Well conclusion bro, that is the fact and reality let's bring people who have something better not mulimi all the way from asamunda no man please Mr president
Chitini chopanda kanthu chimatsokosa kwambiri ndiye mwazioneratu nokha. Ndimayesa amanama that an empty tin makes noise. Thanks bwana pakusakatula maganizidwe aa anthu
Well done brother koma tafufuzaniko za ma passport please malawi wawonongeka wuyu pakufunika ma demo anyone chakwera ndi mphawi wa chabe amene sangatukule ziko
Mr Atupele anayankhula kale kuti lenara samupasa bus or galimoto, Chimene tizawakumbukile agaluwa ndi kuba kowopsa basi ndikupempha pempha. Sindisintha Chichewa changa, kuti mwa Chakwera mulibemo ubwino, munthu wotumidwa ndi satana angapange zokhumba anthu? Mesa akupanga chimene tate wakeyo akufuna? Dont expect anything good from this heartles presdent.
Mupange video yoti ma donating a Cyclone freddy anabwera angati ?kikikiikiki Malawi 🇲🇼 😀 🇲🇼 wanthu akulowera ku ntchire. ♥️ Mapeto ake mitengo it itha, koma nawonso they are failing to empower Malawi 🇲🇼 😢 Shaaaaa.
Ine sindizabweraso ku malawi kulimose kulimanda ku malawi ndizataniko ndizafe. Ndi njala ine ayi Malawi 🇲🇼 anavunda kwambir chakwara zeru alibe wawononga malawi
Atsogoleri a mu africa lero ayamba kutseka zitseko za atsamunda ndipo ali pa mgwilizano wochotsa US dollar mma bank mwao. Pomwe President wa Malawi Ali busy kupempha kwa ma oppressors. A disgraced man. Experience alibe zoona.
Kudzavuta kumuyiwala chakwera ndi team yake wagwiritsa a malawi mafuwa a moto kudzera mu bodza. Ndithu anthu awa palibe choti angapange choposa kupemphetsa nkumagawana ndalamazo mu team mwawo
Achakwela angogwidwa kwachotsa pa u president 90 minutes eterber wakuba
Usogoleli olilisa kwambiri wa chakwera😢😢😢 Malawi will never forget you
😢😢😢😢
I like you Bro , you know how to analysis things . keep it up !
I like you brother thanks you so much
Zikumveka ndithu munthu wankhuru kumeneko ulemuwamu bwana ...ndizoona ndithu kutikodi awa analindani .big guestion sir
Bro i see you a very good analyst, kunena zoona tikifunikadi ma investor enieni kut tiseve zambiri
My man,,,,,,,,,,you deserve,,, much respect,,,,achakwela atipha awaa
Well conclusion bro, that is the fact and reality let's bring people who have something better not mulimi all the way from asamunda no man please Mr president
Chitini chopanda kanthu chimatsokosa kwambiri ndiye mwazioneratu nokha. Ndimayesa amanama that an empty tin makes noise.
Thanks bwana pakusakatula maganizidwe aa anthu
You are king 🤴 of history in our country 'kma chilungamo China kupweteka ndithu
Perfect
Ambuye siyani Dr chakwera agwire nchito mukuoneka kut za mboma simuziziwa mbwerera basi za ziii
Well done brother koma tafufuzaniko za ma passport please malawi wawonongeka wuyu pakufunika ma demo anyone chakwera ndi mphawi wa chabe amene sangatukule ziko
Thanks God bless you
🙏🙏🙏 timakusangalalilani achikulire
Boma ili nde zero pa zero.😢😢😢
Zelo pa ten
The king of history
Kkkkkkkkkk Eeee!!!!!! Koma ndie kwapephedwatu...kungozolowela Chachikhumi.mpaka kukapepha Company yopanga juice.
Zomwe zimandimvetsa Chisoni ndizoti mtsogoleri wadziko akamalephera kugwira bwino ntchito yake pali anthu ena osaukisitsa omwe akuponderezedwa ndi mtsogoleriyo, muwaona akuimbira mmanja ndikumamuchemerera mtsogoleriyo. Ndife olilitsa zedi.
Kkkkkkkk inu ndi big bas amangoona ngat zimangobwera ngat mana lerodi cyclone Freddy yasanduka bizines sopano 😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😂
Koma iwe ndikatundu madzi😂😂😂😂😂😂😂😂🎉🎉
🤣🤣🤣🤣🤣
Bwanji angotula pansi maudindo awowo tatopa nawo ife anthuwa
😢 iiih koma ine chakwera 😢😢
Always I disagree with you but now totally! totally agree with you accordingly
Kupempha like akupenpha chachikhumi ,he must go!!
Mr Atupele anayankhula kale kuti lenara samupasa bus or galimoto,
Chimene tizawakumbukile agaluwa ndi kuba kowopsa basi ndikupempha pempha. Sindisintha Chichewa changa, kuti mwa Chakwera mulibemo ubwino, munthu wotumidwa ndi satana angapange zokhumba anthu? Mesa akupanga chimene tate wakeyo akufuna? Dont expect anything good from this heartles presdent.
Big man ndinu katundu omanga ndi mawaya afukuleni musasiye tiziudziwa usiru wawo akupangawu
Dr chakwera and doog aaaa
Kodi awa adali ndani?
I used to LOVE Boma ili mbuyomo koma pano..
Aaaaaaaa Zosayenda uyu or atangoyerekeza kuyenda wapasi nditha kusanduka DAVID . mwala utha kugwira ntcito
Program iyi imandisegula maso, ndikunditsuka ubongo
Thanks u boss
Kkk big man kutsitsa mfundo zabwino
Salute bro
Tikusowa Mpapaya Mkumat Amakambilana Ndi Company zopanga Juice 😂😂
Chakera awononga ku malawi bwanji mulungu tutandizen tuuu koma ndalama zimenez abweza ndan kod 😢😢😢😢😢😢😢😢😢
Respect to you my brother
Mupange video yoti ma donating a Cyclone freddy anabwera angati ?kikikiikiki Malawi 🇲🇼 😀 🇲🇼 wanthu akulowera ku ntchire. ♥️ Mapeto ake mitengo it itha, koma nawonso they are failing to empower Malawi 🇲🇼 😢 Shaaaaa.
Big mumakwana koma ndaseka mpaka nthiti kuwawa🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 ndiye mwati chakwela amaganiza bwanji???? Eeeeeee
Koma nkhawa zanga ndi ndani yemwe angatipulutsr
2:43 2:46
Wa udindo aliyetse adziba,, akhulukidwa zili ku Malawi,,,pano palibe kuopa kuba chifukwa chikhululuko chilipo,,,koma tsoka ili kwamuthu ovota palibe chimene chikumukomela muthu otsauka.
Dziko lingatha zimayenda ngati Baibulo. Mwawonjezatu pamenepo
Ine sindizabweraso ku malawi kulimose kulimanda ku malawi ndizataniko ndizafe. Ndi njala ine ayi Malawi 🇲🇼 anavunda kwambir chakwara zeru alibe wawononga malawi
Mumatha man keep it upp
nothing to say you man you deserve medo koma ndimafuna nditakuona uli ndimawu aboh
Muluzi anali makina mseu wathyolo mulanje its like built yesterday
Kmans mumamunyoza kut sangapange kanthu koma mwamva lero zimene muluz anapanga ķwa anthu amene amazitsata
Achakwela mukhululukiletso ma prison amene alibe mulandu wakupha,,ogwililila,,ndi opyanya nyumba please atuluseni
Atsogoleri a mu africa lero ayamba kutseka zitseko za atsamunda ndipo ali pa mgwilizano wochotsa US dollar mma bank mwao. Pomwe President wa Malawi Ali busy kupempha kwa ma oppressors. A disgraced man. Experience alibe zoona.
Ngatikuli program yomwe imandinyasa ndimeneyi yokhuzana mcp ndachizawowa
Tenaon amenyo nchewa wasiru amneyo wanonga Malawi 🇲🇼 akuyesa kuvena gule
Amakakumana ndi Sattar ameneyi
Munthu wankulu ulemu wanu 👏👏👏
Komaso trip ya President ya ku Malawi anthu ambiri,there is no war on Malawi but security yambiri
We need to vote again awa zikuoneka Kuti zawakanika basi
Keep it up big
Kodi awa anali ndani?😂😂😂😂 Yankho mulipeza nokha😂😂😂😂
Is true he think like mana like time of Moses
Chakwera ndi anthu ake nzeru alibe ndipo kaya ndinene bwanji?pena ndimalakalaka ntakhala ujeni ndikuthana nawo andale opusawa
Koma nkhawa zanga ndi ndani yemwe angatipulutdr
Ntundu umenewu sibwino kuwupatsa u president m'malawi muno chifukwa ndidzilombo, a malawi tinapanga mistake
Kusowa kolima chifukwa choberekana ngati ntchentche ...palibe chomwe amalawi angapange pawokha .
I think in future Malawi will be part of zambia because it's too much now
Kwathu kuja amene anatiloza akanatikhululukira 😢
Akanatileka koma mfiti ameneyi😢😢😢
Koma ndiye Malawi tifapo 2 chifukwa anthu amenewa akungoba ndalama basi
anyway big timakunyadirani
Chakwera why 😢😢😢
😂😂😂😂 ati kodi awa anari ndani ?? Yakho mulipeza nokha 😂
Mwayi okwela dege analibe kkkk
Mumatha abwana awa anali ndani awa😂
Malawi tili ndi madzi ponsenponse koma boma limangoganiza zokuba ndalama zathu iwo kumalemela
Ndinanena kale kuti mmutu mwa mkulu ameneyo muli mamina okhaokha komanso okuba ndalama za a Malawi
Bomali ndilasatanik coz ngongolezimenezo azabweza ndimagazi amalawi ndichifukwa akusowesa mankhwala zipatala ndi chakudya Kuti amalawi azimwalila azipeza ziwalo ndimagazi sure
Tht true bro
Zikomo kwambiri abraz we vote MCP out
BIG 👍
Kudzavuta kumuyiwala chakwera ndi team yake wagwiritsa a malawi mafuwa a moto kudzera mu bodza. Ndithu anthu awa palibe choti angapange choposa kupemphetsa nkumagawana ndalamazo mu team mwawo
Anazolowera kusonkheledwa ndi mpigo kumati zabusa kuparsidwa chopeleka kudya zachinkhumi
I wish to have chakweras number so that I can send this to him, # this is the most corrupt government in Africa
Uyu mumati chakwerayu ndi chitosi basi aah!
Mbuzi ya President iyo
Ananena kale APM
Kuti ndi Bulutu Chakwera
President cakwera tidzamukumbukira kuti anali wakuba wakupha oononga.
Usaiwaletu Paja dpp yakoyo imanama kupereka ma figures ndipo ndalamaso paja amkangogawana pachilomwe pawo kumangopatsa muli ndalama azigulila gondolosi
Zoona m'bale siukunama koma ubwino wake tili nacho choloza chomwe pitalayo anachita, kusiyana ndi achakwera osabawa tikungoloza ngongole zokha basi.
Kkkkkkk koma ndasekaa kkkkkkkk
Please president chakwela leave presidency and go
kutipweteketsa basi olo misewu ya mamidzimu osapalanso yakumbikakumbika nde ndalamazo akungodya kwawoko ayiwala kuti adzafunaso anthu
Chakwela ndi mbudzi😅
Kkkkkk km man mwayakhula masikini aulesi kkkk ndie mwat chakwela al mgula lamasikini kkkkkkk
Tcheya mani wa anthu ovutikaa kkkkkk
Sibola atsamundawo asatenge malo anga 😢ndikuopa
Mmmm inupenapake paja
Ndinu audf
Akhululuke ndithu Chonde mulungu dalitsani Malawi
Iyeyo anali mbusatu basi kenako president
Boma likulamulidwa ndi zigewenga chakwea ndiwakuba
😂😂😂😂😂 wabaya zed president uyu watitola mudziko Muno kwabas dziko lonse walitenga ngat mudzi wakwao kulamulira dziko ameyesa zibwana eti
Kkkkk k zoopsa abuse opanda nzeru okuba cisiru mbava yachabe chabe mbuya wakumidima okumwA MAGAZI
Anali mkulu wampingo uyu apite akatumikile nkhosa zake
Ichi ndie ayi chichoked 😢😢
Mbatata yamuthu muthu yu kuba anayambira ku assembly
Mwayi okwela ndege alibe kkkk
Tanditukwanireni ameneyu bwana,
Mkulu uyu ndi wa BaBulo basi 😂😂😂😂😂🤣
Tell them bro don't get tired