Woza Friday comrade ntanyiwa more fireeeeeee the spirit of Chilima still moving muyaluka anthu azipembezo chifukwa cha dyera shame Mulungu akulangeni nonse anthu opanda chisoni
Tili Pano mdicholinga cha Yehova sangatisiye tikulira achitapo kathu ndithu amenewa alandire zilonda ndithu mabala osapora ayende maliseche azingobwebweta We love you Ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Koma mizimu ya anthu 9 awa mmm itikantha ndithu pangachedwe maka Ambuye tipatseni vumbulutso ndi mzimu wachidziwitso. Its becoming more scarily especially with this issie involving the clergy eish my Mw serious??
My fellow Malawians the problem we are currently facing is that we cannot differentiate between the righteous and the hypocrites in churches, mosques,politics,and in all human gatherings
Komatu MCP ifa ya chilima mupedza mayo soka mudzimatsa anthu ndalama cholinga wadzelu ndipamene akudxiwa kuti mwapha chilima kuti mupitilile 2025 KKKKK NUTSO ADZIBUTSA MAPHETSA MWANA NDIKUMAPITATSO KOKO PANO ALIYETSE AKUDZIWA KUTI KUKOKOMANA NDI FITI YAFITI CHAKWELA NDE AKAPATSIDWA NDALAMA MAFUMU MABUTSA KAYA ENA AKHALA NDANI KOM ZIWANI NDALAMA YAMAGADZI CHAKWELA 2025 CHAKE PALIBE
Am not fear, am a citizen of Malawi, Malawi is my home country as am home soil i have right of freedom of expression , right to life, so no one can't threat me if am doing right thing, working professionally, same applying to nonsense president Chakwera if you know you're doing right things to Malawians, why most citizens of Malawi were not happy with you? Beware Chakwera, the blood of Chilima and others is on your head you never have a peace in life.
You have nothing to tell Malawians apart from your empty vendetta. Kulibe izoooooooo. Forget about all those idiots you are mentioning. Failed politicians.
Ndipo kungoti dziko lathu transparency ma nkhani ngati izi imasowa. If we are to calculate imfa ya ngoziyi yapangitsa dziko to spend billions of kwacha right away from ndege which beyond repair, all those officers who were involved in to transfer dead bodies to where the Zambian plane collected and flew to LLs. All those press briefing, private mortuary charges, coffins/caskets, all those vehicles to Church, area 12, parliament, BNS and finally to Nsipe. Honestly guys even the venue ku Nsipe and other related processes.
A Malawi tikugulitsa ufulu ndi ndalama imagine to the extent yoti mpaka mipingo nkumakalandira ndalama Kamba ka imfa ya munthu this is very shameful!!!!!!
Additionally the Germany clue, trabsport, hotel charges, daily operstions etc, yet we have trillions of unpaid debt, are we serious? Chenicheni a malawi fe tikufuna chani ngati dziko makamaka atsogoleri? Mulungu tipatseni mavumbulutso otherwise we are moving backward more faster than the opposite direction.
May these innocent Souls of Late Right Honorable Dr Saulos Klaus Chilima and other 8 Malawians continue resting in eternal Peace
Munasowatu comrade,wina athawa state house akuifuna tipemphere kwambili anthu anapha aja azimubwelera onse kuchipinda kwa ndi a kasambara omwe
I will join that fasting zikutipweteka
Woza Friday comrade ntanyiwa more fireeeeeee the spirit of Chilima still moving muyaluka anthu azipembezo chifukwa cha dyera shame Mulungu akulangeni nonse anthu opanda chisoni
Tili Pano mdicholinga cha Yehova sangatisiye tikulira achitapo kathu ndithu amenewa alandire zilonda ndithu mabala osapora ayende maliseche azingobwebweta We love you Ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
We follow you Mr Ntanyiwa Lero simunayimbe nawo kanyimbo kaja mizimu 9 I were pamutu pake pa chalakwe😂😂😂
Honestly speaking, a Mtanyiwa mmatiimilira. Myoyo yaanthu ambili omwe tikulilira justice mitima yathu imakhala nchiyembekezo chifukwa cha inu. Keep the 🔥 burning
You❤❤❤ have to exactly for tell us poor people true god bless you 💕 end keep it up ❤
Jesus said clergies sit on Moses seat believe whatever they tell you but don't follow them because they are hypocrites Matthew 23
Buddy Ntanyiwa ‼️
Ulemu wanu bwana
Keep doing the needful ♥️🔥
Tiuzeni ifeyo Comrade Ntanyiwa tili pambuyo panu ife tili kuno ku South Africa tithana naye akusaka moyo wanuyu
Wosadandaula tizikupemphelela brother we love you so much ❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤❤❤
Mmapemphero anthu tisayiwale kupemphaMulungu kuti apengese misala azibusa ansembe ndi wina aliyense amene wadya ndalama kuti imfa ya aChilima isa wululike
Nkhani yokoma zedi fasting idziyamba nthawi yanji ndipo izintha nthawi yanji tipatseni program
Ngozi yagalimoto anthu amanyenyeka koma ya ndege ai ndithu kungovula ma jacket bas ati afa bwino. Ai zikomo a MCP
Am waiting for you my brother came with it more fire i ❤❤❤❤❤❤ it
Msamasowe a comrade timadalira inu pachilungamo
Zoona brother tiyeini tisale kudya choonadi chidziwike
Osaiwala Amene tikusala kudya tisale ndinyumba momwe
Ntanyiwa we're together from fasting, until something happen, Rip SKC and 8 others
You have my support prayerß job already And God is revange continue to save the people dont sale your grace .God bless u
People's Power, Don't Take People For Granted
Amene akudana ndiyinu mutu sukuyenda ukubebesa ayise
Mvuto kumalawi timangolongolola nthawi nkumatha maiko anzathuwa sangwatero mphamvu zimakhala ndi anthu osati atsogoleri
" Atampachika pa Mtanda anagawana msalu zake napanga mayere" . Those evil men akudziwa komwe kuli tie,Msapato 😂😂😂😂
Dokotalayonso ndopusa amudyesera azinena mawumboni abozawi ayaluka ili ndi dziko awakatha oansi pompano ndithu mulungu wathu ndi wa noyo
Tipemphelere kuti Chakwera akakhara pampando adziyabwidwa mpaka authawe
Koma mizimu ya anthu 9 awa mmm itikantha ndithu pangachedwe maka Ambuye tipatseni vumbulutso ndi mzimu wachidziwitso. Its becoming more scarily especially with this issie involving the clergy eish my Mw serious??
Athu akuzuzika ku malawi plz tiyeni tisangoonerera
Kod pa limpopo pano timafuna kudziwa kuti msilikali wa kamudzu balakisi unja zikuti bwanji alimoyo kapena kulibe
May God protect you sir!
Following mwachidwi always......
Nkhanga izooo!!!!
Tiyeni tipempheledi awakantha mulungu awonekela poyela amene anachita chipongwecho ndithu
Timakunyadilani Comrade mtanyiwa❤we. Love u
Takunyadilani Mr Mtanyiwa.... Mulungu wathu ndiwamoyo ndipo ndiwamayankho
This is true radio number one
Eish tinakusowa welcome back 🙏
God bless you ntanyiwa We're following you
Ndipo live tisara kudya brother allah atiyankha so soon
Kom imfa ya Chilima yosaiwalikatu😭😭 Rest well Legend
Ndpo zoopsa 😢
Ndipo comrade Ntanyiwa tionjezekepo pa ma prayer petitions po kuti: Mulungu akanthenso onse amene akulandira ndalama ndi cholinga chofuna kubisa chilungamo komanso kuwatseka pakamwa Mulungu wodziwa kubwezera (Psalm 94) atero mdithu.
Za mapemphero ndi kusala zakudya. comrade fotokozani bwino bwino nthawi yomasulira fasting imeneyi chifukwa mwangoti 5 days Mon-Fri
My everything radio ❤ watching from Israel 😂
My fellow Malawians the problem we are currently facing is that we cannot differentiate between the righteous and the hypocrites in churches, mosques,politics,and in all human gatherings
Awalanga ndipo asala pang'ono
Salute bigy limpopo
Nanga lamba wa trauzer ndege ndiyomwe inamasulasoooooo
Ine ndayamba kale kutsala
Moti kunyumbaku sindikudya
After Kenya Malawi get ready
Following you
Iwe Mtanyiwa ndikatundu kwambiri. Limpopo ndiyokha radio ya ife 🇲🇼 oxindikira😢😢😢😅
I love you Mr comrade go ahead
Mangochi boys tanola kare zida apa tikungodikila pa 10 ndipo munverako
Number one radio
We proud of guys God bless you
Kodi Ndege ikagwa kumakhalanso kuona nkhope??
Kkkkkk nanenso kudabwa😊
Do your job guy we are proud of you.
Lampopo tioseni zoona
If is rue shame to you Bishops ,,,,bloody money!,!
Timakunyadiran antanyiwa❤
Mudasowatu boss 💪💪🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Lipopo FM good
Limpopo fm number one Ulemu wanu big
Komatu MCP ifa ya chilima mupedza mayo soka mudzimatsa anthu ndalama cholinga wadzelu ndipamene akudxiwa kuti mwapha chilima kuti mupitilile 2025 KKKKK NUTSO ADZIBUTSA MAPHETSA MWANA NDIKUMAPITATSO KOKO PANO ALIYETSE AKUDZIWA KUTI KUKOKOMANA NDI FITI YAFITI CHAKWELA NDE AKAPATSIDWA NDALAMA MAFUMU MABUTSA KAYA ENA AKHALA NDANI KOM ZIWANI NDALAMA YAMAGADZI CHAKWELA 2025 CHAKE PALIBE
Limpopo fm koma iwe wabweraso
You are one mtanyiwaa
Am not fear, am a citizen of Malawi, Malawi is my home country as am home soil i have right of freedom of expression , right to life, so no one can't threat me if am doing right thing, working professionally, same applying to nonsense president Chakwera if you know you're doing right things to Malawians, why most citizens of Malawi were not happy with you? Beware Chakwera, the blood of Chilima and others is on your head you never have a peace in life.
Sabasaba uja bwanji?
😂😂😂😂Apengedi misala amenewa iyaaa
chakwera ndi chigawenga ma chende abambo ake ndithu mfiti satana
Umaitha iweyo umatuimvetsa kukoma. More fire 16:57
Following Limpopo
Fasting baasii titelo ndiithu
Nanga y we didn't see Ring or helicopter took it 😅😅😅😅😅
Mwati a mpingo so konko dollar?????????
Haaa kodi mmabishop omwe akudyya thupi la anthu amene adwalira pangozi ya ndege ku chikangawa ayibo koma ndi my dangerous
Mulungu wathu sangatisiye tikulila chonchi zanyanya
Nkanga zaona🎉
Good prayer points.😢😢
Mumatiimirira Mr ulemu wanu
Ife amalawi mantha nde ndiosayamba koma tikufatu tilimaso nde lets go guys timange malawi wathu
We are ready brother and we are together
Mumatipatsa khawatu comradeee
Mr Mtanyiwa kunja kwacha chilungamo chimveke timadalira inu mwadzuka bwanji kumenekoooooooooo
😂😂😂😂😂😂 km u umakwana Mr mtayiwa 😊😊😊😊😊
Ife kuno ku Capetown tili nanu PA 10 pano
Chakwera atupe mutu
Bwana mulungu akutetrdzan.ndithu
Osaopa, osafooka mpaka zofuna zathu zikwanilisidwe kumanga malawi 🇲🇼 wathu
Number 1 mumatiimilila
Mabishop Misa yoseija mwalandila ndrama
Amen
Ayambe ku pita ma activists wonse apite cause Kupanga support zopusazo
Zibonga zituluka pa 10 tiri chete kayeee...
You have nothing to tell Malawians apart from your empty vendetta. Kulibe izoooooooo. Forget about all those idiots you are mentioning. Failed politicians.
Msunuwako bhuti
You too , you got nothing to answer him
Ndipo kungoti dziko lathu transparency ma nkhani ngati izi imasowa. If we are to calculate imfa ya ngoziyi yapangitsa dziko to spend billions of kwacha right away from ndege which beyond repair, all those officers who were involved in to transfer dead bodies to where the Zambian plane collected and flew to LLs. All those press briefing, private mortuary charges, coffins/caskets, all those vehicles to Church, area 12, parliament, BNS and finally to Nsipe. Honestly guys even the venue ku Nsipe and other related processes.
Naye bakili muluxi waying'alula tu ku
A Malawi tikugulitsa ufulu ndi ndalama imagine to the extent yoti mpaka mipingo nkumakalandira ndalama Kamba ka imfa ya munthu this is very shameful!!!!!!
Komanso kwa omwe akulandira ndalamazi chonde tiziganizile kuti imfa yi ikanatichitikira ife tingamamve bwanji kumva kuti ena akupezerapo cholowa?
Ine ndikumakutsatilan zedi
Additionally the Germany clue, trabsport, hotel charges, daily operstions etc, yet we have trillions of unpaid debt, are we serious? Chenicheni a malawi fe tikufuna chani ngati dziko makamaka atsogoleri? Mulungu tipatseni mavumbulutso otherwise we are moving backward more faster than the opposite direction.
Mulungu atithandizedi pazimenezi
Tikumva