Ndipo chilungamo a chewa ndife zitsiru koipa timangovetsera zopusa kuti ndife a mcp basi ma gofer za zii koma osatukuka mchewa basi mangovina nyau basi tayambitsa nda chewa kusankhana kwa mbiri chitikuko mwangopanga Central Region koma a chewa sitikuona eti toll gate ikapezeka kwathu kwa chatata ndi ku mchezi
Ukunana iwe ndekuti umangokhala manja kotsa iwe udikira za ulele ubwere kuno kumponela udzawone mmmene anthu akugulira fertilizer wa cash iweyo ndiwe chitsiru not chakwera
What is democracy important for if it incourages tribalism. We're the people of the same nation but we're being divided because of democracy. Someone who's brain function properly will realize that the route cause of these all sources of drama is democracy
@@TrizaGeorge-q8w Ndipo ndi anthu achabechabe, umadziwa Nyau ineee kuvotatu sindinavoterepo chipani china chilichonse kuposa DPP Ndipo family yakwathu yonse ndiife a DPP Mpakana kale Tri
Uku ndiye kulankhula, munthu ozindikila ameneyu. Zoona zokha zokha ❤
Inu akulu mulungu apitilize kukuoneserani
Amalawi MCP yawonongadi dzedi iiii dzomvutsa chitsoni anthu akulila pankhani chuma ndikuphatso chilima inu a MCP agalu kwabasi
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Odhala Inu ndi oganiza bhoo
Umunthu uwu kumayankhula mmeene zilili
❤❤❤ ukuoneka nkhati unayendako pang,ono amwene mchifukwa chake mulungu akusegulako manso mulungu apitilize kukuonensa manso phenya
Odala inu ndi olikonda dziko lanu komaso ndiinu munthu odzindikila ife tabadwila mu mtandile achewa amakonda tea lero sugat ndi 5000 from 500
Iwe wayankhula zenizeni mwana reality yeniyeni
That's true
Ine ndine Mchewa, koma Chakwera ayi.
Zoonadi ife ochewa mvitsirutu kkkk ulemu wanu wakulu
Iweyondiozindikila kwambili mall fire
Thanks for mentioning my Tribe Yao
Watching from
Meka Saudi Arabia
Chakwela bulutu la muthu kkkkk akuti tichotse katundu ameneyu waola akununkha
Oputsa sitonse ochewaa olipo wena Openya nithu ah yayi dala mwatiyankhulila chamuna
Inuyo mumayitha chilungamo chokhachokha.🎉🎉🎉🎉
Zoona big man
Achewa koma gule wamkulu basi....
Mdala iwe ndiwe number one komanso chitsanzo chabwino cha mtundu wako
Ndipo mchewa ndichitsiru kwambiri mapeto
From south Africa
Ambuye akhale nawe mdala iwe waonetsa mtima wachikondi osati anthu adyerawa akungomunamiza presedent kumaombera fiti mmanja mzothekanso presedent kukhala wabwino koma atidye nawowa akumulakwitsa mmauphungu awoo
Ndipo chilungamo a chewa ndife zitsiru koipa timangovetsera zopusa kuti ndife a mcp basi ma gofer za zii koma osatukuka mchewa basi mangovina nyau basi tayambitsa nda chewa kusankhana kwa mbiri chitikuko mwangopanga Central Region koma a chewa sitikuona eti toll gate ikapezeka kwathu kwa chatata ndi ku mchezi
Muyao to the world#proudlyndinemuyao
Chakwela ndi ng'ona ya munthu
Mwatiimirira Dara ngati mumaganiza choncho ndinumamuna weniweni,
kkkkk kk😅😅😅 mavuto alipo ndipo sanat nanga akadzawinas kape ameneyu
Live Bola ulamulilo uzipita Ku mpoto or kumwela not agaluwa mmmmm timwat magaz chakachino kusiya tiyi😪😪
Iwe ndiwe mbuzi kwabasi. Utsogoleli sutengela mtundu ayi koma chikhalidwe cha umunthuyo. Iwe ndi mbunde.
Uyu weniweni m'Chewa kulankhula chilungamo.. MCP eni wake ndi mizwanya yoganiza bho ya ku Mpoto ya nthawi imeneyo yomwe inayambitsa chipanichi, komabe ndale zathu zinasokonera ndi azitsogoleri ndikubwera kwa matipate..dziko linagawikana patatu ndipo timavotera kuti uyu wakwathu . Zinalakwika kwambiri ndipo tinadzala mbewu yoipa ..
😂😂😂 mkulu iwe achewa anzakowo akuphatu
Bora pamenepo achewa ena Ali ndi zeru ndimaganiza ngati azathu simukuzuzika ndiyetu mavuto Ali posepose sure MCP yinobwera kuzawononga dziko la Malawi
Kulankhura tchutchutchu
Kodi iwe pulezident wake uti mbuzi yamuthu iwe.akumwera kwake kuti anakupNgira chiyani
Mchewa wakuzindikila uyuyu ulemu wanu
Why am I seeing this now
Sindidaonepo nchewa oganiza ngati uyu.... Ine achewa amandisowesa chonena ndithu
Ndilo zoona muwalangize ochewa anzanuwo kuti akavote moganiza bwino bwino wa nyauyo achoke basi antu apeze mdendele
Koma mchewa wanzeru ngati uyuyu sindinamuone walankhulatu wakumva wamva
Apo mwayakhuladi Baba katundu uyu Kut alowe mu boma adalowa ndima demo kuzatulusaso katundu ameneyu pakufunikiraso pazakhale ma demo
Koma amalawi akanat azinganiza ngati mndala uyu Malawi 🇲🇼tikusimbalokoma kulakhula chilungamo mulungu akuendele ukhalise
Uchisilu wake mmalo mokonza dziko akulimbana ndi activist mpa kumaononga ndalama zambili chifukwa chofunafuna anthu awili pali nzeru or okamakhala alibe manyazi or chikumbu mtima
Mchewa ntchito yake ndikuba bas, not kuyendetsa dziko ai koma amalawi ee mistake tinaipanga Kaya tiyikoza bwanji
Koma he is fact guys mnthuyi inu data mukutsitsayo ipindura chani kwa mnthu waku mudxi tamaganizani please
Mawu awa ndiwodzetsa mpatuko pa mitundu ya anthu. Tiyeni tizinena za ukapolo tilimowu osati za mitunduyi. Galu iwe undinvetse
😂😂😂😂😂achewa dzukani wayankhuladi muchewa iwe
Zikomo poti mwazindikila nokha achewa
Panyini pamako iwe wava kapolo wachabe chabe
Nanga choncho ochewa ozindikira zedi
GOD HAVE MERCY ON US
Izi ndizowona achewa ndi mbuzi zimafela ichi Chipani chagogo anthu
Kachilungamo kabwanji aka??????
😂😂😂😂😂😂😂😂 kkkkk koma abale ai kuli zinthu 😅😅😅😅😅😅
Zosayenda
😂😂😂😂😂😂😂😅😅😅
Koma guys eeeh
Nakondwa nawe nzedi
Ndi mbusi zachabe chabe mcp
Kuyankhula chilungamo uku
😂😂😂😂😂😂😂
Exatly
😂😂😂😂❤❤
Ka mtundu kopusa!!!
😂😂😂
Kkkkkkkkkk
Zoona atiranga
Kkkk
Soon malawi will be like kenya
Malawian are suffering living is so expensive
Ukunana iwe ndekuti umangokhala manja kotsa iwe udikira za ulele ubwere kuno kumponela udzawone mmmene anthu akugulira fertilizer wa cash iweyo ndiwe chitsiru not chakwera
ukuyenda osavara chifukwa cha uchitsilu wakowo ukufuna chakwera akupitise kwamereka mchewa wanji galuu lwe
Ndizowonadi km inetu ndinkadabwa kt ku marawiko kukangot kwagwa njara achewa onse amakazaza kwathu kumpoto chaka ndicha nde kumazifusa kt kodi osayesako njira zina bwanji pot akat chakudya sikut ndi nsima yokha ayi kkkkkkk wandiwaza aise mitu izigwira ntchito osamango swana ayi achewa mwanva
Koma iwe nde mchewa weni weni wapa phata mchewa koma ufumu kuvina gule ndipo sazatheka kusintha
Ndinudi dzisilu dzokonda kupha anthu machende anu achewa😂😂
Chitsilu ndi chimodzi osati a chewa onse Loma chitsilu chikuoneka
Inu ndi munthu woganiza bwino kwambiri ndipo muli ndi nzeru auzeni ndithu
Iweyo anthu aku mwela akulamulila tanena chomwe chinachitika ku lilongwe iweyo za kwanu osati zopusazo nyawu zo nvuto ndichiyani zoti amakuyuzani anthu sumadziwa kodi anthu akukugulani mala nfi anthu akut mbuzi yamuthu
Ndipo live sekulan maso Achewa thaw yatha
Zoona ife achewa tili ndi vuto
Vuto lanji? Mukuona ngati vuto limadza kamba ka mtundu wa munthu? Musapuse gayezi ufiti wa chakwela usakhudze achewa tonseyi
Iwe si chewa ayi iwe ukayelekeze ndianthu akumwela samalima ndiye apa akuwona kuti boma lapana alibe mweya
Kkkkkkkkkk muchimina zonantoza pa president Aku mwera
😂😂😂😂kalikose tikanva ndi kukaona chaka chino
Mmanyang'watu 😂😂before
Kuyanhula monga mmalawi weweni
Anyamata aku danbwe amenewo .
😂😂😂😂😂 katundu ameneyi achokedi
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Mposo kobasi 😢
Paja chakwela ndi nyau 😂😂😂
Kkkk bola mukuziwa
What is democracy important for if it incourages tribalism. We're the people of the same nation but we're being divided because of democracy. Someone who's brain function properly will realize that the route cause of these all sources of drama is democracy
Iwe talemba nchichewa
Or English take no fundo,
Anthu ofoiladi osangolemba chichewa bwanji?
Chilungamo koopsa zedi apapa ndikoyambadi ndikomaliza 2025 kwanu kwatha guys.
Achewa ndi athu oipa ndipo ndi athu ozikindikila achewa ndi wadziwa ndichifukwa ineyo sinamuvotele chakwela mulungu atithandize ku Malawi
@@TrizaGeorge-q8w Ndipo ndi anthu achabechabe, umadziwa Nyau ineee kuvotatu sindinavoterepo chipani china chilichonse kuposa DPP Ndipo family yakwathu yonse ndiife a DPP Mpakana kale Tri
@@RiteRoderick koma tiphele kwambili kuti m,busa ameneu mulungu atichitile mmm ayi ndithu athu tazuzika kwambili
Mandenga wako iwe bulutu siwe mchewa chakwera sanakulakwire adakulakwila ndi abambo ndi amako kukhala osauka iwe galu kwa basi
Ndiwe galu chitsilu mbuzi yamunthu choka usatinyase
Manyazi bwa ifeso ndi achewa koma munthuyi wanena zoona mpaka kuphana chifukwa Cha mipando nafe zikutiwawa,
Chakwela wationesatu zinthu
Koma mr mwalankhulatu ndi gonthi lamuthu chakwela mbudzi akulu hmmmm inuyo mwayedadi ndipo