Zomwe wayankhula Waxy Kay pa Maliro a Bambo ake a Bishop Kapenga ku Robins Park in Blantyre

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 4 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 91

  • @JOHNOlesmasCosmas
    @JOHNOlesmasCosmas 7 หลายเดือนก่อน +22

    imfa ya munthu olungama pamaso pa Yehova pamakhara chimwemwe zilibwino indeed
    waxy mzimu wa Yehova ukuyankhura iye wangokhara chotengera chake
    may His soul rest in internal peace 😭😭😭

  • @ListerMunthali
    @ListerMunthali 7 หลายเดือนก่อน +11

    Ndikukumbuka mu ulaliki wina wake bishop kapenga ananena kuti ngati situation ndiyoti sungayisithe no matter what, osalira just say zikomo ambuye.
    Pachifukwa ichi nane ndikuti zili bwino ndi mzimu wawo for God has relieved him from all his pains🙏

  • @WellosMphonde-wd2cx
    @WellosMphonde-wd2cx 7 หลายเดือนก่อน +6

    Munthu akamwalira kulira kumatanthauza kusowa chiyembekezo pamene mau ake a Mulengi amati tisalire pakuti mu zonse tidziti zilibwino nde mukati speech yolakwika nde kuti chani. Lolani akulimbika mtima akhale akulimbika mtima pakuti ndi mawu ndipo mwa mawu tidzachuta mwa mawu. Say Amen/Ameen

  • @JoaoLazaroMATABICHO
    @JoaoLazaroMATABICHO 7 หลายเดือนก่อน +9

    Ifa ya wamuthu olungama kumwamba kuli chimwemwe mwAna wazelu kwabassi ndiwochepa agazindikile mawu wayakhula mwanayu Kwa amene amakhululupila mulungu wava tathsuzo lake amen

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub 7 หลายเดือนก่อน

      Ndipo imfa ya munthu oyera mtima imakhala yokoma chifukwa amakhala akudziwa za komwe akupita

  • @agnessliwonde
    @agnessliwonde 7 หลายเดือนก่อน +1

    I personally support waxy. All is well indeed. It reminded me of my late mum. She said all is well and the future is so bright. Kwa okhulupirirafe zilibwino ndithu. Chauta salakwitsa. The lapture is here and Go's is taking his righteous ones. Go well bishop .

  • @snowkybeats
    @snowkybeats 7 หลายเดือนก่อน +1

    Beautiful speech for a believer. Celebrating a life well lived.

  • @ALINAFEMKOMERA-cm1md
    @ALINAFEMKOMERA-cm1md 7 หลายเดือนก่อน +6

    He got broken... He wrote a status he was comforted that he should be strong since the father is in a better place
    Now he is strong anthu muyakhulisaso
    Mumtima akuliratu munthuyu

  • @Lozykay
    @Lozykay 26 วันที่ผ่านมา

    Ulemu wanu a waxy kay 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @duncansikwese237
    @duncansikwese237 6 หลายเดือนก่อน +1

    Zilibwino may God be with him

  • @DouglasDazuKamwendo
    @DouglasDazuKamwendo 7 หลายเดือนก่อน +10

    Chomwe walakwitsa Waxy Kay ndi chani anthu inu? Kapena simudziwa mau simudawelenge?

  • @mikemakamo7360
    @mikemakamo7360 7 หลายเดือนก่อน +1

    Koma mwana wakondwelatu 😂😂😂
    Zotindipamalilo wayiwala yoh mphamvu ziko likulowa bola

  • @AnthonyChibwe-bf4de
    @AnthonyChibwe-bf4de 7 หลายเดือนก่อน +6

    He has to say so,, there is no way kut azikhala akudandaula yet zinthunzo zachitika kale komaso sangathe kuzibweza pat. Mmalo moti azingodandaula wasankha kusangalala that's a good choice or adakayankhula zodandaula zidakasintha chan? Umenewo nde umunawo mesa,

  • @MDAmir-ku4lf
    @MDAmir-ku4lf 7 หลายเดือนก่อน +2

    Waxy akunena zoona, mau a munthu okhulupilira ndi oti zilibwino. Abale amzanga munthu akamwalira sinthawi yoti ife tizilira ndi nthawi yosangalala chifukwa chani ndikuyankhula choncho, chisanzo munthu akamagwira ntchito kaya ndi pa company kaya m'boma amayembekezera kuti mwezi ukatha akuyenera kukalandira salary, ndiye funso nali, ndindani amene amapita kokalandira salary akulira tipeza kuti palibe wina aliyense amakhala osangalara kuti lero tikadyera nyama, ndi chimozimozi inu ndi ine mulungu anatisankha ndikutisiya pano pa dziko lampasi cholinga chimene anatisiila pa dziko la pansi ndi chani tizimugwadira nthawi ndi nthawi, ndiye tamugwadira mulungu, mwini wake emweyo yemwe timamutumikira uja watiitana tamwalira ndicholinga choti akatipase malipiro pa ntchito yomwe iye anatipasa takhala tikumugwilira tidakali ndi moyo abale amzanga sinthawi yomalira imene ija ayi ndinthawi yotchulusa kupempha kwa mulungu kumupemphelera m'bale wathu kuti ngati anali ochita ntchito zabwino mulungu amuonjezere zabwino zochuluka pa ntchito yomwe iye anali kugwira adakali ndi moyo komanso ngati anali ochita ntchito pena zoipa mulungu asachulukise kuyang'ana zoipa zake Ameen

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf 7 หลายเดือนก่อน +8

    Speech iyi ndiyofunika azungu koma ife tiziti mwatilawula😢

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 7 หลายเดือนก่อน

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah6448 7 หลายเดือนก่อน +1

    Indeed zili bwino aliyese azafa komano kuluza munthu sichithu chophweka nde kumankhala makolo ako

  • @TemwachiKumwenda
    @TemwachiKumwenda 7 หลายเดือนก่อน +1

    My grandma said when someone passed away within two days ,,,,,,, umawona ngat zocheza koma dikila pathe masiku nde akut zilibwino ??? Pamenepa😢

  • @samuelkapasula-mn6es
    @samuelkapasula-mn6es 7 หลายเดือนก่อน

    Zoonadi.....Zili bwino mwa Yesu khristu.....

  • @alexmaluwa4555
    @alexmaluwa4555 6 หลายเดือนก่อน

    zili bwino..,>all is well waxy

  • @ZaffboyYellows
    @ZaffboyYellows 7 หลายเดือนก่อน

    I'm very sorry 😢Your highness young king. If you want to talk ' I'm here at any time

  • @POker_On1.
    @POker_On1. 7 หลายเดือนก่อน +1

    Zibwíno 🙏🏾

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 7 หลายเดือนก่อน

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤
    0:11

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 7 หลายเดือนก่อน +1

    Osamamuchemerera mfanayu ndikape chisiru paumunthu speech umatulusa malingana ndimaro ache awa anali bambo ake osati ngt kanali kushow koziwonesera kt kaya akazi akafire zachamba

    • @LamekiSamson
      @LamekiSamson 7 หลายเดือนก่อน

      Zoonad man am gree with you

    • @fortunenthala4042
      @fortunenthala4042 7 หลายเดือนก่อน

      Ndipo ndikape

  • @LeahNundwe-wh6vz
    @LeahNundwe-wh6vz 7 หลายเดือนก่อน +2

    Today's children at their parents funeral leaves alot of questions really

    • @FaithZidana
      @FaithZidana 7 หลายเดือนก่อน

      Mmhu nanu

  • @RedKoffii-gl2vx
    @RedKoffii-gl2vx 7 หลายเดือนก่อน +6

    Mwana ulimba mtima

  • @WakisaPhiri-e1e
    @WakisaPhiri-e1e 7 หลายเดือนก่อน

    RIP Pastor 😭 Anthu awa amkavana

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 7 หลายเดือนก่อน

    Mwana wamuna azikhara olimba mtima choncho waxy mbiri yako yabwno umakhara bwno ndi bambo ako ambuye akuze malire amoyo wako ndi abale ako😢

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug 7 หลายเดือนก่อน

    Sizilibwino ndizolilitsa kwambili 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @Choicemw
    @Choicemw 7 หลายเดือนก่อน

    Yesu analira pa maliro a Lazaro

  • @Mazexifeyoh
    @Mazexifeyoh 7 หลายเดือนก่อน

    Powerful

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo 7 หลายเดือนก่อน +1

    Chitsiru chamwana ,nde chojowera-jowera ndichani .ngati zili bwino osangoyankhula bwino bwino kupereka ulemu kwa anthu ena bwanji.kufuna kutchuka ndi uchitsiru udzazindikira bwino patsogolo

  • @jamesbowman-cw8ts
    @jamesbowman-cw8ts 7 หลายเดือนก่อน

    Koma ndiye Kuli mixed bag of comments,... Waxy this Waxy that,... aMalawi musiyeni mwana, walimba mtima ndi chiyembekezo kuti bambo ake ali malo abwino opumula ndi Yesu wawo ndipo palibe chodandaula,... Ndiye mukuti chani anthu "abwino" komanso osunga "chikhalidwe" chachiMalawi inu??
    Pena ngati ndinene kuti dikirani abambo anu akazamwalira muzayankhule speech yanu yabwinoyo,....koma poti imfa si yabwinonso. So whatever,
    Rest well Bishop Kapenga. We knew as man of God and we're sure to God your soul has returned. Rest Bishop rest🕊️🕊️

  • @AyamiPhiri-f6r
    @AyamiPhiri-f6r 7 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841 7 หลายเดือนก่อน

    Muthu akamwarila, timarila pa nthawi imeneyoyo, ndee waxy kay sanalakwitse moti speech yake ili bho ndithu.

  • @mikheykaunda3540
    @mikheykaunda3540 7 หลายเดือนก่อน

    RIP Munthu wakulu Kapenga we shall miss u

  • @Queen-m6f
    @Queen-m6f 7 หลายเดือนก่อน

    May His Soul Rest in Peace 😢

  • @maxyfreeman9691
    @maxyfreeman9691 7 หลายเดือนก่อน

    Kaya mwanayu sanasute koma

  • @BestMtawali
    @BestMtawali 7 หลายเดือนก่อน

    Ndalama unadya zacosoma zja nyimbo zake ndizit unaimba?????😩😩😩😩

  • @chemapa
    @chemapa 7 หลายเดือนก่อน

    zabodzazo zosamvekazo Mulunguyo anamuuzira kuti? pamaliro sitchukira. tisamaseweretse dzina la Mulungu. kulowetsa chibwana pamaliro a mtumiki wamulungu.

  • @nkosikhonasiphiwemdlalose227
    @nkosikhonasiphiwemdlalose227 7 หลายเดือนก่อน +1

    Some of the tribes in Zim they celebrate when they lose someone zili bwino akapumule ali ndi Yesu wao

  • @kondwanibuleya-br9gr
    @kondwanibuleya-br9gr 7 หลายเดือนก่อน

    😢 what a man up

  • @YamikaniThoko
    @YamikaniThoko 7 หลายเดือนก่อน

    Km ine kaya ndi chimodzichi km speech yi sinandivekere mwaumunthu

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 7 หลายเดือนก่อน

    Mau abwino kwa munthu olungam

  • @GetrudeGama-gu5rb
    @GetrudeGama-gu5rb 7 หลายเดือนก่อน +1

    Zowonadi ziribwino kwaiwo kwantha kwatsara kwaife

  • @billykamwendo6517
    @billykamwendo6517 7 หลายเดือนก่อน +1

    Ife ndi a Malawi, izi nzachizungu ndipo naaa ine sindingayankhule chonchi ali oti ndi bambo anga.

    • @TadalaChithope-yg9fo
      @TadalaChithope-yg9fo 7 หลายเดือนก่อน

      Azibambo nthawi zambili amakhala olimba mtim and uyuso panja mean oyamba ayenela kukhala strong komas tiyamike kut bambo ake amwalila waxy atatembenuka mtima komas kwaimayife zovuta kom kwa mamun ngt uyu akudziwa chomwe akuchita komas mwa okhulipilila izi zosavuta ngt munawon live yadzulo mayi ake okhala akaz awo anayimba nyimbo xa phamvuso coz ndi anthu okhulupilila and akudziwa kut akuyakhula mulungu wawo

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa 7 หลายเดือนก่อน +1

    Sitinazolowele spech ngati izi kuno kwathu

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 7 หลายเดือนก่อน

    Wakhutu la uximu wanva

  • @CatherineKumwendaCatherine
    @CatherineKumwendaCatherine 7 หลายเดือนก่อน

    Kwa munthu oti amaziwa za kumwamba mwana wayakhura zomwe Mulungu amatilimbikisa pamavuto or pa Mtender tiziti zili bwno

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 7 หลายเดือนก่อน

    Ku show kapena maliro

  • @eltonnankhwere3284
    @eltonnankhwere3284 7 หลายเดือนก่อน

    Of course am satisfied with the speech it seems unakonzeka ngati ukupita
    ku show.i remember you wrote kuti tiyeni mawa tikakumane pa Robins Park ndikaimba nyimbo in other way its not fitting

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 7 หลายเดือนก่อน

    Wavala mzimuwamji mwanau

  • @ShyreenKwisongole
    @ShyreenKwisongole 7 หลายเดือนก่อน

    Emen

  • @Mphatsolikotima
    @Mphatsolikotima 7 หลายเดือนก่อน

    Rip bishop kapenga 😢

  • @marryrobert7092
    @marryrobert7092 7 หลายเดือนก่อน

    A malawi uziwa kurangiza mwana warakwa chani kod simuziwa kuti muthu akafa sibwino kurira mokweza ndemumatu iyi azirira

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 7 หลายเดือนก่อน

    Owooo chabwino

  • @juaojacojunioh
    @juaojacojunioh 2 หลายเดือนก่อน

    ubusa uli mwa iwe bra

  • @FranckieDambah
    @FranckieDambah 7 หลายเดือนก่อน

    Eeeeee waxy umatha kuyankhura

  • @MarthaMfulusa-vj3xe
    @MarthaMfulusa-vj3xe 7 หลายเดือนก่อน

    Strange

  • @replacefruittreenursery
    @replacefruittreenursery 7 หลายเดือนก่อน +1

    Guys mwanai watani kodi
    Paribe muthu amasangalala pa ifa ai .
    Uyu wandikaikisa chabwino R.I.P pastor kapenga

    • @HannahChingwalu
      @HannahChingwalu 7 หลายเดือนก่อน +1

      Chakaikitsa pamenepo ndichani?? Akuyenera kutero kumene chifukwaso zili mmalemba Mulungu ananena kuti kwaikika kwamunthu kufa,,chamoyo chilichonse chikuyembekeza imfa Ambuye alemekezeke chifukwa wakwanilitsa mau ake,,osati zanuzo apa

  • @Ukondwa_363
    @Ukondwa_363 7 หลายเดือนก่อน

    Rlp pastel

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 7 หลายเดือนก่อน +1

    Iyi ndi lmfa osapanga zibwana kawonesa picture yanji kwa azukulu amipingo pamwambo wamaliro kakuti sharp wachani zachamba

  • @HussainGaffarOlaiza-hy9sg
    @HussainGaffarOlaiza-hy9sg 7 หลายเดือนก่อน

    💔🕊

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 7 หลายเดือนก่อน

    Muzidyatu bwino ganjayo

  • @Tryness-wb6dj
    @Tryness-wb6dj 7 หลายเดือนก่อน

    Rest well Bishop Kapenga

  • @DJcliffBandakhudzanga
    @DJcliffBandakhudzanga 7 หลายเดือนก่อน

    Waxy ndi nfana olimba mwana wamamuna adzitelo

  • @jelblinds2017
    @jelblinds2017 7 หลายเดือนก่อน

    There is nothing wrong jst that we as malawians have poor and shallow minds

  • @BudaEarth
    @BudaEarth 7 หลายเดือนก่อน

    Dadas

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 7 หลายเดือนก่อน

    Waxy akanakhala ngati chija chinthubidwa cha chilima chija akanag'alura

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub 7 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂

    • @SinyoroMoyo
      @SinyoroMoyo 7 หลายเดือนก่อน

      Eish guys 😂😂😂😂😂

  • @daziana2023
    @daziana2023 7 หลายเดือนก่อน

    Zilibwino

  • @AneesaMoosa-nv6bq
    @AneesaMoosa-nv6bq 7 หลายเดือนก่อน

    Rest in peace bishop kapenga

  • @MwayiJoseph
    @MwayiJoseph 7 หลายเดือนก่อน

    Mzimu wawo ukautse mumtendere ngati anachita bwino kudziko lapansi pakuti ntchito zako munthu zimasagana nawe

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 7 หลายเดือนก่อน

    Kuyankhula kotani uku, mwana wachibwana

  • @TadalaChithope-yg9fo
    @TadalaChithope-yg9fo 7 หลายเดือนก่อน

    😭

  • @EmmanuelNgamuti
    @EmmanuelNgamuti 7 หลายเดือนก่อน

    Young man where hv u taken the energy to make this non African speech on a day like this?

  • @YellowmanExen-nw1hy
    @YellowmanExen-nw1hy 7 หลายเดือนก่อน

    I think this man waxy mutu wako sumakoka,ngati chili chamba mmmm.are sure bambo ako apita you can say this nonsense sure?

  • @BlessingsMangwaya-mk4fi
    @BlessingsMangwaya-mk4fi 7 หลายเดือนก่อน +9

    This is not a fitting speech for the day your father passed away 😪😪

    • @lindamyaba
      @lindamyaba 7 หลายเดือนก่อน

      Be serious man, waxy mwaonetsa maturity, zili bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 7 หลายเดือนก่อน

      Sonotu anthu odziwa mawu zimaaiyana ndi osadziwa mau zili bwino basi ambuye walora

  • @SamsonChiwera
    @SamsonChiwera 7 หลายเดือนก่อน

    Mmmm waxy Kay Kuno ndi kumalawi ndye yaaa kumbali Ina it's ok kuti zilibwino koma another side this speech is useless to me when you grow up that's when you will realize that l made silly speech RIP Mr kapenga

  • @DavieChangoima
    @DavieChangoima 7 หลายเดือนก่อน

    Sorry rnp

  • @Ampambachulu
    @Ampambachulu 7 หลายเดือนก่อน

    Bro thought he killed

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys 7 หลายเดือนก่อน

    Komatu for sure now irealize rhst crying during someone's daeth is for us poor imagine what is this speech 😭😭😭😭😭💔💔end with sure
    Anyway rest well pastor kapenga