Devil at work, let's pray for our country, iyi ndi mphulupulu ya dziko imene imabwera cifukwa utsogoleri woyipa wa atsogoleri adzikolo Mulungu amakhala kt wacenjeza, waunikira atsogoleri kumangovitabe zoipa as result, amalola oipayo alamulire nkwiyo wa Mulungu then mukupwetekesa anthu osalakwa
Lero ndatsimikizadi kuti Bon Kalindo Mulungu amamungwilitsa ntchito ndikudziwa ambiri simuvomeleza mudziti amapangira zimenezi ndale koma aiii ndithu Mulungu anamusankha Bon Kalindo Ngati momwe anachitira ndi Mose kwa iguputo kuti akatulutse ana Israel ( GOD BLESS YOU MR KALINDO🙏)
Ndiwe munthu wa nzeru kwambiri iweyo kuzindikira zimenezi
Ameen
Kod athu ndinu otani Muthu akunena zabwino bwino.inu mukut chitsilu.zangozizo zimukumva.
Anthu enatu anangobadwa opusa amangoikila kumbuyo zilizonse.akuti sakuona vuto
Eti inu
Kuyambira lero boni Kalindo ndizikuyitana Mose wa Lero. Soka limugwera munthu odana ndi iweyo
Simunaonepo mfiti? Wina aliyense amene akujijirika ndi MCP ndi mfiti. Achakwera anangobaya chidole chija ndi jakison ku Malawi kunachitika ngozi.
dziko lamalawi eeeee panopa lafika poopsa kwambili
Ndipo inenso ngoxi zimenezi nduudabwa nazo ..Ambuye Mulungu alowererepo
Nanu a fire akumalawi amawelengela za anthu
Mmmm pakana 3days osapeleka what's going on
Ya 🔥 yinabwera
Satana woyamba ndi kalindo enawoakungomalidzitsa, munthu akuti akumenyela ma ufulu anthu wosawuka, anthu ake ati anapitako kukapempha kwa anthu andale ngati iyeyu? Ndili linen anayamba wakapelekako sopo Kwawosawuka akunenawo kalindo, bigiiiiii and smart develop usadyele pamutu pa amphawi moto waselufule ukukudikila
Chakwela amakatani kwa papa Francisco
Zoona.tipephele.amalawi
Ng'alulazation
Ameen
Big devil
Devil at work, let's pray for our country, iyi ndi mphulupulu ya dziko imene imabwera cifukwa utsogoleri woyipa wa atsogoleri adzikolo Mulungu amakhala kt wacenjeza, waunikira atsogoleri kumangovitabe zoipa as result, amalola oipayo alamulire nkwiyo wa Mulungu then mukupwetekesa anthu osalakwa
Today is 24 don't forget
Chakwera ndi wa satanic aliyense amadziwa munthu woyipa
Ili ndiy bodza malamulo afiti sanabwele ler or chakwela anawapeza kamban zina awinik
Yamba kupemphela aisey nthawi yatha uchedwa nazo
Ndiwe mfiti iweyo komaso satanic.
Mudzazindikila but very soon. Choopsa chikudza
iiiiiiiiii.ndipo.zoophwa.kumalawi athungati.agalu.kufa.iiiii.ambuye.atithandizendithu
He says andale adayika malamulo woyipa not Chakwera. Listen again
Choka iweee mbuli ya munthu
Wasala ndiwe usamale
Mbuli ndi iweyo amene sukumva kuwawa kwa imfa zikuchitikazi mpaka wina wakwanu atafa
Chitsiru
Kagwere uko pedegu iwe 😢
Chakwera ndi wa satanic aliyense amadziwa munthu woyipa