Zitsiru ndi azibusawo, povomeleza ma instructions akupelekwdwao. Kumeneko ndikupembeza munthu osati mulungu ayi. Ndiye kuti m' awa ku tchalichi kumeneko mulungu wao akhala Chakwera. Koma dziwani kuti nzimu wa mulungu ukangochoka mawa lino pa tchalichi chimenechi, basi subwelelanso chifukwa mulungu sangamapikisane ndi munthu. U can only serve one Master.
Mizimu yalusa mpingo wa CCAP ndi wake osapita ku Assemblers of God kwawoko bwanji chitsiru cha president wayaluka basi galu ameneyu dzikoli lamalawi lamuchepera akubisala mbatata nsana ukuonekera mumva kuwawa bwana😂😂😂😂😂😂
Ndpu wasiyilanji kupita ku church kwake kt akamuchose ma demons amene Ali naye..walowa chiwewe sanati, kupha mnzake ngati garu anthu angamukonde chitsiru Cha munthu
Monga ine wa ccap woopa Mulungu mulendo sangandiuze zochita pa khomo panga. Iyeyo ali ndi church lake ndikumene skapange zimenezo. And iyeyo si Mulungu wa ccap Mulungu wa ccap ali kumwamba asatenge ulamuliro waluchipani kwake kapena wakuboma or waku church kwa iye ndikubwera nawo mumupingo wathu ayi mupingo umayendesedwa ndi malamulo a Mulungu. Ndiye a tsogoleri athu a ccap musalole zimenezo opani Mulungu. Osaseka pa khomo aliyese phone asazimise ndindani iye akuyesa amaposa Mulungu wamambwa kodi? Ngati ali ndizifukwa ndi anthu ena asabwere ku mupingo wathu please ziko opani Mulungu wosati olengedwa
😂😂😂😂 wayamba ndiye kukhala ndi udindo waukulu?? Zinachitikapo kt zimenez ngt ndi udindo mku politics konko not kumpingo, mulendo safika mkulamulira eni khomo achuruka nzeru mpingo umaendesedwa ndi malamulo a Mulungu not a politics
Aaaaaaaa nde zichani zimenezi? Zinayamba zachitika liti, nde zodabwitsa tu akufuna adzagawe ndlama paja ali nazo zogawatu koma chonsecho mankhwala mzipatala mulibe shame
Be careful people of God,something will be happen there take care
Chakwera anapha president wa assembles of god musazapite ndi chigawenga ichi ndi kale anayamba kupha anthu
Oipa athawa yekha,afuna agawe ndalama ameneyo komatu ndalama zimenezo tizitafunadi koma vote ndiye ndi ija munakakwilira ku nsipe ija,sitikusinthaso chiganizo,pitani akhristu mukamuonere pafupi wakuphayo.
Musadzapiteko nonse!
Mapwala Ake ameneyo
Zitsiru ndi azibusawo, povomeleza ma instructions akupelekwdwao. Kumeneko ndikupembeza munthu osati mulungu ayi. Ndiye kuti m' awa ku tchalichi kumeneko mulungu wao akhala Chakwera. Koma dziwani kuti nzimu wa mulungu ukangochoka mawa lino pa tchalichi chimenechi, basi subwelelanso chifukwa mulungu sangamapikisane ndi munthu. U can only serve one Master.
Aaaaaaaah! Uchimo wamela mphondo Chakwera, bwanji osapemphera kunyumba kwake komweko ndi security yakeyo. Chitsilu cha President.
Chimo limadzuza olo anapeleka yesu uja anazipha yekha uyu siyeni azaseke ziseko zotse inu musade khawa koma lizasala khomo limodzi la mulungu sazakwanisa kuseka khomo limenelo ndilimene lili loopsa kwambili azisamala popanga zithu
Mizimu yalusa mpingo wa CCAP ndi wake osapita ku Assemblers of God kwawoko bwanji chitsiru cha president wayaluka basi galu ameneyu dzikoli lamalawi lamuchepera akubisala mbatata nsana ukuonekera mumva kuwawa bwana😂😂😂😂😂😂
Azimagililatu ameneyi ndikilani muzandinkhululupilila
Chakwela the life of Malawian matters alot
Chakwera ndiwe galu kwabasi, tapitani ku mpingo wanu mwayamba kusokeratu, inu mumkaona ngati mwakhoza kupha chilima hahaha chilima uja sanafe alipo, olo munamupha koma anthu sitikukufunani🎉🎉🎉
Iyai auzeni kut asabwele church si chao apite Ku church kwao
Church ndichanu osawopa osatopa osafooka vuto asogoleliso aku church dyela
Ndagwilizananawe
Osapita ku assembles koo bwaa mesa ndikumene anachokera musamulore akuphani galu yoooo
Muletseni ameneyo ndi nyumba ya mulungu siyoseweletsa mulendo sapelela lamulo pa nyumba yaweni
Bas nonse mumapemphela kumeneko muzakhale osaptakonso akhaleko ndi zikhalenhoma wakeyo
Akuona ngati nayenso azathilidwa poison? Kkkkk
Koma Mahule enawa paja muli mtundu uliwonse wa tchimo eti bodza momwemo eeee
mmene wanenera comrade mtanyiwa... kut musazapiteko. Azapemphere ndi azibusa awoo.. Ku Limpopo yafika kale kkkkkkkkkkkk
Mingo suikilidwa malire
Pita Kaye ukamine usatipangitse nseru
Malamuro awusatana basi kkkkk
Koma ichi nditsilu kobasi amazitenga ngati ndani 😢
Kkkkk kodi chimenechi chikufuna chani kweni kweni
Osapitako kumeneko something will happen there osalola zimenezo
Vuto ndiazibusawo Adya zambili
Komatu galu iwe president wamanyi usatizolowere ndikupha kwakoko
all the best mr president God help you
Zikomo kwambiri madam taziwa n busa ameneyo ndi street wasatanic azingopita kumeneko kuli nzake akubisalawo koma muvumbuluka tikuziwani ponpano Nzimu wachilima ukumuzuza uona sizinati akanakhala kuti alibe ndalama bwezi tikuti wayamba misala poti wandalama akuti Ali pamwamba palamulo keep it up sister 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
Ndpu wasiyilanji kupita ku church kwake kt akamuchose ma demons amene Ali naye..walowa chiwewe sanati, kupha mnzake ngati garu anthu angamukonde chitsiru Cha munthu
Osapitako akhristu akapemphere ndi abusa,mayi oyendela komanso akazawo aabusa kkkk abwere kuno ku MAKATA CCAP izamuimbile chitsitsimutso mutu wanyimbo CHIFUNGA
Osapita kumeneko amalawi chikumbutima chimupha oyo
Nde mapephero ake abwanji amenewo
Mulendo kubwera ndikalumo kakutwa
Chakwera ndi satana kwabasi
Kkkkkkkkkkkk azakupa inu eeeeeeeeeeeee mavuto😅😅😅😅😅
Mukapemphelele pakhomo osapitako
Chikangawa chakwera sunakhuthe nyama za anthu.
Khalani tchelu mamembala nonse olo kakhaleni kunyumba nose akapemphere yekha galuyo
Mukanamukanira Galu wachiwewe uyu
Mama musapiteko kuntchalichiko tiponyako bombaa kumeneko😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂 wa satanic wasowa mtendele mzimu wa chilima ukumusausa wanya uona machende ako
Chilipo chachikulu kukapanga kumeneko, pajatu muthu akalowedwa ziwanda amavuta mmm
Abusa akazapora manyii .asazatyrukeso mmmmm
Musapiteko akakhaleko ndi ndunazakezo bass
Chimo kuzunza kupha anzako ukuyesa suzafa , anthu ayeza usogoleri wako chakwera walephera
Wafa wafa imeneyo
Palibe chimene mwalakhula chazeru mayi, zingowonetsa kuti inuso mulibe zimu wachidziwitso kapena kuti inuso ndale zidakuwonongani.
Kma chakwera akuzioona ndithu 😂😂
Nde mwati ndan ameneyui 😂
Musapiteko apiteko ekha
Apenga mkuluyitu ndikuti ndikaona,,mizimu yakwiya ya a Malawi.
Galu ameneyu alesedwe asapiteko malamulo akapereke ku mpingo wKe kuja anaphako yemwe adamupeza eeee wooipa uyu asogolleri a mcp 3/4 owoneka obadwa mopotoka nkhope komanso ndi mitima yomwe alephera amenewo
😂Kumpanjeeko nkoonkoma kwambili
Chakwera Chikangawa Congress party
Musamale naye ameneo mumusiye apiteko yekha zake ndi zakumidima kkkk ati galu ameneu kkkkk koma chikangawa eish
Fiti fiti ndithu
😂😂 anthu a mcp ndi iyaluka manyazi ndi umunthu alibe Inu pitani mungoima papemphelo lomanga zoipa zakezo ndalamazo agawe ndithu voti ili muntima aziwona 2025 ameneyo
Abale imvani ichi samalani, mukapusa ndi ma church mutha nonse, Musapiteko please amalawi
Komatu mulindi time
Mmmmmmm koma inu
Mumuuze Chakwerayo kuti ndi mbuzi ya ma president yoti sitinakhalepo nayo kumalawi kuno ndiponso siyizapezekaso
A Malawi ndinu dzitsiru, mumafuna president OTAN i?mumafuna president adzikuseserani m'makomo kapena adzikuvulilani Kodi?
Ndalama idyani
Aaaa zavuta ku mpanda basi
Monga ine wa ccap woopa Mulungu mulendo sangandiuze zochita pa khomo panga. Iyeyo ali ndi church lake ndikumene skapange zimenezo. And iyeyo si Mulungu wa ccap Mulungu wa ccap ali kumwamba asatenge ulamuliro waluchipani kwake kapena wakuboma or waku church kwa iye ndikubwera nawo mumupingo wathu ayi mupingo umayendesedwa ndi malamulo a Mulungu. Ndiye a tsogoleri athu a ccap musalole zimenezo opani Mulungu. Osaseka pa khomo aliyese phone asazimise ndindani iye akuyesa amaposa Mulungu wamambwa kodi? Ngati ali ndizifukwa ndi anthu ena asabwere ku mupingo wathu please ziko opani Mulungu wosati olengedwa
Chakwela nd galu ameneyoo kwabasi
Msayiwale kt munthu ochimwa amakhala ndi mantha chifukwa samayenda ndi Yesu... Nde chichakwera ndicha satanic ndipake kukhala ndi mantha.
Mayi pitani mukagone mwadwala chifine.
Kod ndi mulungu ameneyu KAPENA 😢😢
Apenga misala ameneyo zimu wachilima ndi abale anthu Ena aja wina Anya awo a chitsilu cha president
Inuyo musapite ku church ko mukapatsa anthu chimfine
Machende ake
Vuto inuyo simuli molalika uthenga. Muli mowona matchimo amunthu. Kusowa choyankhula inu. Kwanuko kukabwela alendo wopemphela simulankhula pano mukulengeza pamenepo simukuziwa kut uyu ali ndi udindo wa ukulu. Nanga mumene mungalandilile mwana wa bale wanu ndi abusa akumpingo malandilidwe ake angafanane
😂😂😂😂 wayamba ndiye kukhala ndi udindo waukulu?? Zinachitikapo kt zimenez ngt ndi udindo mku politics konko not kumpingo, mulendo safika mkulamulira eni khomo achuruka nzeru mpingo umaendesedwa ndi malamulo a Mulungu not a politics
Mwayankhula bwino koma mwachimwanso potukwana kuti galu ameneyi
Chenjerani akhristu ndi mneneri onyengayo
Musalole a C.C.A.P zausataniki zaozo asakutaiseni yesu
Mukuzawapembeza iwowo
Aaaaaaaa nde zichani zimenezi? Zinayamba zachitika liti, nde zodabwitsa tu akufuna adzagawe ndlama paja ali nazo zogawatu koma chonsecho mankhwala mzipatala mulibe shame
Komatu mutipatsira chimfine.....,😢
Iyeyo ndikandani kodi??
Musamale ampingo akulimbana ndaazibusa poison ameneyo samalani mufa
Osamulola osamunyengerera akuphani satana chikangawa
Hmmm this man called chakwela
Ngati ndi zoona ndye kuti sizapingo ayi
Muziona inu a chalichi sinanga chalichicho ndi chake
Musapiteko
Kd iwowa afika pomadzimva ngati mulungu?ngati akuluakulu avomereze zimenezo onse muwaukire coz sizoona ayi asamalikatu achakwera eti za ubusa zija adazitaya chi khristu anavula akulamulidwa ndi winauja.
Adzapempereko yekha ameneyo
Ok chikangawa titsalandila ndalamaso
Ufiti ,,afuna chani
Akuphelani komweko musamulole ndiopusa akufuna akuphelani mukanizeni akayangane kwina kopemphera
Wamisala Chakwela
Mmmm koma muli busy ndimabodza a Malawi, kodi mkamapeka nkhani zanuzo mumapedzapo chani?? Ine ndimapemphera pompano izozo kulibe, ukudwala mnthu komano busy kunama iiiiiii.
😂😂😂😂 iwe unajomba ku church uli ndi udindo wanji umafuna akuyimbire foni kt udziwe ngt ndiwe secretary
Iweyo nde wabodza musatinamize nkhani yi olo limpmpo yanenso kumapemphera kuti mwana Wa njoka iwe kagwere
Mafoni tinagula na machen amak galu
Asiyeni ma members a church abwere even atachedwa don't stress about that criminal chatsika
Kaya yibwele ya ku ntcheu basi
Zimamina osamina bwanji iwe ngati zakunyasa ungokhala basi ndwe chisilu galu ndiwe ndipo ulibe yesu
😂😂😂
😂😂😂😂. Eeee yabayatu akuulurani ndipo simunati mupenga zenizeni
Chitsiru ndi iweyo mwana Wa njoka 😂😂😂😂😂
komatu guys ziwanda za uyuyu za chikhamu zija zikuchepera, coz chamudimbayi nde wapengeratu apapa
Ku chalichi kwake bwanji osapita kodi iyeyu ndi Mulungu? Wafikapotu Chakwela koma uziwe kuti Mulungu amatsisa mafumu ku mipando ndikakawasiya ku tchire mkumakadya udzu ngati chinyama ask mfumu Nebuchadnezzar
Wadwalamuti wa na mtongo eti
That day will not day for worship God, better to pray at your home.
This is not a leader