Chakwera Apangisa Mkulu Wina Kuzuzula Achewa

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024
  • #chilima #chakwera #news ##malawi #trending #viral

ความคิดเห็น • 103

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 หลายเดือนก่อน +12

    Uku ndiye kulankhula, munthu ozindikila ameneyu. Zoona zokha zokha ❤

  • @MphatsoMwale-it4xd
    @MphatsoMwale-it4xd 3 หลายเดือนก่อน +3

    Inu akulu mulungu apitilize kukuoneserani

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 หลายเดือนก่อน +3

    Amalawi MCP yawonongadi dzedi iiii dzomvutsa chitsoni anthu akulila pankhani chuma ndikuphatso chilima inu a MCP agalu kwabasi

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI 3 หลายเดือนก่อน +4

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 3 หลายเดือนก่อน +3

    Odhala Inu ndi oganiza bhoo

  • @VladimirThagreat
    @VladimirThagreat 3 หลายเดือนก่อน +3

    Umunthu uwu kumayankhula mmeene zilili

  • @IbrahimPhiri-ky5jk
    @IbrahimPhiri-ky5jk 3 หลายเดือนก่อน +8

    ❤❤❤ ukuoneka nkhati unayendako pang,ono amwene mchifukwa chake mulungu akusegulako manso mulungu apitilize kukuonensa manso phenya

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 3 หลายเดือนก่อน +2

    Odala inu ndi olikonda dziko lanu komaso ndiinu munthu odzindikila ife tabadwila mu mtandile achewa amakonda tea lero sugat ndi 5000 from 500

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 หลายเดือนก่อน +3

    Iwe wayankhula zenizeni mwana reality yeniyeni

  • @kaungabondera892
    @kaungabondera892 3 หลายเดือนก่อน +3

    That's true

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 3 หลายเดือนก่อน +6

    Ine ndine Mchewa, koma Chakwera ayi.

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 3 หลายเดือนก่อน +3

    Zoonadi ife ochewa mvitsirutu kkkk ulemu wanu wakulu

  • @AmosKalembo
    @AmosKalembo 3 หลายเดือนก่อน +2

    Iweyondiozindikila kwambili mall fire

  • @LastbornEnd-r9c
    @LastbornEnd-r9c 3 หลายเดือนก่อน +5

    Thanks for mentioning my Tribe Yao
    Watching from
    Meka Saudi Arabia

  • @DineckMalunga
    @DineckMalunga 3 หลายเดือนก่อน +4

    Chakwela bulutu la muthu kkkkk akuti tichotse katundu ameneyu waola akununkha

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 3 หลายเดือนก่อน +2

    Oputsa sitonse ochewaa olipo wena Openya nithu ah yayi dala mwatiyankhulila chamuna

  • @AlexMthunziChimpeni
    @AlexMthunziChimpeni 3 หลายเดือนก่อน +4

    Inuyo mumayitha chilungamo chokhachokha.🎉🎉🎉🎉

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 หลายเดือนก่อน +2

    Zoona big man

  • @SolomonMbewe
    @SolomonMbewe 3 หลายเดือนก่อน +5

    Achewa koma gule wamkulu basi....

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 3 หลายเดือนก่อน +2

    Mdala iwe ndiwe number one komanso chitsanzo chabwino cha mtundu wako

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 3 หลายเดือนก่อน +3

    Ndipo mchewa ndichitsiru kwambiri mapeto

  • @JamesOsman-cz9cw
    @JamesOsman-cz9cw 3 หลายเดือนก่อน +5

    From south Africa

  • @AlexNjanje
    @AlexNjanje 3 หลายเดือนก่อน +3

    Ambuye akhale nawe mdala iwe waonetsa mtima wachikondi osati anthu adyerawa akungomunamiza presedent kumaombera fiti mmanja mzothekanso presedent kukhala wabwino koma atidye nawowa akumulakwitsa mmauphungu awoo

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ndipo chilungamo a chewa ndife zitsiru koipa timangovetsera zopusa kuti ndife a mcp basi ma gofer za zii koma osatukuka mchewa basi mangovina nyau basi tayambitsa nda chewa kusankhana kwa mbiri chitikuko mwangopanga Central Region koma a chewa sitikuona eti toll gate ikapezeka kwathu kwa chatata ndi ku mchezi

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 3 หลายเดือนก่อน +1

    Muyao to the world#proudlyndinemuyao

  • @IshmaelJohn-iz1ej
    @IshmaelJohn-iz1ej 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela ndi ng'ona ya munthu

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 3 หลายเดือนก่อน +3

    Mwatiimirira Dara ngati mumaganiza choncho ndinumamuna weniweni,

  • @louismagongwa
    @louismagongwa 3 หลายเดือนก่อน +1

    kkkkk kk😅😅😅 mavuto alipo ndipo sanat nanga akadzawinas kape ameneyu

  • @AufiThera
    @AufiThera 3 หลายเดือนก่อน +1

    Live Bola ulamulilo uzipita Ku mpoto or kumwela not agaluwa mmmmm timwat magaz chakachino kusiya tiyi😪😪

  • @Floranyimbiri
    @Floranyimbiri 3 หลายเดือนก่อน

    Iwe ndiwe mbuzi kwabasi. Utsogoleli sutengela mtundu ayi koma chikhalidwe cha umunthuyo. Iwe ndi mbunde.

  • @bysongeorge3243
    @bysongeorge3243 3 หลายเดือนก่อน +1

    Uyu weniweni m'Chewa kulankhula chilungamo.. MCP eni wake ndi mizwanya yoganiza bho ya ku Mpoto ya nthawi imeneyo yomwe inayambitsa chipanichi, komabe ndale zathu zinasokonera ndi azitsogoleri ndikubwera kwa matipate..dziko linagawikana patatu ndipo timavotera kuti uyu wakwathu . Zinalakwika kwambiri ndipo tinadzala mbewu yoipa ..

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 3 หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂 mkulu iwe achewa anzakowo akuphatu

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 2 หลายเดือนก่อน

    Bora pamenepo achewa ena Ali ndi zeru ndimaganiza ngati azathu simukuzuzika ndiyetu mavuto Ali posepose sure MCP yinobwera kuzawononga dziko la Malawi

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kulankhura tchutchutchu

  • @YamieManda
    @YamieManda 3 หลายเดือนก่อน

    Kodi iwe pulezident wake uti mbuzi yamuthu iwe.akumwera kwake kuti anakupNgira chiyani

  • @SankhaniHarawaMtungambera
    @SankhaniHarawaMtungambera 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mchewa wakuzindikila uyuyu ulemu wanu

  • @nellybruhan5834
    @nellybruhan5834 2 หลายเดือนก่อน

    Why am I seeing this now
    Sindidaonepo nchewa oganiza ngati uyu.... Ine achewa amandisowesa chonena ndithu

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 3 หลายเดือนก่อน

    Ndilo zoona muwalangize ochewa anzanuwo kuti akavote moganiza bwino bwino wa nyauyo achoke basi antu apeze mdendele

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 3 หลายเดือนก่อน

    Koma mchewa wanzeru ngati uyuyu sindinamuone walankhulatu wakumva wamva

  • @TawongaGSMwale-cc2vm
    @TawongaGSMwale-cc2vm 3 หลายเดือนก่อน

    Apo mwayakhuladi Baba katundu uyu Kut alowe mu boma adalowa ndima demo kuzatulusaso katundu ameneyu pakufunikiraso pazakhale ma demo

  • @MarcosDjussa
    @MarcosDjussa 3 หลายเดือนก่อน

    Koma amalawi akanat azinganiza ngati mndala uyu Malawi 🇲🇼tikusimbalokoma kulakhula chilungamo mulungu akuendele ukhalise

  • @GabrielJulius-c1l
    @GabrielJulius-c1l 2 หลายเดือนก่อน

    Uchisilu wake mmalo mokonza dziko akulimbana ndi activist mpa kumaononga ndalama zambili chifukwa chofunafuna anthu awili pali nzeru or okamakhala alibe manyazi or chikumbu mtima

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 3 หลายเดือนก่อน

    Mchewa ntchito yake ndikuba bas, not kuyendetsa dziko ai koma amalawi ee mistake tinaipanga Kaya tiyikoza bwanji

  • @omaligeorge4296
    @omaligeorge4296 3 หลายเดือนก่อน

    Koma he is fact guys mnthuyi inu data mukutsitsayo ipindura chani kwa mnthu waku mudxi tamaganizani please

  • @Floranyimbiri
    @Floranyimbiri 3 หลายเดือนก่อน

    Mawu awa ndiwodzetsa mpatuko pa mitundu ya anthu. Tiyeni tizinena za ukapolo tilimowu osati za mitunduyi. Galu iwe undinvetse

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 3 หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂achewa dzukani wayankhuladi muchewa iwe

  • @ChifundoJohn-w3t
    @ChifundoJohn-w3t 3 หลายเดือนก่อน

    Zikomo poti mwazindikila nokha achewa

  • @henryhenry6632
    @henryhenry6632 3 หลายเดือนก่อน

    Panyini pamako iwe wava kapolo wachabe chabe

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 หลายเดือนก่อน

    Nanga choncho ochewa ozindikira zedi

  • @MagdaraneChidamula
    @MagdaraneChidamula 3 หลายเดือนก่อน

    GOD HAVE MERCY ON US

  • @LastenWesele-wq8jh
    @LastenWesele-wq8jh 3 หลายเดือนก่อน +1

    Izi ndizowona achewa ndi mbuzi zimafela ichi Chipani chagogo anthu

  • @BillySimkonda
    @BillySimkonda 3 หลายเดือนก่อน

    Kachilungamo kabwanji aka??????

  • @IbrahimJackson-i8h
    @IbrahimJackson-i8h 3 หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂 kkkkk koma abale ai kuli zinthu 😅😅😅😅😅😅

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zosayenda

  • @oscarnamirecah5386
    @oscarnamirecah5386 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂😂😅😅😅

  • @omaligeorge4296
    @omaligeorge4296 3 หลายเดือนก่อน

    Koma guys eeeh

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 3 หลายเดือนก่อน

    Nakondwa nawe nzedi

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 หลายเดือนก่อน

    Ndi mbusi zachabe chabe mcp

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 หลายเดือนก่อน

    Kuyankhula chilungamo uku

  • @chitchohistorical1036
    @chitchohistorical1036 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂😂

  • @DumisaniMhango-e4i
    @DumisaniMhango-e4i 3 หลายเดือนก่อน

    Exatly

  • @JoeMuhamadi
    @JoeMuhamadi 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂❤❤

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 หลายเดือนก่อน

    Ka mtundu kopusa!!!

  • @MamuMagombo
    @MamuMagombo 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂

  • @EdisonNakulenga
    @EdisonNakulenga 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkk

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 3 หลายเดือนก่อน

    Zoona atiranga

  • @JohnNdau-bl4op
    @JohnNdau-bl4op 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkk

  • @StewartGoma
    @StewartGoma 3 หลายเดือนก่อน

    Soon malawi will be like kenya
    Malawian are suffering living is so expensive

  • @EmmanuelKaziyenda
    @EmmanuelKaziyenda 3 หลายเดือนก่อน

    Ukunana iwe ndekuti umangokhala manja kotsa iwe udikira za ulele ubwere kuno kumponela udzawone mmmene anthu akugulira fertilizer wa cash iweyo ndiwe chitsiru not chakwera

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga 3 หลายเดือนก่อน

    ukuyenda osavara chifukwa cha uchitsilu wakowo ukufuna chakwera akupitise kwamereka mchewa wanji galuu lwe

  • @BerthaKasambala-y5k
    @BerthaKasambala-y5k 3 หลายเดือนก่อน

    Ndizowonadi km inetu ndinkadabwa kt ku marawiko kukangot kwagwa njara achewa onse amakazaza kwathu kumpoto chaka ndicha nde kumazifusa kt kodi osayesako njira zina bwanji pot akat chakudya sikut ndi nsima yokha ayi kkkkkkk wandiwaza aise mitu izigwira ntchito osamango swana ayi achewa mwanva

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 3 หลายเดือนก่อน

    Koma iwe nde mchewa weni weni wapa phata mchewa koma ufumu kuvina gule ndipo sazatheka kusintha

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 หลายเดือนก่อน

    Ndinudi dzisilu dzokonda kupha anthu machende anu achewa😂😂

  • @TerryNac
    @TerryNac 3 หลายเดือนก่อน

    Chitsilu ndi chimodzi osati a chewa onse Loma chitsilu chikuoneka

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 หลายเดือนก่อน

    Inu ndi munthu woganiza bwino kwambiri ndipo muli ndi nzeru auzeni ndithu

  • @HendryChiwezo
    @HendryChiwezo 3 หลายเดือนก่อน

    Iweyo anthu aku mwela akulamulila tanena chomwe chinachitika ku lilongwe iweyo za kwanu osati zopusazo nyawu zo nvuto ndichiyani zoti amakuyuzani anthu sumadziwa kodi anthu akukugulani mala nfi anthu akut mbuzi yamuthu

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo live sekulan maso Achewa thaw yatha

  • @ClaudiaarmandoMafunga
    @ClaudiaarmandoMafunga 3 หลายเดือนก่อน

    Zoona ife achewa tili ndi vuto

    • @Floranyimbiri
      @Floranyimbiri 3 หลายเดือนก่อน

      Vuto lanji? Mukuona ngati vuto limadza kamba ka mtundu wa munthu? Musapuse gayezi ufiti wa chakwela usakhudze achewa tonseyi

  • @DamsonSabitt
    @DamsonSabitt 3 หลายเดือนก่อน

    Iwe si chewa ayi iwe ukayelekeze ndianthu akumwela samalima ndiye apa akuwona kuti boma lapana alibe mweya

  • @AufiThera
    @AufiThera 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkk muchimina zonantoza pa president Aku mwera

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂kalikose tikanva ndi kukaona chaka chino

  • @MrUbHassan
    @MrUbHassan 3 หลายเดือนก่อน

    Mmanyang'watu 😂😂before

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 3 หลายเดือนก่อน

    Kuyanhula monga mmalawi weweni

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb 3 หลายเดือนก่อน

    Anyamata aku danbwe amenewo .

  • @alicehananiya
    @alicehananiya 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 katundu ameneyi achokedi

  • @LidasoniManual
    @LidasoniManual 3 หลายเดือนก่อน

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 3 หลายเดือนก่อน

    Mposo kobasi 😢

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 3 หลายเดือนก่อน

    Paja chakwela ndi nyau 😂😂😂

  • @HanifaTabia
    @HanifaTabia 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkk bola mukuziwa

  • @giftdavie240
    @giftdavie240 3 หลายเดือนก่อน

    What is democracy important for if it incourages tribalism. We're the people of the same nation but we're being divided because of democracy. Someone who's brain function properly will realize that the route cause of these all sources of drama is democracy

    • @HassanJameskananjie
      @HassanJameskananjie 3 หลายเดือนก่อน

      Iwe talemba nchichewa

    • @MikeMerecah
      @MikeMerecah 3 หลายเดือนก่อน

      Or English take no fundo,

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 3 หลายเดือนก่อน

      Anthu ofoiladi osangolemba chichewa bwanji?

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 3 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo koopsa zedi apapa ndikoyambadi ndikomaliza 2025 kwanu kwatha guys.

    • @TrizaGeorge-q8w
      @TrizaGeorge-q8w 3 หลายเดือนก่อน +1

      Achewa ndi athu oipa ndipo ndi athu ozikindikila achewa ndi wadziwa ndichifukwa ineyo sinamuvotele chakwela mulungu atithandize ku Malawi

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 3 หลายเดือนก่อน +1

      @@TrizaGeorge-q8w Ndipo ndi anthu achabechabe, umadziwa Nyau ineee kuvotatu sindinavoterepo chipani china chilichonse kuposa DPP Ndipo family yakwathu yonse ndiife a DPP Mpakana kale Tri

    • @TrizaGeorge-q8w
      @TrizaGeorge-q8w 3 หลายเดือนก่อน

      @@RiteRoderick koma tiphele kwambili kuti m,busa ameneu mulungu atichitile mmm ayi ndithu athu tazuzika kwambili

  • @JIMMYWATSON-ph5jg
    @JIMMYWATSON-ph5jg 3 หลายเดือนก่อน

    Mandenga wako iwe bulutu siwe mchewa chakwera sanakulakwire adakulakwila ndi abambo ndi amako kukhala osauka iwe galu kwa basi

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 หลายเดือนก่อน

    Ndiwe galu chitsilu mbuzi yamunthu choka usatinyase

    • @MikeMerecah
      @MikeMerecah 3 หลายเดือนก่อน +1

      Manyazi bwa ifeso ndi achewa koma munthuyi wanena zoona mpaka kuphana chifukwa Cha mipando nafe zikutiwawa,

    • @Aisha-db6ds
      @Aisha-db6ds 3 หลายเดือนก่อน

      Chakwela wationesatu zinthu

    • @NovassTambala
      @NovassTambala 3 หลายเดือนก่อน

      Koma mr mwalankhulatu ndi gonthi lamuthu chakwela mbudzi akulu hmmmm inuyo mwayedadi ndipo