Ndipo boma lokomeladi aliyese osati lakupha kuba ndi kuononga la satana chakwela muthu oti kukamuchela kumangoganiza za upandu basi ndipo mulungu achilange komwe chiliko mawa chisazuke
Akadzawina azachonse, American embassy,ngati sazatelo,azachonsedwatso.amalawi,tilibe two koloko.ichi,chilipochi,chichoka,2025,ngati sitichichotsa,ndi ma demo
Alimi ife fertilizer ndi otchipa urea ndi 85000 koma tikugulitsa two bags ya chimanga kugula thumba ali pa 21000 timagulitsa matumba 7 kt tigule thumba limodzi alimi sitikudandaula fodya amagula no sale lero 600000 bale limodzi tikuva kukoma chakwara 2030 wooooooo
Tsanko lija adzasiya kod kubera alimi fodya adzasia njanje akozayi sadzaletsaso kod auction Canberra 42billion abweza kod malawi leaf 🌿 adzayipatsa ndalama zogulira fodya anayiberayi kod? Ma no sales anja anali ku auction mufuna abwereso kod dpp ndi alimi ndiye ayi sitiyifuna or kuva dzina
May God bless you, so that you can save Malawi from the mouth of thugs.
May Allah protect this man
Please muzasiseko cement ndi malata nyumba yanga chiimileni mu 2021
Apm my vote
Ndipo boma lokomeladi aliyese osati lakupha kuba ndi kuononga la satana chakwela muthu oti kukamuchela kumangoganiza za upandu basi ndipo mulungu achilange komwe chiliko mawa chisazuke
Akadzawina azachonse, American embassy,ngati sazatelo,azachonsedwatso.amalawi,tilibe two koloko.ichi,chilipochi,chichoka,2025,ngati sitichichotsa,ndi ma demo
Mwina fertilizer uja mkufikanso pa 21 pin paja osati 100 thousand 1 bag, olo atafika pa 35 bolabe
agogo msanamize anthu aaa lokomera zigewenga za chilomwe aaa mwakalamba echi mcp simungayi2ine inu mwachepa kwambiri
Alimi ife fertilizer ndi otchipa urea ndi 85000 koma tikugulitsa two bags ya chimanga kugula thumba ali pa 21000 timagulitsa matumba 7 kt tigule thumba limodzi alimi sitikudandaula fodya amagula no sale lero 600000 bale limodzi tikuva kukoma chakwara 2030 wooooooo
Dinner ija imenei?
Mukawagwira asilikali a ku ruandawo mungoapha tione kuti mbuyawo anena kuti chani.
Winayo akut ooh yes zaziiii
Ana achakwela mulibwanji pano mukumva nyunyutu apa😂😂😂😂😂
Mmmmmmm Inu znakukanikan kale mukunamapochan apa tyen uko isaaah!!!!!
Boma iloooo
Boma lake la ntholotu nanga lomweli ndikuliziwali,zanu zinapita bs koma ngati boma la nthyolo mukuza kukawina bs
Boma ilooo
Tsanko lija adzasiya kod kubera alimi fodya adzasia njanje akozayi sadzaletsaso kod auction Canberra 42billion abweza kod malawi leaf 🌿 adzayipatsa ndalama zogulira fodya anayiberayi kod? Ma no sales anja anali ku auction mufuna abwereso kod dpp ndi alimi ndiye ayi sitiyifuna or kuva dzina
Zachipani amakapangira kunyumba kwamuthu mugofuna kumumalizira tindalana tinatsala apm ana adad mmagalimotomu mudzayabeso aaaa zosatheka mulungu salora kt mudzabeso zinakukwanani zomwexija manyazi mulibe? Athu atsakho lodutsa mlingo misewu mumakoza ku mmwera kokha agalu
Same what's up group! Unless you change otherwise malawi will remain a farm of politicians.
A dad liomboleni dziko lanthu moto
Nonsense
Zaziii ukhutukumve uja mwasiya😮😮
I think you should rest sir why African leaders you have been tried and rejected don't take advantage of the people please
inu agogo msanamize anyh1
Sindikunva
Lakula ndi dyela nukalowa boma muzayambilanso zanu zija aaaa