DR CHAKWELA AYANKHULA MOSAONA NKHOPE 🤔🤔🙌🙌8 August 2024

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 301

  • @FungulanReuben
    @FungulanReuben 2 หลายเดือนก่อน +22

    Bwana, muntengo mulimo musika posachedwapa , tikukudikilani tili pansi pantengo pano,

    • @lysonkaselema7321
      @lysonkaselema7321 2 หลายเดือนก่อน +1

      Kkkk chibonga chili mmanja

    • @Santo-B
      @Santo-B 2 หลายเดือนก่อน

      😅😅😅​@@lysonkaselema7321

  • @LloydPhiri-d6f
    @LloydPhiri-d6f 2 หลายเดือนก่อน +3

    Nice speech to those who have right heart .
    Don't hate someone on what you don't have it's evidence.

  • @allahslave7177
    @allahslave7177 2 หลายเดือนก่อน +14

    Chipani chakupha with a president with flowering speech but without action

    • @jestinanamkonda1495
      @jestinanamkonda1495 2 หลายเดือนก่อน

      Nsanje too much enanu

    • @allahslave7177
      @allahslave7177 2 หลายเดือนก่อน

      @@jestinanamkonda1495 ngati mmutu mwanumo muli mwa bwino bwino mukutha kuvomereza kuti ndi zoona , unless otherwise

  • @ChifundoGoster
    @ChifundoGoster 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kulankhula kwa nzeru. Lord have mercy on you Mr President

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 2 หลายเดือนก่อน +11

    Ummmm atsogo chipani cha mcp sichinalowepo m'boma koma tonse alliance mongokonzapo😂😂😂

    • @Angel-dt6oe
      @Angel-dt6oe 2 หลายเดือนก่อน +2

      Auzen asachite. Matama😂

    • @MahamudKambanje
      @MahamudKambanje 2 หลายเดือนก่อน

      Kkk saziwa kut chipanda Chilima uja sakadalowa

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 2 หลายเดือนก่อน +4

    He has done this because of the broadcast of the kwagwanji program.

  • @LameckDanken-tm4rt
    @LameckDanken-tm4rt 2 หลายเดือนก่อน +1

    Wise speak 😊

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน +7

    For the First time in History, respect to the speech writer.

    • @emmax9101
      @emmax9101 2 หลายเดือนก่อน

      Ineso ndadabwa nazo 😂😂

    • @amoschataika7440
      @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน

      @@emmax9101 Kkkkk koma wayankhula bwino kwambiri.

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya 2 หลายเดือนก่อน

      Mostly the narrator knows what he is..

    • @gradsonmayira9336
      @gradsonmayira9336 2 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂 speech writer 😂😂 ndi dolo

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 2 หลายเดือนก่อน +1

    Thanks Mr pr speach ya mphanvu kwambir

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 หลายเดือนก่อน +1

    Follow up from Robin Island CapeTown, this is how a leader must be, not to soult someone , this is what we want, to love one another in warm heart of Africa

  • @BladesBullets-pu5uw
    @BladesBullets-pu5uw 2 หลายเดือนก่อน +7

    Apa ndipomwe ndakhulupirira kuti Sarawa kwawo nkulankhula, nanga anthu omwe amagawa ndalama akuwadziwa nchifukwa chani sanawaitanire kumbali. Angofuna kutamika pamaso pa anthu.

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 2 หลายเดือนก่อน +8

    Linda madzi apite kenaka udziti ndadala chikhla mcp njowina si bwenzi kuli zisankho don't forget mwamuna nzako mpachulutu😅😅😅😅😅😅

  • @FWhite-w3l
    @FWhite-w3l 2 หลายเดือนก่อน +5

    Palibe yemwe akukufuna mr chikangawa wakupha mfiti wasataniki unapha chilima ndi anthu 8 komanso unapha kasambala unapha sidiki miya

  • @danielmagwaya1074
    @danielmagwaya1074 2 หลายเดือนก่อน +8

    Mfiti imadziziwaka kuzibitsa mu dzina la mulungu bwanji

  • @giftjamali8204
    @giftjamali8204 2 หลายเดือนก่อน +3

    Ndine wa DPP but speech iyi nkukuyi walakhura bwino kumbali yachipani chawochi koma kukhani ya dziko ndine wa DPP

  • @kondwanivyalema9449
    @kondwanivyalema9449 2 หลายเดือนก่อน +15

    Mwazi wa Chilima ukukantheni munapha munthu wosalakwa anthu oyipa inu

    • @Aqiec09
      @Aqiec09 2 หลายเดือนก่อน

      Unapha ndiwe chilima only if you have proof we can support the truth

    • @bisweckchimphamba8497
      @bisweckchimphamba8497 2 หลายเดือนก่อน

      If you support the truth ,where is a report of his accident?

    • @leoleonard2103
      @leoleonard2103 2 หลายเดือนก่อน

      Zowonaa

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 2 หลายเดือนก่อน +2

    Uyu ndimwamuna eeh….koma opposition mulimba? Well said your Excellency 👏🏾👏🏾

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ukunama mphwanga chakwela u will never win again,uiwale

  • @yosefemichael7588
    @yosefemichael7588 2 หลายเดือนก่อน +1

    Strong voice Mr president

  • @LuciusScott-h7b
    @LuciusScott-h7b 2 หลายเดือนก่อน +1

    True

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mwayankhula bwino koyambirirako, koma kumapeto mwayankhula mbwereraa.
    1.Simukanawina kupanga Chilima kutiuza ife kut tikakuvotereni.
    2.Zokuti mipando ndiyosirana mwangoyankhula koma inuyo simumafuna kusira ena, thus y mumayankhula Chilima alipo kut muzayimira 2025 ngakhale mumaziwa kut munagwirizana zozasinthana.
    2.

    • @RejoiceKamanga
      @RejoiceKamanga 2 หลายเดือนก่อน

      Iiiiii zoona ndithu sakuganiza komwe uyu.

  • @Frederick-s4h
    @Frederick-s4h 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kuyankula kwabwino km mene mwayankulilamo mutangoyelekeza kutsitsa katundu kmso m'msokho mmmmm mungawineso 2025 km ngati simutelo kkkk kaya

  • @RichardlawyerPatrick
    @RichardlawyerPatrick 2 หลายเดือนก่อน +7

    Iwe ndi zikhale ng'oma wakoyo muzavotane paubale wanu osadanda 😂😂😂

    • @andrewchirwa2193
      @andrewchirwa2193 2 หลายเดือนก่อน

      Msokhano wa chipani cha magazi

  • @LazarousNamakhwa
    @LazarousNamakhwa 2 หลายเดือนก่อน

    Feteleza k200 000
    Chimanga k65000
    Mchele 2000
    Mankkwala muzipatalamu mulibemo Pali chifukwa chovotela mcp apa

  • @TroubleMuthala
    @TroubleMuthala 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zowinazo ndiye aaaaa ayiii. Dzikolino kungowinanso MCP 🐊 dziko lathela pomwepo

  • @TressLuka
    @TressLuka 2 หลายเดือนก่อน +2

    Uyudi ndi oyipitsitsadi 😎🇲🇼

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 2 หลายเดือนก่อน +2

    Why don't you allow people to compete with you as president?

    • @RejoiceKamanga
      @RejoiceKamanga 2 หลายเดือนก่อน

      He doesn't even think of that.

  • @nelsonsikwese5952
    @nelsonsikwese5952 2 หลายเดือนก่อน +3

    Nice speech Mr president

  • @aubreykamwendo4315
    @aubreykamwendo4315 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zowinazo ndy eeee mukutinamiza ngt sipakhla kubela

  • @SABANLOWE
    @SABANLOWE 2 หลายเดือนก่อน +1

    Nice speech

  • @LuciusPatrick-f2c
    @LuciusPatrick-f2c 2 หลายเดือนก่อน +1

    Usatinyase chikangawa ife tikufuna liport landenge bas

  • @AbdullahaziziAmoswalala
    @AbdullahaziziAmoswalala 2 หลายเดือนก่อน +12

    Zowinazo nde zokaikitsa boss 😂😂😂

  • @georgemsowoya6525
    @georgemsowoya6525 2 หลายเดือนก่อน

    Our president has failed us malawians....the confidence of malawians has gone in vain.....tel us what good have you done?

  • @InnocentMtafya
    @InnocentMtafya 2 หลายเดือนก่อน

    Ansanje aphulika ,abwana amadziwa kuyala nfundo,sizachibwana akumachita enawo ngati ana a primary ang'ono achambanso ine sinpanga nawo ayi,abwana konzani dziko mosanyengelera wina oononga mindset ya ana ndi anthu opanda look sharp...power hungry siyiathandiza.

  • @JohnKaudzu
    @JohnKaudzu 2 หลายเดือนก่อน

    Good report imafunika osat kumazinamidza

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 2 หลายเดือนก่อน

    Chakwela yomweyo misewu palipotse town ya Lilongwe yikukwela modetsa khawa abwana tchito mwayiyamba bwino kwambili chatsala kusitsa fertrazer kuti adzipedzeka palipotse Kuti chakudya chikhale palipotse mu malawi,, MCP hoyeeeee wina afune kaya asafune yilamulilanso 2025

  • @AsimenyeMwalwanda-kh8ir
    @AsimenyeMwalwanda-kh8ir 2 หลายเดือนก่อน +4

    Ife tinavotera chilima osati iweyo uthokoze utm

  • @TRIPLE-w1s
    @TRIPLE-w1s 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkk zowinasokhazo Kaya mwina😊

  • @RichardlawyerPatrick
    @RichardlawyerPatrick 2 หลายเดือนก่อน +7

    Ife sitikukufunan bambo😂😂😂😂

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya 2 หลายเดือนก่อน

      Ndiwe opusa ukuona ngati iwe ungafunidwe Ndi munthu wankulu ,gwiritsani brain zanu bwinobwino not these stupidit comments...

    • @godricktsakama3954
      @godricktsakama3954 2 หลายเดือนก่อน

      Uziti ine osati ife ngati takutuma

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 2 หลายเดือนก่อน +3

    Ayi chipanda chilima bwana simukanakhala president ndichifukwa mwamuphaa eti

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya 2 หลายเดือนก่อน

      Nanga popanda bwanawa Ndi pure evidence yao ,nthawi ya Presidential electoral case bwezi mutawina panokha,? History is not forgotten at all, nthawi inafika kuti bwanawa akhale pampando after so much struggle some which are questionable in my brain until date.. NICE SPEECH our head of state ✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✊✌️✌️✌️✌️✌️✌️✌️

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s 2 หลายเดือนก่อน

    Munalowa mboma chifukwa cha Dr Chilima munapha uja panokha mwakhala mukulephera and utm yomweyo ikutulutsani mumbomamu ndipo mudzalira ching"ang'azi next year

  • @Blessingskanyinji-x7s
    @Blessingskanyinji-x7s 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mumene kwachera lero masiku akupita muziweso kt munawina chifukwa cha skc kopanda apo somukanawina manyazi bwaaaa😢😢

  • @jameschibwana2751
    @jameschibwana2751 2 หลายเดือนก่อน

    "Actions speaks louder than words."

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 2 หลายเดือนก่อน

    Koma uku after convention imeneyi kukhala ma exodus "mark my words"

  • @Yanjanani
    @Yanjanani 2 หลายเดือนก่อน +3

    Km ameneyi ndi galudi et? Dr Ch sindimaliza angandidyetse ng'ona😂

  • @PollyLysonLutepo
    @PollyLysonLutepo 2 หลายเดือนก่อน

    Dzikomo kwambiri a President chifukwa cha mau anu.
    Dzikomo kwambiri a khoti polora aliyense kuvoteledwa.
    Funso. = Kodi omwe analetsedwa aja. Angapambane bwanji popanda kupanga Complain?
    Popeza mwatiuza nokha a President kuti ambiri a ononga ndalama zambiri kukopera anthu. Khoti enawo lisanawavomeleze
    Dzikomo a Khoti.

  • @FahadiFalaji-q8y
    @FahadiFalaji-q8y 2 หลายเดือนก่อน

    Mbavayo

  • @SinoliyamuBanda
    @SinoliyamuBanda 2 หลายเดือนก่อน +1

    nice big

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 2 หลายเดือนก่อน +2

    ZIKOMO MFUMU LA FUKO LA MALAWI AMBUYE AKUDALITSENI NDINE MWANA FELIX THOMUSEN TEMBO NSANJE SOUTH CONSITUENCY NSAMBA POLING CENTER

    • @clementmahoka6287
      @clementmahoka6287 2 หลายเดือนก่อน

      introduction imeneyi bwanji? mukuyese abwera kuzakuonani kkkkkkk

    • @TheresaMuthowa
      @TheresaMuthowa 2 หลายเดือนก่อน

      Kikikikikikkkkkk

    • @TiyanjaneMkwate-we8gu
      @TiyanjaneMkwate-we8gu 2 หลายเดือนก่อน

      Mwazipanga introduce bwino ndithu, maluzi omwewa kapena ndipeze loyer?

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 หลายเดือนก่อน +3

    Saulo chifunga chikangawa chakwera

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo 2 หลายเดือนก่อน +3

    Kutipula paground nde kubako

  • @CharityChirwa-t1e
    @CharityChirwa-t1e 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zikomo andevu zamwayi mwayuka mawu nkamwa achakwela kuti ayakhuleko zogwilakobmutu khakhale amangoyakhula zoti sizingatheke amenewo ndiwo Mr chikangawa 😂😂😂

  • @JonathanZaithwa
    @JonathanZaithwa 2 หลายเดือนก่อน

    Moto kuti buuuuuuuuuuuuuuu sakufuna akhale 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 2024 bomaaa

  • @RejoiceKamanga
    @RejoiceKamanga 2 หลายเดือนก่อน

    Sindikutha kuvesa mnthu wamulungu samakhala ndi nitima chonchi. Ndilibe zoyankhala zambiri ayi kma my last word is. Mkuyenera kuziwa nthawi yamulungu. msapusisike ndi chuma ai. nthawi yatha izi mzazisiya ndizikoli simuzanyamula. I can see it. This is challenge speech.

  • @xadrequejohnsantos9188
    @xadrequejohnsantos9188 2 หลายเดือนก่อน

    Good man

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 2 หลายเดือนก่อน

    He's very good on speech, koma kutsatira zomwe anena ndikomwe kumavuta

  • @CELECTRICALCHILOMOH
    @CELECTRICALCHILOMOH 2 หลายเดือนก่อน

    Well speaking Mr president ❤

  • @MadandoChannel
    @MadandoChannel 2 หลายเดือนก่อน

    Alex major is the only one mcp can change than even a chakwera 😂

  • @MaryBanda-n3h
    @MaryBanda-n3h 2 หลายเดือนก่อน +2

    Koma gwenembe aaa

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 2 หลายเดือนก่อน

    After kuchita Ndale za usiku then the path is cleared, someone is buried 7 feet under as we speak.

  • @EviChio
    @EviChio 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ndiye mudzikonze nokha. Chifukwa inu a MCP mukugwilitsa ntchito ndalama pofuna mpando

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mr chikangawa fundo mulibe zowina muchonse inu palibe mapwala ako akukunamiza chifukwa umaba ndikumapasa uwonaso chaka chamawachi

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 หลายเดือนก่อน

    Zikhale ng oma ukumva kumene uliko akukusambilatu manja ineyo chipani changa chosapota bakili muluzi TV koma chakwera lero ndakukonda wayakhula mwazeru

  • @MpapiParadise
    @MpapiParadise 2 หลายเดือนก่อน

    Galu ameneyu uchitsiru udamuyanja - zoti idali ncp sakuziwa mmmm

  • @CHIMWEMWECHILUNGA
    @CHIMWEMWECHILUNGA 2 หลายเดือนก่อน

    Zadziii kodi amphawife nde dzida zanu,tinalakwa kukhara anthu osauka bull shit, kodi mmesa tili mu tonse alliance MCP ndekuti chani

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 หลายเดือนก่อน

    Chakwela machende ako wamva panyo pako iwe tikuwona next year mbuzi ya munthu mfiti yayikulu

  • @MasekoKalimanjira
    @MasekoKalimanjira 2 หลายเดือนก่อน

    Bwana tili pambuyo panu,boma iloooooo😅🎉

  • @ThokozaniDavismlamba
    @ThokozaniDavismlamba 2 หลายเดือนก่อน

    Chikangawa woyeee!!

  • @Kachimera
    @Kachimera 2 หลายเดือนก่อน

    Amene analemba speech iyiyi nd goat😂

  • @MadandoChannel
    @MadandoChannel 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂We are a disgrace as Malawians political parties will never ever develop Malawi.

  • @ErnestManda-iz2sr
    @ErnestManda-iz2sr 2 หลายเดือนก่อน

    Garu iwe kipusa kwako chimutuu chaoko

  • @DanielNamate
    @DanielNamate 2 หลายเดือนก่อน

    MCP mpaka Yesu azabwera ikulamurabe. Wina afune kaya asafune koma boma ndilomweri mpaka kale ndanena ndanena.

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 หลายเดือนก่อน

    Ine monga president wakupha anthu😢😢

  • @JohnBanda-k5y
    @JohnBanda-k5y 2 หลายเดือนก่อน

    Bwana amkaka akukunamizani bola mukanamusiya biyeni apa mwatsekula maso Malawi kuti chipani ichi mchamagazi

  • @CellinaNgolingoli
    @CellinaNgolingoli 2 หลายเดือนก่อน

    Tasauka kale chifukwa chaiwe chakwela bolani mubwelele ku tchalitchi konkuja tatopa nanu inu ndi chisanzo choipa mwapha chilima

  • @FridayKapito
    @FridayKapito 2 หลายเดือนก่อน +1

    Lero apresident mwayankhula zamphamvu kwambili

  • @yakiduidi5752
    @yakiduidi5752 2 หลายเดือนก่อน

    Bola kunyoza pomwe iwe unawinila kupha anthu komaso mademo ndi chisilu kwa basi imeneyo ukuti fundo kodi mesa uayambisa kunyoza ndi iyiweo

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 หลายเดือนก่อน

    Kuwerenga or kuyankhula??

  • @NoohNowa
    @NoohNowa 2 หลายเดือนก่อน

    We want report for chilima's death.. ndege inagwa chifukwa chani??

  • @SaleemEid-sr5ph
    @SaleemEid-sr5ph 2 หลายเดือนก่อน

    Musamazinamize zowina azakuvoteleni ndiokhao omwe mugwila nawo tchito abusainu.😂😂

  • @samsamuel9280
    @samsamuel9280 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi skc mnamtani?

  • @RennieSomba-xt9zk
    @RennieSomba-xt9zk 2 หลายเดือนก่อน

    Awaiting Chikangawa report after this.

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 หลายเดือนก่อน

    Athu ena alibe manyazi nkhani ndi yao koma akuimirira ngati zanzeru ndakhulupiriradi kuti chitsiru sichimakhala ndi manyazi.

  • @HajieMtenje-qm2lj
    @HajieMtenje-qm2lj 2 หลายเดือนก่อน

    Ngatimukudziwa kuti akugawandalama zambirimbiri ozazifusa kuti ma billions amenewa atengakuti bwanji osafufuza

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 หลายเดือนก่อน

    Koma ndiye mukunanaratu azanthu mimba zimenezo.Malawi wake yemweyi? Tikuona ngatitu akunja ife athu mukudya bwino.

  • @LewardPatel
    @LewardPatel 2 หลายเดือนก่อน

    Chilima Rest in Peace!

  • @CellinaNgolingoli
    @CellinaNgolingoli 2 หลายเดือนก่อน

    Mwayakhula bwino ife sitikukufunani amwene mupumeko tione zina

  • @GladsonBanda-m3e
    @GladsonBanda-m3e 2 หลายเดือนก่อน

    Chilima anayamba wawinapo Boma dzaphatikizaneni mudzanyenyedwa nose

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 2 หลายเดือนก่อน

    Nzomwe amafuna kuti azilankhula mokhazula Mulungu akuonatu

  • @TroubleMuthala
    @TroubleMuthala 2 หลายเดือนก่อน

    Chipani chimene chimaphunzitsa zipani kaphedwe, kabedwe, tsakho mkhaza!!!!

  • @SandrahPretty
    @SandrahPretty 2 หลายเดือนก่อน +2

    Ambuye mukuchedwa patii zamukatheni muthuyu chonde ..akuyakhula mwatudzu chifukwa palibe chomwe akukumana nachoo ..kumanizen adziwe kut mulunguu Inu mulipo imvan kulira kwathu ovutikafe ambuye tamukathen

    • @SalomyKamnkhwani
      @SalomyKamnkhwani 2 หลายเดือนก่อน

      Mmm pemphero lopempherera mwana wazanu Ili ali wanu mungamve bwaa? Mmm musatero asisi palibe phindu lilonse apa zotsala timusiile mwini wake namalenga adzaweruza yekha🙏

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 2 หลายเดือนก่อน

      Indeed, God will visit you with a handfull of punishments

  • @Edwardfulutuna1180
    @Edwardfulutuna1180 2 หลายเดือนก่อน

    Malankhulidwe amene malawi wakhala akuyembekezera kwa zaka zochuluka kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko ndiye ndamenewo zikomo a president bola zimenezo zizichitikadi asakunamizeninso ali ku mbuyowo

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 หลายเดือนก่อน

    Munaphelanji chilima chimunthu choipa iwe munalindani inu chifiti😢😢

  • @BeatriceProfessor
    @BeatriceProfessor 2 หลายเดือนก่อน

    Am not mcp member yooo count me out hiyaaa

  • @kellymofo8459
    @kellymofo8459 2 หลายเดือนก่อน

    😂mwapanga chani pa 4yrz mukungogwetsa dziko m,Malo mulitukula munapasana terms panopa mukut muyimaso thats greedness of leadership😢

  • @JonathanMtambo-w6e
    @JonathanMtambo-w6e 2 หลายเดือนก่อน +2

    For the. first time you. have said something. building

  • @ManuelMalunga-j3l
    @ManuelMalunga-j3l 2 หลายเดือนก่อน

    Following up from Capetown

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

    Zowinazo nde mzosatheka uyiwale ase unapha chilima maliro akanali a fresh fiti iwe kumachende kwamako

  • @NTOMBIZANELEFAITHGUSHE
    @NTOMBIZANELEFAITHGUSHE 2 หลายเดือนก่อน

    pamnyopanu achakwera wonani ma massages munya inde takuwonani chikhalidwe chanu

  • @JamesChakwira
    @JamesChakwira 2 หลายเดือนก่อน

    Dr chikangawa