AFORD AKUPEPHA UTM KUTI APANGE ALLIANCE- ZOMWE ZAYANKHULIDWA KU NSOKHANO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 25 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 66

  • @RachelDongolosi
    @RachelDongolosi 3 หลายเดือนก่อน +7

    Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 3 หลายเดือนก่อน +3

    MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO

    • @jameshuwanzulu
      @jameshuwanzulu 3 หลายเดือนก่อน

      ubwino wake simukavota nokha

    • @ThokozireLemani
      @ThokozireLemani 3 หลายเดือนก่อน

      Ndilibe lawyer mkanakuyankha

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 3 หลายเดือนก่อน

    Utm udf my vote

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 หลายเดือนก่อน

    That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 3 หลายเดือนก่อน

    Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 3 หลายเดือนก่อน +1

    Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 3 หลายเดือนก่อน +1

    UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance

    • @KikaImran
      @KikaImran 3 หลายเดือนก่อน

      You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies

  • @AishaChibwana-b8o
    @AishaChibwana-b8o 3 หลายเดือนก่อน

    Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤

  • @WatipaCawinga
    @WatipaCawinga 3 หลายเดือนก่อน

    Magufuli wathu kupoto

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 หลายเดือนก่อน

    Bomo ylo ❤

  • @EnnockNdhlovu
    @EnnockNdhlovu 3 หลายเดือนก่อน +1

    I hope if all mupoto must vote for AFORD

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 3 หลายเดือนก่อน

      Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu

  • @PeterPhiri-u7h
    @PeterPhiri-u7h 3 หลายเดือนก่อน

    MuKufuna alliance mukuopa chani

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 3 หลายเดือนก่อน +1

    Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh 3 หลายเดือนก่อน

    Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe

  • @IshmailDukuturu
    @IshmailDukuturu 3 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi iyi Timothy

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 3 หลายเดือนก่อน

    Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 3 หลายเดือนก่อน

    Chihana is my vote

  • @LuwisKaigwaze-gr6cg
    @LuwisKaigwaze-gr6cg 3 หลายเดือนก่อน

    Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford

  • @BestonChagala
    @BestonChagala 3 หลายเดือนก่อน

    Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd 3 หลายเดือนก่อน

    Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 3 หลายเดือนก่อน

    Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja

  • @AlexSilence-p3l
    @AlexSilence-p3l 3 หลายเดือนก่อน

    My vote afod

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 หลายเดือนก่อน

    Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.

  • @jamessoko9480
    @jamessoko9480 3 หลายเดือนก่อน

    Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.

  • @AishaChibwana-b8o
    @AishaChibwana-b8o 3 หลายเดือนก่อน

    Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 3 หลายเดือนก่อน +1

    I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 3 หลายเดือนก่อน

      Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.

  • @johnussenu2848
    @johnussenu2848 3 หลายเดือนก่อน

    Utm and udf boma

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 3 หลายเดือนก่อน

    Join

  • @ntombiunice8637
    @ntombiunice8637 3 หลายเดือนก่อน

    Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera

  • @BestonChagala
    @BestonChagala 3 หลายเดือนก่อน

    Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 3 หลายเดือนก่อน

    Wabodz uyu
    Mumater mukamafun mavot
    Mumakhal ngat anthabwino
    Chilimanso amater
    Chakweranso amater

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h 3 หลายเดือนก่อน

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk

  • @BestonChagala
    @BestonChagala 3 หลายเดือนก่อน

    Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 3 หลายเดือนก่อน

    Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 3 หลายเดือนก่อน

    Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amen 🙏

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 3 หลายเดือนก่อน

    Move

  • @BwanaGD
    @BwanaGD 3 หลายเดือนก่อน

    Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa

  • @EdenLipenga
    @EdenLipenga 3 หลายเดือนก่อน

    Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 3 หลายเดือนก่อน

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @Donnex-gn2sf
    @Donnex-gn2sf 3 หลายเดือนก่อน +2

    Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 3 หลายเดือนก่อน

      Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂

  • @josephgabriel1016
    @josephgabriel1016 3 หลายเดือนก่อน +3

    Timothy sangatinamize for the second time.....

  • @Syakinongwa
    @Syakinongwa 3 หลายเดือนก่อน

    Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 3 หลายเดือนก่อน

    Zimenezo2 zithera konko mwene

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx 3 หลายเดือนก่อน

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP

    • @spargomw
      @spargomw 3 หลายเดือนก่อน

      I agree with you 100%❤❤

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 3 หลายเดือนก่อน

    Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?

    • @petertaulo8014
      @petertaulo8014 3 หลายเดือนก่อน

      Sangawine mark my words

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 3 หลายเดือนก่อน

    Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂

    • @VungaQueen
      @VungaQueen 3 หลายเดือนก่อน

      Kkkk😂😂😂😂😂

  • @MosesNyalugwe-ll8hh
    @MosesNyalugwe-ll8hh 3 หลายเดือนก่อน

    Maloto achumba

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h 3 หลายเดือนก่อน

    Koma chaka chino ziliko ndithu.

  • @emmanuelsambo1158
    @emmanuelsambo1158 3 หลายเดือนก่อน

    It was only SKC

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip 3 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana

  • @TiyesNayuma
    @TiyesNayuma 3 หลายเดือนก่อน

    Chitsilu iweyo you failed as a minister

  • @FranksonKennethChipande
    @FranksonKennethChipande 3 หลายเดือนก่อน

    Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h 3 หลายเดือนก่อน

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx 3 หลายเดือนก่อน

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela