AMENE ATAPHONYE NKHANI ZA LERO ZAKE (NKHANI ZA LERO PA 9 AUGUST)

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 33

  • @IbrahimRamzy-s9i
    @IbrahimRamzy-s9i หลายเดือนก่อน +1

    Kom Dr Chikangawa ai ndithu Mulungu asakusiye choncho ai

  • @guilty-rz3ek
    @guilty-rz3ek หลายเดือนก่อน

    For the last day, the elders are getting to know each other😂😂😂

  • @allanchangalusa6662
    @allanchangalusa6662 หลายเดือนก่อน +3

    Afika bwanji mdzikomo? Nanga Ngati Boma silinadziwe, ndiye Kuti tili sefe?

  • @user-ld8gb9xm7v
    @user-ld8gb9xm7v หลายเดือนก่อน

    Wakasayina ninja kuti vibizi vinjile mu chalo chithu

  • @user-pg1kc5sg9w
    @user-pg1kc5sg9w หลายเดือนก่อน +2

    Kupanda chitetezo kotani kumeneko dziko mwathu anadutsa Kuti

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l หลายเดือนก่อน

    Pali zotukwananazo apa kukula mopusatu uku

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q หลายเดือนก่อน

    Koma chakwera ukufuna uphe amalawi tose.ndeno uzaramurira ndani komaso anthu akumizi sangaziziwe ayi azingomwa makhwarawo azingofa

  • @giftbanda7690
    @giftbanda7690 หลายเดือนก่อน

    Sopano makhwalawo aziziwika bwanji muthu muthu wakukudzi angaziwe za izii komatu ku Malawi nde sitili self

  • @jescandimbo6030
    @jescandimbo6030 หลายเดือนก่อน +1

    Ine ndamwako tu Amoxachikangawawo koma mtima zomwe umachita mmmhuuuuu

  • @AngellaMkata
    @AngellaMkata หลายเดือนก่อน

    Yomweyo bwamtasa iwe😂😂😂

  • @JonathanMunthali-n3c
    @JonathanMunthali-n3c หลายเดือนก่อน +2

    Waoder zimenezo ndani kufunakumaliza mtundu waamalawi

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 หลายเดือนก่อน +1

    Dziko lathu mulibe chitetezo, Nanga Mankhwala alowa bwanji mdziko opanda chilolezo cha Boma,, Chikangawa atimaliza ndithu!! Sakudziwa kuyendetsa dziko.

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np หลายเดือนก่อน

    Mankhwala alowa bwanji mudziko boma losadziwa?????

  • @evansjohn7766
    @evansjohn7766 หลายเดือนก่อน +2

    Zomvesa chisoni kumva nduna ikulengeza tchonchi,kkkkkkkk.....manga Iwowa ndi anthuwamba angaziwe zamankwalao ndani?akuti ngosaloledwa nanga alowabwanji?very useless

  • @juniortsegula3847
    @juniortsegula3847 หลายเดือนก่อน +1

    Mutipha a congress

  • @ChipiliroSpencer
    @ChipiliroSpencer หลายเดือนก่อน +1

    Afika bwanji kumalawi makhwalawo pomwe ali oopsa

  • @madalitsomakawa9708
    @madalitsomakawa9708 หลายเดือนก่อน

    Tasankhani background music yabwino amthuni

  • @THOCCOChimbali
    @THOCCOChimbali หลายเดือนก่อน

    Koma mcp

  • @OmegaMussa
    @OmegaMussa หลายเดือนก่อน +1

    Phatumbopanu nonse kumeneko

  • @TroubleMuthala
    @TroubleMuthala หลายเดือนก่อน

    Tambala atipha uyu atimaliza

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d หลายเดือนก่อน

    Tsono ka musiki kakubhowa

  • @SteviePatrick-g2p
    @SteviePatrick-g2p หลายเดือนก่อน

    Waitanisa mankhwala ndindan

  • @FadweckLifa
    @FadweckLifa หลายเดือนก่อน

  • @user-vw7tj2ss3l
    @user-vw7tj2ss3l หลายเดือนก่อน

    Yomweyo. Galu iwe

  • @user-mv1ho9pp7o
    @user-mv1ho9pp7o หลายเดือนก่อน

    Komatu boma ili lititha tonse ndithu nanga mankhwala alowa bwanji dziko la malawi ndiyekut chakwela wapanga dala cholinga akhale yekha.

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju หลายเดือนก่อน

    Cholinga achepetse chiwelengero chozabvuta chaka cha mawa.......wagwa nayo chikangawa

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju หลายเดือนก่อน

    Sioneka ndalama imeneyi

  • @JanaMdala
    @JanaMdala หลายเดือนก่อน

    Kwayipa kwathu ku MW

  • @FadweckLifa
    @FadweckLifa หลายเดือนก่อน

    Atipha.

  • @user-ti9yk4eg2l
    @user-ti9yk4eg2l หลายเดือนก่อน

    Zovutatu

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน

    🙄

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w หลายเดือนก่อน

    Pankholo panu nonse agalu