OYENDA NDI LUPANGA/CHOIPA CHITSATA MWINI - NZWANYA CHARLEY PATACHE

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 12 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 33

  • @WysonChilonga
    @WysonChilonga 2 วันที่ผ่านมา

    Mwatikumbutsa kale kkkk,tafufuzaninso 'nawonso akana' album yomweyi

  • @JamesMalango-h4y
    @JamesMalango-h4y 3 วันที่ผ่านมา +1

    Mwatikumbutsa kale abale

  • @JohnWame-u3l
    @JohnWame-u3l 2 วันที่ผ่านมา

    R.I.P. DR

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 วันที่ผ่านมา +7

    Alimoyo Chakwera koma yekha ngt alindi nzeru adziwe kuti anthu atopa nae chfukwa munthu akamwalira anthu amalira osati amaseka ndikunyadra

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 วันที่ผ่านมา +6

    Chakwera yamba kukhal bwino ndi Amalawi nawo ndi anthu amafuna zabwino ichi chikhale chisadzo ngt uli ndi umunthu sintha khalidwe pliz pliz

  • @CosterMustafa-m6h
    @CosterMustafa-m6h 3 วันที่ผ่านมา +5

    Koma ndy kulli kalelangatu nyimbo izii zilipo kom ndy yomweyo dj 🎉🎉🎉😂😂😂😂😂

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 วันที่ผ่านมา +2

    Choipa chitsata mwini Ulemu Wanu mwatikumbutsa kale 💃💃💃💃💃💃❤️❤️❤️❤️❤️

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 วันที่ผ่านมา +5

    Alimoyo sangafe kwacha agwesa ndani akafamo ngongole ija abweza ndani sakuthawatu ameneyo alimoyo ndthu Chakwera alipo

  • @BerthaKasambala-y5k
    @BerthaKasambala-y5k 3 วันที่ผ่านมา +3

    Mwambo wowona nkhope tikachitira mchikangawa guys yomweyo garu iwe

  • @Paul-q2p
    @Paul-q2p 3 วันที่ผ่านมา +1

    Mungoyika zofanana lelo ngati mukuziwapo nenani mutsatithele nthawi

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 วันที่ผ่านมา +2

    Aaaaaa ine nditenga mpando ndiwandikire basi zikuti bwanji?

  • @LafickDickson
    @LafickDickson 3 วันที่ผ่านมา +1

    Mcp achakwela alikuti

  • @HandissoneMaquina
    @HandissoneMaquina 3 วันที่ผ่านมา +3

    Chilima kupezeka wopanda nsapato nkumati inali Ngozi ààààa

  • @ElizaJoseph-q9w
    @ElizaJoseph-q9w 3 วันที่ผ่านมา +3

    Malawi wavuta lelo anthu amwa wa mkaka ngati zili zoona zomwe ndikunganiza

  • @HandissoneMaquina
    @HandissoneMaquina 3 วันที่ผ่านมา +4

    Mzimu WA chilima ndi anthu ema aja ine pheee

  • @HarryKandani
    @HarryKandani 3 วันที่ผ่านมา +3

    Kkkkk koma timva nyimbo

  • @JOHNKANYALA
    @JOHNKANYALA 3 วันที่ผ่านมา +3

    Yomweyo dj😂😂😂

  • @atanazimvuyekure955
    @atanazimvuyekure955 3 วันที่ผ่านมา +2

    Bola asazafe wa pandege ndiopa kuwonongetsa ndege yina

  • @gizzykondwani865
    @gizzykondwani865 3 วันที่ผ่านมา +1

    😂😅😅😅😅😅 mr patache inu mumakwana

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 3 วันที่ผ่านมา +3

    Tiuchape tiutafune mahule mahule omwa fanta abwele pano.awuse muntendele bwanawo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela ukabwela uli ndi moyo chonde mukhale pansi kuwelenga makomeyi onse mmachanel mose ansala muyipedza nokha kuti anthu dziko la malawi akundifuna kapena sandifuna answer muyipedza muti akamadwala anthu amalira koma matenda ayinu 😂😂😂😂😂😂 zachisoni chonde sithani bwana 😂😂😂😂😂

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 3 วันที่ผ่านมา +1

    Nice song

  • @WilliamNyirenda-xq4km
    @WilliamNyirenda-xq4km 3 วันที่ผ่านมา +2

    Tiguliseniko zikuti bwanji Kodi 😂😂😂😂😂😂

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 3 วันที่ผ่านมา +2

    Koma sound imeneyi 😢😢😢😢

  • @JohnWalekana-z2f
    @JohnWalekana-z2f 3 วันที่ผ่านมา +3

    Yashuta

  • @LinlyMatheweKufakwina
    @LinlyMatheweKufakwina 3 วันที่ผ่านมา +1

    Hmmm koma people aaa pliz polani moto

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 3 วันที่ผ่านมา

    Khasu lali fupi limudikirira nayyo😂

  • @HoseKatsekera
    @HoseKatsekera 3 วันที่ผ่านมา +2

    yomweyo, malawi ali boh, tiwuchape bas 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @PatriciaAlomwe-oz8wc
    @PatriciaAlomwe-oz8wc 3 วันที่ผ่านมา

    Yomweyo galu iwe

  • @PaulFrank-tj2mc
    @PaulFrank-tj2mc 3 วันที่ผ่านมา

    Anakonza

  • @JOHNSANGWALI-r2m
    @JOHNSANGWALI-r2m 3 วันที่ผ่านมา +1

    Iiiii zikuti bwanji Kodi
    Okay Dili Ku mastand kuvesera

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 3 วันที่ผ่านมา

    Chakwera ngati uli moyo change please dziwa kukhala bwino ndi anthu, waona momwe ena akusangalalira za maliro? Please Apure sinthani