Achakwera Sakupanga Zinthu Mmene Adalonjezera | Wina Wazuzula Mmene Zinthu Zikukhalira

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 มิ.ย. 2024
  • #chakwera #chilima #malawi #trending #news

ความคิดเห็น • 53

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 วันที่ผ่านมา +5

    Mwayakhura bwino kwambiri ❤ ndipo athu awa achoke mwankhaza mademo achitike ife tikumva kuwawa amalawi

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa 2 วันที่ผ่านมา +4

    Afiti awa a Congress, Congress singasinthe ndi ng'ona zokhazokha izi aaaaaa

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 2 วันที่ผ่านมา +5

    Ndipo zachita kuonetseratu kuti ngozi yandege imeneyi anachita kukoza zimenezi imene taluza abale athu 9 imfa yamamgawa simasowa ayi Lazaro ndi anthu ake ndi dzigawenga

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z 2 วันที่ผ่านมา +4

    NO PAIN NO GAIN TIYEN PASEO ON 10 JULY BASI CHAKWELA ACHOKWE BAS WALEPEL NO PAIN NO GAIN

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 วันที่ผ่านมา +1

    Kulankhura mwa nzeru uku koma oipa adana nazo.Wandale amafuna atakhala zaka zochuluka paudindo yet akapeza mwai mmalo mogwira ntchito to gain trust kwa anthu onse amakhara busy ndi 'kwapsya tonola' mkumaembekezera kuti akaba ndalama ,ndalama zomwezo azapangira campaign kuti awine.Chitani zinthu zabwino kuti zabwinozo zizakupangireni campaign zokha popanda kuononga ndalama zanu
    Mwai munapatsidwa ,mukuutaya nokha

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q 2 วันที่ผ่านมา +3

    Tilankhulireni anzathu inu ife atitseka pakamwa akuti tisamalankhule
    Mau anphanvu amene mwanena ndithu ambuye akudalitseni
    Ifeyo nde tikulira misozi yathu sidzatha 😢😢😢

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 2 วันที่ผ่านมา +3

    This guy is saying zoona, just imagine celebration ya ku sankhidwa kwa Mr Usi ngati VP? Shame shame

  • @user-rm2xv8ys1i
    @user-rm2xv8ys1i 2 วันที่ผ่านมา +3

    Vilombo ivi

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 2 วันที่ผ่านมา +2

    Your speech is good bro, keep it up

  • @HamidaIweni
    @HamidaIweni 2 วันที่ผ่านมา +2

    Mwandiyankhula bwino kwambili❤

  • @TamalaSoko-vg5wq
    @TamalaSoko-vg5wq 2 วันที่ผ่านมา +2

    Munena zoona brother ambuye akudalitsen

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r 2 วันที่ผ่านมา +1

    Vc president ameneyo ngamene agulitsa Chilima amene amakonza zothetsa Tonse Aliance. Iye, pamwambo anati; Chakwera ndi wake komanso Chilima ndi wake. Kodi pamene amanena izi, Chilima ali kuti?

  • @yohanezimba8329
    @yohanezimba8329 2 วันที่ผ่านมา +2

    The problem is Malawians make decision during anger, and 2025 will do the same similar choice because of anger.
    Others they are speaking as if they are wise but the true sense these people if they happen to be chosen they will also worsen this country

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r 14 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Exactly the point

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Poor people feel the pain right now

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 2 วันที่ผ่านมา +2

    Ndi agalu awa brother palibe zonse analonjeza zaboza zonkhazonkha chilibe zeru iiiiichiiiii

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera achina zikhale ng'oma and other team opusa zitsiru za anthu oma ankhula America English koma athu opusa ngati nsima

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x วันที่ผ่านมา

    Security departments kusanduka ya a chakwera aaaa zokhumudwitsa kwambiri 💔
    God knows everything.🙏

  • @TadalaPaul
    @TadalaPaul วันที่ผ่านมา

    Umumu muli mfundo guyz i proud for you vp

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc 2 วันที่ผ่านมา +1

    Ulamuliro upusa even mwana wachichepele sangaganize mopusa ngati chakwerayu

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 15 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Yonseyi ndi mission ya chakwera, koma iye akutsogoza anzake iye azamka kuti sikumanda basi a chakwera be careful pple we watching you 🖕

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 2 วันที่ผ่านมา +1

    4:10 4:10 4:10 4:11 4:11 4:12 4:12 4:12 4:12 4:12 4:13

  • @MphatsoChengetani
    @MphatsoChengetani วันที่ผ่านมา

    Very good speech

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 2 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwera sangarire ayi chifukwa iye.niamene.wapha.chirima kkkkkkkk mubusa kumuchosa ku mzuzu.kukamusiya.ku lirongwe amafuna kuti akamuphe.ndipo akamudwe ku nyanja kuribe magazi ndeno amafuna magazi kkkkkkkk koma chakwera sataniki

  • @user-be3is8rc4r
    @user-be3is8rc4r ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Good speech

  • @hussenadam3786
    @hussenadam3786 2 วันที่ผ่านมา +1

    True Malawian

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op 2 วันที่ผ่านมา +1

    Kuyakhula kwa bwino

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 2 วันที่ผ่านมา +1

    Alibe nzeru awa

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 2 วันที่ผ่านมา +1

    Akulephera kumanga kumkuyu okupha Allan witika koma kulimbana ndi bon kalindo mcp ndi ya satanic

  • @PetroMatias
    @PetroMatias วันที่ผ่านมา

    👍👍👍👍👍👍👍gud

  • @PatriciaMbewe-xn7ke
    @PatriciaMbewe-xn7ke 2 วันที่ผ่านมา +1

    Chipani ichi 🙌🙌 ndimkangomva ine

  • @GrolyGondwe-e9s
    @GrolyGondwe-e9s 2 วันที่ผ่านมา +1

    Zilombo zimenezo

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 วันที่ผ่านมา +1

    Muone ma tie amene ali pakhosi atau afira magazi okhaokha. Onani chithunzi chili pa video imeneyi.

  • @OwenNyangu-nv1yt
    @OwenNyangu-nv1yt วันที่ผ่านมา

    Adafa pa mdipiti wopelekeza maliro aja samalawi? Kodi Malawi ndi anthu amayina okha?

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 2 วันที่ผ่านมา

    Tiyeni Amalawi tigwilizane anthu awa achoke basi

  • @EssaPindani
    @EssaPindani 2 วันที่ผ่านมา

    Koma walephel kuyendesa malawi unku uyu achoke

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp วันที่ผ่านมา

    Namu bwana mukuyangu rabwinino man big

  • @WisdomBlack-uu7zt
    @WisdomBlack-uu7zt 2 วันที่ผ่านมา

    Za kugwa kwa ndege akudziwapo kathu awa ndichifukwa bwana aja anauzidwa kut ndege malo

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 2 วันที่ผ่านมา

    Malawi tinagulisa uyuu

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale 2 วันที่ผ่านมา

    Sitikusowanso zabwino kwa afiti amenewanso atsala ndi masiku owerengeka

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili วันที่ผ่านมา

    Munthu asanafe mumayamba kugontha nimukhutu

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx วันที่ผ่านมา

    A nkava kuwawa mu mtima ankangonena zimenezo koma sakugona asiyeni azuze anthu tsika mu mtengomo a tipeza a Malawi pansi pano

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 2 วันที่ผ่านมา

    Evil men,Greedy, Jealousy men. Wait for your judgement day. Mulingati abwino popeza nyansi zanu zabisika

  • @ziyamikanmakowa5981
    @ziyamikanmakowa5981 วันที่ผ่านมา

    Mfiti za anthu izi

  • @raphaelfanuel4608
    @raphaelfanuel4608 2 วันที่ผ่านมา

    Inu simunalemekeze maliro asanachitike bwqnjiii

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq 2 วันที่ผ่านมา

    😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @AckimMhango-v1x
    @AckimMhango-v1x 2 วันที่ผ่านมา

    You are talking

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc 2 วันที่ผ่านมา +1

    Democracy will never demolishe we are in new generation

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o 2 วันที่ผ่านมา

    Yankhulani tikumveni

    • @chachaamoah3592
      @chachaamoah3592 2 วันที่ผ่านมา +2

      Wa MCP sasowa uyu.mulibe nzeru MCP boma lazitsiru

    • @user-re7fo3be2z
      @user-re7fo3be2z 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Machende ako

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 2 วันที่ผ่านมา

    4:10 4:10 4:10 4:11 4:11 4:12 4:12 4:12 4:12 4:12 4:13