COMRADE NTANYIWA PA LIMPOPO FM - AKAIPUTA NGONGOLE INA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 8 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 30

  • @IbrahimUseni-p8f
    @IbrahimUseni-p8f 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    Amwene Ntanyiwa kuno Ku machinga tikuvutika ndi njala komanso kulandidwa katundu ndi neef

  • @stevenmwamadi3035
    @stevenmwamadi3035 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    More fire comrade osaopa osatopa osafooka Allah atiombore mukaporo tili nawo pano

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Tadswera bwino ifeso❤

  • @stevenmwamadi3035
    @stevenmwamadi3035 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    More fire comrade ntanyita osaopa osatopa osafooka Allah alipo mpaka tituluke mukaporo tilinawo pano ndi boma ra crocodile

  • @stevenmwamadi3035
    @stevenmwamadi3035 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Timpephe Allah atisogorere tonse a Malawi amene tikuvutika komaso Allah amuteteze comrade ntanyiwa mpaka mcp ituluke basi

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mulungu wa moyo akuona zonse

  • @MikeLodzi
    @MikeLodzi 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    katundu waboma uyu

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndalama zawachulukira MCP..mafumu landilani ndalamazo Ku voter umakavota wekha

  • @McshonWilliam
    @McshonWilliam 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Wina atupa mutu kkkkk 2025 dpp kut buuuuuuu whether they like or not kkkkk God already.......... Writen

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Limpopo fm woyeeeeee

  • @FredKanyerere
    @FredKanyerere 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zovetsa chisoni, fertilizer nkhani.. Tsiku ngati boma libe 😢😢😢😢

  • @AmosScott-z9x
    @AmosScott-z9x 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kd chakwera akumusungiranji Sam kawale nde bolaso Lowe yemweujasotu

  • @AusimanKassim
    @AusimanKassim 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Ayende bwino

  • @MariaLevi-e7y
    @MariaLevi-e7y 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Adadiomwewobasi

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Paja kuli maliro Ai rest in piecessss koma imfayo ili bwino koma wamwalirayo alibwino bwino bokosimo koma wafadi zatheka bwanji unyolo unali kutiko

    • @Alice-z7t4z
      @Alice-z7t4z 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Kaya unali kuti unyolo kaya 😂😂😂😂😂😂 apita ambiri angoyambapo

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Anthufe timalakwirana koma anthu awawa ai dziko lonse mkumadandaula iwo

  • @HarryChindiwo
    @HarryChindiwo 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Katundu weni weni

  • @LovemoreCathy
    @LovemoreCathy 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kkkk zokayikitsa kuti tifikadi ku 2025 coz tayamba kale kufa ziwalo

  • @ChrissWtness-e1z
    @ChrissWtness-e1z 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mwabwera madala

  • @JerseyAlfred
    @JerseyAlfred 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Umakwana ntanyiwa 😂😂😂

  • @MariaLevi-e7y
    @MariaLevi-e7y 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Osaopa bg man

  • @ReginaMaxwell-sv8kl
    @ReginaMaxwell-sv8kl 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    ❤❤❤

  • @stevenmwamadi3035
    @stevenmwamadi3035 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mcp yazazana ndi mbuli zokha Zokha basi onse a mcp ndi manganya crocodile team

    • @Alice-z7t4z
      @Alice-z7t4z 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Kkkkkkkkkk

  • @AdamMakala
    @AdamMakala 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Kkkkkki

  • @ReginaMaxwell-sv8kl
    @ReginaMaxwell-sv8kl 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂 ntanyiwa

    • @MateusPhiri-d2f
      @MateusPhiri-d2f 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ziliko 😂😂😂😂😂

  • @BrijlallDularie-d8o
    @BrijlallDularie-d8o 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    😂