Limpopo APM akuthilidwa poizoni ku mangochi masanawa Ntanyiwa akuulura anthu omwe akukapanga izi

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 12 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 81

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo 27 วันที่ผ่านมา +9

    Oh ALLAH tithandizeni malawi tikuvutika mutetezeni peter

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 27 วันที่ผ่านมา +6

    Ineyo ndizakhala okondwa ikazangoluza mcp ndimafuna chakwera,,,mwana wake,,, zikhale,,kunkuyu,,mkaka,,,anthu amenewa azagwire life imprisonment osazawapasa bail

  • @user-hs4bm2yj8r
    @user-hs4bm2yj8r 26 วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu kutetezeni akapolo Anu, amene khumbo lawo ndikuombola dziko lathu

  • @FireKajambe
    @FireKajambe 27 วันที่ผ่านมา +3

    Pharaoh tried to kill Moses when he was young but later pharaoh died before Moses . Eksodus 16

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 วันที่ผ่านมา +4

    Comrade pls muomboreni Mutharika..........muimbiren fon ya direct

  • @TechnicalSupport-lk9im
    @TechnicalSupport-lk9im 25 วันที่ผ่านมา

    Yomweyo galu iwe ulula Thanyuwa agalu amenewa ayaluke

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 25 วันที่ผ่านมา

    Mulungu alowelerepo ndithu,,, ndikuteteza Ana a Malawi

  • @GiftNasila
    @GiftNasila 26 วันที่ผ่านมา

    Mata Nkhanga Zaino ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 27 วันที่ผ่านมา +4

    Angoyelekezaa

  • @OusmanBen-f4o
    @OusmanBen-f4o 27 วันที่ผ่านมา +4

    Utsogoleri wabwino sukhala wamphamvu ndi kukhetsela mwanzi ayi,koma kukhala ndi mphamvu kwa anthu ochuluka okondwela ndi utsogoleri wakowo.Anthu pano sakondwela ndiutsogoleri wa Chakwela ayi nde asapange 4c anthu kut amukonde akulephela zambiri pa utsogoleri wake,achoke!achoke! achoke basi anzake alamulire mpandowu

    • @user-gg2qn7zf4m
      @user-gg2qn7zf4m 27 วันที่ผ่านมา

      Koma kodi amalawi inu chikuchitika ndi chani mungosekelela zopusa ngati zimenezo muziwe kuti mulungu akulanfani chifuka palibe wa muyaya pa zikomo pano muziwe zimenezo

  • @LetweebZwewe
    @LetweebZwewe 26 วันที่ผ่านมา +1

    Amuphe ife chakwelayo tizamupha ndimanja ngati galu wachiwewe

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula 27 วันที่ผ่านมา +2

    Amuthanyiwa tangowaimbilani ku dpp ko muwauze chonde ndinu akuluakulu nonkhanokha 😢

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes5057 26 วันที่ผ่านมา

    mwadzuka sitafu yonse kumeneko. tikudikila zarelo ka 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @CathyYassimin
    @CathyYassimin 27 วันที่ผ่านมา

    Oh ya rabbie tilozeren Muthu wabwino okhulupilira lnu ,lnde kwainu kulibe utsogoreli umenewu

  • @GiftNasila
    @GiftNasila 26 วันที่ผ่านมา

    Limpopo FM ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 27 วันที่ผ่านมา

    Indeeeeee Mr Nkhanga zomwezo timakunyadirani mukuyimirira Amalawi Ambiri.
    Mulungu wathu wamoyo adzikhala Ku Mbali yanu Mr NTANYIWA osayiwalanso Mchimwene uko ku Bakili Muluzi TV Dzanja la Mbuye lidzikutetezani.

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w 26 วันที่ผ่านมา

    Palibe chobitsika pansi panthaka, kwa oipa kulibe mtendere, palibe tchimo lomwe lizabweretse mtendere pa umoyo wa munthu ndiponso zilibwino poti zaululika sapanga abwelerako amenewo

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 27 วันที่ผ่านมา +2

    Dzanja lanu mulungu wamakamu tetezani moyo wa peter langani onse oipayo

  • @LindaTebulo-k4w
    @LindaTebulo-k4w 26 วันที่ผ่านมา

    Just pray for Malawi may God help us

  • @PeterThomas-o9k
    @PeterThomas-o9k 26 วันที่ผ่านมา

    Ukhale nalo dziko uzikonda wekha satana iwe watopesa chakwera your not right stress yakoyo usawaphe azako
    Otsalakwa uzimve muntimamo koma kulibe chamuyaya

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 27 วันที่ผ่านมา +4

    Eeeee koma abale Mcp eishhhhhh mukamachita zanuzo dziwani kuti kunja kuno kuli Mulungu our God in heaven may you protect Peter muntharika in Jesus name Mulungu musalore chititsani manyazi satana

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 27 วันที่ผ่านมา

    Malawi Chikangawa Party yadya Chilope Chosavuka nacho.
    Mpaka kuzapezeka akuwayika pa list anthu omwe anawapha kale Chilope chitalowerera . Koma Mr Lazarus its too much hmmmm

  • @UssenNjirinah
    @UssenNjirinah 27 วันที่ผ่านมา +1

    Nde manganyu akutani ku Mcp ku

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 27 วันที่ผ่านมา +1

    Chikangawa chakwera koma zooona eeeeish ukalibe ukhuta nyama za malemu atisiya popano popano

  • @user-wp9js5vu6s
    @user-wp9js5vu6s 26 วันที่ผ่านมา

    Kuli mulungu kumwambaku 🤝

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula 27 วันที่ผ่านมา +2

    Ayelekeze aone zosaona

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 27 วันที่ผ่านมา

    Mulungu tetezani azitsogoleri ofunila zabwino Malawi amen

  • @NizigiyimanaChantal-c2p
    @NizigiyimanaChantal-c2p 27 วันที่ผ่านมา +2

    Kudziwike kut mumatha Ambuye

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b 27 วันที่ผ่านมา

    Angoyelekeza awone dziko liwaukile tatopanawo ife

  • @wisekanyinji5377
    @wisekanyinji5377 27 วันที่ผ่านมา

    Sakunamatu, mcp njakupha kuyambila kale, ndie sitikudabwa kuti nchito zawo nzamwazi

  • @DysonNakhaphe-bo4dl
    @DysonNakhaphe-bo4dl 27 วันที่ผ่านมา

    😢😢tiudzeni mene zathela

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 27 วันที่ผ่านมา

    Zigandanga zaku ruanda and Israel zizipita mmakwawo, sitikuzifunanso mmalawi muno except those innocent ruandaniz

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 27 วันที่ผ่านมา +1

    Komatu achakwela zomwe mukupangazi mulungu akuwona siku ndilimozi chomanphela ana ayini ndichani kapena mukupeleka sembe kwazanu akunyanjawo mukamakhala muziziwa kuti nanuso makasu akudikila kukakumba zenje lanu mizimu yaathu mukuphawa ndiamene akakulandileni pakhomo lopapatiza

    • @lillynhlema9656
      @lillynhlema9656 26 วันที่ผ่านมา

      Ndipo uyuy he has never been a pastor.....kuubusa kuja ankangobisalako

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 27 วันที่ผ่านมา

    Zikomo Limpopo FM radio station %

  • @mikesandali8425
    @mikesandali8425 27 วันที่ผ่านมา

    Iwe opusa kwambili....

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 27 วันที่ผ่านมา +1

    Moto kut buuuu❤📺💪💪💪💪💪✊✊✊✊🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @HendrinaNyirenda
    @HendrinaNyirenda 27 วันที่ผ่านมา +1

    Ndie mwati hug yaku nsepe ija inali ya Judas Iscariot? Ndile zophana ndizachikape😢

  • @EdnaSiyan
    @EdnaSiyan 27 วันที่ผ่านมา

    Chipani chanji chongokhalira ku khetsa mwazi. A Mbuye ayendereni onse ali ndi maganizo oipa

  • @PhilmonBanda-dm7nj
    @PhilmonBanda-dm7nj 26 วันที่ผ่านมา

    Zophanazo nde zachibwanatu

  • @RajaboGostihno
    @RajaboGostihno 27 วันที่ผ่านมา

    Comrade let's build up our nation...all the corners of the nation 4:44 4:44 4:44 4:44 Durban south....

  • @LuciusMakupe
    @LuciusMakupe 27 วันที่ผ่านมา +1

    DPP guys don't take for granted Samalani bas

  • @JoyceJJames-kj7tg
    @JoyceJJames-kj7tg 27 วันที่ผ่านมา +1

    Zovuta kwambili ambuye andithandize

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa 27 วันที่ผ่านมา +1

    Sikusinja kkkk

  • @ShakilahMbwanaa
    @ShakilahMbwanaa 27 วันที่ผ่านมา

    Please dpp be careful this is getting worse to us all malawian their crying a lot so be careful then listen to Tanyiwa what him saying please

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 27 วันที่ผ่านมา

    Ngati anthuwo ndi aku Rwanda bwanji interview monga kuyankhulana nawo m'modzi m'modzi pomwe akulowa

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 วันที่ผ่านมา +1

    Aimbireni fon ya direct a DPP

  • @BrianJoe-z7u
    @BrianJoe-z7u 26 วันที่ผ่านมา

    Uthenga waurere thanyiwa

  • @clalesschisale3792
    @clalesschisale3792 27 วันที่ผ่านมา +1

    Ndale zomwe akupanga a Mcp zikanakhala kuti nayo DPP OR UDF kapena utm imapanga zomwezi sibwenzi MCP itabwelelaso mu Boma chomwe akulimbirana ndi anzawo ndi chani kwenikweni kodi kukhala ochokela zigawo zosiyana ndikolakwika ?😢😢😢😢😢

    • @user-gg2qn7zf4m
      @user-gg2qn7zf4m 27 วันที่ผ่านมา

      Kodi chakwera iye akuyesa kuti ndi wa muyaya?kudya kuno kuli mulungu

  • @DavieMoyo-pe8vn
    @DavieMoyo-pe8vn 27 วันที่ผ่านมา +1

    Umakwana iweyo

  • @MaryJefry
    @MaryJefry 27 วันที่ผ่านมา +1

    Adadi athu okhawo utisiile

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 27 วันที่ผ่านมา

    Ngati Ku DPP kuli achinyamata ovuta kwambili aja amadziyakhula ma social media kuti iwowo ndi anamandwa iyi ndithawi yawo kuti athane nadzo zigewengadzo,,zikufunika kuti onsewo mawa apedzeke kuti onse ndi wankulu wawo ndi mitembo zigandanga zatchabe chabe

  • @thokogwebe2337
    @thokogwebe2337 27 วันที่ผ่านมา

    May God protect him

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv 26 วันที่ผ่านมา

    Mcp yathapo palibe angaivotere

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly 27 วันที่ผ่านมา

    Mcp Thambani Thambani chipani cha magazi magazi mwazi mwazi

  • @MarthaWemba
    @MarthaWemba 27 วันที่ผ่านมา +1

    Noted

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 27 วันที่ผ่านมา +1

    Imeneyo nde mcp kaya poti enanu mukuionela chilendo koma ife tachoka nayo pakatali nanu muidziwe

  • @FloLuhanga
    @FloLuhanga 27 วันที่ผ่านมา

    Please adziwitseni a DPP awo adziwe tatopa kulira

  • @JozzyNthinda
    @JozzyNthinda 27 วันที่ผ่านมา

    Limpopo imakwana

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 27 วันที่ผ่านมา

    Kukakhala security yokwanila

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o 27 วันที่ผ่านมา

    Mudzakhala nkhondo ya chiweni went mtsogolo muno

  • @modestermalunga
    @modestermalunga 27 วันที่ผ่านมา

    😢

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 27 วันที่ผ่านมา

    Mulungu akuyendele ndi mabodza akowo

  • @swintonchirwa1897
    @swintonchirwa1897 27 วันที่ผ่านมา

    Atinkenawo ndi amene akakamila

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 27 วันที่ผ่านมา

    Kodi page iyi ili pa whatsapp

  • @MartinNyirenda-w7s
    @MartinNyirenda-w7s 27 วันที่ผ่านมา

    Dziko likupita kuti ili?😮

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 วันที่ผ่านมา

    Aimbireni a DPP

  • @ChikumbutsochantzMakumba
    @ChikumbutsochantzMakumba 27 วันที่ผ่านมา

    Amanyengeza

  • @user-fh5yn8xk2k
    @user-fh5yn8xk2k 27 วันที่ผ่านมา

    Muyelekeze

  • @Malani41
    @Malani41 27 วันที่ผ่านมา

    Chamba

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 27 วันที่ผ่านมา +2

    Wabodza iwe galu

    • @mikesandali8425
      @mikesandali8425 27 วันที่ผ่านมา

      Mbuzi iyi yaboza

    • @mashallahleonard2793
      @mashallahleonard2793 26 วันที่ผ่านมา +1

      Galu ndiweyo wachipan chokuphacho

    • @IssacMateyo
      @IssacMateyo 26 วันที่ผ่านมา

      Kodi mesa amay ako ndakazako aja ndamene adavota chipani chakuphacho chikhale boma kulibetu chipani chosapha usanadzinamize galu mbuzi iwe

  • @user-rx4ck9ze1j
    @user-rx4ck9ze1j 27 วันที่ผ่านมา

    Kutelo ndiye ikhala yazikwanje sure

    • @user-hs4bm2yj8r
      @user-hs4bm2yj8r 26 วันที่ผ่านมา

      Kufadi ambiri galuyu watikwana