Mumanga Anthu Angati? - Samuel Lwara

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 22 ส.ค. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara asks how many social media commentators the Malawi Government will arrest. He is saying this after Honorable Minister of Information Moses Kumkuyu said they are after the administrators of the TH-cam channel Bakili Muluzi TV.
    Pa Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara afunsa kuti Boma la Malawi limanga anthu angati pa social media. Akunena izi nduna yolemekezeka Moses Kumkuyu atanena kuti akutsata ma administrator a kanema wa TH-cam Bakili Muluzi TV.

ความคิดเห็น • 73

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 3 หลายเดือนก่อน +5

    Yes we enjoy with bakili muluzi t v

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 3 หลายเดือนก่อน +5

    Nice talk munthu amene uja sakulakwisa

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 3 หลายเดือนก่อน +2

    Bakili muluzi channel always for the truth even not only malawi histories we listen from other countries stories y don't blame him too so y only chakwela government this government must be evil guys sitingapempheze mafano just because u are in power

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 3 หลายเดือนก่อน

      Awuzen kut iwo si Mulungu.Anthu anakana kalero kupembedza Farawo amene samapita Ku toilet mpaka amazitcha kut ndi Mulungu

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka7486 3 หลายเดือนก่อน +1

    Very good...Mulungu Ali pamodz ndi anthu olankhula zoona ..olemekeza Iye ngkhale sakumuona .Palibe chimene mtolankhaniyu amalakwitsa .Amalankhula chilungamo ndipo Ife amalawi eni ndimboni chifukwa zikuchitikadi

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi 3 หลายเดือนก่อน

    Bakili muluzi TV TH-cam channel Never get arrested here we love this channel 🇲🇼🇲🇼🇲🇼✊️✊️✊️✊️✊️✊️

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 3 หลายเดือนก่อน +2

    Malawi aliyense okhala kunoko sangadzunguzidweyi ndi munthu aliyense waku Malawi, kuno ndi dziko loopsa tizatchuta ndimifuti anthu akewo abwelera mitembo yokhayokha wait n c ndipo ife tonse kunoko sitilora imeneyo ndi nkhondo

  • @user-qu9iu7hs8k
    @user-qu9iu7hs8k 3 หลายเดือนก่อน +2

    I agree Malawi muphesa ma saidi kuno kur mifuti atha kuphedwa tyen nazo

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g 3 หลายเดือนก่อน

    Bakili Muluzi tv journalist is the best journalist in malawi please don't arrest him guys,,what wrong has he done for that.

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 3 หลายเดือนก่อน +1

    A CID Amenewo Aombeledwa Ku South Africa kuno,
    Kuno Sikumalawi

  • @ANTHONY-cq3up
    @ANTHONY-cq3up 3 หลายเดือนก่อน

    True the guy is very genius and we like him..
    Kunkuyu ndi mbuzi ya munthu

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 3 หลายเดือนก่อน

    Powerful message and well spoken my brother.

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ku South Africa aphetsa onsewo ayerekeze sakudziwayi south Africa amenewo

  • @JoyMphika
    @JoyMphika 3 หลายเดือนก่อน +2

    Akungofuna kuphetsa ana aeni ake

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 หลายเดือนก่อน

    Amene akuwatumizawo adziwika ndipo kukhala kusakana wina pa mdima wina powala awine ndani asamale kwambiri Jones simaseka

  • @user-ev4or2kg4z
    @user-ev4or2kg4z 3 หลายเดือนก่อน

    Bakili Muluzi TV ndiyabwino kwambiri please andinu zigqirani ntchito zina olo fasani kupanga Kaplan obera

  • @ScrarNation
    @ScrarNation 3 หลายเดือนก่อน

    Bakili muluzi tv is the best

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 3 หลายเดือนก่อน

    Good message Bakili Tv is good

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu 3 หลายเดือนก่อน

    A kukuyu aphesa anthu a ena ake sakuiziwa south Africa funso mkumati muzikamusaka pati munthuyo? waste of resources mulekeni munthu ife we love him and he is protected by the blood of Jesus

  • @jennyx6914
    @jennyx6914 3 หลายเดือนก่อน

    nzomvetsa chisoni kunkuyu ithink magazi awiltika akumuzunguza mutu serious here in RSA chili chonse chimachitika chimene ukufuna ndiye ngati bakili tv akufuna amugwira kufuna kwake koma its not easy ngati ulube mfuti kuno R200 yeni yeni umagula anthu opha anthu so idont know bt may Hid protect bakili guy he is he atrue guy

  • @MajotiMpandasoni
    @MajotiMpandasoni 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ayambe kumanga ntambo iwowonso analowa mboma kamba ka mademo anapha anthu anawononga katundu mabusines awanthu mamilion awanthu kupha wapolice apolice kugwililidwa lero mukukana kuzuzulidwa zoona??

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 3 หลายเดือนก่อน +1

    ine kupanda Bakili muluzi channel sindingakwanitse🤣🤣🤣🤣

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 3 หลายเดือนก่อน

    You have spoken well bro, tell them

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 3 หลายเดือนก่อน

    Kukhuyu sanapuzire

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 3 หลายเดือนก่อน +2

    Dziko lomvesa chison

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c 3 หลายเดือนก่อน

    Very much appreciate nice one

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 3 หลายเดือนก่อน

    Awuuzen akuona ngat kuno south Africa kosewera afako kumeneko
    Ndipo bakili muluzi TV samukwanisa

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi mesa naye ali ndi mulandu wakupha alani wititika athu anu ndi aja akukhapa athu koma bwanji osawamanga

  • @MosesWitness
    @MosesWitness 3 หลายเดือนก่อน

    Muwabwelese tiwaponye mumigodi yakale

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo Kuno athu samawelenga Moyo wamuthu amaopa kupha zinyama ndani amenewo akhutawo abwele aziona mukamangovomela Zina zilinzonse chifukwa chandalama muzipwetekesa Ngati mwakhuta bwelani

  • @Jermah51kennias
    @Jermah51kennias 3 หลายเดือนก่อน

    We love BM TV

  • @user-po6ir6eh4z
    @user-po6ir6eh4z 3 หลายเดือนก่อน +1

    Samukwanisa ngat akumulephera Bon kalindo

  • @morgansilungwe
    @morgansilungwe 3 หลายเดือนก่อน

    its not bakili muluzi tv but bakili tv dont mix the two.bakili ndi dzina la wina aliyense ..

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 3 หลายเดือนก่อน

    Apita ku holiday amenewo sangamupeze BKtv.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 หลายเดือนก่อน

    Aaaa koma MCP ulamulilo wachikale dzedi malo molimbana ndimamvuto anthu kumawononga ndalama akasake anthu ku south Africa bakili maluzi tv ndumunthu emwe amanena chilungamo kwa amalawi nde mukufuna ulamulilo wachipani chimodzi uja tinaukana kale kale uchisilu wa MCP nde umenewo amagadzi manja

  • @user-hm1ys8vd4i
    @user-hm1ys8vd4i 3 หลายเดือนก่อน

    Mwauuze ngati amaukonda moyo asabwele kuno sikumalawi ayi

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp 3 หลายเดือนก่อน

    mzimu wa witika ukumudzunza ameneyo

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 3 หลายเดือนก่อน

    Tayesani kutumiza joz athuo tawaonese

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 3 หลายเดือนก่อน

    Abwere ndipo agwilira patipo ma said awowo azimve kunukha magazi ndipo afaaa muphesa anthu inu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 3 หลายเดือนก่อน

    Chalwera sakuziwa chimene akupanga ....kuononga misonkho ya anthu chifukwa chosaka munthu ... .kunkuyunso ndiye chisilu cha munthu .....tikuonelani ili ndi ziko ....anthutu akuvutika mmalawi muno ndipo anthu mukuwasakawo akunena zoona.

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 3 หลายเดือนก่อน

    Ife Kuno ku keep town tikuti atume athu awo tiwone Ngati abwelele ndi Moyo Ngati mumangova E k 47 tili nazo Kuno tikupan nose

  • @chimwemwecrispo200
    @chimwemwecrispo200 3 หลายเดือนก่อน

    Masi ID amenewo kuno tiwapha khalan pheeee muva

  • @user-rn7wv8ze3v
    @user-rn7wv8ze3v 3 หลายเดือนก่อน

    Matipate yantha ku Malawi chifukwa Cha MCP Chakwera

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v 3 หลายเดือนก่อน

    Kunkuyu adapha Witika bwanji sakumangidwa machende amako Kunkuyu pamodzi ndi Chakwera wakoyo

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 3 หลายเดือนก่อน

    Well spoken💔💔

  • @user-ld1js7dt3b
    @user-ld1js7dt3b 3 หลายเดือนก่อน

    Ndiposangamupeze

  • @dytonmoyo4629
    @dytonmoyo4629 3 หลายเดือนก่อน

    🔥🔥🔥🔥

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 3 หลายเดือนก่อน

    Mizimu ya anthu ikuzunzika chifukwa cha boma limeneli koma dziwani kuti Mulungu akuwona la 40 limakwana

  • @user-po6ir6eh4z
    @user-po6ir6eh4z 3 หลายเดือนก่อน

    Kudana ndi chilungamo mcp paja ntchito yao ndi nkhaza ndi kupha anthu

  • @EuniceLipenga
    @EuniceLipenga 3 หลายเดือนก่อน

    Ulumu wanu munthu wamkuluyu amenewo mawu ngati aliakumva amve

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 3 หลายเดือนก่อน

    Iwowoso akhala akusakidwa

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 3 หลายเดือนก่อน

    Kumkuyu wamba zomwe ayakhula mr ngati uli mdi mutu ndi nzeru wadzimbera wekha

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 3 หลายเดือนก่อน

    Kumkuyu ndi chisiru ndipo alibe nzeru ndi ndzukwa palibe comwe amadziwa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 3 หลายเดือนก่อน

    A kunkuyu asowa zochita, ndipo Ruwala akuneba chilungamo chokha chokha

  • @user-ib7ig3xd2h
    @user-ib7ig3xd2h 3 หลายเดือนก่อน

    Apatu mwalankhula zanzeru atsibwen

  • @user-um6yo6nc3e
    @user-um6yo6nc3e 3 หลายเดือนก่อน

    Mposo Kunkuyu waganiza bwanji kutumiza ma detective ku dziko Loopya ngati ili?

  • @Jacksonmuhackeya
    @Jacksonmuhackeya 3 หลายเดือนก่อน

    Chili chonse chili ndi mathelo tiziona tizimva

  • @AndrewBwanali
    @AndrewBwanali 3 หลายเดือนก่อน

    R10 is much

  • @OweniMalokooweni
    @OweniMalokooweni 3 หลายเดือนก่อน

    That man is staying America not South Africa

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 3 หลายเดือนก่อน

    Adapha witika bwanji iye samangidwa mkukuyuyo? Utsigoleri wawo wa mcp wokupha,wokuba ,wakhaza. Amangidwapo angat akukhalira kukhululukira anthu okuba ma billion pomwe okuba chimanga ndinjala akudzuzika kundende , ineyo utsogoleri wa chakwera sikusiyanisat ndi wa mfumu nebukatineza dzanja lalemba pakhoma kasalako alotesedwa ndipo boni kalindo azapepha kuti atathauzire maloto awo owopsawo ,chifukwa akuzikwezat afikapo pomwera zikho zayehova tikuonetani

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 3 หลายเดือนก่อน

      Nenani chilungamo musakidwa nkuphedwa

  • @KereeditseMotsetse
    @KereeditseMotsetse 2 หลายเดือนก่อน

    Machendache kukuyuyo

  • @partmaulidiPatrick
    @partmaulidiPatrick 3 หลายเดือนก่อน

    nkani ndiyoona kunodi kulianthu athuro

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 หลายเดือนก่อน

    Boma lathu

  • @ManganiStanley
    @ManganiStanley 3 หลายเดือนก่อน

    anthu opusa awa

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 3 หลายเดือนก่อน

    Abwere agalu ameno tipha konkuno mkukuyu chakwela pamtumbo panu

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 3 หลายเดือนก่อน

    Boma lomvesa chisoni Kwabas mbuli zophunzira

  • @RobertDJambo
    @RobertDJambo 3 หลายเดือนก่อน

    What nonses CID kukamusaka muthu oti sakukudzwa kumenevali kkkkk

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 หลายเดือนก่อน

    A kunkuyu futi yawo inapha munthu bwanji sakumangidwa ndiye akamange munthu ongoyankhula nawonso dzenje umakumbilamo zako nawe so udzagwelamo wokha asiyeni amagwidwa pompano atayeni

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 3 หลายเดือนก่อน

    Mkukuyu anapha munthu paja Galuamangdwa 2025

  • @mkhokholasamuzonda5094
    @mkhokholasamuzonda5094 3 หลายเดือนก่อน

    KUNKUYU panyini pa make

    • @spargomw
      @spargomw 3 หลายเดือนก่อน

      Chitsiru cha munthu Kunkuyu, Waiwala milandu yake yopha Witika, Kumkuyu amfa imfa yowawa kwambiri coz nkhani ya Witika yaululika kut adamupha nd iyeyo