Komatu think twice ali ndi mwai kuti samagwidwa , koma atantenga a police kuti akapelereke umboni pa zomwe amayankhula zija apeleke umboni weni weni okhoza kukhumudwa akukana kuti alibe umboni pa zina zimene amayankhula kwa ife zija koma vuto ndilakuti ali ndi mbali ndie zinazi angoyankhulapo mokwiya koma munthu oimilira osauka sakuenela ku khala ndi mbali any government ngati ikuchita bwino mbali zina ayamikile, mbali zina ngati si nachite bwino aneneso, koma kuti timfuse bon kalindo anena kuti boma ili chabwino ya chita ndi chani, akuyankhani kuti ndi zero kufusa alimpopo FM ayankhaso kuti ndi zero. So apa zongooneselatu kuti ali ndi mbali so if you see this guy's akunena chilungamo mbali zonse akugunda eyetu , but sorry umu ndimmeneso ine ndimazionela , koma ndalemekezaso maganizo ako basi.
Ma Tv station apamalawi amapembedza Boma basi ife kuno timamvera Limpopo FM osatizanuzo zomapembedza Bomalo ayi Brian Banda munanchotsa pa Hot current chifukwa samafuna zachinyengo ayi pajatu ndi m,busa weniweni osati ubusawake opha anthu ayi tikufuna Brian Banda abwelere pa hot current tidzayambanso kuikonda TTv
Tifunsireniko a wonder ndi apankuku expenditure ya maliro anthu 8 kuphatikizapo amene anali vice president Dr SKC, we are still waiting from Government
Pempho kwa ayini ake Chanel itchi zingatheke kuti ma program anu special videos kuti muziika full screen not other side pink then videos izikhala pakati I'm saying this because other people's the got small phone please we love your Chanel
The coming term they will be a world war 2, they will come with more excuses, let chakwera and his tonse alliance and his administration must go, we dont need chirichonse chokwera mdziko lathu
Today's hot current has not been realistic.a pankuku akuwoneka kuti ali bias. Coz analysis umanene the good and the bad But zonse zikuoneka ngati pallibiletu chomwe chachitika. Thats not fair l think Rayana chunga is more analytical than a pankuku.and l have missed him. Chonde timakukondani but you can do better than zomwe analysis yanu ya lero.
Ndalama Ali busy kumapeleka kuma fumu akapita ku state house komanso kumangolemelesana ku mipandoko yeti mzipala mankhwala akusowa ku emigration zinthu sizikuyendako machine sakupedzeka tinene kuti zeru zilipo pamenepo
Nkhani zimenezi ife timazinvesa bwino pa Limpopo FM bakili muludzi TV bon kalindo the DC inu tamalambalalani ndi timambanzi mukumadyato kung'alula kung'alula bas chilungamo chimamasula munthu iya.
I'll feel you guys keep it up osamakhala ndi mbali poyankhula, koma awa a MCP -wa zinawavuta zambili why achakwela luso la usogoleri waziko alibe mwina kumpingo analiko mwina coz enafe kunalibeko. Waonekelatu kuti ali ndi nzimu ongopempha basi waubusa-ubusa eeh okama yowonda kale in the name of Jesus ziko sili ngapite pasogolo
Tangoyankhulai zoona mcp yagosaukisa dziko bisi pa 4 years
Tinasiya kuyikhulupilila Times pano ndi Limpopo fm comred m,'tanyiwa more fire m'tanyiwa
Komatu think twice ali ndi mwai kuti samagwidwa , koma atantenga a police kuti akapelereke umboni pa zomwe amayankhula zija apeleke umboni weni weni okhoza kukhumudwa akukana kuti alibe umboni pa zina zimene amayankhula kwa ife zija koma vuto ndilakuti ali ndi mbali ndie zinazi angoyankhulapo mokwiya koma munthu oimilira osauka sakuenela ku khala ndi mbali any government ngati ikuchita bwino mbali zina ayamikile, mbali zina ngati si nachite bwino aneneso, koma kuti timfuse bon kalindo anena kuti boma ili chabwino ya chita ndi chani, akuyankhani kuti ndi zero kufusa alimpopo FM ayankhaso kuti ndi zero. So apa zongooneselatu kuti ali ndi mbali so if you see this guy's akunena chilungamo mbali zonse akugunda eyetu , but sorry umu ndimmeneso ine ndimazionela , koma ndalemekezaso maganizo ako basi.
Exactly!!!!
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
MCP zaka 4 zomwe apangako ndikupha Chilima basi fiti zawathu💔💔💔💔💔
Prgm lzikhara choncho better pangono lero osamabakira zopoyira bomari lachakwera osapanga zinthu ngt mwadyesedwa Bazi atimes yakhulani chilungamo ziko ndilanu plz
Ma Tv station apamalawi amapembedza Boma basi ife kuno timamvera Limpopo FM osatizanuzo zomapembedza Bomalo ayi Brian Banda munanchotsa pa Hot current chifukwa samafuna zachinyengo ayi pajatu ndi m,busa weniweni osati ubusawake opha anthu ayi tikufuna Brian Banda abwelere pa hot current tidzayambanso kuikonda TTv
Azikhale ngati amakanika kuvala bwino okha .angakhale ndinthawi yowasamala apolice .ali bizy kumanga anthu .sakuziwa kuti nthawi yathera angoona ngati adakali chaka choyamba ....APM more fire🔥💪
Amalawife tinasiya kukumverani kalekale and zimenezo muziziwe from today onwards, inu ndamcp crocodile dance party
Tifunsireniko a wonder ndi apankuku expenditure ya maliro anthu 8 kuphatikizapo amene anali vice president Dr SKC, we are still waiting from Government
Pempho kwa ayini ake Chanel itchi zingatheke kuti ma program anu special videos kuti muziika full screen not other side pink then videos izikhala pakati I'm saying this because other people's the got small phone please we love your Chanel
Koma ife tilila mpaka 2025 September. Osati 21 dys yanu iyo 😭😭😭😭
The coming term they will be a world war 2, they will come with more excuses, let chakwera and his tonse alliance and his administration must go, we dont need chirichonse chokwera mdziko lathu
pankuku ndi wa Mcp chimwendo mene akumangozela amalawi angamve kupepesako sitingamva ayi musaipitse Tv yanu ayi lankhulani point yachilungamo kuti chakwela ndi Mcp yakeyo alephera basi ine ndikuwapatsa 1/10 osati 4/10 ayi watimzunza ife amalawi kwambiri
Palibe chimwe achita away mwina pakuopyseza anthu ndikomwe akwanilitsa kumamanga anthu mudzina lacyber crime
Today's hot current has not been realistic.a pankuku akuwoneka kuti ali bias.
Coz analysis umanene the good and the bad
But zonse zikuoneka ngati pallibiletu chomwe chachitika.
Thats not fair l think Rayana chunga is more analytical than a pankuku.and l have missed him.
Chonde timakukondani but you can do better than zomwe analysis yanu ya lero.
Very useless 😕 😒 😑 ufulu nawo palibe nanu muzinena ndikutha kumanenako chilungamo
Tangonenani zowonga gyz 4 yrs MCP palibe chachitika makape a MCP azipita
Minimum wage is nothing with devaluation 80%😂😂😂😂
0
Imagine mene amavalira nachibuluku zikhale ng'oma muja you think angagamgulire wina nsapato
Apankuku musakhale ngati chawezi Banda ayi Kodi kwatsalaku misewuyo aimalizakodi chakachimodzichi kapena mwadyanawo ndalama zamagazi zikungogawidwa chisawawazi musaipitse TTv ifetimaikonda mukapitiliza tikutumizani Ku mibawa muzikayamikira limodzi ndi chawezi Banda
Nanunso sixoti muziti ayamba, ayamba chani nawe chomwe akupanga ndichani? 😡😡
Apamkuku muli Ku rainbow mumaswa mosaopa NDA Aubrey kusakala koma Ku times mukumaopa chifukwa chani. Amsiska muitaneni kusakala azizaswa
Komano izi amakhala ndi nthawi yomazimvera adindowo kapena tikumanvera ndi kuonera akafa tisiyanji tomwefe
CHAKWERA MMUTUMO OKHA MAMINA 2026 NDIZAMUCHINDA MKAZIWAKO IWEYO UKUONA DIKILA UZAZIWA KUTI KHOBWE SI NYEMBA
Palibe chabwino olo chimodzi hiyaaa osamangoti cyclone anasokonedza ngt anachitapo kanthu
Mwadzya ndalama inu musatipusitse ndinu zitsiru za anthu mukubwera so ngati muyakhula za mzeru zili zopusa zokhazokha
Musawanyengelele agalu amenewa palibe chapanga iwo olo chimodzi koma kupha chilima ndikuba ndalama zamisonkho yathu akagwere afiti amenewo
Awuzeni kuti azipita asadikire masankho a malawi sitikufunanso kumamva za tonse a liance, palibenso chomwe ayamba nanu musamachite mantha poyankhula , chomwe achita ndi kupha chilima ndi ena komaso kumanga anthu, palibenso chanzeru mukuyankhula mukanangosiya tikufuna anthu osaikira boma kumbuyo iyaaaa
Mcp siyinabwelele ku zakodza zinthu koma kwao ndi kuba kupha ndikuwononga. anthuwa amadana ndichilungamo ndanena ndanena
Iwe pankhuku zonse pa mmalawi wakumudzi zilibe ntchito anthu akufuna azidya katatu wosati zomwe ukunenazo
Kunena zoona chakwera chazelu chapanga iye muzaka 4 ndi kupha amalawi bas kugwesa kwacha kuwanamiza ndi kugulisa amalawi ku Israel bas
Mbuli za dyera inu mukuyankhula za mcp kapena tonse muli Malawi momuno inu mbuli zeni zeni limpompo fm mofaya
Sakuyankha mofanana ndimafusoo Ali ndimbali mcp palibe chachitika
Times ndiya mcp Anaigula, bakili muluzi tv is the best ❤ ever
Nkhani ndi limpopo fm not ziwanthu ixixi Zoti zidadya kale ndalamazi😡😡
Ndizimvela program ya Banda ? Wander dzakoyo ndi kape ameneyo wa MCP
Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama
kkk hot hot lero ndemwalakhura zanzeru koma 4/10 mwanama amenewo or 2 sanafike ife a pre wo tinatopa nawo
Mwayamba kulephela kuyamkulatu mukuoneka kuti mwamezatu banzi
You're going to loose more customers if you will not caring.
Hot current wodree umafuna kumenyela a mcp compain
Faka moto. Ndanenandanena!
Andevu zamwai mkunena zoona kumakhala kunena kwaumphawi
😂zikhale wake uti angaone zamavalidwe
I repeat..the score is 4% end of story😅😅😅...I do not apologize to anyone..
Koma ndalama zogula anthu ndi zimene zilipo
Kupepesa kwa chani poti amaziwa chomwe akufuna ndi kupanga, kodi muli mbali iti????
Kodi masiku 21 wolira atha kale ku boma?
Tamva Kale za inu mmalawi akutulukani ngati anzanu aja.
Kkkkkk....a Zikhale ndi stretegist wa Tonse?? and the score is 4%😅😅😅😅... not 40%.
Mmmmm kodi nanu mwayamba utabwanji ??
Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama musatitayise nthawi 17:02
Ndalama Ali busy kumapeleka kuma fumu akapita ku state house komanso kumangolemelesana ku mipandoko yeti mzipala mankhwala akusowa ku emigration zinthu sizikuyendako machine sakupedzeka tinene kuti zeru zilipo pamenepo
A Brian alikuti tisrkeko apa
Talking guys 💪💪
Mau oti ayambapo mumayenera kumayankhula two yrs ago now it's too late kuyamba xitukuko...nthawi Yao yatha kale....soon we are going them OUT
Inu ndizisilu ngt muli nd zilu musiya kupanga ma program chakwela wapanga chani nyani ameney
0. Pa 10😂😂😂😂 miliri ya chani
I lespet blian bamba
BMTV is the best
Bakili Muluzi TV.
jona ndi wa mcp uyuakulephera kuya kha
P
P
Mcp palibe yapanga ky kwa athu odya banzi km kunena chilungamo mowopa mulungu awa zawakanika
Ulemu wanu
Inu ndi angalu kobas mokanene kuli ufulu wake uti
Andevu zamwayi akupatsani ndalamainu a mcp
Dziswe dzimenedzi😢
Lost hope
Musatithelepo bando yathu apaa, ife timamvela limpopo FM with mtanyiwa alongside bakili muluzi tv komanso Borne Kalindo
Nkhani zimenezi ife timazinvesa bwino pa Limpopo FM bakili muludzi TV bon kalindo the DC inu tamalambalalani ndi timambanzi mukumadyato kung'alula kung'alula bas chilungamo chimamasula munthu iya.
I'll feel you guys keep it up osamakhala ndi mbali poyankhula, koma awa a MCP -wa zinawavuta zambili why achakwela luso la usogoleri waziko alibe mwina kumpingo analiko mwina coz enafe kunalibeko. Waonekelatu kuti ali ndi nzimu ongopempha basi waubusa-ubusa eeh okama yowonda kale in the name of Jesus ziko sili ngapite pasogolo
Palibe chomwe angapange awoo
Munasiyilanji kwagwanji wakasabola uja lachinayi sanakuopsezani amcp
Cakwera canzeru comwe ampanga mudzaka four ndi kupha chilima imfa zosaneneka
Limpopo FM omwe timamvera imatiuuza zoona!!! Inudi aaaa mwanyambititsidwaaaaa
KUSWAKUSWA,kugagadakuhagada 👍
Kukhapa Kukhapa kkkkkkkkkk.
Mumasiya pati kuzuzula zithu ngati zimenezi muli bho
Jona ndiwe wa mcp kupepetsa kwa chani
Wali kuchitako Mzimba Bridge,
Chakwera must go.
Lelotu Bola azimvere okha 😂😂
Bola lelo Times mwakambako zolongosoka.
Nde mwati zikhale chani kkkkk
Np
kkkkk