BON KALINDO THE D.C2 JULY 2024

แชร์
ฝัง

ความคิดเห็น • 97

  • @LameckLubani
    @LameckLubani 2 วันที่ผ่านมา +5

    Keep it up the good work DC ❤❤❤❤❤

  • @user-tk6wf2eg4z
    @user-tk6wf2eg4z 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ngat ife amalawi tilibe mawu action pa 10 July bs the dc Mwana oopse kwambili❤

  • @marthablessings1314
    @marthablessings1314 18 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Bwana waanthu osauka..we dilute u🎉🎉🎉🎉🎉

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 2 วันที่ผ่านมา +1

    Your sense mr kalindo is very powerful like the Kenyans people they don't tolerate nonsense . it's only you the all fucken Malawians you deserve brave enough i like it.

  • @SkevaMustapher
    @SkevaMustapher 2 วันที่ผ่านมา +2

    😂😂😂😂😂km kalindo iwe wachipongwe ndithu😅😅😅😅msapato kuyasamula ngati mulamba😅😅😅😅😅😅😅kom uko!!!!!!! Kunyasalandi kuli zithu

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 2 วันที่ผ่านมา +1

    I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi umatiimilira MULUNGU akudaliseni president wa anthu osauka.

  • @augustMag
    @augustMag 2 วันที่ผ่านมา +1

    Powerful message the DC Mulungu apitilize kukupasani moyo wautali 🔥♥️

  • @user-yd7di3cf8q
    @user-yd7di3cf8q 2 วันที่ผ่านมา +2

    The only man amene akuyankhula zoona zenizeni
    Pa mavuto omwe ali mdziko muno

  • @JimmyMzozoma
    @JimmyMzozoma 2 วันที่ผ่านมา +1

    MULUNGU azikumenyera nkhondo osalema pakuchita zabwino the dccccc

  • @SkevaMustapher
    @SkevaMustapher 2 วันที่ผ่านมา +1

    Kumangidwa kwanu kukupindura ndithu chifukwa mukuonaso mavuto amene Ali m'boma

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 2 วันที่ผ่านมา +2

    Amalawi anzanga, imvani mawu awa, tikamawona otiyankhulira monga Bon Kalindo, Ntanyiwa pamodzi ndi Limpopo FM, Bakili Muluzi TV, Lwala, ndi ena onse.
    Tikuyenera kumasuntika mumtina mwathu potengapo gawo kumenyera ufulu wathu.
    Dzikoli nde lavunda, chiyenera kuchita tiyeni amalawi chonde pa 10 July pano, tikamuonetse Chakwera kuti eni wake dziko ndiifeyo komanso kuti adziwe zoti tinamuyika pampando ndiifeyo.
    Apolisi komanso asilikali chonde, mudzazipatse ulemu nokha chifukwa pa 10 July, it's a do or die

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 2 วันที่ผ่านมา

      Mawu aphamvu ndinthu anthu amaphweketsa.

  • @twavysibale4751
    @twavysibale4751 2 วันที่ผ่านมา +1

    Boooooon kalindooo the DC ,ati msapato zoyasamula😂😂😂😂

  • @ChristinerGoman
    @ChristinerGoman 2 วันที่ผ่านมา +1

    Mumatiimilira keep it up ❤❤❤❤❤

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 2 วันที่ผ่านมา +1

    The DC ❤❤❤❤❤❤❤ mwana wowopsya kwambiri apolisi ulemu wanu😅😅😂😂😂😂

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา +1

    Bon kalindo apolice akuvaladi sapato zoyasamula kukamwa yasaa😂😂😂😂😂😂❤❤❤❤❤❤

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t 2 วันที่ผ่านมา

    Kkk nsapato yonyamuka ku tsogolo ngati kukamwa kwa nsomba i ❤️ you Bon K umanena chilungamo

  • @user-wx7pw8xg6x
    @user-wx7pw8xg6x วันที่ผ่านมา +2

    Ulemu wako DC umakwana

  • @FrankPhiri-f9w
    @FrankPhiri-f9w วันที่ผ่านมา

    Very Very good Bon Kalindo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 วันที่ผ่านมา

    Bwana Kalindo mukunena zoona ndipo Boma ili mmmmmmm apolice tili pamavuto bwana ndipo ma uniform omwe akuvalidwa panopa ndi anthawi ya Bingu ndi peter mutharika zomvesa chisoni Bwana, ndikungoona kuchedwa 2025 Chakwera is a destroyer

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 2 วันที่ผ่านมา

    Ndipo Malawi amene a kusangalala ndiomwewo saname dziko lathu ayi saname tithera moyenda momwemu koma na kumalawi adzapita chakwera achoka ndipo eeeeish 😢

  • @user-ez1kc7zp9m
    @user-ez1kc7zp9m 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera,s brain is divided into two parts.1part is full Of evil & the other part is empty

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 วันที่ผ่านมา

    Zipalasilo za nkhuku abale koma Ali ndimaphunzilo awo shame

  • @HopesonJailosi-vd6ou
    @HopesonJailosi-vd6ou วันที่ผ่านมา

    Ku South Africa or zimbwete zikupezeka,anthu akuzuzika

  • @BrinoMvula
    @BrinoMvula วันที่ผ่านมา

    Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 2 วันที่ผ่านมา

    DC ❤❤❤❤exactly kale police imaopya komalele aaaa manyaka😂

  • @ChristopherBwanali-i6b
    @ChristopherBwanali-i6b 2 วันที่ผ่านมา +1

    Bon kalindo the DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 2 วันที่ผ่านมา

    Munkafuna kuona zanyuwani lero ndizitu 😂😂😂😂😂😂😂, mcp oyeeee, timkanena anathela mu siizi

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 2 วันที่ผ่านมา

    Dc machine ❤❤ wi love you

  • @moyo77777
    @moyo77777 6 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Very true 🔥🔥🔥

  • @JanaMussa
    @JanaMussa 2 วันที่ผ่านมา +1

    Mumatiyimila man Dc

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b 2 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkkkk zosetera mpakana mapepala a ma statement okhaokha 😂😂😂

  • @user-hg5oj3ko1o
    @user-hg5oj3ko1o 2 วันที่ผ่านมา +1

    Sapato kuyasamula ngat mulamba😂😂😂😂

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi 2 วันที่ผ่านมา

    DC umatha kucheza iweyo kkkkkkkkk anyamata akugulisa mazila kuno ku south Africa

  • @irenioeugeniosumila6647
    @irenioeugeniosumila6647 2 วันที่ผ่านมา

    A Malawi segulani masso, Izi ndizohona

  • @user-ul8fp1ov1k
    @user-ul8fp1ov1k วันที่ผ่านมา +1

    Chilungamo chokhachokha

  • @lloydmalinga1198
    @lloydmalinga1198 2 วันที่ผ่านมา +1

    Big up the SC

  • @kondwaniwhite2871
    @kondwaniwhite2871 2 วันที่ผ่านมา +1

    Good thinking ❤

  • @WinessMatcthuwana
    @WinessMatcthuwana 2 วันที่ผ่านมา

    Umakwana tili pambuyopako. The dccccc!!!!!

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 วันที่ผ่านมา

    Tiyeni pa 10 July kumademo ndipo popita tizatenge mauta komanso maregeni sure

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ulemu wanu ADC

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 วันที่ผ่านมา

    Pachimake pa chilungamo

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 2 วันที่ผ่านมา +1

    Musamasowe a DC ❤

  • @patrickkhomba3446
    @patrickkhomba3446 วันที่ผ่านมา

    Are u avice president?

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 2 วันที่ผ่านมา

    What u r saying is true DC

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd 2 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkk a police akumalawi amangomvera zopoira iwo akuvutikad kumanga munthu akuŵamenyeera ufulu eeee

  • @user-js6xn9qj1r
    @user-js6xn9qj1r วันที่ผ่านมา

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 bwana Nyoo

  • @AcksonSimbeye-pm9po
    @AcksonSimbeye-pm9po 2 วันที่ผ่านมา

    Well done mr

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd 2 วันที่ผ่านมา +1

    Dc mlungu azikudalisan

  • @FisherAction
    @FisherAction 2 วันที่ผ่านมา

    Mukutiimirira zoonadi go on father

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 2 วันที่ผ่านมา

    Good massage

  • @user-lx5he8rv7n
    @user-lx5he8rv7n 2 วันที่ผ่านมา +1

    Mzerutu izi

  • @IsaacSaine-f1f
    @IsaacSaine-f1f วันที่ผ่านมา

    Ku police eeeeee ayi mazuzo

  • @samhussen708
    @samhussen708 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ifeyo iiii chakwera Ali shit

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 2 วันที่ผ่านมา +1

    💥💥💥💥💥

  • @mosesmakawamalawi
    @mosesmakawamalawi 2 วันที่ผ่านมา +1

    Koma DC sazatheka ata

  • @lloydmalinga1198
    @lloydmalinga1198 2 วันที่ผ่านมา +1

    The DC

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 2 วันที่ผ่านมา

    Sapato ngati mlamba😂😂😂😂.

  • @OwenJambo
    @OwenJambo 2 วันที่ผ่านมา

    Akumangatu dala

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 2 วันที่ผ่านมา

    Koma abale kkkkkkk mawu achibande simumawadziwa etiiii This is not Thomas chibade.

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v 2 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 2 วันที่ผ่านมา

    DC MARVEL ❤❤❤

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z วันที่ผ่านมา

    Fact

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 2 วันที่ผ่านมา

    Zomvetsa chisoni,

  • @EliasWotch
    @EliasWotch 2 วันที่ผ่านมา

    DC ulemu wanu

  • @RuthNanthando
    @RuthNanthando 2 วันที่ผ่านมา

    😭😭😭😭

  • @CharlesKachipanda-jz9jv
    @CharlesKachipanda-jz9jv 2 วันที่ผ่านมา

    The DDDDDDCCCCCCC is machine

  • @RonaldodalitigerSpencerDaliRic
    @RonaldodalitigerSpencerDaliRic 2 วันที่ผ่านมา +1

    The DC....kugazakugaza,kuswa kuswa....😅

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 2 วันที่ผ่านมา

    The DC 😂😂😂😂😂😂

  • @Eliza-h6o
    @Eliza-h6o 2 วันที่ผ่านมา

    Kalondo ndiyekhayo Oyankhul chilungamo koma azipan zotsusa Ali chete

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js 2 วันที่ผ่านมา

    I feel sorry for the people in malawi,now we have just seen they have devalued money silently,check on exchange rate,very sad

  • @user-mq1wp9th1d
    @user-mq1wp9th1d 2 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk 😂😂😂😂

  • @kihiyen3100
    @kihiyen3100 2 วันที่ผ่านมา

    😂

  • @cajozocacheuca8034
    @cajozocacheuca8034 2 วันที่ผ่านมา

    D...,.C

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 2 วันที่ผ่านมา

    Mmm galu iwe anthu anayamba kupita kunja kalekale it’s nothing to do with boma….uwafunse ayao ndi atonga!

    • @kihiyen3100
      @kihiyen3100 2 วันที่ผ่านมา

      Galu? Mphapsya mtima tu😂😂😂 kabaya?

    • @ziyamporoma377
      @ziyamporoma377 2 วันที่ผ่านมา

      @@kihiyen3100 mmm malume palibe zopsyera mtima apa. Tikungofuna ma activist apa social media asamaname

    • @kihiyen3100
      @kihiyen3100 2 วันที่ผ่านมา

      ​@@ziyamporoma377I thought ndinu a MCP

    • @BensonChilundu
      @BensonChilundu 2 วันที่ผ่านมา

      Gulu la agalu ngati awa odana ndi Bon Kalindo ndi agalu osakonda dziko lawo.Kodi ndiwe waku Kasiya omwe mukulandila ma 750,000 malawi kwacha.Mulungu akukanthe ndithu.Momwe anthu akuvutikila muno mkumasangalala nazo

    • @marryphili5419
      @marryphili5419 2 วันที่ผ่านมา

      Galu ndiwe wodana ndi bon kalindo chisiru panopa winawake angamasapote MCP stupid

  • @CharlesTambala-zn2bd
    @CharlesTambala-zn2bd 2 วันที่ผ่านมา

    Sapato...ngati Mulamba? Kkkkkk

  • @godfreyalberto7425
    @godfreyalberto7425 2 วันที่ผ่านมา

    Bon kalindo umandinyasa chifukwa ulemu kwa akulu akulu ukamachula kunenakuti mfumu iwe ndikunyoza kwambiri . Iweyo ulibe mwambo sulemekeza akuluakulu sungalitsike choncho ndiwe mwana chosalemekeza akulu nditsoka

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 2 วันที่ผ่านมา

      Kape khala chete iwe, mfumuyo ndimulungu

    • @CharlesmakveliNyirenda
      @CharlesmakveliNyirenda 2 วันที่ผ่านมา

      Uyu panya pake msiye boni kalindo akulakwila chan mungiba basi

    • @user-ty1vq9lq6w
      @user-ty1vq9lq6w 2 วันที่ผ่านมา +1

      Apolice akumvetsadi chisoni komanso zochititsa manyazi angokhala akapolo aanthu andale

    • @lucianojames7555
      @lucianojames7555 2 วันที่ผ่านมา

      Mbuzi

    • @kelvindickson
      @kelvindickson วันที่ผ่านมา

      Galu

  • @BrinoMvula
    @BrinoMvula วันที่ผ่านมา

    Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena

  • @kelvindickson
    @kelvindickson วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk koma DC sapato yayasamula kukamwa ngati mulamba

  • @RuthNanthando
    @RuthNanthando 2 วันที่ผ่านมา

    😭😭😭😭

  • @BrinoMvula
    @BrinoMvula วันที่ผ่านมา

    Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena