Koma MCP ndi zigawenga zoopsa ndithu Koma chakwera wulindi wumunthu chilowere mu boma wunawononga Malawi panopa wuli ndi sanje chifukwa wukuziwa Kuti iwe kuyendesa boma walemphera
Koma chakwera mtima wake ndioyipa kwa basi nthawi yonseyi m'mene tavutikira munthu opanda kuganiza bwino ndi amene azaponya vote kwa iwe koma munthu oganiza bwino adzavotera ena osati iwe chakwera watikwana ife .
Mcp ndi yokupha timaziwa ifeyo kuti mcp ndi zigawenga fisi ndi fisi sangasinthe manga ndie mcp ndi makape okha okha kmaso apolice ndi mdf musamawapange trust kmaso ndi ma judge kod police ndi mcp anaigula panopa ili manja mwa chakwera ndie apolice
Inu a Namiwa tikukuprmphani kuti kutsogoloko musazasithe mawanga chifukwa sitinayiwale kuti nthawi ya DPP inu munali ku State House. Tikudziwa kuti inu mukutumikira chipani chotsusa. DPP ili m'boma inasakaza ndalama za boma zankhani nkhani pogwiritsa ntchito mabungwe monga Escom, Water board ndi zina zambiri. Kunapezeka anthu ambiri a DPP kusanduka ma millionaire munthawi yochepa kwambiri. Palibe chomwe mungatiuze DPP inalepheranso kukwaniritsa zofuna zambiri za a Malawi. Ma blue night ife sitikuwafunanso.
Ndikunenesa apa Kuti chakwera sangawine akazawina chakwera ndiye Kuti chakwera wabera mavoti chifukwa kunena zoona Malawi wawonongeka ndi chakwera zinthu sizilibwino mpang' ono pomwe
I have No doubt Emusipi ndi Chipani Cha Nkhanza
A police akumalawi palibe chimene angapange chifukwa ndiwoledzela ndi umphawi makamaka akalaya zoti kwatsala masiku 400 kuti ufumu uwu ugwe sakudziwa
Ameneyo Ali kubali ya MCP Chakwera ndi a police amene
Chakwela mbuzi
Moses kodi umayakhula bwanji?apolice omwe ukuwayakhulawo bwanji anthu omwe adakhapa anthu aku Lilongwe adagwidwa mpaka pano kuli ziii pena moses ukamayakhula uzidziwa kuti naweso udabadwa ndi munthu,komaso pampandopo padali nzako amayakhulaso ngati mene ukuyakhuliramo koma pano adachokapo nde iweyo ukamayakhula ngatitu suzachokapotu pompo.Nde ife tikupepha apolice agwire ntchito yawo yowafufuza anthu omwe apanga upandu akufufuza asayiwaleso kugwira anthu omwe adakhapa anthu aku Lilongwe,
Kodi akukuyu ndiye ndani galu ya munthu
Nduna yaku bagamoyo, RIP Allan wittka
Ndizithu zovesa chisoni coz aboma sakuonesa chidwi pa ziwembu zikuchitika.
Police singagwile tchito moyenela ndi emusipi gromp imenei koma Malawi anakodza umbuli wausogoleli nde problem
Tisadalile apolice chifukwa apolice akumalawi palibe tchito yomwe akugwila tiyeni titanile pa dzina lamulungu chifukwa ndiye yekhayo angatipilumutse ku zikhanila zimenezi
Kunkuyu time will come for a judgement day
Inuyo a Silvester Namiwa ndiinu munthu yekhayo yemwe akusonyedza kuimilira a Malawi komanso chitsanzo chabwino
Kumalawi mwatipanikiza abale kupuma kulibe tikapuma kumwamba
zopusa agalu inu tikumana 2025 mbuzi zanthu inuu
Namiwa uli bho kwambiri
chakwera ndi chitsiru
Apolicewonso mesa ndi a MCP nso ndiye azifufuza zichani? Za DPP zija si mpaka lero izinso sapanga kanthu
Aaaaa utsogoleri wabwino umaoneka nizipatsozake apa tikuona mathandizo nizina zotelo zikuchitika komaso zikubwera mdziko lino tiwathokoze achakwera
Chongofunika apa ndichoti, Kuykendall okhonzeka India bouncer a bhobho, ndikungokwanitsa kumugwira olo m'odzi, ndikumutikita mpakana aulule amene akuwatuma ndikumpanga record ngati umboni.
Koma Mcp siizatheka ndi nkhaza
boma lazitsiru ili kumkuyu ndi mbuzi ya munthu ndi apolice apolice ndi a mcp ndimakape
Koma MCP ndi zigawenga zoopsa ndithu Koma chakwera wulindi wumunthu chilowere mu boma wunawononga Malawi panopa wuli ndi sanje chifukwa wukuziwa Kuti iwe kuyendesa boma walemphera
Koma chakwera mtima wake ndioyipa kwa basi nthawi yonseyi m'mene tavutikira munthu opanda kuganiza bwino ndi amene azaponya vote kwa iwe koma munthu oganiza bwino adzavotera ena osati iwe chakwera watikwana ife .
Akukanika kugwira anthu amene akupangira chiwembu anthu azipani zina koma munthu amene watukwana iwowo, mulungu atithandize
Ine kunkuyu kungokumana naye azandipha
Mcp ndi yokupha timaziwa ifeyo kuti mcp ndi zigawenga fisi ndi fisi sangasinthe manga ndie mcp ndi makape okha okha kmaso apolice ndi mdf musamawapange trust kmaso ndi ma judge kod police ndi mcp anaigula panopa ili manja mwa chakwera ndie apolice
Apolice akumatan ziwembu zikachitika? Naye Nkukuyu mbuzi
Kunkuyu ndi galu kwabasi, a Chipani cha dpp ana khapidwaso ndi mcp bwanji sakumangidwa?
A kukuyu ndinu mfiti otamba ndi kudya nyama yayiwisi
Chakwera sangatheke olo pang,ono muthu waji osava chison
Nthawi yowopsezana inatha kale and tili mu nthawi ya Democracy not one party system, Chakwera ndi mbamva zinzake adziwiretu kuti nthawi yawo yatha.
Kunkuyu ndi chitsilu kobasi, ndipo adziwa kuti ndi achipani chawo MCP yikuchita zipolowe
Mai uyu ndiwabodza omenyedwa aja sadanenepo kuti Anthu anavala makaka achipani atawafunsa amangoti mabausa
A police amanganidi anthu awa? inu mukukhulupilira ine ndendakayika kobasi
Achinyamata tizikhala mu umbuli mpaka liti? For how long shall we live such a barbaric life? Chonsecho mnyumba mwako umphawi uli tho!
Ndipo zosayenda
Mcp sizatheka ndi nkhaza
Kunkuyu machende ako
Kod awasila bwanj apolic kumachit kt ngakhal apolisio amalamulidw ndi olamul ngakhala A dpp amachit chimodz modz
Mwaiwal chilam adagendedwa kuthyol
Moses kukuyu ndiwe Gulu ndi chakwela 2025 mukupita
Iya chakwera iwe watikwana ife kumupoto nafeso tikhare ni president wathu basi
Palibeso anthu ena opanga anzawo zipongwe ndi amcp basi, iwe Moses kukuyimbiran usamale ndimbuzi inzakoyo chakwera mbuziyo kumpoto msazabwereko agalu inu
Apatu ofunika aliyense kumayenda ndi zida apa diso kulipa diso
MCP ndi yakupha,
Panyini pa mayi ako kunkuyu iwe
A police akulowelela ndale koma awonatu zovuta
UDF mfundo yabwino kwambiri zipangisa Kuti atanbwari osiyasiya zipani Kuti asowe kolowera komanso zilimbikisa kukhazikika pa chipani
MOSES KUKUYU AND GOVERNMENT MUSAMALE KWAMBIRI
Ndipo kwambiri
Amenewotu azaphedwa akukuyo ndi achimundu banda kmaso ndi azizawo onse mpakana ndi chakwera yemweo ka
Andale muphana komaso mutukwanana. Akulu akulu aliphee inu umphawi ukuphetsani lekani kutsatila ndale ingodikilani tsiku lovota
Apolice sangapange chilichose kukhuzana ndichipani cha MCP why apolice athu alimukhwapa mwa chakwela chimozi mozi ngati mene anamuyikila mukhwapa matha chizuma koma pangatalike misonkho ya Malawi mukadya nayo khobwe opanda chele
Cakwera ndi wasatanic palibe comwr angathandidzepo pakhani chifukwa iye ndi yemwe akutuma anthu kt adzivuladza anzawo iyeyo adzitenga magazi adzipita nawo kusatanic cakwera mbusa wakumidima leka kudzudza anthu dziko silako
chakwela ndi kukuyu ndi mbuzi nza wathu
Inu a Namiwa tikukuprmphani kuti kutsogoloko musazasithe mawanga chifukwa sitinayiwale kuti nthawi ya DPP inu munali ku State House. Tikudziwa kuti inu mukutumikira chipani chotsusa. DPP ili m'boma inasakaza ndalama za boma zankhani nkhani pogwiritsa ntchito mabungwe monga Escom, Water board ndi zina zambiri. Kunapezeka anthu ambiri a DPP kusanduka ma millionaire munthawi yochepa kwambiri. Palibe chomwe mungatiuze DPP inalepheranso kukwaniritsa zofuna zambiri za a Malawi. Ma blue night ife sitikuwafunanso.