Omwalira apezeka wa moyo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 2 ก.ย. 2023

ความคิดเห็น • 67

  • @SaidShop-nf3qu
    @SaidShop-nf3qu 3 หลายเดือนก่อน +3

    Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni

  • @user-eu9xe6wl8b
    @user-eu9xe6wl8b 9 หลายเดือนก่อน +1

    Great work prophet❤🎉

  • @tonyteixeira2463
    @tonyteixeira2463 วันที่ผ่านมา

    Tolo
    Thoko😅

  • @nimrodkapingatheu5475
    @nimrodkapingatheu5475 9 วันที่ผ่านมา

    Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....

  • @user-yy6rj5lc4i
    @user-yy6rj5lc4i 10 หลายเดือนก่อน +3

    Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri

  • @hawabanda-xs5fx
    @hawabanda-xs5fx 9 หลายเดือนก่อน +2

    Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh 10 หลายเดือนก่อน +3

    Ukulu wa Mulungu tauona

  • @IvvyMakuluni
    @IvvyMakuluni 10 หลายเดือนก่อน +1

    Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂

    • @user-lc7ji1gn9w
      @user-lc7ji1gn9w 10 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka

  • @user-lz1ry1sm4j
    @user-lz1ry1sm4j 7 หลายเดือนก่อน +1

    Too bad. The name of the Lord is a strong tower

  • @richsambakusi424
    @richsambakusi424 9 หลายเดือนก่อน +1

    Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 13 วันที่ผ่านมา

    Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?

  • @user-rv8gi4ro6r
    @user-rv8gi4ro6r 10 หลายเดือนก่อน +2

    Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya

  • @MadalitsoHope
    @MadalitsoHope 8 หลายเดือนก่อน

    Zamphavu 🙏👏 prophet

  • @collinstrevor
    @collinstrevor 10 หลายเดือนก่อน +1

    Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo

  • @MussaIbla
    @MussaIbla 10 หลายเดือนก่อน +1

    Eish zovesa chisoni kwambiri

  • @esthermakwinja3207
    @esthermakwinja3207 10 หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke

  • @JosophineSolobala-hp5ds
    @JosophineSolobala-hp5ds 4 หลายเดือนก่อน

    So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢

  • @rachealphiri3416
    @rachealphiri3416 10 หลายเดือนก่อน +3

    It happened in Zambia twice

    • @ephraimphiri5789
      @ephraimphiri5789 9 หลายเดือนก่อน

      Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...

  • @BaxterChipofya
    @BaxterChipofya หลายเดือนก่อน

    Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed

  • @CostaCasimiro
    @CostaCasimiro 7 หลายเดือนก่อน

    Blassa semanal agovati ndi agedo

  • @user-lc7ji1gn9w
    @user-lc7ji1gn9w 10 หลายเดือนก่อน

    Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮

  • @oswardmwale216
    @oswardmwale216 8 หลายเดือนก่อน

    Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo

  • @BaxterChipofya
    @BaxterChipofya หลายเดือนก่อน

    Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B

  • @JusticeMakwinja
    @JusticeMakwinja 2 หลายเดือนก่อน

    Tikufuna busayo ndithu

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr 10 หลายเดือนก่อน +3

    Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂

    • @josephnanyanga2012
      @josephnanyanga2012 7 หลายเดือนก่อน

      koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please

    • @user-zc9ku5fw4n
      @user-zc9ku5fw4n 5 หลายเดือนก่อน

      Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 10 หลายเดือนก่อน +3

    Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje

    • @peterbakuwo1249
      @peterbakuwo1249 10 หลายเดือนก่อน

      🙆🙆🙆🙆

    • @adamusaidih8570
      @adamusaidih8570 10 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk

    • @oliviaolivia4979
      @oliviaolivia4979 10 หลายเดือนก่อน

      Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila

    • @mbawabuliyan9704
      @mbawabuliyan9704 10 หลายเดือนก่อน +1

      Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji

    • @florencebonga3211
      @florencebonga3211 10 หลายเดือนก่อน

      Ambuye alandile ulemu 🙏

  • @josephnanyanga2012
    @josephnanyanga2012 7 หลายเดือนก่อน +1

    ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 10 หลายเดือนก่อน +2

    Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi

  • @BlessingsBanda-qn7xr
    @BlessingsBanda-qn7xr 10 หลายเดือนก่อน

    Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu

  • @ChisomoKapanda-jg2uf
    @ChisomoKapanda-jg2uf 10 หลายเดือนก่อน

    Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 13 วันที่ผ่านมา

    Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?

  • @user-dt8nr1zx6e
    @user-dt8nr1zx6e 10 หลายเดือนก่อน

    Taona nawo zikomo

  • @user-zk5nu5fh6l
    @user-zk5nu5fh6l 10 หลายเดือนก่อน

    Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga

  • @marthacassam
    @marthacassam 9 หลายเดือนก่อน

    Zaulendo uno tiona zithu

  • @liki-likiladies---lilongwe6963
    @liki-likiladies---lilongwe6963 10 หลายเดือนก่อน +1

    Divine postmortem

  • @adamusaidih8570
    @adamusaidih8570 10 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti

  • @AmusedSakura-dx1nw
    @AmusedSakura-dx1nw 6 หลายเดือนก่อน

    Lord have mercy

  • @user-ek7vg7ld8h
    @user-ek7vg7ld8h 9 หลายเดือนก่อน

    chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 10 หลายเดือนก่อน

    Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.

  • @KINGMANMAKALA-hb9gs
    @KINGMANMAKALA-hb9gs 10 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂

  • @chimwemwemaquesuwell5841
    @chimwemwemaquesuwell5841 10 หลายเดือนก่อน +3

    Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo

  • @YusufMolesi-vr4pn
    @YusufMolesi-vr4pn 10 หลายเดือนก่อน

    Hy

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 10 หลายเดือนก่อน

    Shame😢

  • @AriohChauluka-lm9oo
    @AriohChauluka-lm9oo 9 หลายเดือนก่อน

    M

  • @hawabanda-xs5fx
    @hawabanda-xs5fx 9 หลายเดือนก่อน

    Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn

    • @rooseveltmtemula2643
      @rooseveltmtemula2643 9 หลายเดือนก่อน

      😂😂 Paja timafera ma jekete... Koma awawa voice yawo ikuchita kumveka kuti ndi a prophet di

    • @patriciacraiton-sf5vu
      @patriciacraiton-sf5vu 8 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂

  • @mbawabuliyan9704
    @mbawabuliyan9704 10 หลายเดือนก่อน

    Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike

  • @user-ux8qz1tg7l
    @user-ux8qz1tg7l 10 หลายเดือนก่อน +1

    Number ya abelo pls pls ol ya abusa

    • @SaidShop-nf3qu
      @SaidShop-nf3qu 3 หลายเดือนก่อน

      Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 10 หลายเดือนก่อน +1

    Zomvesa chisoni kwambili

  • @user-fq3jz4hl4c
    @user-fq3jz4hl4c 10 หลายเดือนก่อน +1

    Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo

    • @rooseveltmtemula2643
      @rooseveltmtemula2643 9 หลายเดือนก่อน +1

      Ineso ndikuifuna ngati munaipeza please share

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh 10 หลายเดือนก่อน

    Abelo ukutiona kupusa