ZOMWE ZACHITIKA KUMENE A MICHAEL USI AYANKHULANSO29 July 2024

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 18 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 246

  • @Prianka567
    @Prianka567 2 หลายเดือนก่อน +8

    May God give you more wisdom Manganya our Vice president, Dont be shaken lots of people are pharisees

  • @GoodsonSame
    @GoodsonSame 2 หลายเดือนก่อน +11

    Iyi inali apayi ndi Group la odyazake alibe mulandu,,palibe wa utm apa.

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 2 หลายเดือนก่อน +14

    Ndichifukwa chake Yesu Khristu atabwela sanalimbane ndi ufumu wa Dziko la pansi iye anangobwela kuzapulumutsa chotaikacho bas...He k ew kut ufumu wa Dziko la pansi ngwa oipayo

  • @InnocentMtafya
    @InnocentMtafya 2 หลายเดือนก่อน

    Utsogoleri wabwino ulimo umu ,, bwana VP, you got it✊✊✊✊✊✌️✌️✌️✌️

  • @KondananiNjakwa
    @KondananiNjakwa 2 หลายเดือนก่อน

    The guy is so wise. Now I know why even President Chakwera did not hesitate appointing him

  • @smallAsima
    @smallAsima 2 หลายเดือนก่อน +3

    Muzithako kupanga zanu komaso kuvomeleza zinthu zikachitika aliyese azamwalila nde musapake ena imfa ya munthu azamwalila nthawi inakwana bas iyi ndinthawi ya Usi mufune musafune

  • @Nya-Jeka
    @Nya-Jeka 2 หลายเดือนก่อน +3

    Osadabwa kuti all this time he never wore UTM uniform….. all of a sudden wakayipeza. Shupiti zako Manganya

  • @JosiahKachali
    @JosiahKachali 2 หลายเดือนก่อน

    Manganya the best man. Keep the vibe

  • @MarvinChilombo.flourish
    @MarvinChilombo.flourish 2 หลายเดือนก่อน +1

    1.kusayankha ma diss it's fearing kut abwera ambiri
    2. Ati nthawi yoyankha alibe koma aziganiza ngongole, kodi akuona ngati wafikapo eti. Apanga mpaka liti?
    5. Lero ndie anaganiza zovala party cloth? Ndie wu betrayer umenewo

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 หลายเดือนก่อน +5

    Suka kamunthu kakupha aka...kamwana ka chikangawa aka😮😮

  • @MemoryMbepula
    @MemoryMbepula 2 หลายเดือนก่อน

    Don't let enermy scatter us. Viva UTM

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 2 หลายเดือนก่อน +3

    Wagwa nayo Usi dziko lakutulukira kale kuti ndiwe wa mcp osokoneza iwe ukuganiza ukawina ku convention

  • @StarchJonas
    @StarchJonas 2 หลายเดือนก่อน

    Tikuferanji at the best level, za drama zenizeni, nanunso oyimba ng'oma kumavina apa mumavinirapo zichani?

  • @PreviousStanley
    @PreviousStanley 2 หลายเดือนก่อน +7

    Chifukwa chani chirima anamunkhulupirila manganya nanga ndichifukwa chani manganya sanachosedwe unduna maulendo onse omwe ankhala akusintha maunduna manganya hi was a trusted person to chirima

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi mukamati chakwera akumakukumbutsa kuti chilima ankati tipangechani kkkkkk seriously manganya bwanji sankamugwilitsa ntchito ngati mmene akupangila iwemo 😢😢😢😢 manganya sudachenjele bwino

    • @lacksonsiyadi943
      @lacksonsiyadi943 2 หลายเดือนก่อน

      Eti eti chilima amangonyozedwa lero zatani manganya bzy bzy chonch chadza ndiyani

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6no 2 หลายเดือนก่อน

    Thank you Mr vice

  • @tblon7441
    @tblon7441 2 หลายเดือนก่อน +3

    VP ndi more fireeee
    Image moto Boma ilo

  • @IshumaerWazakile-u5d
    @IshumaerWazakile-u5d 2 หลายเดือนก่อน

    ndikufuna chisot ndi maglass ndipitilize kupanga masewelo ndi nyimbo ya winiko umandisewelesa

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dr. Chilima had no intentions to quit the alliance? Chilima spent more time in courts with powerless position.... Malawians, learn to use your heads properly in reaction to everything which enters into your heads. God shouldn't be mentioned everywhere brethren because a day is coming. Stay blessed.

  • @JemesMalawa
    @JemesMalawa 2 หลายเดือนก่อน +1

    Palibeso zoti tingakambilane nanu athu okupha inu ngati mukulephela kupeleka ma information yangozi ndiye mukuganiza kuti tingakusekeleleni afiti osekelela 😢😢😢😢😢😢

  • @ayaanchaudhry9370
    @ayaanchaudhry9370 2 หลายเดือนก่อน

    More fire mr vp l love u more , hel

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 2 หลายเดือนก่อน +6

    Zopanda nzeru zomwe akulankhula awa, ngongole kodi aliyese angalandile ? Azimayi mumangoziwa kuyimbira zilizonse ndizopusa zomwe.

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga 2 หลายเดือนก่อน

      Kupusa amalawi eeeeesh 😢😢😢

  • @GladysBanda-h2w
    @GladysBanda-h2w 2 หลายเดือนก่อน

    akutukanani eya mwaonjeza inu aaaaa

  • @DanielPhiri-u5x
    @DanielPhiri-u5x 2 หลายเดือนก่อน

    Yaaaaa coma vice president uyuuu anakonzaa zowonaa

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 2 หลายเดือนก่อน +1

    michael USI ALIBE MFUNDO...NDIPO NDIMA DRAMA ENIENI...PALIBE UTSOGOLERI APA

  • @MzadziWanga
    @MzadziWanga 2 หลายเดือนก่อน +9

    Utm pitani ku conversion zosezo zitha 😢

    • @MandalaChaona
      @MandalaChaona 2 หลายเดือนก่อน

      Thats true Mkumano wa UTM uzathesa zonsezo.

    • @shadreckphiri1799
      @shadreckphiri1799 2 หลายเดือนก่อน

      You are. right

  • @ChanceGondwe
    @ChanceGondwe 2 หลายเดือนก่อน +1

    Manganya ndi khuluku. Posachedwapa mulungu si James. Zomwe Iye amafuna zachitika. Betrayer

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza 2 หลายเดือนก่อน

      Anthu ongoyankhula zopanda umboni.Personal opinion kumaipanga present ngati fact

  • @StevenGJohn
    @StevenGJohn 2 หลายเดือนก่อน +1

    Chisiru ichi chopanda mfundo akukakamira ku MCP coz Cha u vice president ukuonangati a MCP akukuonera kukondwa?

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza 2 หลายเดือนก่อน

      Malemu Chilima anatuluka mu Alliance asanamwalire paja?

  • @francistonysanena5349
    @francistonysanena5349 2 หลายเดือนก่อน

    Ku off camera anagawa ma bwa?😅

  • @LACKSONJULIUS
    @LACKSONJULIUS 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mukhale pa nthuzi mulandire kanganyanse

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy 2 หลายเดือนก่อน

    Only azimayiii km abale tiziona

  • @RaphaelKweve-u5s
    @RaphaelKweve-u5s 2 หลายเดือนก่อน

    Bwana Vp chimwalireni Sck munakumanapo ndi Nec yanu ya Utm ngati mtsogoleri,,,muyenda bwanji ndi alliance kutengera kuti amene anasaina wamwalira?

  • @SabitSamohgruva
    @SabitSamohgruva 2 หลายเดือนก่อน

    Mutifusileko kut Kodi iwowo ngt mtsogoleli wa UTM anayitanitsa ana awo ngt akambilane nawo? Zakutulukako nanga ndizoti UTM ndiyomwe idzakhale patsogolo mu 2025 ngt mwagwilizano wawo?

  • @MikeKanyaza-bm5tp
    @MikeKanyaza-bm5tp 2 หลายเดือนก่อน +2

    Tinalodzedwa ndithu,VP kukhala manganya ,munthu waku Zimbabwe😮😮😮😮😮

  • @PachaloInvestment
    @PachaloInvestment 2 หลายเดือนก่อน

    Come to mcp my friend

  • @francistonysanena5349
    @francistonysanena5349 2 หลายเดือนก่อน +1

    Lero nde mwavala za SKC?😅

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 2 หลายเดือนก่อน +1

    Nose muli kumeneko ndi bambo asikono Mr yudasi tiye uko osakamba za madam mery akulira mwamuna wawo fisi lwe ndi chikangawa anthu okupha analakwachani skc 😢😢😢 manganya lweyo

    • @mwaleronald8325
      @mwaleronald8325 2 หลายเดือนก่อน

      Komatu

    • @SigereAckren
      @SigereAckren 2 หลายเดือนก่อน

      Chikuwalimbikitsa nchiyani kulimbana ndi ngongole mmalo mongogawa ndalamazo akufuna kuwabelanso amphawi

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 หลายเดือนก่อน +2

    Bwanji zomwe ukupanga Bwanji sakamulora chilima kumatero ndi chifukwa utm yeniyeni ukukwiya nawe

  • @YOMALO.
    @YOMALO. 2 หลายเดือนก่อน

    The VP is wise 🎉

  • @Masina515
    @Masina515 2 หลายเดือนก่อน +1

    Awaaa koma? Azimai kutengeka😮

  • @ChrisjuZiyaya
    @ChrisjuZiyaya 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ngati alidi mtsogoleri wa utm bwanji sakupanga push za report ya ngozi ya ndege kuchikangawa kuja ???????????

  • @AboudujanahMawulidi
    @AboudujanahMawulidi 2 หลายเดือนก่อน

    Mzimayi ndiwoyimitsa mutu kwabasi amangoyimbila m'manja zilizotse

  • @edsonphangula5817
    @edsonphangula5817 2 หลายเดือนก่อน +1

    Good speach ndale Zapa internet no good zipani Zina kulemba anthu Kuti aziwapatsa malipilo nchito yake kutukwana mulunga sangakuwiniseni muluzaso

  • @kondwanivyalema9449
    @kondwanivyalema9449 2 หลายเดือนก่อน

    Kamthila kuwiri aka kamunthu kowumila aka kayambise Chipani chake kazafa ngati galu aka

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er 2 หลายเดือนก่อน

    Wamfupiyu mzeru alibe uyu ndiye bambo asikono galu kumtumbo kwako

  • @doublekaizale7903
    @doublekaizale7903 2 หลายเดือนก่อน +1

    Only fools can trust this short man
    Kambelembele uyu

  • @KondwaniMunthali-vf1ws
    @KondwaniMunthali-vf1ws 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mwasoketsa kit ya UTM,,,, KKKKKKK,,, HEEEEDEEEEEE😂😂,,, OCTOBER IS NEAR,,,

  • @swintonchirwa1897
    @swintonchirwa1897 2 หลายเดือนก่อน

    Akufuse ngati ndani? Just wait for convention

  • @NEBERTMVULA
    @NEBERTMVULA 2 หลายเดือนก่อน

    think carefully about this I dont think Saulosi would still be in MCP by this day today

  • @GiftCharlesMuhapala
    @GiftCharlesMuhapala 2 หลายเดือนก่อน +4

    Dr Manga palibe cha nzeru mukunena apa

  • @sandersonmayuni7557
    @sandersonmayuni7557 2 หลายเดือนก่อน +2

    Micheal Usi is a unifying leader regardless of political divide.

  • @JohnFrank-cg1yh
    @JohnFrank-cg1yh 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi Dr manganya Inu ngat msogoleri wachipani Cha Utm mwachitapo Chani kut athu azigwirizana kuchipani Chanu, chifukwa zikuoneka kut mukuyenda nokhatu kuchipaniko akuluakulu onse akukukayikilani mutani,kut athu ayanjane komanso chipani Cha Utm chikhale chaphavu

  • @mkhokholasamuzonda5094
    @mkhokholasamuzonda5094 2 หลายเดือนก่อน

    UYUTU MBOLIYA MAKE AKUPUSITSAI GALU YU

  • @TrustMangando
    @TrustMangando 2 หลายเดือนก่อน

    Aaaaaaaa....iwe sungatputsitse ase......apa pokha wanama bacccccc....Awa wangoveka za UTM...aaaaaaaa ahaaaa!!!!

  • @IshumaerWazakile-u5d
    @IshumaerWazakile-u5d 2 หลายเดือนก่อน

    thiko wa mapoto awir utm and MCP unapha chilima nthiko

  • @AllanChikoti
    @AllanChikoti 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kkkkkkkk
    Ndikamamvera awa ndumasowa chonena zumangondiseketsa

  • @GoodsonSame
    @GoodsonSame 2 หลายเดือนก่อน +1

    Awa si a utm,awa ndi a group yake ijayi amati odyazake alimbe milandu lija 😅

  • @RuthBinali-b8c
    @RuthBinali-b8c 2 หลายเดือนก่อน

    Za dyera basi olo inu mukuyankha pasi pasi muganiza ngati gwilizano amauthesa mwini wake malemu koma a malawi muzachangamuka liti ndindale akufuna kukakamila gwilizano cholinga simukudziwa shame

  • @ChrissySalimu
    @ChrissySalimu 2 หลายเดือนก่อน +3

    Choka okupha munamupha Zanu kut mutenge mpando wake Ausi Muli ndimulandu ndimulungu sure

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mukuyankhula zonsezo chifukwa inuyo zanu zikuyenda, mukuwauza anthu kut tonse ndi amodzi. Funso ngat tili amodzi ndichifukwa chiyani a President akungolemba ntchito abale awo komanso azinzawo??? Kodi umenewo ndi umodzi? Bwanji simudzuzula kusankhana kumeneko.

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity 2 หลายเดือนก่อน

    Akulu awa akufuna agulise chipani cha UTM.chakwela msamale nayo.or iweyo usi usamale akutafuna

  • @giftnyirongo-ey3qy
    @giftnyirongo-ey3qy 2 หลายเดือนก่อน

    Why today?

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 2 หลายเดือนก่อน +3

    Mayi Chilima,,,, tiziwapemphelela chifukwa munawaphela amunao

    • @wisdom20mkango49
      @wisdom20mkango49 2 หลายเดือนก่อน +1

      So many plane crushes in the world achimwene sizinayambe kumalawi

  • @LawrenceBelson
    @LawrenceBelson 2 หลายเดือนก่อน +1

    Oro utani naweso uzafa waphesa chilima iwe mwachidule ndiwe yudasi iskariot ndipo pa exclusive unanena kut umapita kwa achakwera komaso kwa chilima zomwe zikuonesa kuti ndiwe waphesa chilima

  • @stalickkafera3454
    @stalickkafera3454 2 หลายเดือนก่อน +4

    Wa chisokoneza chipani cha UTM

  • @Mtalimanja1
    @Mtalimanja1 2 หลายเดือนก่อน

    Uyu ali ndi fundo zogwira mtima

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 2 หลายเดือนก่อน +12

    This shortman cant be trusted....

  • @StevenMsanyama
    @StevenMsanyama 2 หลายเดือนก่อน

    Wisdom defeats knowledge

  • @Emmamalunga-fj4ey
    @Emmamalunga-fj4ey 2 หลายเดือนก่อน

    Thawi yonseyi bwanji simunkavala uniform ya utm even mwini wakeyo Ali moyo aaahhh we can't trust you bwanj wakakamila ku mcp relo mwayamba kuvala uniform ya utm chifukwa mu kuziwa kuti joka akufelani alimanja aahhh

  • @PaulvinMhango
    @PaulvinMhango 2 หลายเดือนก่อน

    Wayaluka pano angobwebweta

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 2 หลายเดือนก่อน

    Manganya akufuna kuononga chipani cha utm. Anthu amene alipo si a utm wose koma ena ndima khwangwala. Manganya ndi sweet talk. Ndichifukwa chani manganya akukakamira ku mcp pamene chilima anafa ifa yovesa chisoni. Manganya aononga utm ngati pamene nankhumwa anaonongera dpp. Manganya amalawi asakupusiseni akukuyikani mukamwa mwamukango.Akufunako chani ku mcp? Mcp yo ndiyimene yinachedwesa kufufuza ifa ya chilima. Mtsogoleri basi palipose ngongole ngongole pamene pali bungwe limene likuyendesa zangongole koma pule ndi vp busy kuyakhula ngongole munthu opusa zeru ndi amene akusangala ndingongole koma wazeru amazisakira yekha chuma ndipo akachipeza chimakhala changeiro pamaso a Mulungu.Manganya ngati ukufuna khala ku mcp ko ndi ufulu wako koma asiyire azako apange za utm

  • @TisopeMkozo
    @TisopeMkozo 2 หลายเดือนก่อน +2

    Anthu ali apawa palibe wa utm angovala ngati a utm

  • @GilbatChimwaza
    @GilbatChimwaza 2 หลายเดือนก่อน

    Manganya amatha

  • @abdu-razaqxhatiyah
    @abdu-razaqxhatiyah 2 หลายเดือนก่อน

    I like manganya but I smell something fishy in him

  • @MorganMwikhala
    @MorganMwikhala 2 หลายเดือนก่อน +2

    Azimayi muzatiphetsa

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 หลายเดือนก่อน

    Mesa umati suyankha nde ya nthikoyo ukuikambiranji aaaaaa iwe galu wakumpha

  • @ernestphiri2934
    @ernestphiri2934 2 หลายเดือนก่อน

    Panga chako chipani , achilima anachoka pa vice president ku dpp alimboma ndikupanga Chao chipani

  • @frankpreciousmulwa7006
    @frankpreciousmulwa7006 2 หลายเดือนก่อน

    I can't trust this guy now

  • @ClydeNyasulu-tk6fj
    @ClydeNyasulu-tk6fj 2 หลายเดือนก่อน

    Aaaa kamthira kuwiri ako shupit kopereka nzake

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 2 หลายเดือนก่อน

    usi akuti chani kodi???UTM kufika chaka chamawa yikhala ma katani okhaokha😂😂😂😂😂

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe manganya usagawinitse anthu autm koma ndalama ndi satana udamupha chilima

  • @mkhulukinyata5198
    @mkhulukinyata5198 2 หลายเดือนก่อน

    Michael Usi usaganidze kuti an'thu ife ndiwopusa ayi , We know the all strategy that you are Playing .. Iweyo muntima mo ukudziwa kuti UTM Unatuluka chilima ali moyo , Makaka a UTM Wayamba kuvala pomwe CHILIMA wamwalirapa , Iweyo olo utapanga timapulani takoto " Koma a Malawi tikudziwa kuti Imfa yachilima iweyo unatenga nawo gawo ,Even Chilima atati Mulungu amudzutse lerolini " , Iweyo ndimunthu woyamba yemwe ungakhale m'dani wa CHILIMA . Anthu womwe alipamenepowo " We know very well kuti ndi anthu a chipani chako cha MCP , Koma apa wangowaveka makaka a UTM kuti anthufe tidziti" Ukutsatilidwa ndi anthu a UTM , Iweyo palibepo chomwe ungamatiwuze a Malawi ife ' Then nkuyiwala zachipongwe chomwe munamuchita CHILIMA ku chikangawa kuja , Chilima munamupha imfa yowawa kwambiri . Ndipo iweyo siwukuyeneranso kumakamba chilichonse chokhudza CHILIMA , MUNTHU WOYIPA , WOPANDA CHISONI , WOPANDA MANYAZI

  • @AnoldKonde-pd4qt
    @AnoldKonde-pd4qt 2 หลายเดือนก่อน

    Ngat alliance ilipo a pule abwere poyera kut ati akaime pa ballot paper nd ndan ulendo uno?

  • @RaphaelSiyeni
    @RaphaelSiyeni 2 หลายเดือนก่อน

    Ng'oma sound yake ndi mcp

  • @frankpreciousmulwa7006
    @frankpreciousmulwa7006 2 หลายเดือนก่อน

    Palibe chanzeru apa

  • @FrancisSteven-we1dj
    @FrancisSteven-we1dj 2 หลายเดือนก่อน

    Zikuwoneka kuti mungakhale tsogolo umu

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 2 หลายเดือนก่อน +1

    Uyu ndie satana bas

  • @EthelKubalasa
    @EthelKubalasa 2 หลายเดือนก่อน

    kkkkk lero tavala makaka achipani koma zilko, drama sizithu. tisapusepo apa ndi ngongole, tiyeni tilembetseni zimenezo ndi ndalama zathu.

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 2 หลายเดือนก่อน

    Rip SKC only God knows😢😢😢😢😢

  • @TorresBandala
    @TorresBandala 2 หลายเดือนก่อน

    Watenga a mcp okha okha apa manganya

  • @BryanJSimeon
    @BryanJSimeon 2 หลายเดือนก่อน

    Politics. Its something one will never understand. 😂

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 2 หลายเดือนก่อน

    Usi sakuwelenga bible. Munthu wazeru satumikira mabwana awiri nthawi yimozi. Ngati utm ukuyifuna tuluka ku mcp ngati sikuifuna utm khala ku mcp ko ukuganiza kuti marry chilima akusangalala nazo chimene ukuchita. Ifa ya chilima ikutipweteka amalawi munthu inde amakhala ndizifika koma kufa kwa chilima ndi azake cabinet yose yinapanga rigsin ndi president yomwe koma potimanyazi mulibe and amalawi tikuseketera zithu zoduka mutu.

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy 2 หลายเดือนก่อน

    Lero wati avaleko makaka a UTM

  • @ShearstonNyirenda
    @ShearstonNyirenda 2 หลายเดือนก่อน

    Otukwanawa ndi adpp

  • @GladysBanda-h2w
    @GladysBanda-h2w 2 หลายเดือนก่อน

    lero bola mwavalako makaka a UTM

  • @TisopeMkozo
    @TisopeMkozo 2 หลายเดือนก่อน +1

    Lero mpaka kuvala za utm mmm koma dzikoli

  • @Joejere-x3k
    @Joejere-x3k 2 หลายเดือนก่อน +2

    Utm sichipan inu ,,vote Dad

    • @AngelinaMzowa
      @AngelinaMzowa 2 หลายเดือนก่อน

      Kwanu konko

    • @Joejere-x3k
      @Joejere-x3k 2 หลายเดือนก่อน +1

      @@AngelinaMzowa napangani zoti Lero mudye bwwnj

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi 2 หลายเดือนก่อน

    Yudasi anapheleka chilima 🤔🤔

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mwayamba liti kumvala za UTM a manganya

  • @EmmanuelMoyo-hy5ni
    @EmmanuelMoyo-hy5ni 2 หลายเดือนก่อน +11

    Mwana wa Chikangawa

    • @KhumboVumu
      @KhumboVumu 2 หลายเดือนก่อน +1

      Mwanadi wa chikangawa

    • @SigereAckren
      @SigereAckren 2 หลายเดือนก่อน +1

      Akuziwapo kanthu awa pa imfa yachilima

    • @hippochivundi5031
      @hippochivundi5031 2 หลายเดือนก่อน

      Power full