Utsogoleri wabwino sukhala wamphamvu ndi kukhetsela mwanzi ayi,koma kukhala ndi mphamvu kwa anthu ochuluka okondwela ndi utsogoleri wakowo.Anthu pano sakondwela ndiutsogoleri wa Chakwela ayi nde asapange 4c anthu kut amukonde akulephela zambiri pa utsogoleri wake,achoke!achoke! achoke basi anzake alamulire mpandowu
Indeeeeee Mr Nkhanga zomwezo timakunyadirani mukuyimirira Amalawi Ambiri. Mulungu wathu wamoyo adzikhala Ku Mbali yanu Mr NTANYIWA osayiwalanso Mchimwene uko ku Bakili Muluzi TV Dzanja la Mbuye lidzikutetezani.
Ukhale nalo dziko uzikonda wekha satana iwe watopesa chakwera your not right stress yakoyo usawaphe azako Otsalakwa uzimve muntimamo koma kulibe chamuyaya
Eeeee koma abale Mcp eishhhhhh mukamachita zanuzo dziwani kuti kunja kuno kuli Mulungu our God in heaven may you protect Peter muntharika in Jesus name Mulungu musalore chititsani manyazi satana
Malawi Chikangawa Party yadya Chilope Chosavuka nacho. Mpaka kuzapezeka akuwayika pa list anthu omwe anawapha kale Chilope chitalowerera . Koma Mr Lazarus its too much hmmmm
Ngati Ku DPP kuli achinyamata ovuta kwambili aja amadziyakhula ma social media kuti iwowo ndi anamandwa iyi ndithawi yawo kuti athane nadzo zigewengadzo,,zikufunika kuti onsewo mawa apedzeke kuti onse ndi wankulu wawo ndi mitembo zigandanga zatchabe chabe
Oh ALLAH tithandizeni malawi tikuvutika mutetezeni peter
Ineyo ndizakhala okondwa ikazangoluza mcp ndimafuna chakwera,,,mwana wake,,, zikhale,,kunkuyu,,mkaka,,,anthu amenewa azagwire life imprisonment osazawapasa bail
Perfectly said
Mulungu kutetezeni akapolo Anu, amene khumbo lawo ndikuombola dziko lathu
Pharaoh tried to kill Moses when he was young but later pharaoh died before Moses . Eksodus 16
Comrade pls muomboreni Mutharika..........muimbiren fon ya direct
Yomweyo galu iwe ulula Thanyuwa agalu amenewa ayaluke
Mulungu alowelerepo ndithu,,, ndikuteteza Ana a Malawi
Mata Nkhanga Zaino ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Angoyelekezaa
Utsogoleri wabwino sukhala wamphamvu ndi kukhetsela mwanzi ayi,koma kukhala ndi mphamvu kwa anthu ochuluka okondwela ndi utsogoleri wakowo.Anthu pano sakondwela ndiutsogoleri wa Chakwela ayi nde asapange 4c anthu kut amukonde akulephela zambiri pa utsogoleri wake,achoke!achoke! achoke basi anzake alamulire mpandowu
Koma kodi amalawi inu chikuchitika ndi chani mungosekelela zopusa ngati zimenezo muziwe kuti mulungu akulanfani chifuka palibe wa muyaya pa zikomo pano muziwe zimenezo
Amuphe ife chakwelayo tizamupha ndimanja ngati galu wachiwewe
Amuthanyiwa tangowaimbilani ku dpp ko muwauze chonde ndinu akuluakulu nonkhanokha 😢
mwadzuka sitafu yonse kumeneko. tikudikila zarelo ka 🔥🔥🔥🔥🔥
Oh ya rabbie tilozeren Muthu wabwino okhulupilira lnu ,lnde kwainu kulibe utsogoreli umenewu
Limpopo FM ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Indeeeeee Mr Nkhanga zomwezo timakunyadirani mukuyimirira Amalawi Ambiri.
Mulungu wathu wamoyo adzikhala Ku Mbali yanu Mr NTANYIWA osayiwalanso Mchimwene uko ku Bakili Muluzi TV Dzanja la Mbuye lidzikutetezani.
Palibe chobitsika pansi panthaka, kwa oipa kulibe mtendere, palibe tchimo lomwe lizabweretse mtendere pa umoyo wa munthu ndiponso zilibwino poti zaululika sapanga abwelerako amenewo
Dzanja lanu mulungu wamakamu tetezani moyo wa peter langani onse oipayo
Amen
Just pray for Malawi may God help us
Ukhale nalo dziko uzikonda wekha satana iwe watopesa chakwera your not right stress yakoyo usawaphe azako
Otsalakwa uzimve muntimamo koma kulibe chamuyaya
Eeeee koma abale Mcp eishhhhhh mukamachita zanuzo dziwani kuti kunja kuno kuli Mulungu our God in heaven may you protect Peter muntharika in Jesus name Mulungu musalore chititsani manyazi satana
Malawi Chikangawa Party yadya Chilope Chosavuka nacho.
Mpaka kuzapezeka akuwayika pa list anthu omwe anawapha kale Chilope chitalowerera . Koma Mr Lazarus its too much hmmmm
Nde manganyu akutani ku Mcp ku
Chikangawa chakwera koma zooona eeeeish ukalibe ukhuta nyama za malemu atisiya popano popano
Kuli mulungu kumwambaku 🤝
Ayelekeze aone zosaona
Mulungu tetezani azitsogoleri ofunila zabwino Malawi amen
Kudziwike kut mumatha Ambuye
Angoyelekeza awone dziko liwaukile tatopanawo ife
Sakunamatu, mcp njakupha kuyambila kale, ndie sitikudabwa kuti nchito zawo nzamwazi
😢😢tiudzeni mene zathela
Zigandanga zaku ruanda and Israel zizipita mmakwawo, sitikuzifunanso mmalawi muno except those innocent ruandaniz
Komatu achakwela zomwe mukupangazi mulungu akuwona siku ndilimozi chomanphela ana ayini ndichani kapena mukupeleka sembe kwazanu akunyanjawo mukamakhala muziziwa kuti nanuso makasu akudikila kukakumba zenje lanu mizimu yaathu mukuphawa ndiamene akakulandileni pakhomo lopapatiza
Ndipo uyuy he has never been a pastor.....kuubusa kuja ankangobisalako
Zikomo Limpopo FM radio station %
Iwe opusa kwambili....
Moto kut buuuu❤📺💪💪💪💪💪✊✊✊✊🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ndie mwati hug yaku nsepe ija inali ya Judas Iscariot? Ndile zophana ndizachikape😢
Chipani chanji chongokhalira ku khetsa mwazi. A Mbuye ayendereni onse ali ndi maganizo oipa
Zophanazo nde zachibwanatu
Comrade let's build up our nation...all the corners of the nation 4:44 4:44 4:44 4:44 Durban south....
DPP guys don't take for granted Samalani bas
Zovuta kwambili ambuye andithandize
Sikusinja kkkk
Please dpp be careful this is getting worse to us all malawian their crying a lot so be careful then listen to Tanyiwa what him saying please
Ngati anthuwo ndi aku Rwanda bwanji interview monga kuyankhulana nawo m'modzi m'modzi pomwe akulowa
Aimbireni fon ya direct a DPP
Uthenga waurere thanyiwa
Ndale zomwe akupanga a Mcp zikanakhala kuti nayo DPP OR UDF kapena utm imapanga zomwezi sibwenzi MCP itabwelelaso mu Boma chomwe akulimbirana ndi anzawo ndi chani kwenikweni kodi kukhala ochokela zigawo zosiyana ndikolakwika ?😢😢😢😢😢
Kodi chakwera iye akuyesa kuti ndi wa muyaya?kudya kuno kuli mulungu
Umakwana iweyo
Adadi athu okhawo utisiile
Ngati Ku DPP kuli achinyamata ovuta kwambili aja amadziyakhula ma social media kuti iwowo ndi anamandwa iyi ndithawi yawo kuti athane nadzo zigewengadzo,,zikufunika kuti onsewo mawa apedzeke kuti onse ndi wankulu wawo ndi mitembo zigandanga zatchabe chabe
May God protect him
Mcp yathapo palibe angaivotere
Mcp Thambani Thambani chipani cha magazi magazi mwazi mwazi
Noted
Imeneyo nde mcp kaya poti enanu mukuionela chilendo koma ife tachoka nayo pakatali nanu muidziwe
Kkkkk
Please adziwitseni a DPP awo adziwe tatopa kulira
Limpopo imakwana
Kukakhala security yokwanila
Mudzakhala nkhondo ya chiweni went mtsogolo muno
😢
Mulungu akuyendele ndi mabodza akowo
Atinkenawo ndi amene akakamila
Kodi page iyi ili pa whatsapp
Dziko likupita kuti ili?😮
Aimbireni a DPP
Amanyengeza
Muyelekeze
Chamba
Wabodza iwe galu
Mbuzi iyi yaboza
Galu ndiweyo wachipan chokuphacho
Kodi mesa amay ako ndakazako aja ndamene adavota chipani chakuphacho chikhale boma kulibetu chipani chosapha usanadzinamize galu mbuzi iwe
Kutelo ndiye ikhala yazikwanje sure
Kufadi ambiri galuyu watikwana