BON KALINDO PA 9 OCT - TIYIWALE ZA MBIRI YA CHILIMA CHIFUKWA AKU UTM AKUFUNA KUGULISA UTM KWA MCP
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 9 ต.ค. 2024
- AKUTI BASI TIYIWALE ZA MBIRI YA SAULOS CHILIMA CHIFUKWA ANTHU AKU UTM AKUFUNA KUGULISA UTM KWA MCP
Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party and other parties like UDF, AFORD, PP, MMD, and PETRA, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
NOTE : We try to be as neutral as possible when giving you news from all parties. Maybe sometimes we may seem to offer or insult a certain party, kindly forgive us and above all, tell us in the comment section.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
UTM my party and will never end SKC is the winner 2025 mhsrip😢😢
Zama demonstration zili pati?
Now i understand why minister of labour resigned 😮
Munthu wabodza ameneyu.Tinasiya kalekale kumukhulupilira.Ali MP palibe chimene anapanga oipa uyu komanso wakuba.
Chaboza I chi,
Iweyo ukumati kaya ndizoona kaya ukufuna ife tikhulupirire ziti
Mayi Chilima mudakamusiya pliz a kulira mamuna wake 😭😭Ana akudalira iye pliz midakamusiya
Akudya ndalama za mcp ameneyu
The DCCCCCCCC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri
KUSWA KUSWA NG'ALULAIZATION THE D C booooooon kalindoooo
Let's pray for our country,,president uyu sakulabada zaanthu ndiozikonda ,,God will punish him
Koma UTM party will never die whether Ena alandire ndalama or not, alipo Ena ochepa atachiolotse chipanichi mpaka legacy ya SKC sidzafa
Amen
Agree with you ndipo sizingatheke ngat usi akuona ngat agulitsa utm ndi anthu enawo mmmmm akunama ndithu
U hv apoint broh ena ndiolimba mtima pitilizan kuyankhul maganiz owalimbisa mtima broh zoona mwanenazi
UTM singathe chifukwa Cha anthu adyela never
UTM mukuganiza bwanji guys ndalama yokhayokhayo imeneyo mpakana kugulitsa chipani simuzapeza mtendereinu aai zikomo
Zione Kalako
They will sell the name UTM but the followers will return to the mighty blue party DPP....
NDIPO MCP palibe kuwina..
Following
Bon Kalindo mmm
Anthu mukutsutsanu muzazindikila bwino patsogolo
Zekomo Dc
Nakha aifewa atibwelesele km bz kuba
Katundu madzi the DC
Ndipo afuna chani ky
Malawi 🔥
Bon kalindo pano anabwelad
Akunyeraomwemo uwu akuyalutsatu panja ku UDF akutulukila
Na zankhondo sukunama Kalindo Iran Hezbroh Lebanon ndi Palestine panop yakwiya ndpo apapa kutha kwa Israel
mmm koma Malawi
Zopanda phindu bodza lokhalokha anthu anakutulukani kalekale
tikumana povotr achenjele pano
😮😮😮
Utm singa gulusidwe tizawona zenizeni pakutha Kwa zose 17 September bus mabizaso aku chuluka kwambili
If this is true, I will be a disappointed member for life....and will affect negatively many lovers of the party.
I just hope it's FAKE NEWS !!
Dc mukunena zoona anthu awa amalimbikila maboza akatero aziti boma ndilomweli
Netanyahu chimwene wake wachakwera kwasala kumalawi nkhondo uzabwera ma Isreal akufuna chakwera abwezele ndalama zawo akudya panozi😅😅😅
My country 😢😢😢
Waboza ndiwe zanga zikuvutilam ungayamikr chakwel aaaaa ukupenga
Wamisala adaona nkhondo, akunena zoonadi ameneyu
Paja winiko amakomoka anatiuz yekha mbuz yamunthu uyu akatere afuna atikomokole popez mwez wakhal kumene
Zisis za ehova zovumbuluka za ana anthu bs
Amalawindife ogonakwambiri
Zimvere mtolo, wamzeru wamva
Ndizoona kapena ndizaboza,,,,😂😂😂😂
Abon ngat mulib phamv yotenga boma mulibem ingokhalan mutu wanu suyenda bwin
Kalindo muuze Chakwera kuti dzulo lomweri Iran yanena kuti ali 100% kuphulisa Israel ndye muuze Chakwerayo kuti mzake Netanyahu nthawi yake yatha
Ndizoona sakunama ayiii
Kkkkkkkkk nchifukwa chake kunkuyu amakana kuti atolankhani azifunsa mu chizungu mbava zokhazokha
That can not happen to UTM
Koma Bon Kalindo mutu umagwira??????
Humm
The DC mwana woyipa kwambiri ndimanyadira naye amaswa palipose
Kkk😂😂😂😂😂😂😂ndaseka, akuwapusitsa ma supporter awo.
Mwana wovuta kwambili the Dccccccccc
Iwe kalindo ndiwe wabodza, stima ya mafuta itafika un lato simafuts chosecho masna ake stima inayamba kutsitsa. Nthawi zonse mabodza basi. Koma suphura kanthu. MCP ikupitilirabe
Eya vote yako sitikuyifuna
Mulli anaonekako kumenekuja?
Chakwela uli nditsoka zedi chifukwa ukunamiza ndikunzunza mtundu wa amalawi
Ine iww sindikukhulupilila zomwe umanena sizichitika..
Ngati muliko ku Israel tatumizani ma Video, tikuoneneni ngati simunaphulitsidwe 😂😂😂
Kalindo anapenga
Chakwera ni galu basi
Zovita
Ku isreal kwavutaa eti😢😢😢
Sakunama ndizoona
Galu uyu singayamike
Ndpo zomvesa chson panopa nkhondo yavutira ku Israel ndye wina sakupanga kanthu za anthu ake aliku Israel zachison dziko la Israel panopa ngt layamba kusamusa zinthu zawo kuopa nkhondo ndye winawe anthu ako zikuti bwanji
😢😢😢😢😢😢😢😢
L
P
😂umakwana Mr DC put it up
Wa Chamba iwe
The Dcçccc
Kalindo amanena zoona zokhazokha wopenga ndiwe
Akalido mulibodzazedi kodi inuyo ndabodza bas mwalemeranawo manodzawa chifukwa mukufuna kuthwilitsa tchito inuyo muzilemera.aaaaaaa wadziwika t