A Aisha Mambo Alandila 150 Million Kuti Asokoneze UDF - Evance Khaiya
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 27 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Evance Khaiya claims that Honourable Aisha Mambo, chairperson of the UDF convention committee, has allegedly pocketed MWK 150 million from the MCP to sabotage the UDF's political ambitions.
Pa Nyasa Voicebox, Evance Khaiya wati wapampando wa komiti ya chipani cha UDF a Olemekezeka Aisha Mambo ati apereka ndalama zokwana MWK 150 million kuchokera ku MCP pofuna kusokoneza zolinga za chipani cha UDF.
#malawi
Kodi opposition ikhala bwanji ubale ndi MCP?
Komanso UDF monga Chipani cha Opposition chikhalira limodzi ndi cholamula bwanji ? Pangani mgwirizano wo Koma MCP Will never rule again. God will save His people Mphamvu Zanu zingachuluke bwanji inu a MCP Koma simungagonjetse Namalenga. Lets wait and see.
Amen bwana ❤❤
Amen bro❤
Osaculusa kuyankhula muzingotipasa uthengawo
Yes, please mukumamalizatu nokhaso nkhani yonse amatero?
Vuto lake
Umphawi sizinthu muyaluka nazo
Inoyo ndi 2024 osati make zana 1965 kunalibe ma phone 🤳 Facebook
Aisha mambo pamodzi ndi agaru omwe mwawayitanawo mudzagendedwa nawo limodzi komaso kwabwino kumango njamuka kusayana mkuwononga chipan sha UDF please Aisha mambo pamodzi ndi agaru omwe mukut abwere wo Koma a MCP ndat mukufuna mufike 2025 please don't come there this is oning??
A Bakili Muluzi analipo ndi Tembo pa mgwirizano koma DPP idawagwetsa pano zichitikansi akalimbila mgwirizano uwu.ndipo tsopano udf iferatu
Achotsedwe di adzipita Kung, ona ko okha, tengerani chitsanzo cha dpp anachotsa anthu wonse osokoneza
Inde ayisha mambo achoke ku UDF ndi mayi oipa kwabas aaaa hijabu yabodza bas
Ndimaiopa MCP kwambri kupha Chilima ngongole tho fertilizer otchipa chimanga chotchipa eeee MCP mbambande
A phweka chikangawa aliyese akufuna mahule onse akupita nkonko ku mcp
Aisha Mambo ndiwadyela😢...amapanga zinthu Ngati sanatuluke kumatako Kwa anthu bwanji 😢😢😢
Man ulemu wanu ine ndili kuno ku south Africa koma ndakusatani mu VN yanuyi u spoke well Aish mambo is eival wangovala buyi buyi koma ndi mfiti sakumva chisoni ndi anthu mene akuvutikila son beich
Inuyo akupatsani ndalama zingati a DPP? UDF anaipha ndi a DPP osati MCP kuti ikhale ndi ndi aphungu 7 okha out of 36 ku Eastern Region. UDF isaitane DPP ndi njoka.
Hule ameneyo ngt walandiladi ndalama ku mcp aziwe kut malawi sii yambuye akhe..ife tikuvutika mziko muno UDF ndichipani chathu.iyeyo ndi uhule wakheyo akachitile kunja kwa UDF
Muthu sungapange dzokozekera ndi m'dani wako kalipokalipo aishawo asatinamize
A UDF akuyenera kusamala naye nzimaiyu musaiwala kuti ku dpp analiponso anthi amena amasokoneza dpp Anankhimwa atalandira ndalama ku mcp kuti awononge chipani cha dpp a mcp mukhalike komanso Aisha angotuluka achisiye chipanicho iye apite ki mcp ko 150 million ndi chiyani kuti agulitse anthi a UDF ku mcp
AISHA MAMBO NDI GULU LAKO MUKATHERA KU CHIKANGAWA.BASOP!!!
Nkazi ameneyi walandira ndlama zamagazi basi wasatanic imeneyi achoke basi sakufunika ku udf
Achindidwa kangati kuti agulise udf ku mcp pantumbo pako nzimayi iwe
Komatu ngati UDF yathu ikutha chotchi ndichifukwa cha DPP not MCP
Zalowa personal tsopano.Mwina anakukani chibwenzi
Koma Dani lu watukwanika pang'ono koma mayiwa mpaka awakumbusa komwe anatulukira ayi zikomo
amene akunenayo kut inu ndi a DPP ndichisilu komso galu pamozi ndi amakhe
MULUNGU walinyanyala dziko la malawi chifukwa cha mcp
aisha ndalamazo kadyereni ku mcp komweko tulukan mwaulemu
2019 mesa anaphatikizana lero mukut bwa aaaa muzipaganawo
😮 mayi uyu ndi galu kwambasi pa nyini pakenso apite Ku mcp galu ameneyu
Ndi zoona a kunena akhayiyazi ine zinandiwawa pitilizani comrade
Ase umawelenga bwino kwambiri
Aaaaa ndiwe wabodza amadziwadi iweyo ndamenesudziwa Kodi mesa
Achoke zachibwa sitikufuna 😡
Aisha mambo inuyo panyini panu pamodzi ndi amuna anuo mapwala awo
mcp yisapite kumene tikayigendako
Mukunama Kodi audf mesa adpp anathawa.kuudf
Ufulu wakupanyo ulinawo iwe galu wamapolo panja
Ee koma achakwera atha Azeru tsopano
Iwe mayi ndiwe chidebe cheni cheni chobooka
Sanalakwe ai koma kuzolowera kutukwana
Zikudabwitsa ndizakuti anthu onse akukuwa kuwa apapa si a UDF onsewa ndi ADPP. Nonsense nonsenu sindinamve mukusapota UDF amene timamudziwa kuti ndi sapota wa UDF ndi ABDUL basi .Leave UDF alone. Mdani wa UDF ndi DPP si MCP AYI. For your I.nformation mbuli iwe a Tcheya anapangapo mgwirizano ndi John Tembo chifukwa Bingu anaipanga chipongwe UDF. Ndiye DPP ndi mdani number one wa UDF. Usachimvera Chikadeti cha Dpp chimenechi.
Is better DPP than MCP
Anthu zimene akufuna kuti azidya katatu osati zonsezo
Mukakamba za Bingu ndiye muyaluka
Bingu anachita kugula chipani chija chifukwa vice president analipo ndiye palibetso kuyankhula za Bingu
Acheyawo dyera kwambiri
Aishah Mambo Mai mulibe chison
Mayi ameneyo ndi wa MCP ndi galu
Ayi MCP sitikuwamfuna
Bambo ake analind udindo ku MCP
Komaanthu atopa tsopano
Mcp ndiye kuti mukuiwopatu
Nyini yake amenei Aisha ndi m c p yake
Tadziwa kut ndinu adpp zako
Comrade you are not Worthy Freedom fighter
Uchitsilu mayi inuyo
Koma 2009,Bakiri muluzi anapanga alliance ndi mcp.
Ndye zinatha bwanji taswera limodzi tinachangamuka pano ovota ndi anthu osati azavota yekha uyo wankhope ngt mamunayo
Ku constituency komwe amaimila Aisha ndikomwe kumachokera Abdul Lapken anaphedwa ndi MCP uja,zoona amai amenewa angamalimbe mtima kumaitana MCP kuzochitika za UDF zoona,anthu akudera lake azimuona ndidiso lotan maka maka akwachapola kwe Abdul Lapken amachokerako
Shame umunthu alibe ufiti koma eesh ndlama🙌🙌