NKHANI YONSE MWATSATANI TSATANI/ NKHANI ZOMWE ZACHITIKA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 17 พ.ค. 2024

ความคิดเห็น • 56

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 20 วันที่ผ่านมา +1

    Ndikunenesa apa Kuti chakwera sangawine akazawina chakwera ndiye Kuti chakwera wabera mavoti chifukwa kunena zoona Malawi wawonongeka ndi chakwera zinthu sizilibwino mpang' ono pomwe

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 21 วันที่ผ่านมา +2

    I have No doubt Emusipi ndi Chipani Cha Nkhanza

  • @MonicamakwembaKunika
    @MonicamakwembaKunika 22 วันที่ผ่านมา +3

    A police akumalawi palibe chimene angapange chifukwa ndiwoledzela ndi umphawi makamaka akalaya zoti kwatsala masiku 400 kuti ufumu uwu ugwe sakudziwa

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q 19 วันที่ผ่านมา

    Ameneyo Ali kubali ya MCP Chakwera ndi a police amene

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 21 วันที่ผ่านมา

    Chakwela mbuzi

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh 21 วันที่ผ่านมา +1

    Moses kodi umayakhula bwanji?apolice omwe ukuwayakhulawo bwanji anthu omwe adakhapa anthu aku Lilongwe adagwidwa mpaka pano kuli ziii pena moses ukamayakhula uzidziwa kuti naweso udabadwa ndi munthu,komaso pampandopo padali nzako amayakhulaso ngati mene ukuyakhuliramo koma pano adachokapo nde iweyo ukamayakhula ngatitu suzachokapotu pompo.Nde ife tikupepha apolice agwire ntchito yawo yowafufuza anthu omwe apanga upandu akufufuza asayiwaleso kugwira anthu omwe adakhapa anthu aku Lilongwe,

  • @YasinSabili-dj9xe
    @YasinSabili-dj9xe 19 วันที่ผ่านมา

    Kodi akukuyu ndiye ndani galu ya munthu

  • @mrsmoseskita9180
    @mrsmoseskita9180 21 วันที่ผ่านมา

    Nduna yaku bagamoyo, RIP Allan wittka

  • @CharlesChamveka
    @CharlesChamveka 22 วันที่ผ่านมา +1

    Ndizithu zovesa chisoni coz aboma sakuonesa chidwi pa ziwembu zikuchitika.

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 21 วันที่ผ่านมา

    Police singagwile tchito moyenela ndi emusipi gromp imenei koma Malawi anakodza umbuli wausogoleli nde problem

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 21 วันที่ผ่านมา +1

    Tisadalile apolice chifukwa apolice akumalawi palibe tchito yomwe akugwila tiyeni titanile pa dzina lamulungu chifukwa ndiye yekhayo angatipilumutse ku zikhanila zimenezi

  • @kondwanimunthali7401
    @kondwanimunthali7401 21 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu time will come for a judgement day

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 22 วันที่ผ่านมา +1

    Inuyo a Silvester Namiwa ndiinu munthu yekhayo yemwe akusonyedza kuimilira a Malawi komanso chitsanzo chabwino

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 20 วันที่ผ่านมา

    Kumalawi mwatipanikiza abale kupuma kulibe tikapuma kumwamba

  • @LamiziIgshaan
    @LamiziIgshaan 18 วันที่ผ่านมา

    zopusa agalu inu tikumana 2025 mbuzi zanthu inuu

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y 21 วันที่ผ่านมา

    Namiwa uli bho kwambiri

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 21 วันที่ผ่านมา

    chakwera ndi chitsiru

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w 21 วันที่ผ่านมา

    Apolicewonso mesa ndi a MCP nso ndiye azifufuza zichani? Za DPP zija si mpaka lero izinso sapanga kanthu

  • @SinoyaChild
    @SinoyaChild 21 วันที่ผ่านมา

    Aaaaa utsogoleri wabwino umaoneka nizipatsozake apa tikuona mathandizo nizina zotelo zikuchitika komaso zikubwera mdziko lino tiwathokoze achakwera

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 21 วันที่ผ่านมา

    Chongofunika apa ndichoti, Kuykendall okhonzeka India bouncer a bhobho, ndikungokwanitsa kumugwira olo m'odzi, ndikumutikita mpakana aulule amene akuwatuma ndikumpanga record ngati umboni.

  • @BashielSalade
    @BashielSalade 21 วันที่ผ่านมา

    Koma Mcp siizatheka ndi nkhaza

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 21 วันที่ผ่านมา

    boma lazitsiru ili kumkuyu ndi mbuzi ya munthu ndi apolice apolice ndi a mcp ndimakape

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 20 วันที่ผ่านมา

    Koma MCP ndi zigawenga zoopsa ndithu Koma chakwera wulindi wumunthu chilowere mu boma wunawononga Malawi panopa wuli ndi sanje chifukwa wukuziwa Kuti iwe kuyendesa boma walemphera

  • @PatriciaMkwenda-xc4mh
    @PatriciaMkwenda-xc4mh 21 วันที่ผ่านมา

    Koma chakwera mtima wake ndioyipa kwa basi nthawi yonseyi m'mene tavutikira munthu opanda kuganiza bwino ndi amene azaponya vote kwa iwe koma munthu oganiza bwino adzavotera ena osati iwe chakwera watikwana ife .

  • @HopesonJailosi-vd6ou
    @HopesonJailosi-vd6ou 21 วันที่ผ่านมา

    Akukanika kugwira anthu amene akupangira chiwembu anthu azipani zina koma munthu amene watukwana iwowo, mulungu atithandize

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w 21 วันที่ผ่านมา

    Ine kunkuyu kungokumana naye azandipha

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 21 วันที่ผ่านมา

    Mcp ndi yokupha timaziwa ifeyo kuti mcp ndi zigawenga fisi ndi fisi sangasinthe manga ndie mcp ndi makape okha okha kmaso apolice ndi mdf musamawapange trust kmaso ndi ma judge kod police ndi mcp anaigula panopa ili manja mwa chakwera ndie apolice

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 21 วันที่ผ่านมา

    Apolice akumatan ziwembu zikachitika? Naye Nkukuyu mbuzi

  • @isaaczidana2914
    @isaaczidana2914 21 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu ndi galu kwabasi, a Chipani cha dpp ana khapidwaso ndi mcp bwanji sakumangidwa?

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 21 วันที่ผ่านมา

    A kukuyu ndinu mfiti otamba ndi kudya nyama yayiwisi

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 22 วันที่ผ่านมา

    Chakwera sangatheke olo pang,ono muthu waji osava chison

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 22 วันที่ผ่านมา

    Nthawi yowopsezana inatha kale and tili mu nthawi ya Democracy not one party system, Chakwera ndi mbamva zinzake adziwiretu kuti nthawi yawo yatha.

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 21 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu ndi chitsilu kobasi, ndipo adziwa kuti ndi achipani chawo MCP yikuchita zipolowe

  • @CharlesBanda-kv8bh
    @CharlesBanda-kv8bh 22 วันที่ผ่านมา

    Mai uyu ndiwabodza omenyedwa aja sadanenepo kuti Anthu anavala makaka achipani atawafunsa amangoti mabausa

  • @thomasbodo4099
    @thomasbodo4099 21 วันที่ผ่านมา

    A police amanganidi anthu awa? inu mukukhulupilira ine ndendakayika kobasi

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 21 วันที่ผ่านมา +1

    Achinyamata tizikhala mu umbuli mpaka liti? For how long shall we live such a barbaric life? Chonsecho mnyumba mwako umphawi uli tho!

  • @BashielSalade
    @BashielSalade 21 วันที่ผ่านมา

    Mcp sizatheka ndi nkhaza

  • @sungananigondwe2807
    @sungananigondwe2807 21 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu machende ako

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 22 วันที่ผ่านมา

    Kod awasila bwanj apolic kumachit kt ngakhal apolisio amalamulidw ndi olamul ngakhala A dpp amachit chimodz modz
    Mwaiwal chilam adagendedwa kuthyol

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 21 วันที่ผ่านมา

    Moses kukuyu ndiwe Gulu ndi chakwela 2025 mukupita

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 21 วันที่ผ่านมา

    Iya chakwera iwe watikwana ife kumupoto nafeso tikhare ni president wathu basi

  • @BeatriceMANDEVUGONDWE-iv4gr
    @BeatriceMANDEVUGONDWE-iv4gr 22 วันที่ผ่านมา

    Palibeso anthu ena opanga anzawo zipongwe ndi amcp basi, iwe Moses kukuyimbiran usamale ndimbuzi inzakoyo chakwera mbuziyo kumpoto msazabwereko agalu inu

  • @patrickdzombe461
    @patrickdzombe461 22 วันที่ผ่านมา

    Apatu ofunika aliyense kumayenda ndi zida apa diso kulipa diso

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 21 วันที่ผ่านมา

    MCP ndi yakupha,

  • @user-vg3os8xx5t
    @user-vg3os8xx5t 22 วันที่ผ่านมา

    Panyini pa mayi ako kunkuyu iwe

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 21 วันที่ผ่านมา

    A police akulowelela ndale koma awonatu zovuta

  • @Hendersonspoon
    @Hendersonspoon 21 วันที่ผ่านมา

    UDF mfundo yabwino kwambiri zipangisa Kuti atanbwari osiyasiya zipani Kuti asowe kolowera komanso zilimbikisa kukhazikika pa chipani

  • @user-hk1lp2ho9w
    @user-hk1lp2ho9w 22 วันที่ผ่านมา +1

    MOSES KUKUYU AND GOVERNMENT MUSAMALE KWAMBIRI

    • @KENETHMAJASA-ud5ee
      @KENETHMAJASA-ud5ee 21 วันที่ผ่านมา

      Ndipo kwambiri

    • @user-jl6sq3ph1b
      @user-jl6sq3ph1b 21 วันที่ผ่านมา

      Amenewotu azaphedwa akukuyo ndi achimundu banda kmaso ndi azizawo onse mpakana ndi chakwera yemweo ka

  • @user-ml2vw1dc9c
    @user-ml2vw1dc9c 22 วันที่ผ่านมา +1

    Andale muphana komaso mutukwanana. Akulu akulu aliphee inu umphawi ukuphetsani lekani kutsatila ndale ingodikilani tsiku lovota

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 20 วันที่ผ่านมา

    Apolice sangapange chilichose kukhuzana ndichipani cha MCP why apolice athu alimukhwapa mwa chakwela chimozi mozi ngati mene anamuyikila mukhwapa matha chizuma koma pangatalike misonkho ya Malawi mukadya nayo khobwe opanda chele

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 22 วันที่ผ่านมา

    Cakwera ndi wasatanic palibe comwr angathandidzepo pakhani chifukwa iye ndi yemwe akutuma anthu kt adzivuladza anzawo iyeyo adzitenga magazi adzipita nawo kusatanic cakwera mbusa wakumidima leka kudzudza anthu dziko silako

  • @WhitePatson-tw3eu
    @WhitePatson-tw3eu 22 วันที่ผ่านมา

    chakwela ndi kukuyu ndi mbuzi nza wathu

  • @francischikaya3146
    @francischikaya3146 21 วันที่ผ่านมา +1

    Inu a Namiwa tikukuprmphani kuti kutsogoloko musazasithe mawanga chifukwa sitinayiwale kuti nthawi ya DPP inu munali ku State House. Tikudziwa kuti inu mukutumikira chipani chotsusa. DPP ili m'boma inasakaza ndalama za boma zankhani nkhani pogwiritsa ntchito mabungwe monga Escom, Water board ndi zina zambiri. Kunapezeka anthu ambiri a DPP kusanduka ma millionaire munthawi yochepa kwambiri. Palibe chomwe mungatiuze DPP inalepheranso kukwaniritsa zofuna zambiri za a Malawi. Ma blue night ife sitikuwafunanso.