Achita bwino kuwonekera dziko linse akuwona ngati ndi ma champion koma akuziyika pamavuto. Anthu ali mbuuuuu!!! Alibe kalikonse pomwe anzawo akumipando akumwa wa mkaka. Chimwendo sapitatu ku prison apite ndi iwowo. Challenge yabwanji iyi? Ooooooh my Malawi is gone beyond ndi Chakwera.
Latha bas dzikoli chisoni changa chili kwa azigogo anga ndi nthu aulumali 😢 nanga chonchi pot ena za chipanizi ndi zovala zawo atakhala avala mwakusaziwa kut kunja kulinji sibas aphedwa sitili safe dzikoli achitetezo adapita ndi chilima😢
Chakwela ndi president wa dziko koma vuto mphamvu alibe mphamvu dzili ndi nduna osati iye ayi amachita kuudzidwa chilichose akadakhala ndi mphamvu mbwenu uchisiluwu kulibeko nde pano anthu kupanga chipongwe saopa Pena democracy iyi yabweletsa manyi pa dziko
CHIMWENDO BANDA YOMWEYO KUCHEPETSA MA VOTE YA MCP KOMA CHAKWERA SURE ANGATENGE MBUTUMA IYI KUT IPITILIZE KUWONONGA MBIRI KKKKK😂🤣🤣🤣🤣🤣 ZIKHALE NG'OMA,KUKUYU AND MANGANYA AWEEE KUDZANGOVUNDURA MCP
Koma boma lipangepo khatu pa anthu amenewo akwa nsundwe , bima likakhala chete iwoo achigao chonse cha pakati aziganizile okha chifukwa iwo Alipakati kuli ku mpoto ndi ku mwera
kuno ku south africa ufuku umakhala mmanja mwa anthu koma saphwanyilana magalimoto kamba ka zipani olo dera ayi ayi kona ma demo ndiye amapangidwadi but stupid mcp young people kusaphunzira basi anyani
Amwene vuto ndi chimwendo
Cox ndamene anayambitsa kuyankhula mawu wobwetetsa nkhondo
Ndipo mwa chakwera mulibe utsogoleri ndipo ndikape komanso chitsiru cox mtdogoleri wanzeru sayang'anira zopusa
Ndipo nyasi zokha zokha mmm
Achita bwino kuwonekera dziko linse akuwona ngati ndi ma champion koma akuziyika pamavuto. Anthu ali mbuuuuu!!! Alibe kalikonse pomwe anzawo akumipando akumwa wa mkaka. Chimwendo sapitatu ku prison apite ndi iwowo. Challenge yabwanji iyi? Ooooooh my Malawi is gone beyond ndi Chakwera.
Aka kachitatu akuphwanya ndikumenya anthu a DPP, a police aliphee kumangoyang'ana ndikumatenga Kaliati opanda mulandu. Thanks tibweza
ndipodi sindikuziwa kuti bomali likuganiza bwanji
Kodi ku DPP kulibe anyamata azitho odziwa kupambadza ???
Chifukwa sikoyamba mcp kupanga zopusazi , basi kumangosekelelabe ndizopusa zonwe ??
Panopa tisamayendele kuti police ilowelele ,
Because malawi police is very very useless and foolishness .
Kulakwa kwambiri ukutu eish
Ana a chikangawa awa, koma dziko laphwekadi mweee ndi awa omwe kupangitsa road block zoona????? 💔💔💔
Komatso,inu abale.anthuwa,akuoneka kuti,sidziyenda,koma boma lomwelo,lozudza zithu zadula cement ndi zinna zotelo koma ndindalama zingati zomwe akupasidwa.aaaaa,boma la chakwela lalephela,kutetedza.izi,atha kuchitila abale Athu ndikunena monenetsa,azatsiya,achakazawo ndi ana.
Anthu ozolowera kukumba mbewa ndi choncho
Latha bas dzikoli chisoni changa chili kwa azigogo anga ndi nthu aulumali 😢 nanga chonchi pot ena za chipanizi ndi zovala zawo atakhala avala mwakusaziwa kut kunja kulinji sibas aphedwa sitili safe dzikoli achitetezo adapita ndi chilima😢
Ine monga wakuno ku nkhata bay mutonga weniwemi.
Ndingofusa kodi apolice asilikali akuno kumupoto asilikali ndi apolice akumwera mdi kumawa wose akuopa lilongwe ndichifukwa chani anthu apakati akuziva nchochi iyi ndinkhomdo wait and see zimene zichitike mumalawi
Akulemekeza maganizo achikwanje ,achina chisale ndi anamalomba
Amenewa akufunika apezedwe asatenge ngati dziko ndila mcp we are in democracy
Chakwela ndi president wa dziko koma vuto mphamvu alibe mphamvu dzili ndi nduna osati iye ayi amachita kuudzidwa chilichose akadakhala ndi mphamvu mbwenu uchisiluwu kulibeko nde pano anthu kupanga chipongwe saopa Pena democracy iyi yabweletsa manyi pa dziko
CHIMWENDO BANDA YOMWEYO KUCHEPETSA MA VOTE YA MCP KOMA CHAKWERA SURE ANGATENGE MBUTUMA IYI KUT IPITILIZE KUWONONGA MBIRI KKKKK😂🤣🤣🤣🤣🤣 ZIKHALE NG'OMA,KUKUYU AND MANGANYA AWEEE KUDZANGOVUNDURA MCP
Anthuwatu nzotunidwa ndipo apolisi anali atadziwa kale koma sangachite kanthu
Ayi tawona kumene apite nazo ngati iwowo Alibe azitsongoleli, atipeza mbali yakuno
Amalawi tidziwe Kuti iyiyi ndinkhondo ngati mtsogoleli samadzudzula zimenezi mukumbukile ku libia nkhondo inayamba bwanji? inayambilat musika kumayambana okhaokha Adani analowelelelapo apa sizikusiyana tikumayambana tokhatokha Mapeto ake ndinkhondo
Apolisi awamange anthu amene anali pa nsundwe kutseka nsewu. Boma lichitepo kathu izi sizoona, anthuwa siapolisi mwanji akupanga roadblock pansewu.
Iweyonso ndiwe chitsiru mesa umamukalipila ngati makwana munthi una nde apa ukuchita kuwanyengelera naweso ndi wa mcp galu owe chitsiru nyani galu
Kodi mmesa chakwera anaronjeza ntchito onemirion za achinyamata ntchito zija ndizomwezoka moti panopa achinyamata ambiri akupeza zochita mboma rimeneri kkkkkkkkk
Ndiye ntanyiwa akalankhula mukuti ndi propaganda, look now.
And why Malawi ndi watonse ❤Malawi 🇲🇼
Ango pita ndi thilakki ukokolora osewo ndiye kuti chakwera azipanga msokhano koko basi ngati zikhare chocho azindikire iwo mawa zizakhala bwanji
Anthu opanda umunthu awa mukugona nd njar mulipo wakupangiran chan lazalo wanuo anthu aleke kudutsa chifukwa cha zitsiru inuo nd nthaw ya campanie kaa ino
Where is the police in this kodi Apolice whom do you serve Malawians or politicians
Akanakhala adpp atathamanga
aMCP akutenga dzikoli ngati ndilawo chauta wakuona chakwera unalidwe pastor ?
DPP must stop talking nosence.coz niamene akupanga inciet violence awa akungobweza zomwe ma cadet amapanga kummwela
fundo zachikwanje zimenezo 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Koma where is our Malawi Defence Force
Tione mmene MCP ipangike pano pankhaniyi anenando kuti ndi adpp onwe?? nanga roadblock iyo ngati ya mzimbabwr bwanji pali mbendeta a ng'ona party??
Ineyo guys i dont understand kt ili ndi dziko kapena ka village chabe
Eeeee kma xibwino chichi
Kujaila kwambiri
Vuto ndi umbuli ndale sapanga chonchi
Wakamba chilungaamo ndiwe onganiza kampeni amaponda palipose azikudalisani
apolis mukungo Yang,anila zimenezi kodipakati apainu apolis ndi anyamata amenewa oyenela kuteka nseundindan
Pamenepo sipachitika mulandu wa felony koma?😅
Aaaa ndale zakumalawi zausatana mulibemo umulungu zipani zangosaduka zipembedzo zochitilako zoipa
Ndichimwendo Banda ameneyo ndipo kamachende ameneyu
Anthu agwirisiwa ntchitowo ndikusamba kumene sadziwa umbuli ndi kachilombo ndithu
Kwa nsundwe sikumalawi😂
One million jobs uja NDI imeneyi ..ija chikangawa adalonjeza kkk
Paja a. Dpp amayenda ndi zikwanje mmagalimoto musamve kuwawa
Tifunilanji umboni wina apa?kma a mcp apapa angakane?
First class fool
Ineyo ndi mchewa km too minute inayake achewa ndi ofoila aah
Achisale please tiyeni tiyambe kubwezela anthu akupha chilimawa ationjexa
Koma ndiye mwafikapotu, mpaka roadblock anthu wamba?
Ndisamukira ku Karonga.
🤦🏽♂️🤦🏽♂️🇲🇼.
Ku kalongako ndi dxiko lanji kkkk
Anthu ake osasamba ooneka kuti sakudya mokwanira zitsiru zanthu
Anthuyake akupanga zimeneziwa osasambaso ndiyawo
Pano or ndi nyau zomwe zatasatu ku lilongwe kuno zigawenga zikubisalira mu dzina la nyawu.
Mwaiwona mbindelayo ndiya mcp nde sangamangidwe chifukwa zikuchitikazi ndizaboma lolamula
Chakwera simunthu WA bwino ndi galu
Kodi a police ndi arm alikuti ?Kodi awa amyamatawa afikanso poika RoadBlock
Koma boma lipangepo khatu pa anthu amenewo akwa nsundwe , bima likakhala chete iwoo achigao chonse cha pakati aziganizile okha chifukwa iwo Alipakati kuli ku mpoto ndi ku mwera
Achimwendo banda NDA chisiru mburu ya minister opusa kwambiri
Ana amaskin awa
Anthu akenso osasamba ali mbuuuu ngt ngawu
Nawoso a MCP adziwona kumwela kuno ndi nkhondo mwayi yambayi
Koma chakwera ngati sadzudzula nduna zake ndekuti akudziwapo kanthu
Chakwera mburi ndithu no more mcp ever
Where's police akungoyan'ganila wosachitapo kanthu pmf???
Ndikamava kut anyamata akwasu dwe ndmaona ngati osamba kodi nd zasasamba chonchi zosowa zochita
Dziko ili lilimmanja mwa gule wamkulu 😢😢😢
Let the police do their job or else zivuta izi
Kummwera asabwelekonso kudzapanga misonkhano yawo amakanjawa
Zonyasa muziko zimenezo kulibe police kumeneko aaaa
Ndibwera komweko ndizakuvinireni jando ndi pulesidenti wanuyo
Izi ndizotumidwa ndi chinkhumba kmnso kamajekete km masiku akupita tidzawona pokolola popeza siife ana ai
Police ya Malawi ndi MCP chikangawa party
Where is MDF please how can you allow this happen in the country where there is Police and Army sham on you MDF staff you're weak.
Ndiya MCP palibe chomwe angapange
@@GreyMtungamaNdipo brother eeeeee MCP guys mmmm
Koma guys MW watani kod? Eeeeh
izi zakunyasani munakondwa ndimau amzimai kuphalombe kuja
Zitsiru za anthu pali owopnso alibe nkathu komwe agalu
Kusowa khalidwe
Shipani ndi cha manyi cha MCP zikapitilila nafeso tisatila maganizo awo
dpp inayambitsa zoyipa kumati ku phalombe chimwendo asafikeko kugenda chakwera
Big MCP ndiyazitsiru zokhazokha zimasapota zawo zitsiru atsogoleri zitsiru zokhazokha Koma tibweza wait n c
Sopano ma foreigners aziwona chisawawa chotere
May God punish poverty
And more over ma video alipo apezedwe ndithu
Koma shame mbiri ndiya Chikangawa
Gayz mudzifufuza kaye musana falitse anthu ake atatuwo aaaa bodza ili musakokomeze chifukwa ndiwe wadpp
Kkkkkk koma abale nsudwe boyz
Choncho akamangidwa azinena kuti boma ili ndiloipa.
Umbuli ndi msanje
Boma lokomela tonse lija ndili meneli? Zoopsatu
Idzi ndinyasi komaso manyi ene
Komaso chakwerayo akudziwa po kathu
Achewa inu moyo opusa tu umenenewo mwaona ngt dxiko ndilanu
Akuononga chipani amenewo musawa sekelele
This is too much, kujayilatu uku.
kuno ku south africa ufuku umakhala mmanja mwa anthu koma saphwanyilana magalimoto kamba ka zipani olo dera ayi ayi kona ma demo ndiye amapangidwadi but stupid mcp young people kusaphunzira basi anyani
Ths is unexceptional acts
Osangowa womba mbanji
Ichi ndie chibwana chenicheni
Aku jejemera kkkk DPP boma
Mapeto ake dziko ligawanika
Nanenso zandinyasa
akhoza inu mudagenda chakwela
Lidzakwana la 40 bro osadanda