Kulibeko zosakana apa, this song was composed and recorded before all these assassinations of vp happened and messages in this song are clearly without insulting anybody but facts. We are not scared even afraid of anybody. Special messages to the composer my boy Frances keep it up for your good work.
Joice Banda anaba ndalama Kwa zimayi ndazibambo ena ochepa dziko lonse la Malawi lino mudzina lokuti atipatsa ngongole mumuuze kuti adzatenge tima ID take tomwe adatipangira kumakati tsekulitsa ma account Ku FDH kuzuza anthu osauka kumatandala Ku fdh ma account ochuluka anatsekulidwadi omwe sakugwira nthito zikanandiwawa ine ndipo zidzandiwawa mpaka kufa ambuye amuone
Woow what a good song .. this song deserve to award
I'm telling you brother he deserved to get award for this song but you know malawi 😢
Mwalo mwa award amangidwa😭😭💔
@@tyrachiumia3681Zoopsa zedi mmm
Listening to this song, misozi ikutsika. God is watching from a distance.
You can say that again
Ichi ndye chilungamo zonsezi ankanena okha ndipakamwa pawo ndye tikakumbutsa azitiophyeza.this is good song
Kulibeko zosakana apa, this song was composed and recorded before all these assassinations of vp happened and messages in this song are clearly without insulting anybody but facts. We are not scared even afraid of anybody.
Special messages to the composer my boy Frances keep it up for your good work.
He's my favourite brother ❤❤❤
Yaa that's great songs , palibe zomalozana zala apa yaaaaa❤
@@WillmotChiuimia-vr6ouNdipo koopsa zedi boss
Its all facts only koma poti boma li limadana ndi chilungamo pajatu
Very well said brotherman 😍😍
I cried listening and watching this song
😢 😭
God have mercy on our nation
I have been listening to this song for the whole day
akumusakawo ndidzitsiru munthu waphuritsa nyimbo uyu God bless you bro
Waiphuritsaditu ndiwosaka omwewo zawonso sizikuyenda taaaaaa (apolisiwo mmmmmmm hhhhmn)
Wow!!!! What a sweetest song❤❤❤❤❤❤❤❤ keep it up brother mbambande zedi eeeeee chinyimbotu mmmm❤❤❤
What a song bring us a messege of our history in Malawi
Wow! What brought me to this song? My time not wasted
chilombo pogwira ntchito ndimanganyayu
Nice song akumusaka Kut watani nyimbo ayamba kumvera yoyimbidwa bwino pa Moyo wawo ndiimeneyo
Ndipo mmmm
This song it's very good hope wayivela kale iyeyo
Nice composition well done boy
Nice song brother, nthawi zina 🌶 chimakhala ngati mwano
I love this hit guys big up bro
Good song km iye skc inaiva iyi 😭😭😭 km akanayiva sakanapita ku chikangawa
Evance and your producers u are so genius to the core,this piece drops tears from my eyes, it's tough to be a Malawian during this week in particular.
Which Evance???😢😢😢😢😢😢 This song it's for Francis Jameca bro
😭😭😭😭😭 its indeed a bitter pill bro & it has even touched us beyond the borders of Malawi. We're mourning with u
Penapake ndi bwino kukhala chete ngati sukudziwa.
❤❤❤❤ mwana wakwathu kuntchewu uyu amayimba zenizeni ndipo ayelekeze kukamumanga akaphwanyidwako uyu nde namalila weniweni proud of fj timakukonda
Good song mwanayu amatha kuyimba ndipo nyimbo yonveka bwino
Nice song ......... osaopa man ife tili mbali yanu palibe chitachitike
Beautiful song ❤
This song deserves award this year
Nice song ndipo idatuluka sanamwalire
Good song waimba ndendeee ndeee zomwe zinachitika
chomusakila ndichiyani Apapa kuZolowera kumanga anthu DPP yachulidwayo sopano koma Malawi ETI
It's good song 🎵 guys keep it up ❤❤❤❤❤❤ 👌
Mwaza malume keep it up mmmmmmm ma gens adaa awawa ali fire chan!!!
Ndipo asati mitu gwaa, Atiyankhe basi. 😎😎😎😎😎😎😎😎😎👍👍👍👍👍👍👍
Nice song, koma boma ili ndi zoophyezana mmm
I love the song from Zambia 🇿🇲
Wow, this song deserves some recognition from the activists it kind of tarcoz the vital corners of our dying political landscape in the county ❤❤❤
This song just made my day,,may the soul of skc rest in internal power
Good song keep it up Malawi now is in Bagamoyo
I'm so in love with this song❤❤❤ndipoo ndiyogwira moyo❤❤❤ ndipoo mau a SKC shall forevermore echoi in our hearts n mind MTSRIP 🌹
Nice song,alichete🙌
Good song l ❤ loved it
powerful massage kip it up
Nice song 🔥🔥🔥
Chomusakira ndichani,akufuna amuphenso
Joyce Banda sakonda Malawi ndipo ndi munthu Oipa kwambiri, anangokhala ndi Dumbo chane😢😢
Mfiti ijaa brother
ndi momwemo ndithu esh mayi aja Dumbo basi
Km
Joice fit yayikaz inasainira mwaz
Joice Banda anaba ndalama Kwa zimayi ndazibambo ena ochepa dziko lonse la Malawi lino mudzina lokuti atipatsa ngongole mumuuze kuti adzatenge tima ID take tomwe adatipangira kumakati tsekulitsa ma account Ku FDH kuzuza anthu osauka kumatandala Ku fdh ma account ochuluka anatsekulidwadi omwe sakugwira nthito zikanandiwawa ine ndipo zidzandiwawa mpaka kufa ambuye amuone
Wow❤❤ amazing song
What a nice song
Who sang this beautiful piece of music and whats the tittle..with love from Rhodesia Zambia
Good song chief
Tinakunyadilani pa dzana paja poti munapha njobvu ndi buma. Ndipo timaona ngati ndinu munthu opemphera koma za ziiiiiiiii😢
kkkkkkk komadi bale galu amaneyi
This song need to be given award, song of the year award❤❤❤❤❤❤
I like this song baibulodi ❤and muli mfundo zothyakuka
Keep on playing this songs facts are there u can not see pictures of the alliance day.
Man 🔥
Malawi yanukha
Eish man
Am very impressed with this song
More fire alliance
Some times we shud think where we are coming from
And see where we are going to 😢😢😢😢😢😢😢
Very nice song❤
Ambuye ndinu mwini kulanga ndikuweluza. Please mumufikire chakwera aliko mumuzindikilitse mwazi wanthu 10 ataya miyoyo yawoyi mwazi wawo ukhale pa mutu pake
Best and beautiful song.
Aise ulikuti ndikutumizire ya fanta..... Massively song osati ija atulusa asoja ija❤
Soja ndi chisiru
Soldier ndi achitsiru brother kuyambira kale
Woow this hit is so nice
Wow❤ wat a good song
I like this wow wow ❤
Mfana adzatisaka ambiri pachilungamo koma mmmm enafe ndinyimboyi mmm yabayiratu mawu tiribe .
Kambani inchipotiquizi ena ave
Iwetu uhv done great session mulungu akudalitse waphaso njovu ndimwala
good song who sing this song please i need this song to download plz
Very nice this song❤❤❤❤❤
That's nice song eeee 😂😂😂
Beautiful song❤️
Mmmmm great thinking
zoona nice song
Mwapita basi akulu tidzakupedzani basi koma mwatisiyira mabvuto omwe inuyo munawapanga
Brother mwanena ngati mmene ine ndanenelanso muli ndi mnzeru chongodandaulitsa ndi choti wamwalira ali muuchimo basi
@@MarthaJafalimwaweluzatu brother
Nice song who produce this this song ❤❤
Amakwanisa eti?
Fransis Jomeca ndioyimba owopsa waluso zedi poluka nyimbo komanso creativity ❤❤❤❤❤
Nice 👍❤❤❤❤❤❤ receive your flowers 🌺
Koma wayimba ndani please eeeh this song
Nice one
Lulu your the king bes.t this song means alot
Akumbunse iwe ixikhala pa repeat mwina akumbukula zomwezo anagwilizana😅
😂😂😂😂 wow a nice song mother malawi
What a hit the song is about memories why police looking for the guy
Nice song from............
My brother Francis Jomeka anyamata a mudzi mwa kwanthu ❤️🔥
Mwana owopsa zedi eeeeee❤❤❤❤ apatseni Moni boss munene Kuti Manuel Malunga atii Moni mumatha kuimba zedi❤❤❤❤❤❤❤❤
Mbambande a very good song
Or kuidako nyimboyi uyambila pat...message on point, ma producers nawo anaigwira 😂😂
Wow that's great message
Kuimba kwabwino keep itup.
Choka iwenso mmai oipitsitsa...iwe ndi amene wakolezera malawi, kuthira parafin nkuyatsa moto...lero muli chete! Anthu akuwauka ku Chigwiri...😂😂😂😂😂
Foram Mozambike the Song is very good.
Irmãos do Malawi, como posso ter esse áudio gostei muito da música.
My favourite song ever❤❤❤ eeeeee guys chilungamo ichi zedi❤❤❤❤❤
Agalatiya mwataya chipangano 😢😢
@@WilliamMatanya 😃😃😃😃Ndipo zedi brother
Kodi kumangana bwanji kodi ahhh plzzz mavuto anthu sakuwaziwa😢
Kkkk nyimbo yabho kwambili no mantha ayi 💪💪💪🇲🇼
Tili mdziko la democracy. No kucheuka . Koma vuto chipan chamagazichi mmmmmmm. Koma God protect him
What a song fantastic
nice song
Dziko la malawi likufunika anthu olimba mtima Ngati awaaaaa onena chilungamo ❤❤❤❤
What a song 🎵 ❤
❤❤❤ good song
I'm in love with this song
Kkkk ndipo waiswadi nyimboyi man wa ndioganiza bho heavy😂😂😂😂
I like this song 🔥💯
Number 1. Mnyimbo yii
Keep it up brother nyimboyi ndiyabwino kwambiri 🎉🎉🎉🎉🎉
🔥🔥🔥🔥 powerful song
I like this song its very nice
great song
Iiiiiiiu koma inu ndipo Chilima mzimu wake uuse mumtendere amen
I this Francis Jomeka from Ntcheu?
Ndiwetu galu kwa basi chakwela udzikalamulila banja lakotu osatitu ifeyo mayazi Allah Akbar 😅
Good song