Achinyamata Akunongeka Chifukwa Chosowa Zochita - Bon Kalindo
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 27 ก.ย. 2024
- Today on Nyasa VoiceBox, we feature one of our top contributors, Human Rights Activist, Bon Kalindo. In his audio today, Bon Kalindo begins by bring to light an issue that some would describe as an epidemic in Malawi. Young people engaging in excessive drinking of illicit alcohol, which Bon Kalindo claims not only put the youth’s health and future at risk but also the future of development in Malawi. Thank you for tuning in and let stick together as we listen to what Bon Kalindo has to say about this issue and many other in today's audio…
Lero pa Nyasa VoiceBox, tikuwonetsa m'modzi mwa omwe adathandizira kwambiri, Womenyera Ufulu Wachibadwidwe, Bon Kalindo. M'mawu ake lero, Bon Kalindo wayamba ndi kuwulula nkhani yomwe ena anganene kuti ndi mliri m'Malawi. Achinyamata omwe akumwa mowa mopitirira muyeso, zomwe Bon Kalindo akuti sizikuyika thanzi ndi tsogolo la achinyamata pachiwopsezo komanso tsogolo lachitukuko m’Malawi. Zikomo chifukwa chomvetsera komanso kukhala limodzi pamene tikumvetsera zomwe Bon Kalindo akunena pa nkhaniyi ndi zina zambiri mu audio ya lero ...
#malawi
Kunena chilungamo mopanda mantha Mr bon kalindo.
Mulungu azikuteteza komanso upitilize kumenyera nkhondo amalawi.
God bless you Mr kallindo 🎉🎉🎉🎉🎉
Yeah Mr Bon Kalindo that's realistic history
Is true Mr president bon kalindo
Ndimakunyadira mr bon kalindo!!
I'm to just say we have to take this matter seriously because we have no leadership from tonse alliance from the judges, police, Malawi army, ministers, bishops, pastors because of what they are corrupted with money from the idiot Lazarus Chakwera. So what we have to listen from this man here MR BON KALINDO the only person who is trying to convince the Malawian the best direction for us poor people.
Mr born APA ndiye foni tapezeka chode padziko pano sopano pakuchitika zowophya tikufuna APA muzipezeka tsiku nditsiku
Mr bc Kodi wamva namanama amugendatu uku pa hhi koma DC ndiwe ooopsaaaa kwambiri🙆🙆🙆🙆
Bon kalindo chiuta awe nawe ukupanga history yabwino kwambili ndipo okuganizila zoipa back to the sender anthuwa ndipo ndioipa kwambili kuposa manyi agalu
MOWAWU NDI ACHINYATA ATHU ...BOMA LIKUYENERA KUCHITAPO KANTHU....KOMANSO NDIKUPEMPHA AMBUYE MULUNGU KUTI ADALITSE NDI TETEZERA MR BON KALINDO KU ADANI ATSIKU NDI TSIKU....
Continue with what you are doing we are 100% HAPPY who is NOT he/she is NOT of this COUNTRY
Umakwanira born kalindo
Malawi muno akutsogola ndi achinyamata,atsale iwowo atchuke nanga chomutengera munthu. Woti anapanga retire nkupatsa ntchito ndi chani 😢😢
Kumalawi kulibe nsogoleri kuli njoka yapansi pa nyanja msogoleri anagulitsa mzimu wake kumidima kalekale ikulamulira ndi njoka
mofaya boni kalindo
Amawaguliranso ndi iwo omwewo kuti adzikamenya anthu m'malo mowalemba ntchito. Kongelesi yatha basi. Enatu ananena kuti kuyendetsa boma si phada.
Ife sitisiya kumukuwa mpaka atule pansi akhala akumunamidza Kuti zinthu zilibwino ndiye APA timuwowozadi akhulupilile yekha Kuti azakewo amamu amamunamizadi
Ndipo inu mmmmmhu
Atolankhani anatha pa Malawi amaopa kufunsa mafunso anthu audindo akuti ulemu kkk zoopsya kobasi
The DC mwana wachabe kwambiri
Zowona dc malawi kwafuta
Akalondo mumakwan mau mukunena zoona mowa opanda maina monga u wa zigubu 5 liter
Mr DDD CCCC Wellcome back god be with you boss
Chilungamo chimapezeka mu mphamvu ya mau anu moya
👏👏👏👏🤝🤝🤝🤝🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼👏👏🤝
🎉🎉🎉🎉🎉
Bon kalindo bwelani pa straight mukuti bwanji?
Following with confidence
Mr boooooon
Mowa si edzi brother
Iyayi venselani bwino achimwene aaaaa
Anawa ndi edz
Nanga munthu ukakhala nchonchita nthawi yokapangula za chisembwele uyitenga ukuti vuto ndikusowa zochitako
Ndopodi achinyama akufa chifukwa cha mowa chifukwa akusowa zochita mulungu akhululukile Malawi 😢😢
Ma guys akumwa ethanol uja otsukira zitsulo..so sad
The DC Born Kalindo mawu amphamvu
Umatiyimila
Weniweni Dec
Dc power
Bon kalindo ndiwa chilungamo bs
Mulungu aziptlila kusamala moyo wanu Mr kalindo, timakunyadlan