#PROFESSOR_HASSAN_SAID_ZAMBIA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 25 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 204

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 3 หลายเดือนก่อน +9

    I am proud from Christian to be Muslim ☪️ ❤❤❤

  • @GoldenBarnet-hv3wj
    @GoldenBarnet-hv3wj 3 หลายเดือนก่อน +9

    Am proud to be a Muslim,Allah is great

  • @BysonBanda-z8q
    @BysonBanda-z8q 2 หลายเดือนก่อน +3

    I am proud to be a Muslim

  • @FayazNhlema
    @FayazNhlema 3 หลายเดือนก่อน +5

    Ndinali msilamu koma ndinasiya Chisilamu nditazindikira kuti YESU ndiye njira yowonadi.

    • @EdwardZuze-r7w
      @EdwardZuze-r7w 3 หลายเดือนก่อน

      Mulungu akudalitseni kwambiri, munapanga chisankho chabwino.

    • @HakeemJossam
      @HakeemJossam 2 หลายเดือนก่อน

      munali msilamu koma Osazindikila kungopitako poti makolo Anu amkapita kumeneko

    • @EdwardZuze-r7w
      @EdwardZuze-r7w 2 หลายเดือนก่อน

      Ambuye akudalitseni chifukwa ndi ochepa amene akumaona patali mu uzimu, ambiri ali komweko chifukwa anabadwila momwemo kapena makolo awo anawasiya mzikiti omwe anamanga,
      ambuye akuthandizeni in everything especially moyo wanu wa uzimu

    • @felixsaidi6715
      @felixsaidi6715 หลายเดือนก่อน

      Dzivere chisoni m'bale wangaa. Akati Islam mean, kuchita chifunilo cha Mulungu. Ndemukamati munatuluka chisilam, mudziwe kuti munasiya kumugonjera Mulungu. Tsopano mukutsatira satana yemwe wasochoretsa anthu ambiri padziko lonse lapasi

  • @GiftBonomali
    @GiftBonomali 3 หลายเดือนก่อน +6

    Allah bless you professor mashalah❤❤❤

  • @idreesahjafari5093
    @idreesahjafari5093 หลายเดือนก่อน +1

    I am proud to be a Muslim Alhamdulillah ❤❤❤

  • @EmmanuelstoneyJere
    @EmmanuelstoneyJere 2 หลายเดือนก่อน +2

    Afarisi a lero ndamenewa ntchito yao nkuphwekesa Yesu basi

  • @clesheinvestments
    @clesheinvestments 3 หลายเดือนก่อน +6

    Alhamdulillah kuti ndine Msilamu.
    Ma videos ngati awa adzipezeka ndithu pa TH-cam.
    In so doing zithandizira uthenga wa Allah kufikira ena omwe ali kutali mosavuta

  • @RedsonRichard
    @RedsonRichard 3 หลายเดือนก่อน +7

    Nthawi yatha amsilamu inu musasokoneze choonadi

    • @AndersonBishop-i2t
      @AndersonBishop-i2t 3 หลายเดือนก่อน

      Akusokoneza ndi chani amenepo mmm

    • @sharifhenderson6982
      @sharifhenderson6982 2 หลายเดือนก่อน

      Asokonesa pati 😂😂😂

    • @AbdulAzeezChapita
      @AbdulAzeezChapita หลายเดือนก่อน

      Chilungamo chakufika mutima mwako

    • @MtengowaPadambo-ub4ji
      @MtengowaPadambo-ub4ji หลายเดือนก่อน

      Tsopano kusokoneza fukwa akukuuzan ngamo? He is quoting from the Bible

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w 3 หลายเดือนก่อน +1

    Hohn 14 v 6, Yesu anati ine ndine njira choonadi ndi moyo.
    palibe munthu adza kwa atate koma mwa ine.
    Most of theses things brings conflicts among peoople, Palibe mpikitsano pa mawu a mulungu

  • @mickchiliko2796
    @mickchiliko2796 3 หลายเดือนก่อน +2

    Alhamdulillah am proud to be Muslim. May Allah guide me and protect me In shaa Allah.

  • @TennisMatandika
    @TennisMatandika หลายเดือนก่อน

    I'm proud to be a Muslim

  • @ChrispinLunda
    @ChrispinLunda 3 หลายเดือนก่อน +2

    Zamasiku otsiliza amenewa ndiwo omkana yesu aja zimene munthu udakhazikikamo sikopheka kukusutha amenewa simungawauze za mzimu oyela sangave ndiwo umaulula umazindikilitsa umaphuzitsa ngat ulibe mzimu oyela ungalive baibulo ukamaliva kuthupi mzimenezo zovetsa chison ambuye akuzindikilitsen amen

    • @tauhidtimba
      @tauhidtimba 3 หลายเดือนก่อน

      Kumva chichewa umafunikira kukhala ndi Zimu oyera kod?

    • @chiogamata2560
      @chiogamata2560 3 หลายเดือนก่อน

      Ine anthu inu mmandiwaza apapa
      Kumva language yako yomwe zufunaso nzimu oyela??
      Kukuuza kut iyo ndi kapu yomwela madzi, sumva coz ulibe nzimu oyera??
      This thing of nzimu oyera, koma mmaudziwa, mungaufotokoze ndi malemba maumboni??
      Concept iyiyi eeeeti eeeeeeish mumadyera guys 🤣🤣🤣🤣🤣

    • @sharifhenderson6982
      @sharifhenderson6982 2 หลายเดือนก่อน

      Mzimu oyelawo anaulenga ndan??? 😂😂😂

    • @sharifhenderson6982
      @sharifhenderson6982 2 หลายเดือนก่อน

      ​@@tauhidtimbakayatu 😂

    • @ALICKMASANGANO
      @ALICKMASANGANO 2 หลายเดือนก่อน

      Mmm baba moti ma verse akupereka muthuyu si amu bible

  • @MtengowaPadambo-ub4ji
    @MtengowaPadambo-ub4ji หลายเดือนก่อน

    Please upload another episode

  • @HarleemahJamesMatolah
    @HarleemahJamesMatolah 28 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤Mashallah

  • @swalienkhumbwa7338
    @swalienkhumbwa7338 12 วันที่ผ่านมา

    I am proud to be Muslim

  • @KhadijaJambo
    @KhadijaJambo 14 วันที่ผ่านมา

    Proud to be a muslim❤❤❤

  • @MpondaBanda
    @MpondaBanda 3 หลายเดือนก่อน +1

    Alhamdu lillah proud to be one hu follows Allah's submission

  • @MussaMalon
    @MussaMalon 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mashallaah Sheikh mulungu akudalitseni ❤.

    • @blessingsdouglas3
      @blessingsdouglas3 3 หลายเดือนก่อน

      Aaaaaaa ine saidi Zambia nakhala nayepo ndi tambwali uyu

  • @SUWEDSHAMWKUPE
    @SUWEDSHAMWKUPE 2 หลายเดือนก่อน

    Allihamdulilah to be a Muslim my dad please protect pokhala slamu paka ifa

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od 2 หลายเดือนก่อน

    Mashalla Allah ndi silamu ndipo tikuphemba kwa Allah ndizafe ndi silamu

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 3 หลายเดือนก่อน +2

    Im proud to b Muslim, mpaka imfa idzanditenge ndili msilamu

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 3 หลายเดือนก่อน +1

    I am proud to be a muslim ,
    Komafunso langandiloti ,
    Ndichifukwachani Muhammad timamupemphela chikhululuko komanso madaliso kwa mulungu ?
    Kodi Muhammad ndi azibale athu omwe anamwalila oyenela kuwafunila zabwino kwa mulungu ndindani ?

    • @JohnstoneMwandira
      @JohnstoneMwandira 3 หลายเดือนก่อน

      Dzina la mtumiki Muhammed likatchulidwa timanena kuti swalalah alaih wasalamah,( meaning , mtendere ndi madalitso amulungu apite kwa iye).
      Zimenezi even zimachitikaso kwa Azitumiki ena onse . Issah(Yesu) ndiye timati Alaih Salam Wasalatuh(Meaning, madalitso amulungu apite kwa iye).
      Nde zimenezi zimanenedwa kwa mtumiki winaaliyese akatchulidwa dzina.

    • @rashidadan2533
      @rashidadan2533 3 หลายเดือนก่อน

      @@JohnstoneMwandira ok , ndichifukwa chani okhala atumiki a mulungu timawafunila mtendele ndi madaliso , chikhalilenicho anapanga ntchitoya mulungu .

    • @JohnstoneMwandira
      @JohnstoneMwandira 3 หลายเดือนก่อน

      @@rashidadan2533 Zimenezi akulamula ndi Mulungu akuti mfunireni zabwino mtumiki wanu. Nde Ife ndindani kukanira.

    • @AndersonBishop-i2t
      @AndersonBishop-i2t 3 หลายเดือนก่อน

      Iweso sisilamu tachoka apa

  • @SuperSave-r8u
    @SuperSave-r8u หลายเดือนก่อน +1

    Allah akbar

  • @YatoRoy-kt4lh
    @YatoRoy-kt4lh 3 หลายเดือนก่อน

    I once met this Saidi Zambia for almost 8 hrs.
    Anafika pokwiya titamufotokozera zinthu zomwe iye samadziwa za chiyambi chachisilamu ndipo anakwiya heavy.
    Amene mumamudziwa ask him za anyamata omwe anakumana nawo usiku mnyumba ina ku mangochi.
    He ended up a failure on that meeting.

    • @GiftStephano
      @GiftStephano 3 หลายเดือนก่อน

      Chinayamba bwanji tiziwe nao

  • @BesterMagetsi
    @BesterMagetsi หลายเดือนก่อน

    Alihamudulilah ine kukhala msilamu

  • @UmarAjussu
    @UmarAjussu 3 หลายเดือนก่อน +3

    Allah akudaliseni ma sheikh nonse

  • @FathimaMa2
    @FathimaMa2 3 หลายเดือนก่อน +1

    Alihamudulilahi kwaine mpakana kwa asilamu ose pano pa dhunia mashaalhaa

  • @ishmaelmadalet2591
    @ishmaelmadalet2591 3 หลายเดือนก่อน

    When was this debate held

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 3 หลายเดือนก่อน

    Dawa koma imeneyo osati zakuti Achibeketi adali mfiti adakuphera agogo ako muzichita Dawa yolimbana ndi amene Sali Asilam timakunyadiran big kep it up

    • @AKHTARLINGSON
      @AKHTARLINGSON 3 หลายเดือนก่อน

      Anayankhulapo choncho iyeyu?

  • @muhammadisaid3968
    @muhammadisaid3968 หลายเดือนก่อน

    Mashallah

  • @PhiladelphiaManyumba
    @PhiladelphiaManyumba 2 หลายเดือนก่อน

    Devil's deception 😢😢 beware my fellow Christian this is one of the last events
    Aim of this ceremony is to contradict your faith keep watching 😢😢

  • @ghadaffmoosa7535
    @ghadaffmoosa7535 2 หลายเดือนก่อน

    Ma sha Allah may Allah bless u sheikh SAID HASSAN ZAMBIA

  • @danielmangalisobanda8356
    @danielmangalisobanda8356 3 หลายเดือนก่อน

    Mr Hassan munaphunzira koma ndinu mbuli yothelatu kuuzimu ndichifukwa chake mukupembedza wovumbulutsa Quran naganiza ndikukhulupilila kuti mukupembedza Mulungu wamoyo, chonsecho ndiSATANA weniweni adamunamidza muhammad kuti ndiiyeyo adili kuvumbulitsila aneneneli amuBible

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kwamuthu yemwe sawerenga ndikutsata za zipembedzo adupha nkhani zonse ndikumangosankha momwe akufuna pokwanilitsa zolinga zanu koma choonadi mukuchidziwa

    • @AustinManes-m3w
      @AustinManes-m3w 3 หลายเดือนก่อน

      Pelekan lemba nanu

    • @chiogamata2560
      @chiogamata2560 3 หลายเดือนก่อน

      Pelekani zomwe mmawelenga inuzooo
      Ndanga izi zikuchoka mmitu mwao ngat?? 🤣🤣🤣🤣🤣

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chiweluzo chidzapelkedwa chifukwa Cha zintchito zarhu osati proud to be a Moslem or proud to be a chriastian nzopanda pake

  • @YusufuYunusuSavielMakey
    @YusufuYunusuSavielMakey 2 หลายเดือนก่อน +1

    Masha Allah pondipanga kukhara msilam ❤

  • @JUBRANBULAYHl-yb4ke
    @JUBRANBULAYHl-yb4ke 3 หลายเดือนก่อน

    Mwenyezi Mungu, hapana mungu ila Yeye, Aliye hai, Msimamizi wa milele, Amekuteremshieni Kitabu kwa haki, kinachosadikisha yaliyokuwa kabla yake, na ameteremsha Taurati na Injili kabla yake kuwa ni uwongofu kwa watu. Na akateremsha upambanuzi: Hakika walio kufuru Ishara za Mwenyezi Mungu watapata adhabu kali, na Mwenyezi Mungu ni Mwenye nguvu, Mwenye kulipiza kisasi wewe katika Mwingi wa rehema, vipi hakuna mungu ila yeye ni mpendwa, Mwenye hikima ni yule aliyeteremshiwa kwako Ama waliomo nyoyoni mwao wanafuatwa Hawakusema kuwa kila mmoja Kwa Mola wetu Mlezi. na hawakumbuki ila wenye akili, tusipotoke nyoyo zetu baada ya kutuongoza bila shaka Mwenyezi Mungu hatavunja ahadi yake, mojawapo ya makusudio ya surah.
    Kudumu katika Uislamu baada ya ukamilifu na ubainifu wake, na kukanusha shaka za Watu wa Kitabu, hususan Wakristo
    Ni surah ya Madina iliitwa Surah Al Imran kwa sababu familia ya Imran imetajwa ndani yake katika aya ya surah.
    Herufi hizi zilizotengana zimemtangulia mwenzao katika Sura Al-Baqarah, na zinaonyesha kutoweza kwa Waarabu kutoa Qur’ani kama hiyo ingawa inaundwa na herufi ambazo Sura ilianza nazo, na kutoka kwao wanatunga hotuba yao.
    Mwenyezi Mungu ndiye ambaye hana mungu wa kuabudiwa kwa haki isipokuwa Yeye pekee na hakuna mwingine aliye hai ni maisha makamilifu yasiyo na kifo au upungufu.

  • @IbrasyaicheWizyx
    @IbrasyaicheWizyx 3 หลายเดือนก่อน

    Alhamdulillah for choosing me to be a Muslim❤

  • @HarnetJauma
    @HarnetJauma 2 หลายเดือนก่อน

    Am proud to be a Muslim ❤

  • @AnthonyLushu
    @AnthonyLushu หลายเดือนก่อน

    Komatu a seneth day mwapanga zopoira mwaganiza ngat nkhuku pomunyozensa yesu mulungu akukanthen inu pamozi ndi a siramu anuo sipangakhare ntendere pakat pa asiramu ndi khrisitu

  • @Chayibujackison
    @Chayibujackison 3 หลายเดือนก่อน

    Mashah allah sheikh awuzen ndithu❤❤❤

  • @frankkasamala6956
    @frankkasamala6956 2 หลายเดือนก่อน

    We need you here at ntonda in ntcheu

  • @tomthompson4429
    @tomthompson4429 3 หลายเดือนก่อน

    Where is the other part of Seventh Day part? Let's PRAY that each one of us here on Earth meets GOD's Grace and know the truth, I Pray for you my muslim brothers. Amen

  • @dennismachemba9514
    @dennismachemba9514 2 หลายเดือนก่อน

    Masha Allah may Allah Grant him jannat firdaus

  • @AfredMbeta-pk1cn
    @AfredMbeta-pk1cn 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ndizomwe timadikilira,go ahead

  • @JafaliChiwimbi
    @JafaliChiwimbi หลายเดือนก่อน

    Marshall

  • @mariamhassan6788
    @mariamhassan6788 3 หลายเดือนก่อน

    Proud to be a Muslim Alhamdulilah ❤

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w 2 หลายเดือนก่อน

    Anthu timasokoneza pakati pa Mulungu ndi Alla, palitu kusiyana kwakukulu, ndipo mudzadzindikira koma mochedwa kusiyana kwa awiriwa

  • @UlandaHarjisonstone
    @UlandaHarjisonstone 3 หลายเดือนก่อน

    Allihamdulillah pokhala msilam chonde Allah muzanditenge ndili msilam

  • @AbdurashidAhmad
    @AbdurashidAhmad 2 หลายเดือนก่อน

    Tiyeni tafunile zabwino zonse makolo athu omwe anayima pakati pachowonadi chisilamu omwe alimoyo mpakana omwe anasogolera kale kumanda mulungu awapatse jan'na please

  • @Lionelmosse
    @Lionelmosse 2 หลายเดือนก่อน

    Allahmdulillah ❤❤❤❤❤❤

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 3 หลายเดือนก่อน

    Manshaallah brother

  • @khadijailiyasa5315
    @khadijailiyasa5315 3 หลายเดือนก่อน +2

    Kodi simungayike apapa dawa yonse please tikuyifuna

    • @abdul-rasheedsalika
      @abdul-rasheedsalika 3 หลายเดือนก่อน

      Mposo abaleee, nanga kwinako tikakupezera kutiko sono

  • @JummahbinhoPartison
    @JummahbinhoPartison 3 หลายเดือนก่อน

    Salaam aleykum...video muzimalidza osamayidula

  • @danielmangalisobanda8356
    @danielmangalisobanda8356 3 หลายเดือนก่อน

    Mulungu wamoyo wovumbulutsa Uthenga wamuBible akuchitileni chifundo kuti mumudziwe.

  • @mramir.s.smkubwa3985
    @mramir.s.smkubwa3985 3 หลายเดือนก่อน

    Komano kunena chilungamo Alhamdulillah asilamu mulungu anawapasa mzelu ndithu

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 2 หลายเดือนก่อน

    Asilamu olambila mwala wa ku arabia saudi dzipumi biii ngati zoona

  • @raphicallan5331
    @raphicallan5331 3 หลายเดือนก่อน

    Proud to be a Muslim

  • @JazraJeffm
    @JazraJeffm 3 หลายเดือนก่อน

    I'm proud to be a musilim

  • @HaliJana
    @HaliJana 2 หลายเดือนก่อน

    MULUNGU AKUONJEZELENI MASIKU AMOYO WANU ADALISESO MU MZELU ZANU

  • @SaymonMawaya
    @SaymonMawaya 3 หลายเดือนก่อน

    Maashallah

  • @GiftSinalo-ku6zb
    @GiftSinalo-ku6zb 3 หลายเดือนก่อน

    Alhamudulillah to be a Muslim

  • @martinchimwala
    @martinchimwala 2 หลายเดือนก่อน

    Proud to be Muslim

  • @MarthaChizi-h1u
    @MarthaChizi-h1u 3 หลายเดือนก่อน

    MBULI ZA ANTHU NDIPO PALIBE CHIMENE MMADZIWA

  • @HarryChindiwo
    @HarryChindiwo 3 หลายเดือนก่อน

    Nawe hule Zambia ukuziona ngati ndi mngero

  • @ShaibuJackson
    @ShaibuJackson 2 หลายเดือนก่อน

    Mashaalla

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 3 หลายเดือนก่อน

    Ndimafun ndipemphe kt pls tiyen tiphunzir kuwereng Quruan ngat sitidziw tiyen tikaphunzir ngakhal kt ndife ochuk kumbal inayo

  • @YAZIDU-l9s
    @YAZIDU-l9s 2 หลายเดือนก่อน

    Allahu Akbar. Ma sha Allah. Na am ❤❤😂

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 2 หลายเดือนก่อน

    Asilamu nonse ndi ma judger ndekha nonse moto ma vindictivist shupiti

  • @BindulaMtambo
    @BindulaMtambo 3 หลายเดือนก่อน

    Mashallah, please upload some more

  • @adamuhwaduh1080
    @adamuhwaduh1080 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipepha Allah kut ndidzamwalire kanali silam

  • @cassimmeleka40
    @cassimmeleka40 2 หลายเดือนก่อน

    ان الدين عند الله الإسلام

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 3 หลายเดือนก่อน

    Pakut ngat wakhungu alondole njira akukhungu onse awili azagwa mmbuna....mukazaziwa choona choona chizakumasulani

    • @HollyManthepa
      @HollyManthepa 3 หลายเดือนก่อน

      Inu chilungamo munachiona bwanji

  • @danielmangalisobanda8356
    @danielmangalisobanda8356 3 หลายเดือนก่อน

    Ndikudziwa chimene ndikunenachi and i Challenge you

  • @IssahNgalinje
    @IssahNgalinje 3 หลายเดือนก่อน

    Sheikh musiponya zambili kuti tizinva zambari chonde chonde ❤❤

  • @BornwellOtala-dm1zm
    @BornwellOtala-dm1zm 3 หลายเดือนก่อน

    ❤Ma shaaAllah

  • @Chayibujackison
    @Chayibujackison 2 หลายเดือนก่อน

    Mashah allah ❤ ♥ 🙏

  • @DIMZYRECORDS
    @DIMZYRECORDS 2 หลายเดือนก่อน

    Minika ❤❤❤❤

  • @UmariBashiri
    @UmariBashiri 3 หลายเดือนก่อน

    Ma Sha AllAh Amee

  • @AshrafSaidi
    @AshrafSaidi 3 หลายเดือนก่อน

    Jazakum llah khaira

  • @AsanteBilly
    @AsanteBilly 3 หลายเดือนก่อน

    MashaAllah ❤❤

  • @LacksonLungu-e2q
    @LacksonLungu-e2q 3 หลายเดือนก่อน

    Kampen kumphatsa koma mmm pot mwati yesu ndee yesu basi Kaya silam Kaya Christi ndi yesu basi.

  • @Creslevison-vj2sl
    @Creslevison-vj2sl 3 หลายเดือนก่อน

    SDA don't do this again cox contextual reading of the bible is vry important,astichocherese awa

    • @abdul-rasheedsalika
      @abdul-rasheedsalika 3 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂 chilungamot always chimapweteka ndithu. Spend your time by searching for the truth.

  • @chiogamata2560
    @chiogamata2560 3 หลายเดือนก่อน

    Kulowa kumoto kulipo ndiiithu 😂😂😂😂

  • @IssahNgalinje
    @IssahNgalinje 3 หลายเดือนก่อน

    Mashaa Allah sheikh ❤❤

  • @PatienceNgulinga
    @PatienceNgulinga 3 หลายเดือนก่อน

    Aaaaa Sheik openga uyu kanundu akumupweteka,, mutuwo kukulako ukumulemera

    • @chiogamata2560
      @chiogamata2560 3 หลายเดือนก่อน

      Kung'alula zomwe mmazidutsa kutchalitchikoka nde mwadabwa nazotu??
      Akutenga zammutu kapena??
      Else likunama ndi Bible lotu pamenepoo 😂😂😂😂

  • @KassimShaibu-f6h
    @KassimShaibu-f6h 3 หลายเดือนก่อน

    Machalawu

  • @omarmanduwa4127
    @omarmanduwa4127 3 หลายเดือนก่อน

    MAA SHAA ALLAH

  • @ElickBanda
    @ElickBanda 3 หลายเดือนก่อน

    Ma shaallah

  • @RashowLajabuh
    @RashowLajabuh 3 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤

  • @AustinManes-m3w
    @AustinManes-m3w 3 หลายเดือนก่อน

    Mashaalah

  • @AbgirlChinheya
    @AbgirlChinheya 3 หลายเดือนก่อน

    Alihamudulilah❤

  • @KelvinMangwengwe
    @KelvinMangwengwe 3 หลายเดือนก่อน

    Ma sha Allah ❤

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 หลายเดือนก่อน

    Macha hallah ❤❤

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 3 หลายเดือนก่อน

    Ameen thummah Ameen

  • @SABITISABITI-yv9jq
    @SABITISABITI-yv9jq 3 หลายเดือนก่อน +1

    🕋🕋🕋🕋🕋☝️☝️

  • @JannahMajola
    @JannahMajola 3 หลายเดือนก่อน

    Komano pamawakanika kunvesa anthuwa ndipati??

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote 3 หลายเดือนก่อน

    Asilamu zitsilu kwmbr mulungu wawo allah amene amakhl ku saudi arabia anawanamiza kwmbr ndpo mohammed sanali prophet ai koma mulimi olima tende(dates) kuchimbedzo chachisilamu kulibe mphamvu liliyonse ya mulungu

    • @AndersonBishop-i2t
      @AndersonBishop-i2t 3 หลายเดือนก่อน

      Chisilu ndi iweo ndipo khwiya wa mulungu upite kwa iweyo mulungu akupase chilango uli keye moyo wamva ufe ziwalo pa mawu amenewo ameen 🙏

    • @IgnatiousFote
      @IgnatiousFote 3 หลายเดือนก่อน

      @@AndersonBishop-i2t Bulutu allah bd mulungu wasilamu udziwe zimenezo kuyambila lero mohammed sanali prophet ai bible mulibemo mohammed nde munamutenga kut

    • @TristanSymon
      @TristanSymon 3 หลายเดือนก่อน

      Ase pakamwapo uziyankhula pang'ono..... Uzimvere chisoni

    • @ShamirahShaffie
      @ShamirahShaffie 2 หลายเดือนก่อน

      Allah Aku khululukile sukudziwa chomwe ukuyakhula ​@@IgnatiousFote

  • @abhentomwcmwanjeza5771
    @abhentomwcmwanjeza5771 3 หลายเดือนก่อน

    MaShaallah