Your sense mr kalindo is very powerful like the Kenyans people they don't tolerate nonsense . it's only you the all fucken Malawians you deserve brave enough i like it.
Bwana Kalindo mukunena zoona ndipo Boma ili mmmmmmm apolice tili pamavuto bwana ndipo ma uniform omwe akuvalidwa panopa ndi anthawi ya Bingu ndi peter mutharika zomvesa chisoni Bwana, ndikungoona kuchedwa 2025 Chakwera is a destroyer
Keep it up the good work DC ❤❤❤❤❤
Ngat ife amalawi tilibe mawu action pa 10 July bs the dc Mwana oopse kwambili❤
Bwana waanthu osauka..we dilute u🎉🎉🎉🎉🎉
Your sense mr kalindo is very powerful like the Kenyans people they don't tolerate nonsense . it's only you the all fucken Malawians you deserve brave enough i like it.
😂😂😂😂😂km kalindo iwe wachipongwe ndithu😅😅😅😅msapato kuyasamula ngati mulamba😅😅😅😅😅😅😅kom uko!!!!!!! Kunyasalandi kuli zithu
😂😂😂
I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi umatiimilira MULUNGU akudaliseni president wa anthu osauka.
Powerful message the DC Mulungu apitilize kukupasani moyo wautali 🔥♥️
The only man amene akuyankhula zoona zenizeni
Pa mavuto omwe ali mdziko muno
100%
200%
MULUNGU azikumenyera nkhondo osalema pakuchita zabwino the dccccc
Kumangidwa kwanu kukupindura ndithu chifukwa mukuonaso mavuto amene Ali m'boma
Amalawi anzanga, imvani mawu awa, tikamawona otiyankhulira monga Bon Kalindo, Ntanyiwa pamodzi ndi Limpopo FM, Bakili Muluzi TV, Lwala, ndi ena onse.
Tikuyenera kumasuntika mumtina mwathu potengapo gawo kumenyera ufulu wathu.
Dzikoli nde lavunda, chiyenera kuchita tiyeni amalawi chonde pa 10 July pano, tikamuonetse Chakwera kuti eni wake dziko ndiifeyo komanso kuti adziwe zoti tinamuyika pampando ndiifeyo.
Apolisi komanso asilikali chonde, mudzazipatse ulemu nokha chifukwa pa 10 July, it's a do or die
Mawu aphamvu ndinthu anthu amaphweketsa.
Boooooon kalindooo the DC ,ati msapato zoyasamula😂😂😂😂
Mumatiimilira keep it up ❤❤❤❤❤
The DC ❤❤❤❤❤❤❤ mwana wowopsya kwambiri apolisi ulemu wanu😅😅😂😂😂😂
Bon kalindo apolice akuvaladi sapato zoyasamula kukamwa yasaa😂😂😂😂😂😂❤❤❤❤❤❤
Kkk nsapato yonyamuka ku tsogolo ngati kukamwa kwa nsomba i ❤️ you Bon K umanena chilungamo
Ulemu wako DC umakwana
Very Very good Bon Kalindo
Bwana Kalindo mukunena zoona ndipo Boma ili mmmmmmm apolice tili pamavuto bwana ndipo ma uniform omwe akuvalidwa panopa ndi anthawi ya Bingu ndi peter mutharika zomvesa chisoni Bwana, ndikungoona kuchedwa 2025 Chakwera is a destroyer
Ndipo Malawi amene a kusangalala ndiomwewo saname dziko lathu ayi saname tithera moyenda momwemu koma na kumalawi adzapita chakwera achoka ndipo eeeeish 😢
Chakwera,s brain is divided into two parts.1part is full Of evil & the other part is empty
Zipalasilo za nkhuku abale koma Ali ndimaphunzilo awo shame
Ku South Africa or zimbwete zikupezeka,anthu akuzuzika
Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena
DC ❤❤❤❤exactly kale police imaopya komalele aaaa manyaka😂
Bon kalindo the DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Munkafuna kuona zanyuwani lero ndizitu 😂😂😂😂😂😂😂, mcp oyeeee, timkanena anathela mu siizi
Dc machine ❤❤ wi love you
Very true 🔥🔥🔥
Mumatiyimila man Dc
Kkkkkkkk zosetera mpakana mapepala a ma statement okhaokha 😂😂😂
Sapato kuyasamula ngat mulamba😂😂😂😂
DC umatha kucheza iweyo kkkkkkkkk anyamata akugulisa mazila kuno ku south Africa
A Malawi segulani masso, Izi ndizohona
Chilungamo chokhachokha
Big up the SC
Good thinking ❤
Umakwana tili pambuyopako. The dccccc!!!!!
Tiyeni pa 10 July kumademo ndipo popita tizatenge mauta komanso maregeni sure
Ulemu wanu ADC
Pachimake pa chilungamo
Musamasowe a DC ❤
Are u avice president?
What u r saying is true DC
Kkkkkk a police akumalawi amangomvera zopoira iwo akuvutikad kumanga munthu akuŵamenyeera ufulu eeee
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 bwana Nyoo
Well done mr
Dc mlungu azikudalisan
Mukutiimirira zoonadi go on father
Good massage
Mzerutu izi
Ku police eeeeee ayi mazuzo
Ifeyo iiii chakwera Ali shit
💥💥💥💥💥
Koma DC sazatheka ata
The DC
Sapato ngati mlamba😂😂😂😂.
Akumangatu dala
Koma abale kkkkkkk mawu achibande simumawadziwa etiiii This is not Thomas chibade.
❤❤❤
DC MARVEL ❤❤❤
Fact
Zomvetsa chisoni,
DC ulemu wanu
😭😭😭😭
The DDDDDDCCCCCCC is machine
The DC....kugazakugaza,kuswa kuswa....😅
The DC 😂😂😂😂😂😂
Kalondo ndiyekhayo Oyankhul chilungamo koma azipan zotsusa Ali chete
I feel sorry for the people in malawi,now we have just seen they have devalued money silently,check on exchange rate,very sad
R1=k140 mmmm
Kkkkk 😂😂😂😂
😂
D...,.C
Mmm galu iwe anthu anayamba kupita kunja kalekale it’s nothing to do with boma….uwafunse ayao ndi atonga!
Galu? Mphapsya mtima tu😂😂😂 kabaya?
@@kihiyen3100 mmm malume palibe zopsyera mtima apa. Tikungofuna ma activist apa social media asamaname
@@ziyamporoma377I thought ndinu a MCP
Gulu la agalu ngati awa odana ndi Bon Kalindo ndi agalu osakonda dziko lawo.Kodi ndiwe waku Kasiya omwe mukulandila ma 750,000 malawi kwacha.Mulungu akukanthe ndithu.Momwe anthu akuvutikila muno mkumasangalala nazo
Galu ndiwe wodana ndi bon kalindo chisiru panopa winawake angamasapote MCP stupid
Sapato...ngati Mulamba? Kkkkkk
Bon kalindo umandinyasa chifukwa ulemu kwa akulu akulu ukamachula kunenakuti mfumu iwe ndikunyoza kwambiri . Iweyo ulibe mwambo sulemekeza akuluakulu sungalitsike choncho ndiwe mwana chosalemekeza akulu nditsoka
Kape khala chete iwe, mfumuyo ndimulungu
Uyu panya pake msiye boni kalindo akulakwila chan mungiba basi
Apolice akumvetsadi chisoni komanso zochititsa manyazi angokhala akapolo aanthu andale
Mbuzi
Galu
Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena
Kkkkkkkk koma DC sapato yayasamula kukamwa ngati mulamba
😭😭😭😭
Mmmmmm mpaka transfer kumaiko ena