❤❤❤ mr DC. Opposition please wakeup ndinakuwuzani kuti mec inene anthu wose omwe ali ndi ma ID district by district. Ife tili kumbuyo kwanu osusa koma musagone tikufuna kukoza.
Akulimbana chifukwa ndi driver wa Malawi right now, bus ngati sikuyendesedwa bwino anthu samaloza ma passangers ai a maloza driver, wabwadwa liri let me remind you, ma presidents onse ngakhale chakwera amazuzula a dpp kuti sakuyendesa bwino
Mukungolimbana ndi a chakwera koma chakwerayo sakuyankhani nkomwe, ndie vuto lanu nchiyani? Mbuyomu mwakhala mukuti muvula n muyenda munseyu muli chivulireni chifukwa chot ma alubino akungofa koma lero muli kumbuyo kuikiraso omwewo amene ankapha alubinowooo ndie nkumati amalawi azikutsatani inuyo?? Shame on u akalindo. Chanzerutu ndikuyang'ana kwa Yehova basi not munthu obadwa kwamunthu ai coz ulamurilo wolamulidwa ndi anthu ndiolephera basi
Yes opposition wake up pls 🙏 we don't need this government again be strong 💪 guys 🇲🇼 opposition pls wake up now 🙏 💙 😢 we begging you guys 🙏
❤❤❤ mr DC. Opposition please wakeup ndinakuwuzani kuti mec inene anthu wose omwe ali ndi ma ID district by district.
Ife tili kumbuyo kwanu osusa koma musagone tikufuna kukoza.
Awuzen Dc...Boma lolephera ili
Chipatala chasalima chikukozedwa pan akalindo kazikamban haq osat zokuuzan anthu akunamizan
Ma audio nde aaaa anenedwa koma amalawi iiii alitulobe ndithu zovesa chisono ngati action sikhalapo mcp iiii live izatengaso boma
Ulemu wanu bwana DC timakunyadilani
Kod aboni kalindo angopanga zachakwera vuto chani kwenikweni moti azipangako zazeru akuchedwa nazo ine chizonda matapila ndatero
Akulimbana chifukwa ndi driver wa Malawi right now, bus ngati sikuyendesedwa bwino anthu samaloza ma passangers ai a maloza driver, wabwadwa liri let me remind you, ma presidents onse ngakhale chakwera amazuzula a dpp kuti sakuyendesa bwino
Auzeni awa anthu osanva
Zomvela anthu aulesi izi
Mukungolimbana ndi a chakwera koma chakwerayo sakuyankhani nkomwe, ndie vuto lanu nchiyani? Mbuyomu mwakhala mukuti muvula n muyenda munseyu muli chivulireni chifukwa chot ma alubino akungofa koma lero muli kumbuyo kuikiraso omwewo amene ankapha alubinowooo ndie nkumati amalawi azikutsatani inuyo?? Shame on u akalindo. Chanzerutu ndikuyang'ana kwa Yehova basi not munthu obadwa kwamunthu ai coz ulamurilo wolamulidwa ndi anthu ndiolephera basi
Nanga si magazi amuchulukira mmanja ayankha bwanji
Musapake central region njala yakoyo. Yakukulila ndi nsanje. DPP sikuwina next year
DPP WOYEEEEEEEEEEEEEEEEE💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙
Elijah kasawala vote is for Dpp 💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙
❤❤❤❤❤❤❤❤❤
The DC mwana woyipa kwambiri
Boma lake lachikangawa haaa paka ndikuopa2 kukwela ndege
A opposition akumakhumudwitsa kwambiri, nowoso chemuthalika must come out and start to be more active in these issues
Mphavu azitenga kuti?
The dc
Ife tikanavota mcp
The DC
The DCCCCCCCC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri
Paja mulibe zochita inu zilubwani km musamalote kt mcp idzachoka m'boma mukunamizana mukhalila zomwezo or mutamaphatikiza mkulila km boma linapita ili vomelezani
Mcp isachoke boma kuti ikupanga chani
Kom pangan manyazi inu mcp mene akusuzila anthu aaaaaaaa ukuzinamoza ndiwe ndiboma lakho lakupha anthu lo zaziiii 😏😏😏😏😏😏😏
Amene akuimila Boma ili kumbuyo mitu yawo sigwira
Zanzii iwe ukakhl ukuona ngat ziko likuynda bwino ndeno Boma lake liti asazachokeyo
CADET OPUSA ULI MBUUUUUUUU KULI IWEKO
Ndipo mukuyakhula kma apposition sakumva
DC 😅
Kod aboni kalindo angopanga zachakwera vuto chani kwenikweni moti azipangako zazeru akuchedwa nazo ine chizonda matapila ndatero