ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก
ต่อไป
เล่นอัตโนมัติ
ACHEWA AKU DOWA ASAMBWAZA EE!!🙌🙌HOT 265
มุมมอง 18K
ZINTHU ZODABWITSA ZOMWE ZAONEKERA POKONZEKERA ZISANKHO🤔🤔🤔HOT 265
มุมมอง 38K
[UNCUT] The Loyal Pin ปิ่นภักดิ์ EP.3 (3/4)IDOLFACTORY OFFICIAL
มุมมอง 600K
เปิดหน้าพ่อแม่ครั้งแรก! ไม่เคยบอกใครมาทั้งชีวิตเพราะ?Ajumma Nammy
มุมมอง 504K
10ปี ไม่สาย หมิว-วิลลี่ ใน ตีท้ายครัว | หมิว ลลิตา | ตีท้ายครัว 18 ส.ค.67 คลิปเต็ม (Eng Sub)เงาะ ทีวี ngoa tv
มุมมอง 183K
Jacob Omutuuze alaze byayize mu kufa kwa Tamale Mirundi | Unveiled ExperienceSalt Media Uganda
มุมมอง 1.2K
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDOZodiak Malawi
มุมมอง 76K
NKHANI YONSE MWATSATANI TSATANI/ NKHANI ZOMWE ZACHITIKAHOT 265
มุมมอง 16K
Zomwe Zinachitika Kut Ndege IsoweSam Malvitha
มุมมอง 228K
Secretary-General Zara Mohammed at Islam channel GalaMuslim Council of Britain
มุมมอง 12K
ZOMWE AYANKHULA VICE PRESIDENT MICHAEL USI.21 June 2024HOT 265
มุมมอง 194K
ฟังสดเดอะโกสเรดิโอ 18/8/2567 เรื่องเล่าผีเดอะโกสTheghostradioOfficial
มุมมอง 543K
อดีตตำรวจเตะเณรปากแตก ข้อหาซุกเมียผม ลั่นเคลียร์มาให้จบจะเอายังไง l EP.1738 l 16 ส.ค.67โหนกระแส [Hone-Krasae] official
มุมมอง 1.5M
[TH] VALORANT Champions Seoul - Playoffs Day 5 - FNC vs SENVALORANT Esports Thailand
มุมมอง 136K
ลุงตู่มาเหนือเมฆจริงๆทักษิณติดกับดักรัฐธรรมนญปี60แล้วจ่อโดนยุบพรรคอีกมอเตอร์ไซค์ อินดี้
มุมมอง 140K
居然见到了图片上的红烧牛肉面!该死!又被秀到了! #funny#生活#搞笑东东一家
มุมมอง 3.1M
"มนต์ชัย" ชนะขาดลอย นั่งนายก อบจ.พิษณุโลก อีกสมัยสํานักข่าวไทย TNAMCOT
มุมมอง 146K
คราวหลังอย่าให้พ้ออีกประธานฮ่าง Channel
มุมมอง 226K
Uku ndiye kulankhula kwachilungamo.
Mwayakhula bwino mr namalomba ambuye akutetedzeni
That’s exactly good speech!!!!
A DPP malamulo mumawadziwa koma? Komanso malemu akoma lero chifukwa atisiya? Suja mumati ndi njoka yosafunika kuweta. Use your heads please
Inutu mulibe umunthu wamva
Very true 😢imfa iyi will stay in our hearts, MTSRIP 🌹,
After the Death of Bingu DPP was busy that night to abuse the law by trying to replace Bingu with APM.
Malawi has lost a true leader. A man of wisdom. RIP Dr Chilima. It's sad indeed.
Kuyankhula kwa umunthu uku Mr Namalomba mulungu akudalitseni ndipo akulise malire anu
Replacement ya Bingu before death announcement kuti Peter alowe.
DPP afuna awoneke ngati Ma angele😂😂😂😂 .izi ndiye mbava za mbava
Yes kuyankhula mr Namalomba big up
Ku yowoya, unenesko dpp chipani cha mutendele Dpp my vote u munthu nde umenewo
Mwayankhula zoona Mr Namalomba,tinataya munthu amene ifeyo timayan'ganapo maso athu kuti azatithandiza ndimaso mphenya amene adali nawo.
😂😂Koma dziko ndi ndale eee anakonza lero DPP kulira kuli kufuna mavote a UTM 😂😂😂
Ndizowona ife tikulira maliro sitingakhale tikuvina bale wantchu titaluza😢
Palibe cha nzeru mwalankhula apa paja ukakhala otsutsa umafuna kukhala wa nzeru..
Ndipo ndi zoona DPP ndiyoferedwa
Osati boza lnu enafe president wanthu anamwalira osati lzi zamanganya yudasi uyo anamupereka chilima
Namalomba usatitsokoneze mitu wamva pangani zanu ndi gogo wako wa DPP
Namalomba mudzaziona mukadzatenga boma
Namalomba wasowa chorankhura pamenepa, ndibwino akanangoti ndiribe mawu .
😂😂😂bro choyankhula ndichimenecho
Koma ndizoonad umuthu uzikhalapo nanga malikhwelu ameneaja zulo ayi sizoona
Malamulo azikhala ndi umunthu mmmmmh inu ndachitsilu eti who made the constitution Dr Laz M Chakwela?
Malawi and politics
No one above the laws ....lamulo likuenera ligwire ntchito posaendera umunthu or chikhalidwe
I mourning SKC RIP
Koma Malawi umunthu udaticgokeladi eti inu A DPP Chilima akome lero poti watisiya? Si zija Peter Mtharika akhala kuti anakuchosani mu Boma mwakhala mukumunyoza lero mukati eni imfa kuti chani sopano? Ndipo mwachita bwino kubwela poyela taziwano kuti Maliro mwapezelapo campaign umboni ndi ma 1 billion timawona ngati kulila kuli kunyengelela kuti mloweso mu Boma.
Malamulo wakupanga mbanthu wene wawo wa wangasinthaso
Namalomba nice tolk
eeeee kuyankhula kopanda chigamba thank you namalomba
Pajatu chilungamo chimawawa anyapalawa mchaka sakumvetsa,point yawo akuti imfa ija yawawa kusonyeza kuti mphamvu alibe musakakamile,imfa yatameki ndiyodwanzika imakhala yosiyana kalilidwe khalani ndi umunthu point taken
Chakwela samagwila Muthu Kodi tisiwisen zoona
Chilimatu ndale anayambira ku DPP ndiye a MCP chilichonse akuyesa ochenjera adzaziona
Nambalomba tauzen zoona amalawi kuti a dpp mukanali buzy kusangalala kumwa wine 🍷 ndi imfa ya achilima
Izi zikufunika mukakambilane ku nyumba ya malamulo anthu adayamba kukakhula kuti wadutsa thawi
DPP maboza kulira kuposa eni ake maliro? Lamuro ndi umunthu ndizosiyana zikuwapweteka awa ndipo sazabwelanso muboma
Mumafuna asankhe wa mcp, kuti mupezerepo zoyankhula kuwagawanitsa a utm ndi mcp😂😂😂
Zoona .anthu awa ndi a chameleon
Sichifukwa choti inu kaya mzalowa m boma kapena ayi koma ndinu chisilu adpp mulibe nzelu nkuona mathangisa anzanu mchipani nzelu mlibe
It's too early, samayenera kusankha panopa mlowa mmalo ai
A Namalomba ndinu member of Parliament, bwanji osakasintha malamulo????
Kusintha malamulo si kwa a Namalomba okha komanso lero ndi lero sizingatheke aphungu kapena phungu amangopereka maganizo oterwo kenako nyumba ikambirane komanso a dzamalamulo awunike ngati ndikoyenera kutero sasintha ngati Malaya monga mmene Inu mukuganiziramo 😂😂😂😂😂😂
Pitala wakoyo adameza miyala sadzafa anthu oipa kwambiri ngakhale mumayankhilako mulibe nzeru mfiti pano malonino akhala mwamtendele kwambiri
namalomba palibe chimene uzayamikila ngakhale adakasankha mkazi wako
Koma ndale za anamalomba ndizoseketa kwa basi
Iwe nde sugaiza
Mwayankhula bwino kwambiri a Namalomba
Nalomba Usamati president wathu ayi chakwela ayi agalu yu chichakwela mbudzi yachakwela chi machendake jfe kumalawi tidzakhala ndi president 2025 Peter muthalika ndamene tikudikila
Uziyambira kutchula machende a bambo ako aja usananene amunthu wina
Uilondole ku nyanja konko nkhalamba yakoyo izikakutuma kokagula kachasu😊😊😂😂
Kutukwana ndikumene anthu ambiri sitikonda dpp, mukatukwana mumasonyeza kuchepa nzeru ndipo mukuchotsa ma voti
Awa ndi achisilu kwambiri chilichose chandale chomwe angalakhule Mesa chilima munamukana
Kodi iweyotu ndi bwampini palibe chamzeru chimene umachiona kamtima ka ngona ku mcp kwakoko usamatinyase apa 😢
@@SolomonNjolomole panyapako pa mako wava
Udachokera kutiko swiswiri iwe paja adakuponya mchimbudzi chitsiru chamunthu iwe.
Mmafuna asankhe vice ku DPP
Boza inu adpp inuyo mwasangalala kuti achilima amwalila bingu anamwalira koma lamulo linagwila ntchito inu mwaziwona liti anamalomba ndinu ausilu msapange ndale pamaliro ayi
Amene mwasangalala ndi inu a MCP sipaja mukufuna Chakwera apezeke pa ballot paper.
Mulungu akunkhululukile iweyo wa MCp iwe anthu 9 anafa Anja iweyo Uli gulumo
Za ziiii
Zilikutiko