BLACK BOX YA NDEGE IJA AKUTI ILI KU STATE HOUSE TAMVANI ZOMWE AKUNENA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 93

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll หลายเดือนก่อน +10

    😅 Lucifer chakwera , 2025 uzikalamulira ku Maula prison

  • @Mamahashim-xw2bg
    @Mamahashim-xw2bg หลายเดือนก่อน +7

    Ambuye mulungu wowona zapaziko lapasi ndi kumwamba anthu amenewo awonekere poyera ndithu ayaluke wallah😭😭😭💔

    • @BrownMulipaa
      @BrownMulipaa หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkk( mbuzi zawanthu amaona ngat abisala

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน +4

    Fufuzani zonse zibwele poyela, , sakugona Chakwera ndi mizimu , nchifukwa chake wayamba kupemhela lero, wanya.

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 หลายเดือนก่อน +2

    May the souls rest in peace,tisasiye imfa yawo ulele,Malawi tuyeni timenyele nkhondo ufulu wathu,ngati anzathu AK kenya

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np หลายเดือนก่อน +3

    Kumwamba kuli Yehova palibe chobitsika pansi pathambo

  • @FloraRonard
    @FloraRonard หลายเดือนก่อน +2

    Ayi zikomo.Mizimu yawo iwuse ndi mtendere

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja หลายเดือนก่อน +3

    Zobisika zonse zizabwela poyera

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 หลายเดือนก่อน +1

    Mulungu malungu mulungu wanga chonde chonde chonde titandidzeni ife

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz หลายเดือนก่อน +6

    chikangawa party kumwamba kuli mulungu ndithu prison woyeeeeeee😂

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye mwatisiyila mikango

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela you mast go ❤

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r หลายเดือนก่อน

    Zilibwino kuti ili ku state house Ndi kumalo otetezeka kwambili musade nkhawa 😅😅😅😅😂😂

  • @AnthonyMhango-e9q
    @AnthonyMhango-e9q หลายเดือนก่อน +1

    Thanks for let us known watching in Cape town Athlon

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje หลายเดือนก่อน +2

    Ambuye ndiwabwino tiyenazoni

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera he is very wicked man under the sun

  • @DavidJoel-l5q
    @DavidJoel-l5q หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu wabwino masiku omaliza za chinsinsi zizaululika

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp หลายเดือนก่อน +2

    Chakwera akafera kundende 2025 aafune asafune simeneso sitekanditu musawonaso zicomo

  • @KattieKamangirah
    @KattieKamangirah หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo chilungamo chiyende ngati madzi onse amene anatenga gawo pa imfa za anthu amenenewa ambuye awakathe pansi pompano.

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv หลายเดือนก่อน +3

    Mitima itsika pokhapoka chakeraxo afe basi

  • @user-fd2su4ig1f
    @user-fd2su4ig1f หลายเดือนก่อน +2

    Saima nawo

  • @CharityMkandawire-t8u
    @CharityMkandawire-t8u หลายเดือนก่อน +1

    Pa dziko lapansi palibe chinsinsi, nd tikulira ndi amalawi ambiri mulungu akumva ma dandaulo athu

  • @Prekkaq
    @Prekkaq หลายเดือนก่อน

    God keep on blessing chakwera

  • @DevisonHala
    @DevisonHala หลายเดือนก่อน

    Manyazi bwaaaa

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he หลายเดือนก่อน +2

    Ayaluka bas

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg หลายเดือนก่อน

    Oh my God
    Ambuye achite nanu inu nonse mudampha anthu awaaaa palibe chinsinsi padziko la pansi

  • @IssahAluba
    @IssahAluba หลายเดือนก่อน

    Uyuyu chakwerayu murandu ukadziwika bwinobwino akuyenera kukhara Ku perisson

  • @user-px9jd9co3v
    @user-px9jd9co3v หลายเดือนก่อน

    By and by, the truth is being uncovered

  • @elias.m.chunga
    @elias.m.chunga หลายเดือนก่อน +1

    Koma mbuli zinazi... GPS? Imatanthauza chani mwati?? 😅😂😅😂

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂 awuze iweeee

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya หลายเดือนก่อน

      Tifotokozere inu anzerunu

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 หลายเดือนก่อน +1

    Obviously boma la chakwera ndilomwe linapha chilima

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 หลายเดือนก่อน

      Iwe udalipo?

    • @cassimyusuf6683
      @cassimyusuf6683 หลายเดือนก่อน

      Ayi, koma iweyo ndi a MCP amzakowo.

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Inuso ndinu achisilu mulindiumboni ​@@cassimyusuf6683

  • @HoseKatsekera
    @HoseKatsekera หลายเดือนก่อน

    mulungu ndiwachifundo, ziwululika

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i หลายเดือนก่อน

    Mulungu alipo ndipo ifa ya chilima ndiathu ena 8 ziziwika kuti anafa bwanji

  • @Prekkaq
    @Prekkaq หลายเดือนก่อน

    MCP boma tikayivotelabe

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera sapuma ndi maliro amenewa, adzazimangilila ameneyu.

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz หลายเดือนก่อน

    Wanya basi galu ameneyi chakwela

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 หลายเดือนก่อน +1

    Alibe manyazi ayima

  • @JasonMailos
    @JasonMailos หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela ndiwakupha

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 หลายเดือนก่อน +4

    Mundege munali zigawenga Ambuye tiyankhulen

    • @eunicesaiti
      @eunicesaiti หลายเดือนก่อน +1

      😢😢😢😢😢😢😢

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 หลายเดือนก่อน

      Iyeyu adakwera nawo ndegeyo ndi zigawengazo?

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 หลายเดือนก่อน +1

      Inenso ndikuti, Uyu agwidwa posachedwa, pakuti Mulungu adzaulula chilichonse kuphatikiza uyu akudzitcha mboni yu.

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 หลายเดือนก่อน

      @@philemontitusnkhoma7740 angakwere nawo akudziwa kut ndege yo waitchera? Mtsogoleri wathu ndi chigawenga chachikuru. Koma mulungu simunthu. Mzimu wa chilima suzagona mpaka chilombochi chitalangika.. He will never know peace in this world

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q หลายเดือนก่อน

    Apodi ndekt anthu amenewa anali mudege mommo

  • @Jerry-vm6mo
    @Jerry-vm6mo หลายเดือนก่อน

    Guys olo munene zotani mzanu chilima anapita inuyo muli Moyo nde bola mugosiya nkhani Yii coz palibe chomwe chingatike nde musatinyase so chilima anapita basi zikomo

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Srs ndipo or ayankhule motani kunatha uja basi lasala ndi tsiku lachiukitso ndinthawi yokoza mitima yathu osati mabozawa atichimwisa ulele ndithu anthuwa mumutu mwawo kaya muyenda chani

  • @michaelamon9691
    @michaelamon9691 หลายเดือนก่อน +2

    Koma yaaa, papa muli NDI bodza

    • @petertaulo8014
      @petertaulo8014 หลายเดือนก่อน +1

      Iwe ndiye kape kwambili, nkhani yoti ilipalipose.

    • @MercyChimaliro-fi6mv
      @MercyChimaliro-fi6mv หลายเดือนก่อน +1

      Ngati ndi bodza ndiye iweyo tiwuze chilungamo chako.

    • @Jasper-xk9iv
      @Jasper-xk9iv หลายเดือนก่อน +1

      @@michaelamon9691 iwe macende ako ife zikutiwawatu timufuna chilima

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +2

      Muthu uyu amakonda kuikila kumbuyo chakwela thawi zose mungutu adzakulangani kwambili chifukwa ifa zimenezija aliyese m,pakana panopa samavetsetse muyaluka mwasala pang,ono

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d หลายเดือนก่อน

      @@petertaulo8014pamtumbo pamako galu iwe, iweyo panga wekha GPS uikepo number ya ndege ija ikupatsa option ya black box nde ufufuze uwone Komwe kuli black box galu iwe

  • @solomonlapson
    @solomonlapson หลายเดือนก่อน

    Kodi ndindani ameneyu akulankhulayi,, and channel yake ndi yanji

    • @user-lp8wj3vq4x
      @user-lp8wj3vq4x หลายเดือนก่อน

      Ukufuna mukamupheso anthu amcp inu. Manyazi bwa

  • @patrickscott9086
    @patrickscott9086 หลายเดือนก่อน

    Km ndye kuli kuyesesa kut chilungamo chisawoneke km Only God knows

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga หลายเดือนก่อน

    mbuli zazikulu ndinuyo kulongolora kwanuko mukuwapasa mapulani kuti akataye blac box mmadzi kupusa basi kamene mwva kukamwa mbwembwembwe kharani chete afufuze chomwe cili mkati mwa black box

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkk sayimanso ndithu

  • @SandreckBezai
    @SandreckBezai หลายเดือนก่อน

    Iwe ndiopusa udzazindkil okay

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s หลายเดือนก่อน +2

    Pangani mulimose ife tikufuna zenizeni zibwele poyela

  • @lillynhlema9656
    @lillynhlema9656 หลายเดือนก่อน

    Ku statehouse yikutqniko

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b หลายเดือนก่อน

    Chakwela you're evil evil

  • @philemontitusnkhoma7740
    @philemontitusnkhoma7740 หลายเดือนก่อน

    Galu iwe usaoutsitse a Malawi. Kodi enanu mukungoti ndondondo kwa atolankhani abodza awa moti simudadzukebe kuti uyu angifuna kuononga Malawi? Iweyo umati Achakwera asiye blackbox kuthengo komweko mpaka lero? Amalawi dzukani. Sukusulani. Uyu apezeka posachedwa. Mwana wa mfiti

    • @user-qn9vc8em6z
      @user-qn9vc8em6z หลายเดือนก่อน

      Kagwere uko akutma et? Tisiye ife ndipo tidakamverabe untill 2025 woooooo ku chonguuuuu

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel หลายเดือนก่อน

    Komano minthu akadziwa chilungamo samakhara ndimantha gyz

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa หลายเดือนก่อน

    Inu mkususanu kuti ndizonama tatiuzeni black box yilikuti mitumbo yamanu

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Ubwino wake amako alibe sorry for that 😂

  • @Prekkaq
    @Prekkaq หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 mcp ikukuvetsani kuwawa

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Ndipo akusehula nayo mumimba 😅😅😅

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali หลายเดือนก่อน

    Ayaluka basi chakwera

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Kkkk munayamba liti nanu apa nthawi yamalilo mumati poyika chilima chakwera nayeso agone apa kuti mukuwona ngati moyo wachakwera uli mumanja mwanu timvomeleze imfa iliko aliyese adzafa ndindani angamulese mulungu zofuna zake

  • @BenedictChikaoneka
    @BenedictChikaoneka หลายเดือนก่อน

    Mudzakhumudwatu report litatchula zosiyana ndimaganizo anu.Chakwera ine Ndikuona kut Ali innocent sure.

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      Ndipo srs akungotekeseka nwini wake aliphee akudziwa choonadi

  • @EdnaChiumia-h4d
    @EdnaChiumia-h4d หลายเดือนก่อน +2

    Trading Lie's.... Nawe kumwamba sukalowa....let the truth revealed first b4 judging any one

  • @FrankBaison
    @FrankBaison หลายเดือนก่อน

    Chakwera amangidwe

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel หลายเดือนก่อน

    Kut gyz social media simunayizolowelembe stt house yakut?

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d หลายเดือนก่อน

      Panyopa pako iwe ndi Chakwera wakoyo munyera muona simunati

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน

      ​@@Musa1828-l5dkkkkk koma ndiye muli srs tuuu nganti amako alibe

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q หลายเดือนก่อน

    Mulungu yekha ndi amene akudziwa koma chilungamo chidziwika