President wa Malawi first ali kumalire Zambia komwe Amalawi ena alandidwa malo awo.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 41

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 2 หลายเดือนก่อน +16

    Awa ndamene akuyimilira anthu kumalawi awa mulungu aziwadalisa kwambiri

  • @lyiemax
    @lyiemax 2 หลายเดือนก่อน +5

    Proud of you guys, may the Lord continue to bless, guide and protect you, proud of you always 🔥🔥🔥🔥

  • @blessingmnomanda
    @blessingmnomanda 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dc my uncle me your nephew am proud of you uncle live in kenya

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 2 หลายเดือนก่อน +7

    Awa ndi omwe akuima pachilungamo viva Malawi first

  • @AustinBanda-r8i
    @AustinBanda-r8i 2 หลายเดือนก่อน +3

    Viva Malawi first peoples first

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 2 หลายเดือนก่อน +5

    Ndiamene asalamulile Malawi. Mawa likubwelali

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 2 หลายเดือนก่อน +2

    ❤❤❤❤❤❤🙏🙏🙏🙏

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน +5

    Mbambandetu malawi first osati CHIKANGAWA ndi mbava zinzake nohani iyi ndi yapakanthawi koma CHIKANGAWA palibe chomwe amachitapo koma kuba ndi kupha ndi kumanga anthu ulemu wanu malawi first Ambuye adzikutsogolerani

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc 2 หลายเดือนก่อน

    Proud of you 😊 the DC 💪💪

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤ the Malawi first people first we love you all

  • @TasoMuyande
    @TasoMuyande 2 หลายเดือนก่อน +3

    Viva Mr DC

  • @MussahJenala
    @MussahJenala 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 2 หลายเดือนก่อน

    Nkhani iyabwino kwambili❤

  • @HamanjaManyela
    @HamanjaManyela 2 หลายเดือนก่อน +2

    We love you

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 2 หลายเดือนก่อน

    Malawi Fest number 1

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 2 หลายเดือนก่อน +2

    Zapamwamba ndazikonda kwambiri viva malawi first ❤❤❤

  • @MussaChilembwe
    @MussaChilembwe 2 หลายเดือนก่อน

    Tizafera mbenderaimeneyi 🇲🇼

  • @AbudulJohn
    @AbudulJohn 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤thanks guys

  • @DaudRashid-sp3sk
    @DaudRashid-sp3sk 2 หลายเดือนก่อน +3

    Mulibho guys ntchito yanu ikuwoneka ndithu

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 2 หลายเดือนก่อน +2

    Booooon kalindoooo ❤❤❤❤❤

  • @MussaChilembwe
    @MussaChilembwe 2 หลายเดือนก่อน

    The DC uremu wanu mukuyimirela malawi

  • @BrendaMwale-l3d
    @BrendaMwale-l3d 2 หลายเดือนก่อน

    Malawi first zikomo kwambili pa ntchito mukugwila

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 หลายเดือนก่อน

    Malawi first ikugwila ntchito kuposa president wa mdziko

  • @MonicaBvumbwe
    @MonicaBvumbwe 2 หลายเดือนก่อน +2

    Booon ♥️♥️

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 หลายเดือนก่อน +3

    Apolice ndi Amey tchito Yao ndikuteteza boma la chikangawa party osati amalawawi ayi ulemu wanu Mr boni kalindo ndi timu yanu mulungu azikudalitsani

  • @happymumba2261
    @happymumba2261 2 หลายเดือนก่อน +2

    Yeah ndichoncho ndithu

  • @IsaqueFernandoAntônioAntônio
    @IsaqueFernandoAntônioAntônio 2 หลายเดือนก่อน

    Ndinu anthu ofunikila

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 2 หลายเดือนก่อน

    Malawi tadzuka iweh

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 2 หลายเดือนก่อน

    Boma lichte manyaz mwaona kufunka kwa kalindo?mummangeso mwamva? dziko lidzakwiya

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe 2 หลายเดือนก่อน

    Anthu a kuZambia A wemba ndi anthu a nkhaza kwambiri zikomo.kwambiri malawi first mwalowererapo apa zikomo @ Malawi First mulowererenso .kuti malawi peesident .chakwera asalolenso ngomgole ya I M F ndi world Bank omwe zimapatsa mohamvu azunguwa kupanga devalue malawi kwacha yomwe imàkhala njira imodzi yobera chuma chakumalawi. Cifukwa interest ya azunguwa imachuluka nkhani nkhani

    • @RuthChilobwe
      @RuthChilobwe 2 หลายเดือนก่อน

      President not peesent

  • @JimmyMhone-b5p
    @JimmyMhone-b5p 2 หลายเดือนก่อน +2

    Wovala ma jekete abwino abwino sanakafike?

  • @OsmanChisi
    @OsmanChisi 2 หลายเดือนก่อน

    Koma bon ai mulungu akhale nawe

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 2 หลายเดือนก่อน +1

    Inuyo ndi reporter kapena commentator? Tiuzeni zimene akukambiranazo

    • @SteveKanongwa
      @SteveKanongwa 2 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkk ine uyuyu sindkumvesesa ka report lake limamvekaso kaya handiziwa

  • @Malume2024
    @Malume2024 2 หลายเดือนก่อน

    DC ndi katundu

  • @benjaminmvuma-rk6mu
    @benjaminmvuma-rk6mu 2 หลายเดือนก่อน

    That's ur job not zandale

    • @HamanjaManyela
      @HamanjaManyela 2 หลายเดือนก่อน +1

      Sapanga zandale komano amayimilira amalawi ngati penapake sipakuyende bwino they take an action

  • @YamieManda
    @YamieManda 2 หลายเดือนก่อน

    Inu ameneyu angapulumutse ndani ?mbuzi yamunthu ngati imeneyi

  • @NoohNowa
    @NoohNowa 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤