Follow up from Robin Island CapeTown, this is how a leader must be, not to soult someone , this is what we want, to love one another in warm heart of Africa
Nanga popanda bwanawa Ndi pure evidence yao ,nthawi ya Presidential electoral case bwezi mutawina panokha,? History is not forgotten at all, nthawi inafika kuti bwanawa akhale pampando after so much struggle some which are questionable in my brain until date.. NICE SPEECH our head of state ✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✌️✌️✌️✌️✌️✌️✌️
Munalowa mboma chifukwa cha Dr Chilima munapha uja panokha mwakhala mukulephera and utm yomweyo ikutulutsani mumbomamu ndipo mudzalira ching"ang'azi next year
Dzikomo kwambiri a President chifukwa cha mau anu. Dzikomo kwambiri a khoti polora aliyense kuvoteledwa. Funso. = Kodi omwe analetsedwa aja. Angapambane bwanji popanda kupanga Complain? Popeza mwatiuza nokha a President kuti ambiri a ononga ndalama zambiri kukopera anthu. Khoti enawo lisanawavomeleze Dzikomo a Khoti.
Sindikutha kuvesa mnthu wamulungu samakhala ndi nitima chonchi. Ndilibe zoyankhala zambiri ayi kma my last word is. Mkuyenera kuziwa nthawi yamulungu. msapusisike ndi chuma ai. nthawi yatha izi mzazisiya ndizikoli simuzanyamula. I can see it. This is challenge speech.
Zikhale ng oma ukumva kumene uliko akukusambilatu manja ineyo chipani changa chosapota bakili muluzi TV koma chakwera lero ndakukonda wayakhula mwazeru
Malankhulidwe amene malawi wakhala akuyembekezera kwa zaka zochuluka kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko ndiye ndamenewo zikomo a president bola zimenezo zizichitikadi asakunamizeninso ali ku mbuyowo
Bwana, muntengo mulimo musika posachedwapa , tikukudikilani tili pansi pantengo pano,
Kkkk chibonga chili mmanja
😅😅😅@@lysonkaselema7321
Nice speech to those who have right heart .
Don't hate someone on what you don't have it's evidence.
Chipani chakupha with a president with flowering speech but without action
Nsanje too much enanu
@@jestinanamkonda1495 ngati mmutu mwanumo muli mwa bwino bwino mukutha kuvomereza kuti ndi zoona , unless otherwise
Kulankhula kwa nzeru. Lord have mercy on you Mr President
Ummmm atsogo chipani cha mcp sichinalowepo m'boma koma tonse alliance mongokonzapo😂😂😂
Auzen asachite. Matama😂
Kkk saziwa kut chipanda Chilima uja sakadalowa
He has done this because of the broadcast of the kwagwanji program.
Wise speak 😊
For the First time in History, respect to the speech writer.
Ineso ndadabwa nazo 😂😂
@@emmax9101 Kkkkk koma wayankhula bwino kwambiri.
Mostly the narrator knows what he is..
😂😂😂 speech writer 😂😂 ndi dolo
Thanks Mr pr speach ya mphanvu kwambir
Follow up from Robin Island CapeTown, this is how a leader must be, not to soult someone , this is what we want, to love one another in warm heart of Africa
Apa ndipomwe ndakhulupirira kuti Sarawa kwawo nkulankhula, nanga anthu omwe amagawa ndalama akuwadziwa nchifukwa chani sanawaitanire kumbali. Angofuna kutamika pamaso pa anthu.
Linda madzi apite kenaka udziti ndadala chikhla mcp njowina si bwenzi kuli zisankho don't forget mwamuna nzako mpachulutu😅😅😅😅😅😅
Palibe yemwe akukufuna mr chikangawa wakupha mfiti wasataniki unapha chilima ndi anthu 8 komanso unapha kasambala unapha sidiki miya
Mfiti imadziziwaka kuzibitsa mu dzina la mulungu bwanji
Ndine wa DPP but speech iyi nkukuyi walakhura bwino kumbali yachipani chawochi koma kukhani ya dziko ndine wa DPP
Mwazi wa Chilima ukukantheni munapha munthu wosalakwa anthu oyipa inu
Unapha ndiwe chilima only if you have proof we can support the truth
If you support the truth ,where is a report of his accident?
Zowonaa
Uyu ndimwamuna eeh….koma opposition mulimba? Well said your Excellency 👏🏾👏🏾
Ukunama mphwanga chakwela u will never win again,uiwale
Strong voice Mr president
True
Mwayankhula bwino koyambirirako, koma kumapeto mwayankhula mbwereraa.
1.Simukanawina kupanga Chilima kutiuza ife kut tikakuvotereni.
2.Zokuti mipando ndiyosirana mwangoyankhula koma inuyo simumafuna kusira ena, thus y mumayankhula Chilima alipo kut muzayimira 2025 ngakhale mumaziwa kut munagwirizana zozasinthana.
2.
Iiiiii zoona ndithu sakuganiza komwe uyu.
Kuyankula kwabwino km mene mwayankulilamo mutangoyelekeza kutsitsa katundu kmso m'msokho mmmmm mungawineso 2025 km ngati simutelo kkkk kaya
Iwe ndi zikhale ng'oma wakoyo muzavotane paubale wanu osadanda 😂😂😂
Msokhano wa chipani cha magazi
Feteleza k200 000
Chimanga k65000
Mchele 2000
Mankkwala muzipatalamu mulibemo Pali chifukwa chovotela mcp apa
Zowinazo ndiye aaaaa ayiii. Dzikolino kungowinanso MCP 🐊 dziko lathela pomwepo
Uyudi ndi oyipitsitsadi 😎🇲🇼
Why don't you allow people to compete with you as president?
He doesn't even think of that.
Nice speech Mr president
Zowinazo ndy eeee mukutinamiza ngt sipakhla kubela
Nice speech
Usatinyase chikangawa ife tikufuna liport landenge bas
Zowinazo nde zokaikitsa boss 😂😂😂
Our president has failed us malawians....the confidence of malawians has gone in vain.....tel us what good have you done?
Ansanje aphulika ,abwana amadziwa kuyala nfundo,sizachibwana akumachita enawo ngati ana a primary ang'ono achambanso ine sinpanga nawo ayi,abwana konzani dziko mosanyengelera wina oononga mindset ya ana ndi anthu opanda look sharp...power hungry siyiathandiza.
Good report imafunika osat kumazinamidza
Chakwela yomweyo misewu palipotse town ya Lilongwe yikukwela modetsa khawa abwana tchito mwayiyamba bwino kwambili chatsala kusitsa fertrazer kuti adzipedzeka palipotse Kuti chakudya chikhale palipotse mu malawi,, MCP hoyeeeee wina afune kaya asafune yilamulilanso 2025
Ife tinavotera chilima osati iweyo uthokoze utm
Kkkkk zowinasokhazo Kaya mwina😊
Ife sitikukufunan bambo😂😂😂😂
Ndiwe opusa ukuona ngati iwe ungafunidwe Ndi munthu wankulu ,gwiritsani brain zanu bwinobwino not these stupidit comments...
Uziti ine osati ife ngati takutuma
Ayi chipanda chilima bwana simukanakhala president ndichifukwa mwamuphaa eti
Nanga popanda bwanawa Ndi pure evidence yao ,nthawi ya Presidential electoral case bwezi mutawina panokha,? History is not forgotten at all, nthawi inafika kuti bwanawa akhale pampando after so much struggle some which are questionable in my brain until date.. NICE SPEECH our head of state ✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✌️✌️✌️✌️✌️✌️✌️
Munalowa mboma chifukwa cha Dr Chilima munapha uja panokha mwakhala mukulephera and utm yomweyo ikutulutsani mumbomamu ndipo mudzalira ching"ang'azi next year
Mumene kwachera lero masiku akupita muziweso kt munawina chifukwa cha skc kopanda apo somukanawina manyazi bwaaaa😢😢
"Actions speaks louder than words."
Koma uku after convention imeneyi kukhala ma exodus "mark my words"
Km ameneyi ndi galudi et? Dr Ch sindimaliza angandidyetse ng'ona😂
Dzikomo kwambiri a President chifukwa cha mau anu.
Dzikomo kwambiri a khoti polora aliyense kuvoteledwa.
Funso. = Kodi omwe analetsedwa aja. Angapambane bwanji popanda kupanga Complain?
Popeza mwatiuza nokha a President kuti ambiri a ononga ndalama zambiri kukopera anthu. Khoti enawo lisanawavomeleze
Dzikomo a Khoti.
Mbavayo
nice big
ZIKOMO MFUMU LA FUKO LA MALAWI AMBUYE AKUDALITSENI NDINE MWANA FELIX THOMUSEN TEMBO NSANJE SOUTH CONSITUENCY NSAMBA POLING CENTER
introduction imeneyi bwanji? mukuyese abwera kuzakuonani kkkkkkk
Kikikikikikkkkkk
Mwazipanga introduce bwino ndithu, maluzi omwewa kapena ndipeze loyer?
Saulo chifunga chikangawa chakwera
Kutipula paground nde kubako
Zikomo andevu zamwayi mwayuka mawu nkamwa achakwela kuti ayakhuleko zogwilakobmutu khakhale amangoyakhula zoti sizingatheke amenewo ndiwo Mr chikangawa 😂😂😂
Moto kuti buuuuuuuuuuuuuuu sakufuna akhale 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 2024 bomaaa
Sindikutha kuvesa mnthu wamulungu samakhala ndi nitima chonchi. Ndilibe zoyankhala zambiri ayi kma my last word is. Mkuyenera kuziwa nthawi yamulungu. msapusisike ndi chuma ai. nthawi yatha izi mzazisiya ndizikoli simuzanyamula. I can see it. This is challenge speech.
Good man
He's very good on speech, koma kutsatira zomwe anena ndikomwe kumavuta
Well speaking Mr president ❤
Alex major is the only one mcp can change than even a chakwera 😂
Koma gwenembe aaa
After kuchita Ndale za usiku then the path is cleared, someone is buried 7 feet under as we speak.
Ndiye mudzikonze nokha. Chifukwa inu a MCP mukugwilitsa ntchito ndalama pofuna mpando
Mr chikangawa fundo mulibe zowina muchonse inu palibe mapwala ako akukunamiza chifukwa umaba ndikumapasa uwonaso chaka chamawachi
😮
Zikhale ng oma ukumva kumene uliko akukusambilatu manja ineyo chipani changa chosapota bakili muluzi TV koma chakwera lero ndakukonda wayakhula mwazeru
Galu ameneyu uchitsiru udamuyanja - zoti idali ncp sakuziwa mmmm
Zadziii kodi amphawife nde dzida zanu,tinalakwa kukhara anthu osauka bull shit, kodi mmesa tili mu tonse alliance MCP ndekuti chani
Chakwela machende ako wamva panyo pako iwe tikuwona next year mbuzi ya munthu mfiti yayikulu
Bwana tili pambuyo panu,boma iloooooo😅🎉
Chikangawa woyeee!!
Amene analemba speech iyiyi nd goat😂
😂😂😂😂We are a disgrace as Malawians political parties will never ever develop Malawi.
Garu iwe kipusa kwako chimutuu chaoko
MCP mpaka Yesu azabwera ikulamurabe. Wina afune kaya asafune koma boma ndilomweri mpaka kale ndanena ndanena.
Ine monga president wakupha anthu😢😢
Bwana amkaka akukunamizani bola mukanamusiya biyeni apa mwatsekula maso Malawi kuti chipani ichi mchamagazi
Tasauka kale chifukwa chaiwe chakwela bolani mubwelele ku tchalitchi konkuja tatopa nanu inu ndi chisanzo choipa mwapha chilima
Lero apresident mwayankhula zamphamvu kwambili
Bola kunyoza pomwe iwe unawinila kupha anthu komaso mademo ndi chisilu kwa basi imeneyo ukuti fundo kodi mesa uayambisa kunyoza ndi iyiweo
Kuwerenga or kuyankhula??
We want report for chilima's death.. ndege inagwa chifukwa chani??
Musamazinamize zowina azakuvoteleni ndiokhao omwe mugwila nawo tchito abusainu.😂😂
Kodi skc mnamtani?
Awaiting Chikangawa report after this.
Athu ena alibe manyazi nkhani ndi yao koma akuimirira ngati zanzeru ndakhulupiriradi kuti chitsiru sichimakhala ndi manyazi.
Ngatimukudziwa kuti akugawandalama zambirimbiri ozazifusa kuti ma billions amenewa atengakuti bwanji osafufuza
Koma ndiye mukunanaratu azanthu mimba zimenezo.Malawi wake yemweyi? Tikuona ngatitu akunja ife athu mukudya bwino.
Chilima Rest in Peace!
Mwayakhula bwino ife sitikukufunani amwene mupumeko tione zina
Chilima anayamba wawinapo Boma dzaphatikizaneni mudzanyenyedwa nose
Nzomwe amafuna kuti azilankhula mokhazula Mulungu akuonatu
Chipani chimene chimaphunzitsa zipani kaphedwe, kabedwe, tsakho mkhaza!!!!
Ambuye mukuchedwa patii zamukatheni muthuyu chonde ..akuyakhula mwatudzu chifukwa palibe chomwe akukumana nachoo ..kumanizen adziwe kut mulunguu Inu mulipo imvan kulira kwathu ovutikafe ambuye tamukathen
Mmm pemphero lopempherera mwana wazanu Ili ali wanu mungamve bwaa? Mmm musatero asisi palibe phindu lilonse apa zotsala timusiile mwini wake namalenga adzaweruza yekha🙏
Indeed, God will visit you with a handfull of punishments
Malankhulidwe amene malawi wakhala akuyembekezera kwa zaka zochuluka kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko ndiye ndamenewo zikomo a president bola zimenezo zizichitikadi asakunamizeninso ali ku mbuyowo
Munaphelanji chilima chimunthu choipa iwe munalindani inu chifiti😢😢
Am not mcp member yooo count me out hiyaaa
😂mwapanga chani pa 4yrz mukungogwetsa dziko m,Malo mulitukula munapasana terms panopa mukut muyimaso thats greedness of leadership😢
For the. first time you. have said something. building
Following up from Capetown
Zowinazo nde mzosatheka uyiwale ase unapha chilima maliro akanali a fresh fiti iwe kumachende kwamako
pamnyopanu achakwera wonani ma massages munya inde takuwonani chikhalidwe chanu
Dr chikangawa