Kodi ku ungaku united nations meetings amakonda kulodza ma president athu à.kumalawi..Ndiye pano akamdzapitanso adzikakhala ku visitors lodge where they will be cooking and eating.and bathing alone..by theor own malawi cooks.amen.but not the wicked azungus doing or hosting them.
Komatu ku UNGA uku anthu amapangako zinthutu,si amutharika a Peter nawonso zanja lakumazele lidafa that time amachokelanso ku UNGA komwekoso. Nde katemela wake nde waukalitu yomwe amalandila kumeneko.
Rest in peace 😂ngati zili Zowona, ife timawona ngati ndiwoposa Mulungu tu, amuyaya
I dont wait msg say lessen that ...Any way rest in peace chikangawa go well ❤❤🙌🙌
Ndipo ther is no peace for the weaked ndipo sindingamvere chisoni munthu oipisisa Malawi muno uyu!..apite kumene olo ntamva kuti zatero ndizangoti “rip skc and 8pipo”..justice shall be served..Mulingo umene umamulinga nawo nzako naweso uzalingidwa omweo..ndipo munthu sungakhale ndimtendere dziko lonse kumakamba zoipa za iweyo never..mxiew
Ngat ndichoncho ai akapume watidyesa chiteze 😂😂😂😂
Ntanyiwa, ntanyiwa, ntanyiwa ndakuitana kangat ndi maboza ako kuyipa nkhope ndi mau omwe chitsiru Cha munthu
Iwe ndiwausilu umatinamiza
Chimwalire bas chimunthu choipa mtima 😢
Azaweluza akha mlungu
Dziko ndila yehova
CHEERS CHIKANGAWAAAA AMBUYE KUMWAMBAKO CHONDE DULANI MOYO WA LAZARUS CHAKWERA PLZ GOD IN HEAVEN
Amen
Ngat Sanafe ine ndituma Anthu Kt Akamaleze Mission Kuzinga Ngati Mbuzi
Dziko ndi la yehova ndi zozala zake zomwe. Kwa iye ku khale ulemerelo lero ndi nthawi zonse
Amen
Why mcp is hiding this store
Ndayamba kukaika zokamba zanu a Ntanyiwa including Bakali Muluzi tv. Nanga munthu kudwala choncho angapange ma press ups chonchija
Akanamugoneka kuzipatala zakwathu konko kumene sakugurirako mankhwala iye waba ndalama zamalawi nanga anthu akumuzi akadwala apanga bwa
Achakwera awona zokhoma kwambili chifukwa cha nkhanza zawo ndipo chakwera atafa lelo ineyo ndiye ndisangalala koopsa
Yes! We can confirm that here report from galden city tilimbe mtima basi Mikel usi has to appoint his vice president 😢
Zosatira zakuchingawa zayamba kufika 😊
Limpompo yonama makape😅😅😅😅
Akhala President wakumalawi, oyamba kuchira ku Garden city
Achipatala chonde yesetsani kuno sitikumufunanso tikamupeza komweko watizumza munthu ameneyi kwakwana anthu 9 osalakwa ajaa mizimu yawo myokwiya anasiya anthu omwe amawathandiza Yesu ndi ambuyedi
😂😂😂 yomweo chikangawa satanic
Dan lu waigwetsa mcp ndinyimbo
Chikangawa woyeee
Ambuye chonde malidzan 100%😂😂
Koma ngati wafad kumwamba kidyele nyama
Iiiiiii
😂@@handsomenkonde2552
Mzukwa umeneu watitopesa
😂😂😂😂my people ✋ @kullu nafs malikul kitaba kkkk ayi xikomo washiyao wangalusa yakuona eee.
Alimoyo chikangawa koma kukumununkhula kusabwera
😂😂😂😂😂😂 ndudikila apeleke report aboma ndipomwe ndi comment ok
My country is not going well
Asafe koma azingozuzika nd kudwala mesa amat Peter wathu ndi wokalamba😂😂😂😂MULUNGU mwini moyo wapanga zoziwa yekha😂😂😂😂😂
Zoona kod nanga Dan lu apanga bwanji kkkk
Amwelile ndigaluuyu
Tsitsani mbendera chikangawa watisiya🕺🕺🕺🕺chisangalalo chake kuposa chapa 1 january😂😂
😅😅😅😅😅
Tasisa kale apite uyu galu
Ndizoonadi chilimawamwalira ine ndimaona ngatiiye ndimulungu😂😂 8:31
President or kaya ndindani akadwala asamapite kunja koma adzipita kuchipatala cha m'Malawi mommuno.
Kodi ku ungaku united nations meetings amakonda kulodza ma president athu à.kumalawi..Ndiye pano akamdzapitanso adzikakhala ku visitors lodge where they will be cooking and eating.and bathing alone..by theor own malawi cooks.amen.but not the wicked azungus doing or hosting them.
Yawa asaname ,,, pretoria ndi jozi ndika mtundatu komanso akulankhulamo angadziwe chani or ku Garden City ko angayandikire 🤣🤣🤣🤣
Pita yomweyo abwelele olo bakhili abwelele
Komano ngati wamwarira zitisangarasa chifukwa athu amazuzika 😂😂😂😂😂
Kod chitedzechi chabwela bwanji ndi chakwela tiyeni tizidzilimbikila osamaloza chala munthu masiku omaliza ano kudzakhala njala basiiiii
Aganyu ama 2000 ndiomwe angadandaule
Akuchedwa kufa nyani hule chigawenga ameneyo mbuzi
Kkkkkkkk
🎉RIP CHIKANGAWA
Anakomoko bwanji sanamwalile amwalile
Malawi ndimaziwa ine ameneyo 😂🤣
Ngati wamwalila akaphume sitimufuna galuameneyo
Ndipo ngati sakumwalila m,sanga chilima ndi athu ena anawapha kuchikangawa aja asamusiye amukoke sangamulephele kumuko amwalile changu asatinyase ife
Zoonazake are basi
Bola next life asakakhaleso president 😭
Kkkkkkkkkkllkkkkk tiziona ndi ntanyiwa
Ma Cadet mukhalabe choncho mpaka YESU adzabwela osapeza mtendele, mudazolowela kudya zodzipenta
RIP Mr Chakwela 😮😮😮
😂😂😂 athu angundika akuti 20 30 wooo 😮
Km ineso zothela data dzina aaaa za ziiii afe ndilibe naye mission
Achile asathawe zisankho
Oh zonse nthawi kaya ali moyo kaya wafa akudziwa ndi mulungu
Geyezi ndidzoona
Tiyeni tizikondana
Yawina 😂😂😂😂😂 watizuza kokwana
Yawina kkkkk
Akause mu mtendere tikampeza 2099
Mwagwa nayotu ma cadet apa. Bodza lija balalaa. Manyazi bwaa?
Komatu ku UNGA uku anthu amapangako zinthutu,si amutharika a Peter nawonso zanja lakumazele lidafa that time amachokelanso ku UNGA komwekoso. Nde katemela wake nde waukalitu yomwe amalandila kumeneko.
Zonama zonse mwalankhula umu.
Chepetsani kutalitsa nkhani zonama.
Mawa President akupita kukamenya Golf.
Mwanya nayo mwakhaula
Ngati ndizoonad ambuye tengeni bas
Koma Makomenti mbweeeeee kukunena kut oipa,, enaaaa pamaliro po mukamva anali wabwino ayi abwino sakhalitsa chabwino.......
Ine sindingalile aaaaa
Okumba dzenje agweramo Linda madzi kuti adutse umazisempha iwe mtanyura
Chimwalire basi chimunthu choipa
Koma tisayembekeze kuti atalowa wina kuti zinthu zingayende even atalamula abambo anu sangasinthe dziko ngati ulesi wake ukhale omapemphetsawu ayi
Kkkkkk km ndye yaaa mwayankhulatu man ohool olila akhale a MCP okha
Koma zilibwino kwambiri iiii ambuye ayakha pephero lamawi
Makolo apita chkangawa woyeeeeeeee kkkkkkkkkkk
Amwarire nde bwino amene adati phera chirima
Igwe Basi mbendela
AKAPUME CHAKWELA WANAMA NTHAWI YAITALI LA 10 LAFIKA 😂😂😂😂😂😂😂RSP
Utsi subuka popanda Moto HA lero ndachedwa ku NTCHITO,kodi kumudziko zikuti bwanji?😢
RIP chakwera 😂😂😂😂😂😂😂😂
Tiyamike mulungu
Apitebwino
Apite watikwana
Rest well chikangawa
Wasala Gesebelo ndi azilongo ache Chimwendo Banda ndi Kamajekete
😂😂😂 chikangawa
Unapha chilima umaona ngati iwe suzafa ......ineyo chakwera akuyenela kufa ndithu ....watizunza mokwanila chisilu cha munthu
Alipo ndipo akharapobe mpaka wina achita manyazi 2025.
, Mabodza awa pano ai.
Mbole yache afe basi
Pathako panu nonse a dpp, amene wamwalila ndi Peter mathanyula
KUMENYA KUGWETSAAAAAAA MUNYERAAAAA MUNYAAAA MA CADET AMAGAZIIII
Akufa nd m"bale wakoyo
Chafwa ichoo iwe😂😂😂
Ngati chilima anafa iye kulibwanji? Tikasake ku chikangawa naye
Bambo asikono mwai wanu ndiumeneo
Ayi zicomo zabwino soze😂😂😂😂
Eee khristu wachita bwino kumwalira
Kumenya kugwesadi😅
Asabwereso ameneyo watizuza kwambiri munthu opanda chisoni
Choipa chisata mwini
Ndizoona wamwaliladi
Ngati wafa chikangawa akause muntendere chifukwa watinzuza a Malawi
Km akachedza ndichilima bwino bwino?? 😂😂😂😂
Galu anadya nsima yanga,pano amwalira achita bwino amwalira.galuwe mzimu wako usawuse mmtendere.hehede ulu
😢
Opha ndi lupanga
Mungobwereza nkhani basi kutithera ma data basi.
Chakwela Wachita bwino kumwalila ,
Ndipo ayesese kuti amwalile zenizeni
Kkkkkkkkkk ayesetse
@@moreenkagalu7392 eya zisalepheleke