ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

Kachikenaso Born Kalindo 😂🙌😂😂🙌 pa Chi Sunday 14 July 2024

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 13 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 85

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน +9

    Ndalama zingowonongedwa anthu angofa mdzipatalamu mankhwala kulibe anthu angofa sisawawa Mulungu akuwoneni mwapaderadera

  • @user-nz7bd7lm4i
    @user-nz7bd7lm4i หลายเดือนก่อน +8

    Born mulungu azikudalitsa kwambiliiiiiiiiiiii ndipo azikuteteza🙏🙏🙏

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim หลายเดือนก่อน +6

    Chakwera akuwalipira azungu pa ntchito yomwe adagwila pakupha chilima

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb หลายเดือนก่อน +5

    Achakwera akuwononga dziko lathu kwambiri.

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n หลายเดือนก่อน +4

    Dziko lochitisa manyanzi, nkumati achakwera akugwira ntchito ngati president.

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f หลายเดือนก่อน +3

    Tiyamike kubwera kwa tonse Alliance anthu mukung'alula kuti anthu tiziwe zenizeni more 🔥 🔥

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz หลายเดือนก่อน +5

    Koma this very very shameful 😢😢😢😢😢

  • @cjaymw496
    @cjaymw496 หลายเดือนก่อน +1

    Ya balance I think so too😂😂😂

  • @fredsemu7136
    @fredsemu7136 หลายเดือนก่อน +2

    KOMA CHIKANGAWA ATIPWETEKA NDITHU

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo หลายเดือนก่อน +3

    Chakwera mchifukwa chake anakapemphera ku CCAP kamutu kataya mission yapheduka, umkaona ngati wapha chilima zako ziziyenda, chilima sanafe akanalipo muona zakuda inu😂

  • @ThokozaniMunkhondia
    @ThokozaniMunkhondia หลายเดือนก่อน

    A born kalindo,inu ndi mbambande😢😢

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 หลายเดือนก่อน

    Koma bon mulungu akuteteze

  • @ClearKondowe-m3j
    @ClearKondowe-m3j 28 วันที่ผ่านมา

    Very sorry a Malawi kaya dziko lathu likonzedwa. Yoooo

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm หลายเดือนก่อน

    Mulungu wakiya nawe chakwera waona mulungu wakwiya ndpo mulungu achita nawe iweyo

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i หลายเดือนก่อน

    Ati akukonza zinthu!....😅😅😅😅😅😅😅...koma kukonza kunasintha..

  • @ZettaImuranYunusu
    @ZettaImuranYunusu หลายเดือนก่อน

    Osati Ifeyo Amalawi ai.... But all opposition party's we are with you Trap

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f หลายเดือนก่อน

    Ima poyela ndipo aliyense azimva ndithu.Tinasankha satana

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403 หลายเดือนก่อน +2

    Kung'alulaaaa😂😂😂😂

  • @robertkamtimaleka4394
    @robertkamtimaleka4394 หลายเดือนก่อน

    a Born Kalindo 42 million yommweyi basi

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 หลายเดือนก่อน

    Chakwera iweyooo

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e หลายเดือนก่อน

    Auze DC ❤ agaru amenewo

  • @SumanJames
    @SumanJames หลายเดือนก่อน

    Akalindo sakunama

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 หลายเดือนก่อน

    Tiuzeni zambiri bwana .kma dziko lathu lomwe kuzunzika

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela หลายเดือนก่อน

    Ma mafia ati😂😂😂

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e หลายเดือนก่อน

    The DiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiCiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @JamesTeacher-b3o
    @JamesTeacher-b3o หลายเดือนก่อน +1

    Bwana inuyo mmatha kuyankhula ulemu wanu

  • @AufiThera
    @AufiThera หลายเดือนก่อน

    Wathu wathu born kalindo ✌️🔥 Kung,alula💯💪

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon หลายเดือนก่อน

    KKKKKKKKKK BALANCE KUWAMALIZIRA PANTCHITO YOMWE ANAGWIRA PAKUPHA CHIRIMA NDI ANZAKE SHAME CHAKWERA

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v หลายเดือนก่อน

    Munyengo yakung'alula

  • @Mikekajawo-pq9nr
    @Mikekajawo-pq9nr หลายเดือนก่อน +1

    At we are building Malawi yet ndalama zikutuluka

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d หลายเดือนก่อน

    Ndalamq zathu misokho yutha ukupeleka kwazigawenga azipha azibale anthu osalakwa Chakwera sukuwina ase ndakuuza

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 หลายเดือนก่อน

    Malawi akulowera kuti abale? Long live the DC

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน

    The DC ❤❤❤

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela หลายเดือนก่อน

    Ma mafia 😂

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw หลายเดือนก่อน

    The DC 😅😅😅

  • @user-xx4mt8ox8e
    @user-xx4mt8ox8e หลายเดือนก่อน

    Mwati ndi Balance?

  • @RitaKainga
    @RitaKainga หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu the DC

  • @GeoffreyMaulana-rh5rx
    @GeoffreyMaulana-rh5rx หลายเดือนก่อน +1

    Ng'ona zalusa kufuna kusaulisa Malawi

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 หลายเดือนก่อน

    Mr Bon Kalindo ndinu oyankhuliradi a Malawi tonse, keep it up the DC.

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawaza หลายเดือนก่อน

    Tell them DC

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 หลายเดือนก่อน

    Ayi zikomo

  • @BlessingsMikeyasi
    @BlessingsMikeyasi หลายเดือนก่อน

    Nazoooo

  • @adzonzicomedy
    @adzonzicomedy หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน

    Chili chonse chingowululika kumwamba kulandire ulemu

  • @AnnastasiaChakwiya
    @AnnastasiaChakwiya หลายเดือนก่อน

    Ai zikomo achakwera

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz หลายเดือนก่อน

    😢😢😢😢😢

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k หลายเดือนก่อน

    Koma what is the use of our currency in Zambia? I don't understand this.

  • @BornfiyesignalSignalmtema
    @BornfiyesignalSignalmtema หลายเดือนก่อน

    The dc

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 หลายเดือนก่อน

    Ya balance 😢
    RIP SKC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r หลายเดือนก่อน

    Choka iwe mbuli zokhazokha zomwe ziimakunvera iwe gawanani ndlmazo paja ndiyo ntchito yanu 😂😂😂mwayi ndi MCP ukudya bwino kamba ka mabodza akowo azipani akumakulipila 😅😅😅uziyamklika wamva

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 หลายเดือนก่อน +1

      Mbuli ndiwe mavuzi okhwimawo

    • @Dysonkhofi
      @Dysonkhofi หลายเดือนก่อน +1

      Iwenso ndiwe galu,chitsiru

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r หลายเดือนก่อน +1

      @@Dysonkhofi fisi,chule,mbuzi,,bulu munayiwala zimenezo zikomo God bless you 😊😊❤️❤️❤️ work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 หลายเดือนก่อน

      ​@@user-bd5kw8oq1rutukwana anzako..opanda chifukwa ena akubwexera utchula dzina la Mulungu shame on you.

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 หลายเดือนก่อน

      Vuto u need attention

  • @JamesAlinafe
    @JamesAlinafe หลายเดือนก่อน

    Tha DDDDD ccccccccc

  • @katalamajames4947
    @katalamajames4947 หลายเดือนก่อน

    Koma keni nsonda amadya mutu nkhope the same sekeleton ma R. V.sakugwira nchito

    • @zimmekapachika6784
      @zimmekapachika6784 หลายเดือนก่อน

      😅😅😅😅😂😂😂mankwala anapima sakugwila 😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no หลายเดือนก่อน

    Kukuyu nyamayake

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n หลายเดือนก่อน

    Komanso chibadwireni ine ntchito ya asilikali athu muno mu malawi sindikuiziwa, chifukwa ngati nkuteteza dziko .bwezi atalipanga boma ili held responsible pa nkhani iyi infact predent akadamuchosa.

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g หลายเดือนก่อน

    Balance

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so หลายเดือนก่อน

    koma amalawi

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee หลายเดือนก่อน +1

    Amazalandila malipilo a ntchito yomwe adagwila

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl หลายเดือนก่อน

    Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s หลายเดือนก่อน

    Zovetsa chisoni 😢

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi หลายเดือนก่อน

    The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔

  • @kelvinsibande8779
    @kelvinsibande8779 หลายเดือนก่อน

    The DDDDDCCCCCCC

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili หลายเดือนก่อน

    Mmmmm haa?

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz หลายเดือนก่อน +1

    Ma 20kwachawooo??

    • @MinhoMasanza
      @MinhoMasanza หลายเดือนก่อน

      Yah ndima mk20 koma each carton contains more than a million

    • @hudycorex1893
      @hudycorex1893 หลายเดือนก่อน

      Mk20 Sindalama????? Iwe ndendiopepera bwanji!!!

    • @rhodricksalima5387
      @rhodricksalima5387 หลายเดือนก่อน

      Paliso ma 5 pin tu

    • @CharityChikomo-hl1gz
      @CharityChikomo-hl1gz หลายเดือนก่อน

      Opepela ndi amako

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 หลายเดือนก่อน

    ANTHU PANO MMANGO PANGA MA COMMENT KOPANDA KUSATILA ZINTHU . NDALAMA ZOMWE ZAPEZEKA KU ZAMBIA NDI ZAMAYIKO ANGAPO KUPHATIKIZA MALAWI ANTHU OMWE APEZEKA NAZO NDIZINKA ZA KU RUSSIA OMWE AKUPANGA MA BUSSINES A MA DRUGS OSATI ZOTI BOMA AYI MMM KALINDO ECHI BOZA LENILENI ZINAMIZA ACHILOMWE AKOWO

    • @TysonMwenye
      @TysonMwenye หลายเดือนก่อน

      Ndiye anthu aku Russia wo angapeze ndi ndalama zathu chifukwa choti akugulitsa ma Drugs? Ifeyo tikamapita ku mayiko akunja timasintha ndalama zadziko lomwe tikupitako.Ndipo tikamaliza business yathuyo tisanatuluke mudzikolo timasinthilatu zamalawi.Ndiye awowo apezeka bwanji ndi ndalama zathu (Mwk) koma kudziko lina chinawakanikitsa kusintha kumalawi konko ndichani ngati ndizachilungamo ndalamazo

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 หลายเดือนก่อน

      Ndalama zama drug mpaka sealed? Iwe ndichimbutumwa wamva

    • @munashemoyo4190
      @munashemoyo4190 หลายเดือนก่อน

      Kusonyeza kt zomwe zikuchitika dziko muno iwe zikukusangalasa et i uzaziwona ukazakwatila ukasiya kudyesedwako mbudzi yamunthu iwe kape

    • @AmosScott-z9x
      @AmosScott-z9x หลายเดือนก่อน

      Kape iwe

    • @chadreckchibwithala1493
      @chadreckchibwithala1493 หลายเดือนก่อน

      mbutuma ndinu osaziwa zinthu alomwe matama basi tiyeni uko .
      mleke kutivuska mngalamuliraso yai chalo ichi jiiiiiiiii peter wanuyo no

  • @user-si8vm5vj8s
    @user-si8vm5vj8s หลายเดือนก่อน

    Shame on you chakwera

  • @warrenmwambazi8342
    @warrenmwambazi8342 หลายเดือนก่อน

    Very bad 😊😊😊

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki หลายเดือนก่อน

    Kalindo ndi nyatwa auze zitsiru izi.

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela หลายเดือนก่อน

    Ma mafia 😂