Zomwe wayankhula Waxy Kay pa Maliro a Bambo ake a Bishop Kapenga ku Robins Park in Blantyre

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 1 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 74

  • @JOHNOlesmasCosmas
    @JOHNOlesmasCosmas 2 วันที่ผ่านมา +20

    imfa ya munthu olungama pamaso pa Yehova pamakhara chimwemwe zilibwino indeed
    waxy mzimu wa Yehova ukuyankhura iye wangokhara chotengera chake
    may His soul rest in internal peace 😭😭😭

  • @ListerMunthali
    @ListerMunthali 2 วันที่ผ่านมา +9

    Ndikukumbuka mu ulaliki wina wake bishop kapenga ananena kuti ngati situation ndiyoti sungayisithe no matter what, osalira just say zikomo ambuye.
    Pachifukwa ichi nane ndikuti zili bwino ndi mzimu wawo for God has relieved him from all his pains🙏

  • @user-pn7cj9hb3t
    @user-pn7cj9hb3t 2 วันที่ผ่านมา +8

    Chomwe walakwitsa Waxy Kay ndi chani anthu inu? Kapena simudziwa mau simudawelenge?

  • @WellosMphonde-wd2cx
    @WellosMphonde-wd2cx วันที่ผ่านมา +3

    Munthu akamwalira kulira kumatanthauza kusowa chiyembekezo pamene mau ake a Mulengi amati tisalire pakuti mu zonse tidziti zilibwino nde mukati speech yolakwika nde kuti chani. Lolani akulimbika mtima akhale akulimbika mtima pakuti ndi mawu ndipo mwa mawu tidzachuta mwa mawu. Say Amen/Ameen

  • @user-uo3lm5wl5j
    @user-uo3lm5wl5j 2 วันที่ผ่านมา +5

    Ifa ya wamuthu olungama kumwamba kuli chimwemwe mwAna wazelu kwabassi ndiwochepa agazindikile mawu wayakhula mwanayu Kwa amene amakhululupila mulungu wava tathsuzo lake amen

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub 2 วันที่ผ่านมา

      Ndipo imfa ya munthu oyera mtima imakhala yokoma chifukwa amakhala akudziwa za komwe akupita

  • @AnthonyChibwe-bf4de
    @AnthonyChibwe-bf4de 2 วันที่ผ่านมา +4

    He has to say so,, there is no way kut azikhala akudandaula yet zinthunzo zachitika kale komaso sangathe kuzibweza pat. Mmalo moti azingodandaula wasankha kusangalala that's a good choice or adakayankhula zodandaula zidakasintha chan? Umenewo nde umunawo mesa,

  • @ALINAFEMKOMERA-cm1md
    @ALINAFEMKOMERA-cm1md 2 วันที่ผ่านมา +2

    He got broken... He wrote a status he was comforted that he should be strong since the father is in a better place
    Now he is strong anthu muyakhulisaso
    Mumtima akuliratu munthuyu

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf 2 วันที่ผ่านมา +7

    Speech iyi ndiyofunika azungu koma ife tiziti mwatilawula😢

  • @samuelkapasula-mn6es
    @samuelkapasula-mn6es วันที่ผ่านมา

    Zoonadi.....Zili bwino mwa Yesu khristu.....

  • @RedKoffii-gl2vx
    @RedKoffii-gl2vx 2 วันที่ผ่านมา +6

    Mwana ulimba mtima

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah6448 2 วันที่ผ่านมา

    Indeed zili bwino aliyese azafa komano kuluza munthu sichithu chophweka nde kumankhala makolo ako

  • @WakisaPhiri-e1e
    @WakisaPhiri-e1e 2 วันที่ผ่านมา

    RIP Pastor 😭 Anthu awa amkavana

  • @ZaffboyYellows
    @ZaffboyYellows 2 วันที่ผ่านมา

    I'm very sorry 😢Your highness young king. If you want to talk ' I'm here at any time

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano วันที่ผ่านมา

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤

  • @Choicemlw
    @Choicemlw วันที่ผ่านมา

    Yesu analira pa maliro a Lazaro

  • @user-wz1jy3uj8p
    @user-wz1jy3uj8p 2 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤❤

  • @POker_On1.
    @POker_On1. วันที่ผ่านมา +1

    Zibwíno 🙏🏾

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 2 วันที่ผ่านมา

    Owooo chabwino

  • @chemapa
    @chemapa 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    zabodzazo zosamvekazo Mulunguyo anamuuzira kuti? pamaliro sitchukira. tisamaseweretse dzina la Mulungu. kulowetsa chibwana pamaliro a mtumiki wamulungu.

  • @nkosikhonasiphiwemdlalose227
    @nkosikhonasiphiwemdlalose227 2 วันที่ผ่านมา +1

    Some of the tribes in Zim they celebrate when they lose someone zili bwino akapumule ali ndi Yesu wao

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo วันที่ผ่านมา

    Chitsiru chamwana ,nde chojowera-jowera ndichani .ngati zili bwino osangoyankhula bwino bwino kupereka ulemu kwa anthu ena bwanji.kufuna kutchuka ndi uchitsiru udzazindikira bwino patsogolo

  • @CatherineKumwendaCatherine
    @CatherineKumwendaCatherine วันที่ผ่านมา

    Kwa munthu oti amaziwa za kumwamba mwana wayakhura zomwe Mulungu amatilimbikisa pamavuto or pa Mtender tiziti zili bwno

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841 วันที่ผ่านมา

    Muthu akamwarila, timarila pa nthawi imeneyoyo, ndee waxy kay sanalakwitse moti speech yake ili bho ndithu.

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug 2 วันที่ผ่านมา

    Sizilibwino ndizolilitsa kwambili 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @MDAmir-ku4lf
    @MDAmir-ku4lf 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Waxy akunena zoona, mau a munthu okhulupilira ndi oti zilibwino. Abale amzanga munthu akamwalira sinthawi yoti ife tizilira ndi nthawi yosangalala chifukwa chani ndikuyankhula choncho, chisanzo munthu akamagwira ntchito kaya ndi pa company kaya m'boma amayembekezera kuti mwezi ukatha akuyenera kukalandira salary, ndiye funso nali, ndindani amene amapita kokalandira salary akulira tipeza kuti palibe wina aliyense amakhala osangalara kuti lero tikadyera nyama, ndi chimozimozi inu ndi ine mulungu anatisankha ndikutisiya pano pa dziko lampasi cholinga chimene anatisiila pa dziko la pansi ndi chani tizimugwadira nthawi ndi nthawi, ndiye tamugwadira mulungu, mwini wake emweyo yemwe timamutumikira uja watiitana tamwalira ndicholinga choti akatipase malipiro pa ntchito yomwe iye anatipasa takhala tikumugwilira tidakali ndi moyo abale amzanga sinthawi yomalira imene ija ayi ndinthawi yotchulusa kupempha kwa mulungu kumupemphelera m'bale wathu kuti ngati anali ochita ntchito zabwino mulungu amuonjezere zabwino zochuluka pa ntchito yomwe iye anali kugwira adakali ndi moyo komanso ngati anali ochita ntchito pena zoipa mulungu asachulukise kuyang'ana zoipa zake Ameen

  • @kondwanibuleya-br9gr
    @kondwanibuleya-br9gr 2 วันที่ผ่านมา

    😢 what a man up

  • @jamesbowman-cw8ts
    @jamesbowman-cw8ts วันที่ผ่านมา

    Koma ndiye Kuli mixed bag of comments,... Waxy this Waxy that,... aMalawi musiyeni mwana, walimba mtima ndi chiyembekezo kuti bambo ake ali malo abwino opumula ndi Yesu wawo ndipo palibe chodandaula,... Ndiye mukuti chani anthu "abwino" komanso osunga "chikhalidwe" chachiMalawi inu??
    Pena ngati ndinene kuti dikirani abambo anu akazamwalira muzayankhule speech yanu yabwinoyo,....koma poti imfa si yabwinonso. So whatever,
    Rest well Bishop Kapenga. We knew as man of God and we're sure to God your soul has returned. Rest Bishop rest🕊️🕊️

  • @Mphatsolikotima
    @Mphatsolikotima 2 วันที่ผ่านมา

    Rip bishop kapenga 😢

  • @GetrudeGama-gu5rb
    @GetrudeGama-gu5rb 2 วันที่ผ่านมา +1

    Zowonadi ziribwino kwaiwo kwantha kwatsara kwaife

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 2 วันที่ผ่านมา +1

    Osamamuchemerera mfanayu ndikape chisiru paumunthu speech umatulusa malingana ndimaro ache awa anali bambo ake osati ngt kanali kushow koziwonesera kt kaya akazi akafire zachamba

  • @BestMtawali
    @BestMtawali วันที่ผ่านมา

    Ndalama unadya zacosoma zja nyimbo zake ndizit unaimba?????😩😩😩😩

  • @jelblinds2017
    @jelblinds2017 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    There is nothing wrong jst that we as malawians have poor and shallow minds

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano วันที่ผ่านมา

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤
    0:11

  • @Tryness-wb6dj
    @Tryness-wb6dj 2 วันที่ผ่านมา

    Rest well Bishop Kapenga

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 2 วันที่ผ่านมา

    Wavala mzimuwamji mwanau

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q วันที่ผ่านมา

    Km ine kaya ndi chimodzichi km speech yi sinandivekere mwaumunthu

  • @AneesaMoosa-nv6bq
    @AneesaMoosa-nv6bq 2 วันที่ผ่านมา

    Rest in peace bishop kapenga

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 2 วันที่ผ่านมา

    Ku show kapena maliro

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa 2 วันที่ผ่านมา

    Sitinazolowele spech ngati izi kuno kwathu

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 2 วันที่ผ่านมา

    Mwana wamuna azikhara olimba mtima choncho waxy mbiri yako yabwno umakhara bwno ndi bambo ako ambuye akuze malire amoyo wako ndi abale ako😢

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano วันที่ผ่านมา

    Mau abwino kwa munthu olungam

  • @maxyfreeman9691
    @maxyfreeman9691 16 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kaya mwanayu sanasute koma

  • @eltonnankhwere3284
    @eltonnankhwere3284 2 วันที่ผ่านมา

    Of course am satisfied with the speech it seems unakonzeka ngati ukupita
    ku show.i remember you wrote kuti tiyeni mawa tikakumane pa Robins Park ndikaimba nyimbo in other way its not fitting

  • @ShyreenKwisongole
    @ShyreenKwisongole 12 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Emen

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 วันที่ผ่านมา

    Wakhutu la uximu wanva

  • @billykamwendo6517
    @billykamwendo6517 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ife ndi a Malawi, izi nzachizungu ndipo naaa ine sindingayankhule chonchi ali oti ndi bambo anga.

    • @TadalaChithope-yg9fo
      @TadalaChithope-yg9fo 2 วันที่ผ่านมา

      Azibambo nthawi zambili amakhala olimba mtim and uyuso panja mean oyamba ayenela kukhala strong komas tiyamike kut bambo ake amwalila waxy atatembenuka mtima komas kwaimayife zovuta kom kwa mamun ngt uyu akudziwa chomwe akuchita komas mwa okhulipilila izi zosavuta ngt munawon live yadzulo mayi ake okhala akaz awo anayimba nyimbo xa phamvuso coz ndi anthu okhulupilila and akudziwa kut akuyakhula mulungu wawo

  • @HussainGaffarOlaiza-hy9sg
    @HussainGaffarOlaiza-hy9sg 2 วันที่ผ่านมา

    💔🕊

  • @DJcliffBandakhudzanga
    @DJcliffBandakhudzanga 2 วันที่ผ่านมา

    Waxy ndi nfana olimba mwana wamamuna adzitelo

  • @mikemakamo7360
    @mikemakamo7360 2 วันที่ผ่านมา

    Koma mwana wakondwelatu 😂😂😂
    Zotindipamalilo wayiwala yoh mphamvu ziko likulowa bola

  • @marryrobert7092
    @marryrobert7092 2 วันที่ผ่านมา

    A malawi uziwa kurangiza mwana warakwa chani kod simuziwa kuti muthu akafa sibwino kurira mokweza ndemumatu iyi azirira

  • @FranckieDambah
    @FranckieDambah 2 วันที่ผ่านมา

    Eeeeee waxy umatha kuyankhura

  • @MarthaMfulusa-vj3xe
    @MarthaMfulusa-vj3xe 16 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Strange

  • @daziana2023
    @daziana2023 2 วันที่ผ่านมา

    Zilibwino

  • @TadalaChithope-yg9fo
    @TadalaChithope-yg9fo 2 วันที่ผ่านมา

    😭

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 2 วันที่ผ่านมา

    Muzidyatu bwino ganjayo

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 2 วันที่ผ่านมา +1

    Iyi ndi lmfa osapanga zibwana kawonesa picture yanji kwa azukulu amipingo pamwambo wamaliro kakuti sharp wachani zachamba

  • @EmmanuelNgamuti
    @EmmanuelNgamuti วันที่ผ่านมา

    Young man where hv u taken the energy to make this non African speech on a day like this?

  • @DavieChangoima
    @DavieChangoima 2 วันที่ผ่านมา

    Sorry rnp

  • @Ampambachulu
    @Ampambachulu วันที่ผ่านมา

    Bro thought he killed

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 2 วันที่ผ่านมา

    Waxy akanakhala ngati chija chinthubidwa cha chilima chija akanag'alura

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub 2 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂

    • @SinyoroMoyo
      @SinyoroMoyo วันที่ผ่านมา

      Eish guys 😂😂😂😂😂

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 2 วันที่ผ่านมา +1

    Guys mwanai watani kodi
    Paribe muthu amasangalala pa ifa ai .
    Uyu wandikaikisa chabwino R.I.P pastor kapenga

    • @HannahChingwalu
      @HannahChingwalu 2 วันที่ผ่านมา +1

      Chakaikitsa pamenepo ndichani?? Akuyenera kutero kumene chifukwaso zili mmalemba Mulungu ananena kuti kwaikika kwamunthu kufa,,chamoyo chilichonse chikuyembekeza imfa Ambuye alemekezeke chifukwa wakwanilitsa mau ake,,osati zanuzo apa

  • @SamsonChiwera
    @SamsonChiwera 2 วันที่ผ่านมา

    Mmmm waxy Kay Kuno ndi kumalawi ndye yaaa kumbali Ina it's ok kuti zilibwino koma another side this speech is useless to me when you grow up that's when you will realize that l made silly speech RIP Mr kapenga

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o 2 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula kotani uku, mwana wachibwana

  • @BlessingsMangwaya-mk4fi
    @BlessingsMangwaya-mk4fi 2 วันที่ผ่านมา +9

    This is not a fitting speech for the day your father passed away 😪😪

    • @lindamyaba
      @lindamyaba วันที่ผ่านมา

      Be serious man, waxy mwaonetsa maturity, zili bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 วันที่ผ่านมา

      Sonotu anthu odziwa mawu zimaaiyana ndi osadziwa mau zili bwino basi ambuye walora

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys 2 วันที่ผ่านมา

    Komatu for sure now irealize rhst crying during someone's daeth is for us poor imagine what is this speech 😭😭😭😭😭💔💔end with sure
    Anyway rest well pastor kapenga