzukwa ameneyu
Amakhala kut sanafe,anangosungidwa kumagwilisidwa ntcito nde amathawako kosungidwako
Pena kumakhala kuti mwini wake amene amawasunga matsengayo wamwalira ndi palibenso owasamalira basi awatsegulira kuti adzipita zoopsatu eee
Part 2 please
Eti osawaonetsa?
Nzukwa umenewo
Nde mpaka zovala zamunthu wakufa Sept amasungabe
Ku Lilongwe ayendako bwanji
Vdormc
Mutitumizilekonso akabwela kumapemphelo uthenga umenewu
Angofanana
Watching from KATETE Zambia
Mwina ndizoona kuli apulofet kulilongwe nsewu wa kasia
That's just jiin
Malawi
Aaaaa osamuona
We need to see her face why don't you show her face?
Tiyamike kumwamba kuti Ambuye akuchita z
Chikulupililo chani ndi chachabe
Zozizwitsa sizizatha
Muzatiuzenso kuti kulilongweko mwaendako bwanji
Zoopsa
Za mstsenga munthu samwalira
mbwerera za channel
mzimayi uyu?
Bodza.... Mzosatheka munthu kufa mkuukanso...... Anali asanafe ameneo
Zaziiii
Nkhaniyi isanthere pompho mudzatipasilitso
Zodabwisa
Headline yamtundu wanji iyii Kodi mumangoziyamba osadziwa malembedwe ankhani etiii mxiii
Koma masiku otsiriza timva mkuona zinthu 😮
timakukondani komanopenapake mukamasakaniza zinthu mumatipatsa peee kuti kodi akutibwanji amenewa
Zongofuna kuwagunguza mitu anthu basi
Alady didn't die, a devil is a liar
Yooo 😢
Nde simunayitane A police bwanji!?
Why don't you show the picture of a person
Show the face of the risen .
👿 Demons power😈
Chezani ndi waukayo osati akhansala ngat zandele,mafumu kulibe?? Osamatinamizatu
Muli mzimayi uyu wauka kwakufa ,mzimai wake uti?
Umboni akafukule pomwe adamuika
Zochitika m'masiku otsiriza machenjera amdyerekezi
Osakhulupira kwa tonse owerenga tiyeni tikhale mmaso,wakufa sadziwa kanthu bii
Kodi inu bambo osapeza mkazi wina,ndikupemphera ,ngati mutachita bwino nkudzakumana ku ulemerero wa mulungu
L no UN
Last days
Is this true
Munthuyo ndiyemweyo, ngati anafika ndikuyitana ana ake komanso kukumbukira munthu woti anamusambitsa panthawi yaima yake. Ndiye choti, anthu mukayikirenso ndi chiyani?
Koma ndi omwewo
Why don't you show the face of the particular person?
Exactly
You don't just post someone's face without his/her consent. You can be sued. I guess thats the reason. Komanso a councilor kufikila Popeleka umboni ndiye kuti ndi zoona..
Show us the person pliz
Nanga osationesa mumthuyo bwanji???
Tam Navy from Zambia that's total lie
That is not true😂😂😂😂😂 wait for God's judgement. The problem is that these people live for a while and then die forever.
Iiiiiiii Inu munawagwilaso? Mmmmmmm zolilisa
Kodi anthuwo samamuzindikira meaning kuti anasintha nkhope?
Ali kuti!?
The demons and Satanic devils
Do you realise your age to be cheating people like this.
Amapempere ena akufunika asiyisidwe msanga kumalawiko, akupengetsa anthu kwambiri
Kkkkkk mulungu akuulula zisisi zake
Why don't you she person's face?
Familiar spirits operations and impersonation
Wonder shall never end
She was not dead
Bible ndi Colani sanena choncho??????
Ayi sanali wakufa, Koma nzamasenga zija amakonza abathwa aja kapena ndondocha zotenga ndalama zija ndima ziwa bwino za kumeneko nkwamasenga panopa Wanthu ambiri mbiri panopa akuma bwerera nzosadabwisa kumene ndiri kuno Wanthu ambiri akufa akuma bwera ati ku Blantyre mkumene amaka gwira Ntchito mwa A mwenye
It will end in tears. Akamazazindikira kuti Prophet akuwabera it will be too late.
A similar episode of 2010. Ask me
Tiuzeni, what happened in 2010?